Kalozera wa Mawu a MʼBaibulo
A
ABBA
, Aro 8:15 timafuula kuti: Abba, Atate!
ABELE
, Ge 4:8 Kaini anamenya Abele nʼkumupha
Mt 23:35 Kuyambira magazi a Abele wolungama
ABIGAYELI
, 1Sa 25:3 Abigayeli anali wanzeru
ABULAHAMU
, Ge 21:12 anauza Abulahamu kuti mumvere
2Mb 20:7 Abulahamu, bwenzi lanu
Mt 22:32 Mulungu wa Abulahamu, Mulungu wa
Aro 4:3 Abulahamu anakhulupirira Yehova
ABWERERANE
, 1Ak 7:11 asakwatiwe, abwererane
ACHIBALE
, Mac 10:24 atasonkhanitsa achibale
ACHIFWAMBA
, Lu 10:36 anakumana ndi achifwamba
ACHIKULIRE
, Aef 4:13 tidzakhala anthu achikulire
ACHINYAMATA
, Sl 110:3 Gulu la achinyamata
ADAMU
, Ge 5:5 Adamu anakhala ndi moyo zaka 930
1Ak 15:22 anthu onse amafa chifukwa cha Adamu
1Ak 15:45 Adamu womalizira anakhala mzimu
1Ti 2:14 Adamu sanapusitsidwe, koma mkaziyo
ADANI
, Sl 110:2 Pita pakati pa adani ako
Mt 5:44 Pitirizani kukonda adani anu
Mt 10:36 adani adzakhala a mʼbanja lake
ADYO
, Nu 11:5 Tikukumbukira adyo
ADZADZIWA KUTI NDINE YEHOVA
, Eks 7:5 Aiguputo adzadziwa kuti ndine Yehova
Eze 39:7 a mitundu adzadziwa kuti ndine Yehova
ADZITAME
, 1Ak 1:31 adzitame mwa Yehova
AGOGO
, 1Ti 5:4 Azibwezera kwa agogo awo
AKANI
, Yos 7:1 Akani anatenga zina mwa zinthu
AKAZI
, De 31:12 amuna, akazi, ana ndi alendo
1Mf 11:3 akazi olemekezeka 700
Miy 31:3 Usamapereke mphamvu kwa akazi
1Ak 9:5 ufulu woyenda ndi akazi athu
Aef 5:22 Akazi azigonjera amuna awo
Aef 5:28 amuna azikonda akazi awo
AKAZI AMASIYE
, Yak 1:27 Kusamalira ana ndi akazi amasiye
AKHRISTU
, Mac 11:26 anayamba kutchedwa Akhristu
AKUBA
, Mt 6:20 kumene akuba sangathyole
1Ak 6:10 akuba sadzalowa mu Ufumu
AKUFA
, Mla 9:5 akufa sadziwa chilichonse
Lu 20:38 Mulungu wa amoyo, osati akufa
Aef 2:1 munali akufa mʼmachimo anu
1At 4:16 amene anafa mwa Khristu
Chv 14:13 akufa ali ogwirizana ndi Ambuye
AKULA
, Mac 18:2 anapeza Myuda dzina lake Akula
AKULU
, Tit 1:5 uike akulu mumzinda
AKULUAKULU
, Aro 13:1 azimvera olamulira akuluakulu
1Ak 14:20 khalani anthu akuluakulu
ALEFA
, Chv 1:8 ndine Alefa ndi Omega
ALEVI
, Eks 32:26 Alevi onse anapita kwa Mose
Nu 3:12 Aleviwo adzakhala anga
2Mb 35:3 anauza Alevi, alangizi a Aisiraeli onse
ALIBE
, Yak 2:15 mʼbale kapena mlongo alibe zovala
ALIPODI
, Yoh 7:28 amene anandituma alipodi
AMBUYE
, Mt 6:24 sangatumikire ambuye awiri
1Ak 8:5 milungu yambiri ndi ambuye ambiri
Akl 4:1 inunso muli ndi Ambuye kumwamba
AMBUYE WAMKULU KOPOSA
, Sl 73:28 Yehova Ambuye Wamkulu Koposa
Mac 4:24 Ambuye Wamkulu, inu munapanga
AME
, 1Ak 14:16 anganene bwanji Ame?
2Ak 1:20 kudzeranso mwa iye, Ame amanenedwa
AMUNA
, Aef 5:25 Amuna, pitirizani kukonda akazi anu
Akl 3:18 akazi, muzigonjera amuna anu
ANA
, Ge 6:2 ana a Mulungu woona anatenga akazi
De 31:12 Sonkhanitsani anthu, ana ndi alendo
1Sa 8:3 Ana akewa sanatsatire chitsanzo chake
Yob 38:7 ana a Mulungu anayamba kufuula
Sl 8:2 mʼkamwa mwa ana ndi mwa makanda
Yes 54:13 Ana ako azidzaphunzitsidwa
Yes 66:8 Ziyoni anabereka ana aamuna
Mt 11:16 ngati ana aangʼono mʼmisika
Mt 18:3 nʼkukhala ngati ana aangʼono
Mt 19:14 Asiyeni anawo ndipo musawaletse
Lu 10:21 zimenezi mwaziulula kwa ana
Aro 8:14 ndi anadi a Mulungu
Aro 8:21 ufulu waulemerero wa ana a Mulungu
1Ak 7:14 ana anu sakanakhala oyera
1Ak 14:20 Koma khalani ana pa zoipa
2Ak 12:14 si udindo wa ana kusunga chuma
Aef 6:1 Ana inu, muzimvera makolo anu
1Yo 3:2 tsopano ndife ana a Mulungu
ANA AAKAZI
, Yow 2:28 ana aamuna ndi ana aakazi adzalosera
Mac 21:9 ana aakazi 4 osakwatiwa
2Ak 6:18 ana anga aamuna ndi aakazi
ANA AMASIYE
, Yak 1:27 Kusamalira ana amasiye
ANA A NKHOSA
, Yes 40:11 adzasonkhanitsa ana a nkhosa
Yoh 21:15 Dyetsa ana a nkhosa anga
ANEFILI
, Ge 6:4 padziko lapansi panali Anefili
ANENERI
, 1Mf 18:4 Obadiya anabisa aneneri 100
Amo 3:7 Asanaulule chinsinsi kwa aneneri
Mac 10:43 Aneneri amachitira umboni
ANENERI ABODZA
, Mt 7:15 Chenjerani ndi aneneri abodza
Mt 24:11 Kudzakhala aneneri abodza
Mko 13:22 kudzabwera aneneri abodza
ANGELO
, Ge 28:12 angelo akukwera ndi kutsika
Yob 4:18 angelo ake amawapezera zifukwa
Mt 13:41 adzatumiza angelo ake
Mt 22:30 adzakhala ngati angelo akumwamba
Mt 24:31 angelo adzasonkhanitsa osankhidwa ake
1Ak 4:9 tili mʼbwalo lamasewera kwa angelo
1Ak 6:3 simukudziwa kuti tidzaweruza angelo?
Ahe 13:2 anachereza angelo mosadziwa
1Pe 1:12 Angelo amafunitsitsa atamvetsa
Yuda 6 angelo amene anasiya utumiki
ANGWIRO
, Mt 5:48 Choncho khalani angwiro
ANNA
, Lu 2:36, 37 mneneri wamkazi, Anna
ANSEMBE
, Mik 3:11 Ansembe ake amaphunzitsa
Mac 6:7 ansembe anakhala okhulupirira
Ahe 2:17 mkulu wa ansembe wachifundo
1Pe 2:9 ansembe achifumu, mtundu woyera
Chv 20:6 ansembe a Mulungu adzalamulira
ANTCHITO ANZAKE
, 1Ak 3:9 antchito anzake a Mulungu
ANTHU
, 1At 2:14 kuvutitsidwa ndi anthu akwanu
ANTHU ANZERU
, Lu 10:21 anthu anzeru mwawabisira
ANTHU WAMBA
, Mac 4:13 osaphunzira ndiponso anthu wamba
ANYAMATA
, Miy 20:29 Ulemerero wa anyamata
ANZAKE
, Miy 14:20 amakhala ndi anzake ambiri
Yoh 15:13 wapereka moyo chifukwa cha anzake
ANZANGA
, Yoh 15:14 mukhala anzanga
ANZANU
, Lu 16:9 Pezani anzanu ndi chuma chosalungama
ANZERU
, Yes 5:21 amadziona ngati anzeru
Mt 11:25 anthu anzeru ndi ozindikira mwawabisira
1Ak 1:26 anthu amawaona kuti ndi anzeru
APHUNZITSI
, Sl 119:99 kuposa aphunzitsi anga
Aef 4:11 kuti akhale abusa ndi aphunzitsi
APOLO
, Mac 18:24 Apolo, ankalankhula mwaluso
APOZI
, Miy 25:11 maapozi agolide mʼmbale zasiliva
ARAMAGEDO
, Chv 16:16 mʼChiheberi, Aramagedo
ARARATI
, Ge 8:4 chinaima pamapiri a Ararati
AREKABU
, Yer 35:5 vinyo pamaso pa Arekabu
AREOPAGI
, Mac 17:22 anaima mʼbwalo la Areopagi
ASADYE
, 2At 3:10 osagwira ntchito, asadye
ASODZI A ANTHU
, Mt 4:19 ndikusandutsani asodzi a anthu
ATATE
, Yes 9:6 dzina lakuti Atate Wamuyaya
Mt 6:9 Atate wathu wakumwamba
Mt 23:9 musamatchule aliyense kuti atate
Lu 2:49 ndiyenera kupezeka mʼnyumba ya Atate
Yoh 5:20 Atate amamuonetsa zonse
Yoh 10:30 Ine ndi Atate ndife amodzi
Yoh 14:6 Palibe amafika kwa Atate osadzera
Yoh 14:9 Amene waona ine waona Atate
Yoh 14:28 Atate ndi wamkulu kuposa ine
Yoh 14:28 ndikupita kwa Atate wanga
ATEMI
, Mac 19:34 Wamkulu ndi Atemi
ATUMIKI
, 1Ak 4:2 chofunika kwa atumiki
2Ak 3:6 oyenera kukhala atumiki
2Ak 6:4 tikusonyeza kuti ndife atumiki a Mulungu
ATUMIKI APAKACHISI
, Eza 8:20 panali atumiki apakachisi
ATUMIKI OTHANDIZA
, 1Ti 3:8 atumiki othandiza akhale
ATUMWI
, Mt 10:2 Mayina a atumwi 12 ndi awa
Mac 15:6 atumwi ndi akulu anasonkhana
1Ak 15:9 ndine wamngʼono kwambiri pa atumwi
2Ak 11:5 atumwi anu apamwambawo
AWIRIAWIRI
, Lu 10:1 nʼkuwatumiza awiriawiri
AYUDA
, Aro 3:29 kodi ndi Mulungu wa Ayuda okha?
B
BAALA
, Yer 19:5 ngati nsembe kwa Baala
BABELE
, Ge 11:9 unatchedwa Babele
BABULO
, Yer 51:6 Tulukani mʼBabulo nʼkuthawa
Yer 51:30 Asilikali a ku Babulo asiya kumenya
Yer 51:37 Babulo adzakhala milu yamiyala
Chv 17:5 Babulo Wamkulu, mayi wa mahule
Chv 18:2 Wagwa! Babulo Wamkulu wagwa
BADWA
, Yob 14:1 Munthu wobadwa kwa mkazi
Sl 51:5 Ndinabadwa ndili wochimwa
1Pe 1:3 anachititsa kuti tibadwenso mwatsopano
BALAMU
, Nu 22:28 bulu analankhula kwa Balamu
BAMBO
, Ge 2:24 adzasiya bambo ndi mayi ake
Sl 2:7 Lero, ine ndakhala bambo ako
Sl 89:26 Inu ndinu Bambo anga
Sl 103:13 Mofanana ndi bambo wachifundo
Lu 15:20 bambo anathamanga nʼkumukumbatira
BANJA
, 1Ak 7:25 amene sali pabanja
1Ak 7:38 amene sanalowe mʼbanja wachita bwino
Aef 2:19 ndinu a mʼbanja la Mulungu
Aef 3:15 amapangitsa banja kukhala ndi dzina
BARANABA
, Mac 9:27 Baranaba anamuthandiza
BARUKI
, Yer 45:2 Ponena za iwe Baruki, Yehova
BATI-SEBA
, 2Sa 11:3 Bati-seba, mkazi wa Uriya
BATIZA
, Mt 3:13 kwa Yohane kuti amubatize
Mt 28:19 Muziwabatiza mʼdzina la Atate
Mac 2:41 amene analandira mawu anabatizidwa
Mac 8:36 Chikundiletsa kubatizidwa nʼchiyani?
Aro 6:4 tinabatizidwa mu imfa yake
BAYA
, Zek 12:10 adzayangʼana amene anamubaya
BELISAZARA
, Da 5:1 Belisazara anakonza phwando
BEREKA
, Eks 23:26 mkazi wosabereka
De 7:14 sipadzapezeka chiweto chosabereka
Yes 54:1 mkazi amene sunaberekepo mwana
Yes 66:7 anabereka asanayambe kumva zowawa
BETELEHEMU
, Mik 5:2 Iwe Betelehemu Efurata
BETELI
, Ge 28:19 anawapatsa dzina lakuti Beteli
BEZALELI
, Eks 31:2 Inetu ndasankha Bezaleli
BISA
, Miy 28:13 Wobisa machimo sizidzamuyendera
BISIKA
, Sl 91:1 mʼmalo obisika a Wamʼmwambamwamba
BODZA
, Sl 101:7 wabodza sadzaima pamaso panga
Mt 26:59 ankafunafuna umboni wabodza
Yoh 8:44 Mdyerekezi, tate wake wa bodza
2At 2:11 kuti azikhulupirira bodza
BUKU
, Eks 32:33 ndimufufute mʼbuku langa
Yos 1:8 Buku la Chilamulo ili lisachoke
Mla 12:12 adzapitirizabe kulemba mabuku ambiri
Mki 3:16 Buku la chikumbutso linalembedwa
Mac 19:19 anasonkhanitsa mabuku nʼkuwatentha
Chv 20:15 dzina silinalembedwe mʼbuku la moyo
BULU
, Nu 22:28 anachititsa bulu kulankhula
Zek 9:9 mfumu ikubwera itakwera bulu
BUNTHWA
, Mla 10:10 Ngati nkhwangwa yabunthwa
BUULA
, Eks 2:24 Mulungu anamva kubuula
Yes 35:10 chisoni ndi kubuula zidzachoka
Eze 9:4 akuusa moyo komanso kubuula
Aro 8:22 chilengedwe chonse chikubuula
BWALO LA MILANDU
, Da 7:10 Bwalo la milandu linayamba kuzenga
BWANA
, Aro 14:4 udindo wa bwana kumuweruza
BWENZI
, 2Mb 20:7 Abulahamu, bwenzi lanu
Miy 16:28 amalekanitsa mabwenzi
Yak 4:4 akufuna kukhala bwenzi la dziko
BWERA
, Yes 55:1 bwerani mudzamwe madzi
Mac 1:11 adzabwera mʼnjira yofanana
Chv 22:17 amene wamva anene kuti, Bwera!
BWEREKA
, Sl 37:21 woipa amabwereka osabweza
Miy 22:7 wobwereka amakhala kapolo
BWERERA
, Yow 2:12 bwererani ndi mtima wonse
Mki 3:7 Bwererani ndipo ndidzabwerera kwa inu
Aga 4:9 kubwerera ku mfundo zamʼdzikoli
Ahe 10:39 obwerera kupita kuchiwonongeko
BWEZA
, Sl 37:21 woipa amabwereka osabweza
BWEZERA
, De 32:35 Kubwezera ndi kwanga
Sl 116:12 Yehova ndidzamubwezera chiyani
Miy 20:22 Ndidzabwezera choipa
Aro 12:19 Okondedwa, musamabwezere zoipa
Aro 12:19 Malemba amati: Kubwezera ndi kwanga
2At 1:8 adzabwezera chilango
BWINO
, Ge 1:31 zonse zinali zabwino
Ge 3:5 Mudzadziwa zabwino ndi zoipa
De 10:13 kuti zinthu zikuyendereni bwino
Mt 25:21 Wachita bwino kwambiri
Aro 5:7 angalimbe mtima kufera munthu wabwino
Aro 7:19 Zinthu zabwino zimene ndimafuna
Aga 6:10 tiyeni tichitire onse zabwino
C
CHACHINGʼONO
, Lu 16:10 wokhulupirika pa chachingʼono
CHAKA
, Nu 14:34 tsiku limodzi kuwerengera chaka
CHAKA CHA UFULU
, Le 25:10 Chizikhala Chaka cha Ufulu
CHAKHUMI
, Ne 10:38 magawo 10 a chakhumicho
CHAKUDYA
, Ne 9:15 chakudya chochokera kumwamba
Sl 37:25 ana ake akupemphapempha chakudya
Sl 145:15 Mumazipatsa chakudya
Yes 55:2 polipirira zinthu zimene si chakudya
Mt 4:4 sangakhale ndi moyo ndi chakudya
Mt 6:11 Mutipatse chakudya chimene tikufunikira
Mt 24:45 chakudya pa nthawi yoyenera
Yoh 4:34 Chakudya, kuchita zofuna zanu
Yoh 6:27 chakudya chomwe chimawonongeka
Yoh 6:35 Ine ndine chakudya chopatsa moyo
Mac 14:17 Anadzaza mitima yanu ndi chakudya
1Ak 8:13 ngati chakudya chikukhumudwitsa
CHAKUDYA CHAMADZULO
, 1Ak 11:20 Chakudya Chamadzulo cha Ambuye
CHAKUKHOSI
, Le 19:18 musasunge chakukhosi
CHALA
, Eks 8:19 Chimenechi ndi chala cha Mulungu!
Eks 31:18 yolembedwa ndi chala cha Mulungu
CHAMOYO
, Sl 150:6 Chamoyo chitamande Ya
CHANGWIRO
, Sl 19:7 Chilamulo cha Yehova ndi changwiro
CHEDWA
, Yes 46:13 chipulumutso sichidzachedwa
Hab 2:3 Ngakhale atachedwa uziwayembekezera
Hab 2:3 masomphenyawa sadzachedwa
Lu 12:45 Mbuye wanga akuchedwa kubwera
2Pe 3:9 Yehova sakuchedwa kukwaniritsa
CHEMWALI
, De 27:22 wogona ndi mchemwali wake
CHENJERA
, Miy 12:23 wochenjera amabisa
Miy 14:15 wochenjera amaganizira zotsatira
Miy 22:3 wochenjera akaona tsoka amabisala
Mt 10:16 muzichita zinthu mochenjera ngati njoka
CHENJEZA
, Eze 3:17 ukuyenera kuwachenjeza
Eze 33:9 ukachenjeza munthu woipa
1Ak 10:11 zinalembedwa kuti zitichenjeze
CHENJEZO
, Eze 33:4 koma osamvera chenjezolo
CHEPA
, Zek 4:10 munayamba ndi zinthu zochepa
CHEREZA
, Aro 12:13 Khalani ochereza
Tit 1:7, 8 akhale wochereza alendo
Ahe 13:2 Musaiwale kuchereza alendo
1Pe 4:9 Muzicherezana popanda kudandaula
3Yo 8 ndi udindo wathu kuwachereza
CHEZA
, Ge 19:14 ankangoona ngati akunena zocheza
Miy 26:19 Inetu ndimangochita zocheza
CHEZERA
, Mac 15:36 tikachezere abale, tikawaone
CHIBADWA
, Le 18:23 nʼzosemphana ndi chibadwa
Aro 1:26 akazi anasiya njira yachibadwa
Aro 1:27 Amunanso anasiya njira yachibadwa
Yuda 7 mʼnjira imene si yachibadwa
CHIDA
, Yes 54:17 Chida chilichonse sichidzapambana
CHIDAKWA
, Miy 23:21 chidakwa chidzasauka
1Ak 5:11 musamagwirizane ndi chidakwa
1Ak 6:10 zidakwa sizidzalowa mu Ufumu
CHIDANI
, Ge 3:15 Ndidzaika chidani
Aef 4:31 Chidani chachikulu, kupsa mtima
CHIDINDO
, Nym 8:6 pamtima pako ngati chidindo
2Ak 1:22 watidinda chidindo chake
2Ak 1:22 Chidindo chimenechi ndi mzimu woyera
Aef 1:13 ndi mzimu woyera anakuikani chidindo
Chv 7:3 mpaka titadinda chidindo pazipumi
CHIFANIZIRO
, Ge 1:26 munthu mʼchifaniziro chathu
Eks 20:4 Musadzipangire chifaniziro
Da 2:31 mukuona chifaniziro chachikulu
CHIFUKWA
, Mla 7:25 chifukwa chake zinthu zimachitika
Aro 13:5 chifukwa chabwino choti muzigonjera
CHIFUKWA CHOMVEKA
, Aro 1:20 alibenso chifukwa chomveka
CHIFUNDO
, De 4:31 Yehova ndi Mulungu wachifundo
1Mb 21:13 chifundo chake nʼchachikulu
Ne 9:19 simunawasiye chifukwa cha chifundo
Sl 78:38 ankawamvera chifundo
Miy 28:13 adzachitiridwa chifundo
Yes 55:7 abwerere, adzamuchitira chifundo
Mt 5:7 Osangalala ndi anthu achifundo
Mt 9:13 Ndikufuna chifundo, osati nsembe
Mt 20:34 Yesu atagwidwa ndi chifundo
Lu 6:36 achifundo mofanana ndi Atate wanu
Yak 2:13 Chifundo chimaposa chiweruzo
Yak 5:11 Yehova ndi wachikondi, wachifundo
1Yo 3:17 koma osamusonyeza chifundo
CHIFUNDO CHACHIKULU
, 2Ak 1:3 Bambo wachifundo chachikulu
Akl 3:12 valani chifundo chachikulu
CHIFUNIRO
, Mac 21:14 Chifuniro cha Yehova chichitike
Aro 12:2 muzindikire chifuniro cha Mulungu
Ahe 13:21 muchite chifuniro chake
CHIFUWA
, Yes 40:11 adzawanyamulira pachifuwa
CHIGOLOLO
, Eks 20:14 Musachite chigololo
Mt 5:28 wachita naye kale chigololo mumtima
Mt 19:9 nʼkukwatira wina wachita chigololo
1Ak 6:9 achigololo sadzalowa mu Ufumu
CHIGUMULA
, Ge 9:11 sizidzawonongedwanso ndi chigumula
Mt 24:38 Chigumula chisanafike, ankadya
2Pe 2:5 anabweretsa chigumula padziko
CHIHEMA
, Yos 18:1 chihema chokumanako
Sl 78:60 anasiya chihema cha ku Silo
Sl 84:1 ndimakonda chihema chanu
Chv 21:3 Taonani! Chihema cha Mulungu
CHIKHULUPIRIRO
, Sl 27:13 kukhala ndi chikhulupiriro
Lu 17:6 chikhulupiriro chofanana ndi kanjere
Lu 18:8 akadzafika, adzapezadi chikhulupiriro?
Aro 1:17 chifukwa cha chikhulupiriro chake
Aro 4:20 chikhulupiriro chinamupatsa mphamvu
2Ak 4:13 tili ndi chikhulupiriro, tikulankhula
2Ak 5:7 tikuyenda ndi chikhulupiriro
Aga 6:10 abale ndi alongo athu mʼchikhulupiriro
Aef 4:5 chikhulupiriro chimodzi, ubatizo umodzi
2At 3:2 si onse ali ndi chikhulupiriro
2At 3:4 tili ndi chikhulupiriro mwa inu
2Ti 1:5 chikhulupiriro chopanda chinyengo
Ahe 11:1 Chikhulupiriro ndi kusakayikira
Ahe 11:6 popanda chikhulupiriro nʼzosatheka
Yak 2:26 chikhulupiriro chopanda ntchito
1Pe 1:7 Chikhulupiriro chanu chayesedwa
CHIKOLE
, Miy 17:18 amalonjeza kuti akhala chikole
Aef 1:14 chikole chotsimikizira
CHIKONDI
, Nym 8:6 chikondi sichigonja
Mt 24:12 chikondi cha ambiri chidzazirala
Yoh 15:13 Palibe amene ali ndi chikondi kuposa
Aro 8:39 kutisiyanitsa ndi chikondi cha Mulungu
Aro 13:10 chikondi chimakwaniritsa lamulo
1Ak 8:1 chikondi chimalimbikitsa
1Ak 13:2 ngati ndilibe chikondi, zilibe ntchito
1Ak 13:8 Chikondi sichitha
1Ak 13:13 Koma chachikulu ndi chikondi
1Ak 16:14 Zonse muzizichita mwachikondi
Akl 3:14 chikondi chimagwirizanitsa mwamphamvu
1At 2:7 tinakusonyezani chikondi
1Pe 4:8 chikondi chimakwirira machimo
1Yo 4:8 Mulungu ndi chikondi
Chv 2:4 kusonyeza chikondi ngati poyamba
CHIKONDI CHACHIKULU
, Yak 5:11 Yehova ndi wachikondi chachikulu
CHIKONDI CHOKHULUPIRIKA
, Eks 34:6 Yehova, wachikondi chokhulupirika
Sl 13:5 ndakhulupirira chikondi chokhulupirika
Sl 136:1-26 Chikondi chokhulupirika chidzakhalapo
Ho 6:6 chikondi chokhulupirika, osati nsembe
CHIKUMBUMTIMA
, 1Pe 3:16 Muzikhala ndi chikumbumtima chabwino
1Pe 3:21 kupempha chikumbumtima chabwino
1Ti 4:2 chikumbumtima chili ngati chipsera
Aro 2:15 chikumbumtima chimawachitira umboni
Aro 13:5 chifukwanso cha chikumbumtima chanu
1Ak 8:12 nʼkumavulaza chikumbumtima chawo
CHILAKOLAKO
, Aef 2:3 motsatira zilakolako za thupi
Akl 3:5 chilakolako chosalamulirika
1At 4:5 chilakolako chosalamulirika chogonana
2Ti 2:22 thawa zilakolako za unyamata
Yak 1:14 amayesedwa ndi chilakolako
1Yo 2:16 thupi limalakalaka, maso amalakalaka
CHILALA
, Yer 17:8 pa chilala sadzada nkhawa
CHILAMULO
, Sl 19:7 Chilamulo cha Yehova ndi changwiro
Sl 40:8 chilamulo chanu chili mumtima mwanga
Sl 119:97 Ndimakonda kwambiri chilamulo chanu!
Yer 31:33 Ndidzaika chilamulo changa mwa iwo
Aro 10:4 Khristu ndi kutha kwa Chilamulo
Aga 3:24 Chilamulo chinatitsogolera kwa Khristu
Aga 6:2 mukukwaniritsa chilamulo cha Khristu
CHILANGO
, Miy 23:13 usalephere kumupatsa chilango
1Ak 11:29 akudzibweretsera chilango
Ahe 12:11 palibe chilango chosangalatsa
CHILANKHULO
, Ge 11:7 nʼkukasokoneza chilankhulo
Zef 3:9 ndidzasintha chilankhulo cha anthu
Chv 7:9 chilankhulo chilichonse
CHILEMA
, Le 22:21 nyama yopanda chilema
CHILIMWE
, Mt 24:32 chilimwe chili pafupi
CHILUNGAMO
, Yob 34:12 sakhotetsa chilungamo
Yob 40:8 Kodi ndine wopanda chilungamo?
Sl 37:28 Yehova amakonda chilungamo
Sl 45:7 Unkakonda chilungamo
Miy 29:4 Mfumu ikamachita zachilungamo
Mla 5:8 Ukaona zopanda chilungamo usadabwe
Yes 26:9 amaphunzira zokhudza chilungamo
Yes 32:1 Mfumu idzalamulira mwachilungamo
Yes 32:1 adzalamulira mwachilungamo
Yes 60:17 chilungamo chikhale okupatsa ntchito
Mik 6:8 kuti uzichita chilungamo
Lu 18:7 kuti chilungamo chachitika?
Mac 28:4 Chilungamo sichinamulole
Aro 9:14 Mulungu alibe chilungamo? Ayi ndithu
2Pe 3:13 mmenemo mudzakhala chilungamo
CHIMAKE
, 1Ak 7:36 pachimake pa unyamata
CHIMANJAMANJA
, De 16:16 kukaonekera chimanjamanja
CHIMBALANGONDO
, 1Sa 17:37 mʼkamwa mwa chimbalangondo
Yes 11:7 Ngʼombe ndi chimbalangondo
CHIMWA
, Ge 39:9 nʼkuchimwira Mulungu?
2Sa 12:13 Ndachimwira Yehova
1Mf 8:46 Anthu anu akakuchimwirani
Sl 1:5 ochimwa sadzapezekanso
Mt 18:15 ngati mʼbale wako wachimwa
Lu 15:7 munthu wochimwa amene walapa
Lu 18:13 ndikomereni mtima wochimwa ine
Yoh 9:31 Mulungu samvetsera ochimwa
Aro 3:23 onse ndi ochimwa ndipo amalephera
Aro 5:8 pamene tinali ochimwa, Khristu anatifera
Yak 4:17 koma sakuchichita, akuchimwa
CHIMWEMWE
, Ne 8:10 chimwemwe chimene Yehova amapereka
1At 1:6 chimwemwe cha mzimu woyera
1Ti 1:11 Mulungu wachimwemwe
CHIMWITSA
, Mt 5:29 diso limakuchimwitsa
CHINGALAWA
, Ge 6:14 Upange chingalawa
CHINGWE
, Mla 4:12 chopotedwa ndi zingwe zitatu
Yes 54:2 Talikitsa zingwe za tenti yako
CHINGWE CHA NYALE
, Yes 42:3 chingwe cha nyale sadzachizimitsa
CHINSINSI
, Miy 11:13 amasunga chinsinsi
Miy 20:19 amayendayenda nʼkumaulula zinsinsi
Miy 25:9 usaulule zachinsinsi zimene unauzidwa
Amo 3:7 Asanaulule chinsinsi chake kwa aneneri
Afi 4:12 ndaphunzira chinsinsi chokhala wokhuta
CHINSINSI CHOPATULIKA
, Aro 16:25 chinsinsi chopatulika chakhala chobisika
Aef 3:4 kuzindikira chinsinsi chopatulika
CHINTHU CHONYANSA
, Mt 24:15 mukadzaona chinthu chonyansa
CHINTHU CHOSEKETSA
, Yer 20:7 Ndakhala chinthu choseketsa
CHINYENGO
, Sl 34:13 milomo isalankhule chinyengo
Miy 15:27 wopeza phindu mwachinyengo
Da 6:4 Danieli sankachita zachinyengo
Mki 2:15 musachitire zachinyengo akazi anu
Aro 16:18 amagwiritsa ntchito mawu achinyengo
Aga 2:4 abale achinyengo analowa
Aef 4:25 tayani chinyengo, lankhulani zoona
2Pe 2:3 azidzagwiritsa ntchito mawu achinyengo
CHIONETSERO
, 1Ak 4:9 waika atumwi pachionetsero
CHIPEWA
, Aef 6:17 valani chipewa cha chipulumutso
CHIPHAMASO
, Miy 3:32 amanyansidwa ndi wachiphamaso
Miy 26:28 pakamwa polankhula mwachiphamaso
Miy 29:5 woyamikira mnzake mwachiphamaso
Aro 12:9 Chikondi chisakhale chachiphamaso
CHIPHUPHU
, Mla 7:7 chiphuphu chimawononga
CHIPILALA
, Ge 19:26 anasanduka chipilala
Eks 13:22 Chipilala cha mtambo sichinkachoka
CHIPONGWE
, Lu 18:32 akamuchitira chipongwe
Lu 22:63 anamuchitira zachipongwe, kumumenya
1Pe 2:23 sanabwezere zachipongwe
CHIPULULU
, Yes 35:1 Dera lachipululu lidzakondwa
Yes 35:6 mʼdera lachipululu mudzayenda mitsinje
Yes 35:6 Mʼchipululu mudzatumphuka madzi
Yes 41:18 Chipululu ndidzachisandutsa dambo
CHIPULUMUTSO
, Est 4:14 chipulumutso chidzachokera kwina
Sl 3:8 Chipulumutso chimachokera kwa Yehova
Lu 21:28 chipulumutso chanu chikuyandikira
Aro 13:11 chipulumutso chathu chili pafupi
Chv 7:10 Chipulumutso chachokera kwa Mulungu
CHIPUMI
, Eze 3:9 chipumi chikhale ngati mwala
CHIRITSA
, 2Mb 36:16 chiyembekezo cha kuchiritsidwa
Sl 147:3 Iye amachiritsa anthu osweka mtima
Miy 12:18 lilime la anzeru limachiritsa
Lu 4:23 Wochiritsa iwe, dzichiritse wekha
Lu 9:11 anachiritsa ofunika kuchiritsidwa
Lu 10:9 muzichiritsanso odwala
Mac 5:16 Ndipo onsewo ankachiritsidwa
Chv 22:2 Masamba ochiritsira anthu
CHISAUTSO
, Mt 24:21 kudzakhala chisautso chachikulu
Chv 7:14 atuluka mʼchisautso chachikulu
CHISHANGO
, Sl 84:11 Yehova ndi chishango
Aef 6:16 chishango chachikulu chachikhulupiriro
CHISOKONEZO
, 1Ak 14:33 Mulungu si wachisokonezo
CHISONI
, Sl 31:10 ndi wodzaza ndi chisoni
Sl 34:18 amapulumutsa odzimvera chisoni
Sl 38:6 ndili wachisoni tsiku lonse
Sl 51:17 kudzimvera chisoni mumtima
Sl 78:41 ankachititsa kuti amve chisoni
Sl 90:10 zodzaza ndi mavuto komanso chisoni
Mla 7:3 Ndi bwino kumva chisoni
Yes 51:11 chisoni ndi kulira zidzachoka
Mt 5:4 Osangalala ndi amene akumva chisoni
Mt 9:36 Ataona anthu, anawamvera chisoni
1Ak 15:19 ndife omvetsa chisoni
2Ak 2:7 angakhale ndi chisoni chopitirira malire
2Ak 7:9 Popeza munamva chisoni
Aef 4:30 musamamvetse chisoni mzimu woyera
1At 4:13 musakhale ndi chisoni chofanana
Ahe 4:15 amene sangatimvere chisoni
CHISOTI
, Miy 12:4 Mkazi wabwino ndi chisoti
Mt 27:29 analuka chisoti chachifumu chaminga
CHISWE
, Aro 16:4 anaika miyoyo yawo pachiswe
CHITA
, Eks 19:8 tidzachita zomwezo
Mla 12:13 zimene munthu akuyenera kuchita
Aro 7:15 zimene ndimafuna kuchita, sindizichita
2At 3:14 musiye kuchitira naye zinthu limodzi
1Yo 3:6 chizolowezi chochita tchimo
CHITETEZO
, Sl 18:2 Yehova ndi malo anga achitetezo
Yes 32:17 chilungamo chidzabweretsa chitetezo
Zef 3:12 adzapeza chitetezo mʼdzina la Yehova
Afi 3:1 Kubwereza kulemba ndi chitetezo
CHITIKA
, Yes 46:10 zimene zidzachitike
Yes 55:11 zimene ndinawatumizira zidzachitikadi
CHITIRA UMBONI
, Le 5:1 akachitire umboni za tchimolo
CHITITSA
, 1Sa 22:22 ndachititsa kuti anthu aphedwe
CHITSA
, Yes 11:1 idzaphuka pachitsa cha Jese
Da 4:15 musiye chitsa ndi mizu yake
CHITSAMBA
, Mac 7:30 anaonekera pachitsamba
CHITSANZO
, Yoh 13:15 ndakupatsani chitsanzo
2Ak 4:2 takhala chitsanzo chabwino
1Ti 4:12 ukhale chitsanzo kwa okhulupirika
2Ti 1:13 chitsanzo cha mawu olondola
Ahe 8:5 wapanga zonse motsatira chitsanzo
Yak 5:10 tengerani chitsanzo cha aneneri
1Pe 2:21 Khristu anakusiyirani chitsanzo
1Pe 5:3 chitsanzo chabwino kwa nkhosa
CHITSIME
, Miy 5:15 Imwa madzi amʼchitsime chako
CHITSIRU
, Miy 22:15 Uchitsiru umakhazikika
CHITSOTSO
, Mt 7:3 kachitsotso mʼdiso
CHITSULO
, Miy 27:17 Chitsulo chimanola chitsulo
Yes 60:17 Mʼmalo mwa chitsulo ndidzabweretsa
Da 2:43 chitsulo sichingasakanikirane ndi dongo
CHIWANDA
, Mac 16:16 chiwanda cholosera
CHIWAWA
, Ge 6:11 dziko linadzaza ndi chiwawa
Sl 5:6 Yehova amadana ndi anthu achiwawa
Sl 11:5 amene amakonda chiwawa
Sl 72:14 kuchitiridwa zachiwawa
CHIWEREWERE
, Mt 15:19 maganizo a chiwerewere
Mac 15:20 apewe chiwerewere ndi magazi
1Ak 5:9 musiye kugwirizana ndi achiwerewere
1Ak 6:9 Achiwerewere sadzalowa mu Ufumu
1Ak 6:18 Thawani chiwerewere
1Ak 10:8 tisamachite chiwerewere
Aga 5:19 ntchito za thupi ndi chiwerewere
Aef 5:3 Nkhani zachiwerewere zisatchulidwe
Akl 3:5 ziwalo zikhale zakufa ku chiwerewere
1At 4:3 Mulungu akufuna muzipewa chiwerewere
CHIWERUZO
, 1Pe 4:17 chiweruzo chiyambira panyumba yake
CHIWIYA
, Mac 9:15 ameneyu ndi chiwiya changa
CHIWOMBANKHANGA
, Yes 40:31 adzauluka ngati chiwombankhanga
CHIWONONGEKO
, Mt 25:46 kupita kuchiwonongeko
2At 1:9 chilango cha chiwonongeko chamuyaya
CHIYAMBI
, Mt 24:8 chiyambi cha mavuto aakulu
Mt 25:34 kuchokera pachiyambi cha dziko
CHIYEMBEKEZO
, Sl 146:5 chiyembekezo chake chili mwa Yehova
Aro 8:24 sichikhalanso chiyembekezo
Aro 12:12 Kondwerani ndi chiyembekezo
Aro 15:4 tikhale ndi chiyembekezo
Aef 1:18 chiyembekezo chimene wakupatsani
Aef 2:12 Munalibe chiyembekezo
Ahe 6:19 Chiyembekezo chili ngati nangula
CHIZINDIKIRO
, Eze 9:4 ulembe chizindikiro pazipumi
Mt 24:3 chizindikiro cha kukhalapo kwanu
Mt 24:30 chizindikiro cha Mwana wa munthu
2At 3:14 muikeni chizindikiro, osachita naye zinthu
Chv 13:17 kupatulapo ngati ali ndi chizindikirocho
CHOBISIKA
, Lu 8:17 palibe chobisika
CHODZITETEZERA PACHIFUWA
, Aef 6:14 mutavala chodzitetezera pachifuwa
CHOIPA
, Sl 101:3 Sindidzayangʼana choipa
Aro 12:17 Musamabwezere choipa pa choipa
CHOKA
, Yer 23:5 yochokera mʼbanja la Davide
1Ak 7:15 wosakhulupirirayo wasankha kuchoka
CHOLEMERA
, Ahe 12:1 titaye cholemera chilichonse
CHOLINGA
, Miy 16:4 chikwaniritse cholinga
Aro 8:28 mogwirizana ndi cholinga chake
Aro 9:11 Mulungu anasonyeza cholinga chake
Aef 3:11 nʼzogwirizana ndi cholinga chamuyaya
CHOLOWA
, Nu 18:20 ndine gawo ndi cholowa chako
Sl 127:3 Ana ndi cholowa
Mlr 3:24 Yehova ndi cholowa changa
1Pe 1:4 cholowa chosadetsedwa, chosasuluka
CHONDERERA
, Aro 8:34 amatilankhulira mochonderera
Ahe 5:7 anapereka mapemphero ochonderera
CHOONADI
, Sl 119:160 Mawu anu ndi choonadi
Miy 23:23 Gula choonadi ndipo usachigulitse
Yoh 4:24 kulambira ndi mzimu komanso choonadi
Yoh 8:32 Mudzadziwa choonadi, chidzakumasulani
Yoh 14:6 Ine ndine njira, choonadi ndi moyo
Yoh 16:13 mzimu wa choonadi, adzakutsogolerani
Yoh 17:17 Ayeretseni ndi choonadi
Yoh 18:38 Pilato anati: Choonadi nʼchiyani?
2Ak 13:8 sitingachite chotsutsana ndi choonadi
2Pe 1:12 ndinu olimba mʼchoonadi
3Yo 4 ana anga akuyendabe mʼchoonadi
CHOTSA
, 1Ak 5:13 Mʼchotseni munthu woipayo
CHULUKA
, Sl 40:12 Zolakwa zanga ndi zochuluka
Lu 12:15 atakhala ndi zochuluka chotani
Yoh 10:10 zikhale ndi moyo wochuluka
CHUMA
, Eks 19:5 mudzakhaladi chuma chapadera
Sl 62:10 Ngati chuma chanu chachuluka
Miy 2:4 kuzifufuza ngati chuma chobisika
Miy 10:2 Chuma chopeza pochita zoipa
Miy 11:4 Chuma chidzakhala chopanda phindu
Miy 11:28 Munthu amene amadalira chuma
Miy 18:11 Chuma cha munthu wolemera
Miy 30:8 Musandipatse umphawi kapena chuma
Mla 5:10 wokonda chuma sakhutira
Yer 9:23 wachuma asadzitame
Eze 28:5 unadzikuza chifukwa cha chuma
Mt 6:21 kumene kuli chuma chako
Mt 6:24 kutumikira Mulungu ndi Chuma
Mt 13:22 chinyengo champhamvu cha chuma
Mt 13:44 uli ngati chuma chobisika
Lu 6:45 amatulutsa zabwino mʼchuma chabwino
Lu 12:33 chuma chosatha kumwamba
Lu 14:33 akulephera kusiya chuma chake
Lu 16:9 Pezani anzanu ndi chuma chosalungama
2Ak 4:7 tili ndi chuma mʼziwiya zadothi
1Ti 6:17 achuma asakhale odzikweza
Ahe 10:34 chuma chabwino kwambiri
D
DALA
, Ahe 10:26 Ngati tikuchita machimo mwadala
DALAKIMA
, Lu 15:8 zokwana madalakima 10
DALIRA
, Sl 56:11 ndimadalira Mulungu; Sindikuopa
2Ak 1:9 tisamadzidalire, tizidalira Mulungu
Sl 62:8 Muzimudalira nthawi zonse
Miy 3:5 usamadalire luso lako
Miy 3:26 uzidzadalira kwambiri Yehova
Miy 28:26 wodalira mtima wake ndi wopusa
Aro 9:11 cholinga chidzadalira amene amaitana
1Pe 4:11 modalira mphamvu ya Mulungu
DALIRIKA
, Sl 33:4 chimene amachita ndi chodalirika
DALITSA
, Ge 1:28 Mulungu anawadalitsa
Ge 32:26 Sindikusiya mpaka utandidalitsa
Nu 6:24 Yehova akudalitseni
Owe 5:24 Mkazi wodalitsika kwambiri ndi Yaeli
Lu 6:28 kudalitsa amene akukutembererani
Yoh 12:13 Wodalitsidwa ndi amene akubwera
Aro 12:14 Pitirizani kudalitsa anthu
DALITSO
, De 30:19 ndaika dalitso ndi temberero
Miy 10:22 Madalitso a Yehova amalemeretsa
Mki 3:10 ngati sindikukhuthulirani madalitso
DAMA
. Onani CHIWEREWERE.
DANA
, Le 19:17 Usamadane ndi mʼbale wako
Sl 45:7 unkadana ndi zoipa
Sl 97:10 okonda Yehova, muzidana ndi zoipa
Miy 6:16 zinthu 6 zimene Yehova amadana nazo
Miy 8:13 kumatanthauza kudana ndi zoipa
Amo 5:15 Muzidana ndi choipa
Mt 24:9 adzadana nanu
Lu 6:27 amene akudana nanu
Yoh 7:7 Dziko limadana ndi ine
Yoh 15:25 Anadana nane popanda chifukwa
1Yo 3:15 amadana ndi mʼbale wake
DANDAULA
, Akl 3:13 chodandaulira za mnzake
Yuda 16 amakonda kungʼungʼudza, kudandaula
DANDAULIRA
, Aro 12:1 ndikukudandaulirani
DANDAULO
, Aro 8:26 madandaulo amene sitingawafotokoze
DAVIDE
, 1Sa 16:13 Samueli anadzoza Davide
Lu 1:32 mpando wachifumu wa Davide
Mac 2:34 Davide sanapite kumwamba
DAZI
, Le 13:40 Mwamuna akayamba dazi
2Mf 2:23 Choka kuno wadazi iwe!
DEKHA
, Miy 17:27 wozindikira amakhala wodekha
2Ti 2:24 ayenera kukhala wodekha
1Pe 3:4 atavala mtima wodekha
DERA
, Aro 15:23 sindinafikeko mʼmadera amenewa
DETSA
, Eze 39:7 Sindidzalolanso kuti lidetsedwe
DIKIRA
, 1Ak 7:5 ngati mwagwirizana kudikira
DINA
, Ge 34:1 Dina ankakonda kukacheza
DINARI
, Lu 7:41 ngongole ya madinari 500
DIPO
, Sl 49:7 kumuperekera dipo kwa Mulungu
Mt 20:28 kudzapereka moyo wake dipo
Aro 8:23 kutimasula ndi dipo
DISO
, Mt 5:38 Diso kulipira diso
Mt 6:22 diso likuyangʼana chimodzi
1Ak 12:21 Diso silingauze dzanja
1Ak 15:52 mʼkuphethira kwa diso
DOKOTALA
, Lu 5:31 abwino safunikira dokotala
DONGO
, Yes 45:9 Kodi dongo lingafunse woumba?
Yes 64:8 ndife dongo, inu ndinu Wotiumba
Da 2:42 chitsulo chosakanikirana ndi dongo
DONGOSOLO
, 1Ak 14:40 moyenera ndi mwadongosolo
Aef 1:10 akakhazikitse dongosolo
1Ti 3:2 wochita zinthu mwadongosolo
DORIKA
, Mac 9:36 wophunzira dzina lake Dorika
DOTHI
, Ge 2:7 anamuumba kuchokera kudothi
DWALA
, Sl 41:3 pamene akudwala pabedi lake
Yes 33:24 adzanene kuti: Ine ndikudwala
Yak 5:14 pali akudwala pakati panu?
DYERA
, Lu 12:15 chenjerani ndi dyera
1Ak 5:11 musiye kugwirizana ndi wadyera
1Ak 6:10 adyera sadzalowa mu Ufumu
Akl 3:5 dyera ndi kulambira mafano
DYERA MASUKU PAMUTU
, 2Ak 7:2 sitinadyere masuku pamutu
DYETSA
, Yoh 21:17 Yesu anati: Dyetsa ana a nkhosa
DZALA
, Mla 11:6 Dzala mbewu zako
Yes 65:22 sadzadzala kuti ena adye
1Ak 3:6 ndinadzala, Apolo anathirira
DZANJA
, Sl 145:16 Mumatambasula dzanja lanu
Yes 41:10 Ndikugwira mwamphamvu ndi dzanja
Zek 14:13 adzagwira dzanja la mnzake
Mt 6:3 dzanja lako lamanzere
Yoh 12:38 dzanja la Yehova laonetsedwa
DZANZI
, Sl 143:4 mtima wanga wachita dzanzi
DZAZA
, Ge 1:28 mudzaze dziko lapansi
DZENJE
, Miy 26:27 Amene akukumba dzenje
Da 6:7 mʼdzenje la mikango
Mt 15:14 onse awiri adzagwera mʼdzenje
DZIDZIMUTSA
, Lu 21:34 lingadzakufikireni modzidzimutsa
DZIKO
, Ge 1:28 mudzaze dziko lapansi
Eks 9:29 dziko lapansi ndi la Yehova
Yob 38:4 maziko a dziko lapansi
Sl 37:11 adzalandira dziko lapansi
Sl 37:29 adzalandira dziko lapansi
Sl 104:5 dziko silidzasunthidwa
Sl 115:16 dziko analipereka kwa anthu
Miy 2:21 owongoka mtima adzakhala padziko
Yes 45:18 anaumba dziko lapansi
Yes 66:8 dziko lingabadwe tsiku limodzi?
Mt 5:5 ofatsa adzalandira dziko
Lu 9:25 zonse zamʼdzikoli
Yoh 15:19 simuli mbali ya dziko
Yoh 17:16 Iwo sali mbali ya dziko
1Ak 2:14 wokonda zinthu zamʼdziko
1Ak 3:3 mukuganiza ngati anthu amʼdzikoli
1Yo 2:15 Musamakonde dziko
1Yo 2:17 dzikoli likupita
DZINA
, Ge 11:4 tidzipangire dzina kuti titchuke
Eks 3:13 nʼkundifunsa kuti, Dzina lake ndani?
Eks 3:15 Dzina langa ndi limeneli
Eks 9:16 dzina langa lilengezedwe
Eks 20:7 wogwiritsa ntchito dzina molakwika
1Sa 17:45 ndikubwera mʼdzina la Yehova
1Mb 29:13 kutamanda dzina lanu lokongola
Sl 9:10 odziwa dzina adzakukhulupirirani
Sl 79:9 Chifukwa cha dzina lanu
Miy 18:10 Dzina la Yehova ndi nsanja yolimba
Miy 22:1 Ndi bwino kusankha dzina labwino
Yer 23:27 anthu anga aiwale dzina langa
Eze 39:25 ndidzateteza dzina langa loyera
Mki 1:11 dzina langa lidzakwezeka
Mki 3:16 amene ankaganizira za dzina lake
Mt 6:9 dzina lanu liyeretsedwe
Yoh 12:28 Atate lemekezani dzina lanu
Yoh 14:14 Ngati mutapempha mʼdzina langa
Yoh 17:26 ndachititsa kuti adziwe dzina lanu
Mac 4:12 palibe dzina lina padziko lapansi
Mac 15:14 anthu odziwika ndi dzina lake
Aro 10:13 woitana pa dzina la Yehova
Afi 2:9 anamupatsa dzina loposa lililonse
DZIWA
, Miy 14:15 amene sadziwa zambiri
Mla 7:14 asamadziwe chilichonse
Yes 11:9 lidzadzaza ndi odziwa Yehova
Yer 31:34 Mumʼdziwe Yehova, adzandidziwa
Ho 4:6 Popeza akana kundidziwa
1Ak 9:26 osadziwa kumene ndikupita
2Ak 2:11 tikudziwa bwino ziwembu zake
1Ti 1:13 ndinkachita zinthu mosadziwa
DZIWA MOLONDOLA
, Aro 10:2 koma sakumudziwa molondola
Akl 3:10 mukudziwa Mulungu molondola
1Ti 2:4 adziwe choonadi molondola
DZIWIDWA
, Aga 4:9 mwadziwidwa ndi Mulungu
DZIWIKA
, 2Ak 6:9 ngati osadziwika koma odziwika
DZOZA
, 1Sa 16:13 Samueli anadzoza Davide
Sl 2:2 Mafumu akulimbana ndi wodzozedwa
Sl 105:15 Musakhudze odzozedwa anga
Yes 61:1 Yehova anandidzoza kuti ndilengeze
DZUDZULA
, Sl 141:5 Akandidzudzula wandidzoza mafuta
Miy 3:11 usanyansidwe ndi kudzudzula
Miy 27:5 Kudzudzula mosabisa mawu
Miy 29:1 amaumitsa khosi podzudzulidwa
Mla 7:5 kumvetsera wanzeru akamakudzudzula
1Ti 5:1 Usadzudzule mokalipa wachikulire
DZUTSA
, Yoh 11:11 ndikupita kukamudzutsa
DZUWA
, Yos 10:12 Dzuwa, ima pamwamba
Mt 24:29 dzuwa lidzachita mdima
Mac 2:20 Dzuwa lidzasanduka mdima
E
EDENI
, Ge 2:8 anadzala munda ku Edeni
EFESO
, 1Ak 15:32 zilombo ku Efeso
ELI
, 1Sa 1:3 ana a Eli anali ansembe
ELIYA
, Yak 5:17 Eliya anali ngati ife tomwe
EODIYA
, Afi 4:2 Ndikudandaulira Eodiya
ESAU
, Ge 25:34 Esau ananyoza ukulu wake
Ahe 12:16 wosayamikira ngati Esau
EZARA
, Eza 7:11 Ezara wokopera Malemba
F
FAFANIZA
, Mac 3:19 machimo anu afafanizidwe
FANO
, Da 3:18 sitilambira fano lagolide
FATSA
, 1Ak 4:13 timayankha mofatsa
Akl 3:12 valani kufatsa komanso kuleza mtima
1Pe 3:4 mtima wodekha komanso wofatsa
FESA
, Sl 126:5 akukhetsa misozi pofesa
Aga 6:7 chimene munthu wafesa
FIIRA
, Yes 1:18 machimo anu ndi ofiira kwambiri
FILIPO
, Mac 8:26 mngelo analankhula kwa Filipo
Mac 21:8 mlaliki wina dzina lake Filipo
FOOKA
, Miy 24:10 Ukafooka pa nthawi ya mavuto
Aro 14:1 chikhulupiriro chofooka
Aro 15:1 chikhulupiriro chofooka
1Ak 1:27 anasankha zinthu zofooka
2Ak 12:10 ndimasangalala ndi kufooka
1At 3:3 chikhulupiriro chafooka
1At 5:14 muzithandiza ofooka
FOTOKOZA
, Ne 8:8 kuchifotokoza momveka bwino
Yoh 1:18 anafotokoza za Mulungu
Mac 17:3 ankafotokoza ndi kusonyeza umboni
FUFUZA
, De 13:14 muzifufuza mosamala
Sl 26:2 Ndifufuzeni, inu Yehova
Miy 21:2 Yehova amafufuza mitima
Miy 25:2 ulemerero wa mafumu ndi kufufuza nkhani
Lu 15:8 kusesa mʼnyumba nʼkuifufuza
1Ak 11:28 Munthu azidzifufuza kaye
1At 5:21 Muzifufuza zonse, nʼkugwira zabwino
1Pe 1:10 anafufuza za chipulumutso
1Yo 4:1 muzifufuza mawu ouziridwawo
FUKO
, Ge 49:28 mafuko 12 a Isiraeli
FULUMIRA
, Miy 29:20 ofulumira kulankhula
Yes 60:22 zichitike mofulumira
Yak 1:19 asamafulumire kukwiya
FUMBI
, Ge 3:19 ndiwe fumbi, udzabwerera
Sl 103:14 Amakumbukira kuti ndife fumbi
Yes 40:15 amawaona ngati fumbi pasikelo
FUNA
, De 10:12 akufuna muzichita chiyani?
1Mb 29:17 ndapereka mwakufuna kwanga
Yob 23:12 zimene amafuna kuti ndichite
Sl 40:8 kuchita zimene mumafuna
Sl 143:10 Ndiphunzitseni zimene mumafuna
Mik 6:8 Yehova akufuna uzichita chiyani?
Mt 6:10 Zofuna zanu zichitike padziko
Mt 7:21 zimene Atate wanga amafuna
Lu 22:42 osati zofuna zanga
Yoh 4:23 Atate akufuna anthu ngati amenewo
Yoh 6:38 osati zofuna zanga
Aro 7:18 Chifukwa ndimafuna kuchita zabwino
1Ak 12:18 anaika ziwalo mmene anafunira
1Ak 13:5 sichisamala zofuna zake zokha
Afi 2:4 muziganiziranso zofuna za ena
Afi 2:13 mtima wofuna kuchita zinthu
Afi 2:21 akungoganizira zofuna zawo
1At 4:3 Mulungu akufuna mukhale oyera
1Pe 5:7 chifukwa amakufunirani zabwino
1Yo 2:17 wochita zimene Mulungu amafuna
1Yo 5:14 mogwirizana ndi zimene amafuna
FUNAFUNA
, 1Mb 28:9 Ukamufunafuna, udzamupeza
Sl 119:176 Ndifunefuneni ine mtumiki wanu
Yes 55:6 Funafunani Yehova
Eze 34:11 ndidzafunafuna nkhosa zanga
Zef 2:3 Funafunani Yehova, inu ofatsa
Mac 17:27 anthuwo afunefune Mulungu
Akl 3:1 pitirizani kufunafuna zakumwamba
FUNIKA
, Aga 6:3 akudziona kuti ndi wofunika
FUNIKIRA
, Mt 6:32 mumafunikira zonsezi
FUNITSITSA
, Eks 35:5 mtima wofunitsitsa
Eks 35:21 wa mtima wofunitsitsa anabweretsa
Sl 51:12 mtima wofunitsitsa kukumverani
Sl 110:3 adzadzipereka mofunitsitsa
Aro 1:15 ndikufunitsitsa kudzalalikira
Afi 1:8 ndikufunitsitsa nditakuonani
1Pe 1:12 Angelo amafunitsitsa atamvetsa
FUPA
, Ge 2:23 uyu ndi fupa la mafupa anga
2Mf 13:21 Mtembowo utakhudza mafupa a Elisa
Sl 34:20 Amateteza mafupa a wolungama
Miy 25:15 mawu okoma akhoza kuthyola fupa
Yer 20:9 moto umene watsekeredwa mʼmafupa
Yoh 19:36 Sadzathyola fupa lake
G
GABIRIELI
, Lu 1:19 Gabirieli, pamaso pa Mulungu
GALASI
, 1Ak 13:12 galasi losaoneka bwino
Yak 1:23 kudziyangʼanira nkhope pagalasi
GALU
, Miy 26:17 wogwira makutu a galu
Mla 9:4 galu wamoyo ali bwino
2Pe 2:22 Galu wabwerera kumasanzi
GAMALIYELI
, Mac 22:3 kuphunzitsidwa ndi Gamaliyeli
GANIZA
, Yob 6:3 ndalankhula mosaganiza bwino
Miy 15:28 amaganiza asanayankhe
Aef 4:23 atsopano pa kaganizidwe kanu
GANIZIRA
, Sl 8:4 munthu ndani kuti muzimuganizira?
Sl 41:1 moganizira wonyozeka
Mt 24:44 pa ola limene simukuliganizira
Aro 8:6 kuganizira za thupi kumabweretsa imfa
Aro 12:3 musamadziganizire kuposa mmene
Aro 15:1 olimba aziganizira ofooka
Afi 3:19 amangoganizira zapadziko lapansi
Akl 3:2 Pitirizani kuganizira zinthu zakumwamba
GANIZIRA MOZAMA
, Sl 19:14 ndimaganizira mozama
Sl 77:12 Ndidzaganizira mozama za ntchito zanu
GAWANA
, Aro 12:13 Gawanani ndi oyera
GAWO
, Da 12:13 udzauka kuti ulandire gawo
GEHAZI
, 2Mf 5:20 Gehazi anati, ndimʼthamangira
GEHENA
, Mt 10:28 kuwononga zonse ziwiri mʼGehena
GETI
, Mt 7:13 Lowani pageti lalingʼono
GIBIYONI
, Yos 9:3 anthu a ku Gibiyoni anamva
GIDIYONI
, Owe 7:20 Yehova ndi Gidiyoni!
GOGODA
, Mt 7:7 Pitirizani kugogoda
GOLI
, 1Mf 12:14 anakusenzetsani goli lolemera
Mt 11:30 goli langa ndi losavuta kunyamula
2Ak 6:14 Musamangidwe mʼgoli ndi osakhulupirira
GOLIDE
, Eze 7:19 golide sadzawapulumutsa
Da 3:1 Nebukadinezara anapanga fano lagolide
GOLIYATI
, 1Sa 17:4 ngwazi dzina lake Goliyati
GOLOGOTA
, Yoh 19:17 ankatchulidwa kuti Gologota
GOMORA
, Ge 19:24 sulufule ndi moto ku Gomora
GONA
, Miy 6:10 Ukapitiriza kugona pangʼono
2Ak 6:5 kusagona tulo ndiponso kukhala osadya
2Ak 11:27 Nthawi zambiri usiku sindinkagona
1At 5:6 tisapitirize kugona ngati ena onse
Ahe 13:4 pogona pa okwatirana posadetsedwa
GONJERA
, Ahe 13:17 ndipo muziwagonjera
1Pe 2:13 pogonjera ulamuliro uliwonse
GONJETSA
, Yer 1:19 Koma sadzakugonjetsa
Yoh 16:33 limbani mtima. Ine ndaligonjetsa dziko
Aro 8:37 tikugonjetsa zinthu zonsezi
Aro 12:21 pitirizani kugonjetsa choipa
GULA
, 1Ak 7:23 Munagulidwa pa mtengo wokwera
Chv 5:9 ndi magazi anu munagula anthu
GULU
, Eks 23:2 Musamachite zoipa pongotsatira gulu
Ahe 12:1 tazunguliridwa ndi gulu lalikulu la mboni
1Pe 2:17 Muzikonda gulu lonse la abale
GULU LACHIWAWA
, Mac 17:5 gulu lachiwawa mumzinda
GULU LANKHONDO
, Zek 4:6 sipakufunika gulu lankhondo koma mzimu
GUWA LANSEMBE
, Ge 8:20 Nowa, guwa lansembe
Eks 27:1 Upange guwa lansembe lamatabwa
Mt 5:24 patsogolo pa guwa lansembe
Mac 17:23 guwa lansembe la Mulungu Wosadziwika
GWEDEZA
, Hag 2:7 Ndigwedeza mitundu yonse
GWETSA
, 2Ak 10:4 zimatha kugwetsa zinthu zozikika
GWIRA
, Afi 2:16 mugwire mawu amoyo
GWIRA NTCHITO
, Yoh 5:17 Atate akugwirabe ntchito
1At 2:9 Tinkagwira ntchito usiku ndi masana
GWIRITSA NTCHITO MOLAKWA
, 1Ak 9:18 ndisagwiritse ntchito molakwa ufulu
GWIRITSIRA
, Sl 90:12 tingagwiritsire ntchito moyo
1Ak 7:31 Amene amagwiritsira ntchito
GWIRIZANA
, Sl 133:1 akakhala mogwirizana
Zef 3:9 Nʼkumamutumikira mogwirizana
Mac 15:25 Choncho tonse tagwirizana
Aro 3:25 anthu agwirizanenso ndi Mulungu
1Ak 1:10 nonse muzilankhula mogwirizana
1Ak 5:9 musiye kugwirizana ndi achiwerewere
1Ak 7:5 pokhapokha ngati mwagwirizana
1Ak 15:33 Kugwirizana ndi anthu oipa
Aga 5:25 kuchita mogwirizana ndi mzimuwo
Aef 4:1 muzichita zinthu mogwirizana
Aef 4:13 mpaka tidzakhale ogwirizana
Afi 2:2 ndinu ogwirizana kwambiri
Akl 1:10 mukhale ndi khalidwe logwirizana
GWIRIZANITSA
, Aro 5:10 ngati tinagwirizanitsidwa
Aro 8:28 amagwirizanitsa zochita zake zonse
2Ak 5:19 Mulungu ankagwirizanitsa dziko ndi iyeyo
Aef 4:3 chomangira chotigwirizanitsa
Akl 3:14 chikondi chimagwirizanitsa
H
HANANIYA
, Mac 5:1 Hananiya ndi Safira
HATCHI
, Chv 6:2 hatchi yoyera
Chv 19:11 ndinaona hatchi yoyera
HEZEKIYA
, 2Mf 19:15 Hezekiya anapemphera
HULE
, Miy 7:10 Atavala ngati hule
Lu 15:30 anawononga chuma ndi mahule
1Ak 6:16 amene wagonana ndi hule
Chv 17:1 chiweruzo cha hule lalikulu
Chv 17:16 zidzadana ndi hulelo
I
IGUPUTO
, Mt 2:15 atuluke mu Iguputo
IKA
, Lu 22:37 anaikidwa mʼgulu la osamvera
IMA
, Yob 37:14 Imani ndi kuganizira mozama
1Ak 10:12 amene akuganiza waima bwinobwino
IMBA
, 1Mb 15:16 asankhe abale awo oimba
Sl 96:1 Imbirani Yehova
Mt 26:30 atamaliza kuimba nyimbo
Aef 5:19 Muziimba nyimbo zotamanda
IMFA
, Ru 1:17 kupatulapo imfa
Sl 89:48 Kodi pali amene sadzafa?
Yes 25:8 adzameza imfa kwamuyaya
Eze 18:32 sindisangalala ndi imfa
Ho 13:14 Imfa, mphamvu yako ili kuti?
Yoh 8:51 wosunga mawu, sadzaona imfa
Aro 5:12 imfayo inafalikira kwa onse
Aro 6:23 malipiro a uchimo ndi imfa
1Ak 15:26 Imfa, idzawonongedwa
1At 4:13 amene akugona mu imfa
Ahe 2:9 Yesu analawa imfa
Ahe 2:15 ukapolo chifukwa choopa imfa
Chv 21:4 imfa sidzakhalaponso
IMFA YACHIWIRI
, Chv 2:11 sadzakhudzidwa ndi imfa yachiwiri
Chv 20:6 Imfa yachiwiri ilibe ulamuliro
Chv 20:14 Nyanja yamoto ikuimira imfa yachiwiri
IMVI
, Miy 16:31 Imvi ndi chisoti cha ulemerero
IMWA
, Mt 20:22 Kodi mungamwe?
INDE
, Mt 5:37 mukati Inde akhaledi inde
INOKI
, Ge 5:24 Inoki anayenda ndi Mulungu
IPA
, Ge 3:5 Mudzadziwa zabwino ndi zoipa
Yes 5:20 akunena kuti chabwino nʼchoipa
Aro 7:19 koma zoipa zimene sindifuna kuchita
IPITSA
, 2Ak 7:1 tidziyeretse ku choipitsa thupi
ISAKI
, Ge 22:9 anamanga Isaki mwana wake
ISIRAELI
, Ge 35:10 dzina lako likhala Isiraeli
Sl 135:4 Wasankha Isiraeli kukhala chuma
Aga 6:16 Isiraeli wa Mulungu akhale ndi mtendere
ITANA
, Aro 10:13 woitana pa dzina la Yehova
Aef 4:1 muzichita zinthu mogwirizana ndi kuitana
IWALA
, De 4:23 musaiwale pangano
Sl 119:141 sindinaiwale malamulo anu
Yes 49:15 mayi angaiwale mwana?
Afi 3:13 Ndikuiwala zinthu zakumbuyo
Ahe 6:10 kuti angaiwale ntchito yanu
K
KACHISI
. Onaninso NYUMBA, Sl 11:4 Yehova ali mʼkachisi
Sl 27:4 ndiyangʼane kachisi wake
Yer 7:4 kachisi wa Yehova
Eze 41:13 anayeza kachisi nʼkupeza kuti
Mki 3:1 adzabwera kukachisi wake
Mt 21:12 analowa mʼkachisi nʼkuthamangitsa
Yoh 2:19 Gwetsani kachisiyu
Mac 17:24 sakhala mu akachisi opangidwa
1Ak 3:16 ndinu kachisi wa Mulungu
KAGULU KA NKHOSA
, Lu 12:32 Musaope, kagulu ka nkhosa
KAINI
, 1Yo 3:12 Kaini, anapha mʼbale wake
KAISARA
, Mt 22:17 kupereka msonkho kwa Kaisara
Mko 12:17 Perekani za Kaisara kwa Kaisara
Yoh 19:12 ndiye kuti si inu mnzake wa Kaisara
Yoh 19:15 Tilibe mfumu ina koma Kaisara
Mac 25:11 Ndikuchita apilo kwa Kaisara
KAKAMIZA
, Mac 26:11 kuwakakamiza kuti asiye
KALAMBA
, Sl 71:9 Musanditaye pamene ndakalamba
Sl 92:14 Ngakhale atakalamba zidzawayendera
KALATA
, De 24:1 kalata yothetsera ukwati
Mt 19:7 azipereka kalata yothetsera ukwati
KALEBE
, Nu 13:30 Kalebe anawakhazika mtima pansi
Nu 14:24 Kalebe anali wosiyana ndi ena
KALIPENTALA
, Mko 6:3 Kodi iyeyu si kalipentala?
KALONGA
, Sl 45:16 akhale akalonga padziko
Yes 9:6 Kalonga Wamtendere
Yes 32:1 akalonga adzalamuliranso
Da 10:13 kalonga wa ufumu wa Perisiya
KAMBIRANA
, Miy 15:22 ngati anthu sakambirana
Mac 17:2 anakambirana mfundo za mʼMalemba
KAMBUKU
, Yes 11:6 kambuku adzagona ndi mbuzi
Da 7:6 chilombo chooneka ngati kambuku
KAMWA
, De 25:4 Usamange ngʼombe pakamwa
Sl 8:2 ochokera mʼkamwa mwa ana
Ho 14:2 tidzakutamandani ndi pakamwa pathu
Aro 10:10 ndi pakamwa pake amalengeza
Yak 3:10 Pakamwa pomwepo, mawu otamanda
KANA
, Yer 8:9 Iwo akana mawu a Yehova
Yoh 2:1 ku Kana kunali ukwati
KANGANA
, Mac 15:39 anakangana koopsa
2Ti 2:24 Kapolo sakangana ndi anthu
KANIZA
, 1Ak 7:5 Musamakanizane
KANJERE KA MPIRU
, Lu 13:19 ngati kanjere ka mpiru
KANTHAWI
, Yes 26:20 Mukabisale kwa kanthawi
2Ak 4:17 mavuto ndi akanthawi
KAPHUNZITSIDWE
, Mt 7:28 ndi kaphunzitsidwe kake
KAPOLO
, Miy 22:7 kapolo wa wobwereketsa
Mt 24:45 kapolo wokhulupirika
Mt 25:21 ndiwe kapolo wabwino
Lu 17:10 Ife ndi akapolo opanda pake
Yoh 8:34 ndi kapolo wa tchimo
1Ak 7:23 siyani kukhala akapolo a anthu
KAPU
, Lu 22:20 Kapu ikuimira pangano latsopano
Lu 22:42 ndichotsereni kapu iyi
1Ak 11:25 chimodzimodzi ndi kapu
KASUPE
, Sl 36:9 Inu ndinu kasupe wa moyo
Yer 2:13 kasupe wa madzi amoyo
KATATU
, De 16:16 katatu pa chaka
KATUNDU
, Sl 38:4 zolakwa, katundu wolemera
Sl 68:19 Yehova amanyamula katundu wathu
Yes 60:5 Katundu wa anthu adzabwera
Lu 11:46 mumasenzetsa anthu katundu
Aga 6:5 kunyamula katundu wake
Ahe 10:34 katundu wanu akulandidwa
Chv 2:24 Sindikusenzetsani katundu wolemera
KAYIKA
, 1Mf 18:21 Kodi mukayikakayika mpaka liti?
Yak 1:8 ndi wokayikakayika, amasinthasintha
KAYIKIRA
, Mt 21:21 ngati simukukayikira
Aro 4:21 sankakayikira kuti ali ndi mphamvu
Aro 15:14 Abale anga, ine sindikukayikira
Akl 4:12 musamakayikire ngakhale pangʼono
Yak 1:6 azipempha, asamakayikire
Yuda 22 anthu amene amakayikira
KAZEMBE
, 2Ak 5:20 akazembe mʼmalo mwa Khristu
KEFA
, 1Ak 15:5 anaonekera kwa Kefa kenako atumwi
Aga 2:11 Kefa atabwera ku Antiokeya
KERUBI
, Ge 3:24 anamuthamangitsa nʼkuika akerubi
Eze 28:14 kuti ukhale kerubi wodzozedwa
KHALA
, Eks 3:14 Ndidzakhala Amene Ndidzafune Kukhala
Sl 110:1 Khala kudzanja langa lamanja
Yes 45:18 analiumba kuti anthu akhalemo
Lu 22:28 inu ndi amene mwakhalabe
Aro 8:15 munalandira mzimu wakuti mukhale ana
1Ak 9:22 Ndakhala zinthu zonse
Aga 6:16 lamulo la mmene tiyenera kukhalira
1Pe 2:12 Mukhale ndi khalidwe labwino
1Yo 2:17 adzakhala mpaka kalekale
KHALA CHETE
, Sl 4:4 ndipo mukhale chete
Sl 32:3 ndinakhala chete osaulula machimo
Mla 3:7 Nthawi yokhala chete
Yes 53:7 imene yangokhala chete
KHALANI MASO
, Mt 26:41 Khalani maso, mupitirize
Lu 21:36 Choncho khalani maso
1Ak 16:13 Khalani maso, khalani ndi chikhulupiriro
1Pe 4:7 khalani maso, muzipemphera
Chv 16:15 Wosangalala amene akukhalabe maso
KHALANI OLIMBA
, 1Ak 15:58 abale, khalani olimba
1Ak 16:13 khalani olimba mʼchikhulupiriro
KHALIDWE
, Miy 31:29 akazi amakhalidwe abwino
Aga 5:22 makhalidwe a mzimu woyera
1Pe 3:1 akopeke ndi khalidwe lanu
1Pe 3:16 chifukwa cha khalidwe lanu labwino
KHALIDWE LOPANDA MANYAZI
, Aga 5:19 chiwerewere, khalidwe lopanda manyazi
2Pe 2:7 ankavutika ndi khalidwe lopanda manyazi
Yuda 4 chochitira khalidwe lopanda manyazi
KHALIDWE LOYENERA
, Aro 13:13 tikhale ndi khalidwe loyenera
KHAMA
, Miy 10:4 wogwira mwakhama adzalemera
Miy 12:27 khama ndi chuma cha munthu
Miy 21:5 Mapulani a munthu wakhama
Mac 5:42 kuphunzitsa mwakhama
Aro 12:11 Khalani akhama osati aulesi
Ahe 6:11 kusonyeza khama lapoyamba
2Pe 1:5 yesetsani mwakhama
KHAMU LALIKULU
, Chv 7:9 khamu lalikulu la anthu
KHATE
, Nu 12:10 Miriamu anagwidwa ndi khate
Lu 5:12 munthu wakhate thupi lonse
KHOKA
, Mt 13:47 Ufumu uli ngati khoka
KHOLA
, Yoh 10:16 nkhosa zimene si zamʼkhola ili
KHOMA
, Da 5:5 kulemba pakhoma lapulasitala
Yow 2:7 Amakwera khoma ngati asilikali
KHOMEREZA
, De 6:7 muziwakhomereza mwa ana
KHOMO
, 1Ak 16:9 khomo la utumiki landitsegukira
Chv 3:20 Ndaima pakhomo, ndikugogoda
KHOTA
, Mla 1:15 chokhota sichingawongoledwe
KHOTI
, Mko 13:9 Anthu adzakutengerani kumakhoti
1Ak 6:6 azitengera mʼbale wake kukhoti
KHOTI LALIKULU LA AYUDA
, Mac 5:41 anachoka pa Khoti Lalikulu la Ayuda
KHRISTU
, Mt 16:16 Khristu, Mwana wa Mulungu
Lu 24:26 kuti Khristu amve zowawa
Yoh 17:3 Yesu Khristu, amene munamutuma
Mac 18:28 posonyeza kuti Yesu ndiyedi Khristu
1Ak 11:3 mutu wa Khristu ndi Mulungu
KHUDZA
, Miy 6:29 wokhudza mkaziyo adzalangidwa
Yes 52:11 musakhudze chodetsedwa
Mt 8:3 nʼkumukhudza ndipo anati: Ndikufuna
2Ak 6:17 Musakhudze chinthu chodetsedwa
KHULULUKA
, Ne 9:17 wokonzeka kukhululuka
Miy 17:9 amene amakhululuka zolakwa
Yes 55:7 adzamukhululukira ndi mtima wonse
KHULULUKIDWA
, Mt 26:28 machimo awo akhululukidwe
KHULULUKIRA
, Sl 25:11 Mundikhululukire tchimo
Sl 103:3 amakukhululukira zolakwa
Mt 6:14 Mukamakhululukira anthu
Mt 18:21 ndizimukhululukira kangati
Akl 3:13 Yehova anakukhululukirani
KHULUPIRIKA
, Eks 18:21 oopa Mulungu, okhulupirika
1Mb 29:17 mumakonda okhulupirika
Yob 27:5 sindidzasiya kukhala wokhulupirika
Sl 25:21 Kukhala wokhulupirika kunditeteze
Sl 26:11 ndidzachita mokhulupirika
Sl 101:2 ndi mtima wokhulupirika
Lu 16:10 wokhulupirika pa chachingʼono
Tit 2:10 akhale okhulupirika pa chilichonse
KHULUPIRIRA
, Sl 9:10 anthu adzakukhulupirirani
Sl 84:12 Wosangalala amakukhulupirirani
Miy 3:5 Uzikhulupirira Yehova ndi mtima wonse
Yer 17:5 wokhulupirira munthu
Yoh 3:16 womukhulupirira asawonongedwe
Yoh 20:29 Osangalala amakhulupirira
2At 2:12 chifukwa sanakhulupirire choonadi
KHUMUDWA
, Sl 119:165 Palibe chingawakhumudwitse
Aro 5:5 Chiyembekezo sichitikhumudwitsa
Aro 9:33 wokhulupirira sadzakhumudwa
Akl 3:21 asakhale okhumudwa
KHUMUDWITSA
, Sl 78:40 ndipo ankamukhumudwitsa
Lu 17:2 akhumudwitse mmodzi wa tiana
Aro 14:13 chimene chingakhumudwitse
1Ak 8:13 chikukhumudwitsa mʼbale wanga
1Ak 10:32 Muzipewa kukhumudwitsa Ayuda
Afi 1:10 osakhumudwitsa ena
KHUNGU
, Ge 19:11 anachititsa khungu amuna
Mt 15:14 Iwo ndi atsogoleri akhungu
2Ak 4:4 mulungu wa nthawi ino wachititsa khungu
KHUNYU
, Mt 4:24 akhunyu ndi akufa ziwalo
KHUTHULA
, Sl 62:8 Mukhuthulireni zamumtima
KHUTIRA
, Afi 4:11 ndaphunzira kukhala wokhutira
1Ti 6:8 tizikhala okhutira ndi zinthu zimenezi
2Ti 3:14 unakhulupirira pambuyo pokhutira
KISI
, Lu 22:48 ukupereka Mwana wa munthu ndi kisi?
KIYI
, Lu 11:52 munalanda kiyi yowathandiza
KOKA
, Yoh 6:44 pokhapokha Atate atamukoka
KOKOMEZA
, 1Ak 2:1 sindinkalankhula mokokomeza
KOLOLA
, Mla 11:4 woyangʼana mitambo sadzakolola
Ho 8:7 adzakolola mphepo yamkuntho
Mt 9:37 zinthu zambiri zofunika kukolola
2Ak 9:6 wodzala moumira adzakolola zochepa
Aga 6:7 adzakololanso chomwecho
Aga 6:9 tidzakolola tikapanda kutopa
KOMETSERA
, Tit 2:10 kuti azikometsera
KONDA
, Le 19:18 Uzikonda mnzako
De 6:5 Muzikonda Yehova ndi mtima wonse
Sl 1:2 amakonda chilamulo cha Yehova
Mt 10:37 amakonda kwambiri bambo kapena mayi
Mt 22:37 Muzikonda Yehova
Mko 10:21 Yesu anamukonda
Yoh 3:16 Mulungu anakonda dziko
Yoh 12:25 amene amakonda moyo akuuwononga
Yoh 13:1 anawakonda mpaka pamapeto
Yoh 13:34 kuti muzikondana
Yoh 14:15 Ngati mumandikonda, mudzasunga
Yoh 21:17 Simoni, kodi umandikonda kwambiri?
Aro 13:8 ngongole, kupatulapo kukondana
2Ak 2:8 mumutsimikizire kuti mumamukonda
Aga 2:20 Mwana wa Mulungu anandikonda
Aef 5:29 amalidyetsa ndi kulikonda
Akl 3:19 pitirizani kukonda akazi anu
1Ti 6:4 amakonda kukangana ndi kutsutsana
1Yo 2:15 Musamakonde dziko kapena
1Yo 3:18 tisamakondane ndi mawu okha
1Yo 4:10 anatikonda, osati ifeyo tinamukonda
1Yo 4:20 wosakonda mʼbale, sangakonde Mulungu
1Yo 5:3 Kukonda Mulungu kumatanthauza
Yuda 21 Mulungu azikukondani
Chv 3:19 amene ndimawakonda, ndimawadzudzula
KONDA ABALE
, Aro 12:10 Pokonda abale, chikondi
KONDEDWA
, Mt 3:17 Mwana wanga wokondedwa
KONDERA
, De 10:17 amene sakondera munthu
KONDWA
, Sl 100:2 Tumikirani Yehova mokondwera
Aro 12:12 Kondwerani chifukwa cha chiyembekezo
KONDWERETSA
, Aro 15:1 kumangodzikondweretsa
Aro 15:2 aziyesetsa kukondweretsa mnzake
Aro 15:3 sankachita zinthu zodzikondweretsa
1Ak 7:33 angakondweretsere mkazi wake
KONELIYO
, Mac 10:24 Koneliyo anasonkhanitsa
KONGOLA
, Miy 6:25 Usasirire kukongola kwake
Miy 19:11 kumamʼchititsa kukhala wokongola
Miy 31:30 kukongola sikungachedwe kutha
Eze 28:17 unadzikweza chifukwa cha kukongola
KONGOZA
, Miy 19:17 akukongoza Yehova
Lu 6:35 kukongoza popanda chiwongoladzanja
KONZA
, Yoh 14:2 ndikupita kukakukonzerani malo
KONZEKA
, Mt 24:44 khalani okonzeka
1Pe 3:15 okonzeka kuyankha aliyense
KONZEKERA
, Aro 13:14 musamakonzekere kuchita
Aef 6:15 pokonzekera kulengeza uthenga
KOPA
, Aro 16:18 amagwiritsa ntchito mawu okopa
1Ak 2:4 mawu anga sanali okopa
2Ak 5:11 tikupitiriza kukopa anthu
KOPERA
, De 17:18 ayenera kukopera Chilamulo
KORA
, Nu 26:11 ana a Kora sanafe
Yuda 11 polankhula moukira ngati Kora
KORESI
, Eza 6:3 Koresi anaika lamulo
Yes 45:1 wodzozedwa wake Koresi, wamugwira
KOTULUKIRA DZUWA
, Yes 41:2 kuchokera kotulukira dzuwa
KUBA
, Eks 20:15 Musabe
Le 19:13 Musamabere anzanu
Miy 30:9 Ndiponso ndisasauke nʼkukaba
Aef 4:28 wakuba asiye kubako
KUBEREDWA
, 1Ak 6:7 Bwanji osalola kuberedwa?
KUBEREKA ZIPATSO
, 2Pe 1:8 zidzakuthandizani kubereka zipatso
KUCHITA ZOYENERA
, Yob 1:8 amachita zoyenera
KUDYA
, 1Ak 5:11 ngakhale kudya naye, ayi
KUDZICHEPETSA
, De 8:2 akuphunzitseni kudzichepetsa
Miy 15:33 umabwera ndi kudzichepetsa
Zek 9:9 Ndi yodzichepetsa, inakwera bulu
Mt 18:4 amene adzadzichepetse ngati mwana
Yak 4:6 odzichepetsa amawakomera mtima
Yak 4:10 Dzichepetseni pamaso pa Yehova
1Pe 5:6 dzichepetseni pamaso pa Mulungu
KUDZIKANA
, Mt 16:24 adzikane yekha
KUDZIKONGOLETSA
, 1Pe 3:3 Kudzikongoletsa kusakhale kwa kunja
KUDZIKUZA
, De 17:12 amene adzachite zinthu modzikuza
1Sa 15:23 kuchita zinthu modzikuza
Sl 19:13 mundiletse kuchita zinthu modzikuza
Aro 12:16 Musamaganize modzikuza
KUDZIKWEZA
, Miy 11:2 Kudzikweza kukafika
KUDZILETSA
, 1Ak 7:5 mukalephera kudziletsa
Aga 5:22, 23 chikhulupiriro, kufatsa ndi kudziletsa
KUDZIONETSERA
, 1Yo 2:16 kudzionetsera ndi zimene ali nazo
KUDZIPATULA
, Miy 18:1 aliyense wodzipatula
KUDZIPEREKA
, Eks 34:14 azidzipereka kwa iye yekha
Eks 36:2 amene anadzipereka mofunitsitsa
Sl 69:9 Kudzipereka panyumba yanu
Nym 8:6 kudzipereka ndi mtima wonse
2Ak 12:15 ndidzadzipereka ndi mtima wonse
KUDZIPEREKA KWA MULUNGU
, 1Ti 4:7 ukhalebe wodzipereka kwa Mulungu
1Ti 4:8 kudzipereka kwa Mulungu nʼkothandiza
1Ti 6:6 kukhala wodzipereka kwa Mulungu
2Ti 3:12 moyo wodzipereka kwa Mulungu
KUDZIWA ZINTHU
, Miy 1:7 chiyambi cha kudziwa zinthu
Miy 2:10 kudziwa zinthu kukakhala kosangalatsa
Miy 24:5 wodziwa zinthu amawonjezera mphamvu
Yes 5:13 ku ukapolo chifukwa chosadziwa zinthu
Da 12:4 adzadziwa zinthu zambiri zoona
Lu 11:52 kiyi yowathandiza kudziwa zinthu
1Ak 8:1 Kudziwa zinthu kumachititsa kudzikuza
KUDZIYESA
, 2Ak 13:5 Pitirizani kudziyesa
KUFA
, Ge 3:4 simudzafa ayi
Yob 14:14 Munthu akafa, angakhalenso ndi moyo?
Yoh 11:26 amene amandikhulupirira sadzafa
Aro 14:8 tikafa, timafera Yehova
2Ak 5:15 wosangalatsa amene anawafera
KUFANANA
, 2Ak 8:14 kuti pakhale kufanana
Afi 2:6 akhale wofanana ndi Mulungu
KUFA ZIWALO
, Lu 5:24 anauza wakufa ziwalo
KUGANIZA BWINO
, Miy 1:4 wachinyamata aziganiza bwino
KUGANIZIRA MOZAMA
, Yos 1:8 Uziliwerenga ndi kuganizira mozama
Sl 1:2 amawerenga ndi kuganizira mozama
KUGAWANIKA
, 1Ak 1:10 pasakhale kugawanika
KUGAWANITSA
, Mt 10:35 Ndinabwera kudzagawanitsa
Aro 16:17 musamale ndi ogawanitsa
KUGWA
, Miy 24:16 wolungama angagwe maulendo 7
Mla 4:10 ngati mmodzi atagwa
1Ak 10:12 asamale kuti asagwe
KUGWA ULESI
, 2Mb 15:7 musagwe ulesi
KUGWIRA NJAKATA
, Afi 1:23 Ndagwira njakata ndisankhe chiti
KUGWIRA NTCHITO
, Aro 12:4 ziwalo sizigwira ntchito yofanana
Aef 4:16 chikamagwira ntchito yake
KUIPA
, 2At 2:7 kuipa kwayamba kugwira ntchito
KUKANA
, Miy 30:9 ndisakhute nʼkukukanani
Mko 14:30 undikana katatu
Tit 1:16 amamukana ndi zochita
KUKHALAPO
, Mt 24:3 chizindikiro cha kukhalapo kwanu
Mt 24:37 kukhalapo kwa Mwana wa munthu
2Pe 3:4 kukhalapo kolonjezedwa kuli kuti?
KUKHALA WATSOPANO
, Aro 12:2 khalani watsopano posintha maganizo
KUKHAZIKITSA MWALAMULO
, Afi 1:7 kukhazikitsa mwalamulo uthenga wabwino
KUKHULUPIRIKA
, Mik 6:8 uzichita chilungamo, uzikukhulupirika
Hab 2:4 chifukwa cha kukhulupirika
1Ak 4:2 chofunika kwa atumiki ndi kukhulupirika
1Ak 10:13 Mulungu ndi wokhulupirika
Chv 2:10 Sonyeza kukhulupirika mpaka imfa
KUKHULUPIRIRA MIZIMU
, Aga 5:20 kulambira mafano, kukhulupirira mizimu
KUKOMA MTIMA
, Miy 11:17 wokoma mtima zimamuyendera
Miy 31:26 lamulo la kukoma mtima lili palilime
Mt 16:22 Dzikomereni mtima Ambuye
Mac 28:2 Anthu anatisonyeza kukoma mtima
KUKOMA MTIMA KWAKUKULU
, Yoh 1:17 kukoma mtima kwakukulu mwa Yesu
1Ak 15:10 kukoma mtima kwakukulu kumene
2Ak 6:1 musalandire kukoma mtima kwakukulu
2Ak 12:9 Kukoma mtima kwakukulu nʼkokwanira
KUKONZEKA
, 2Ti 3:17 wokonzeka mokwanira
KULA
, Sl 37:25 Ndinali mwana, tsopano ndakula
KULAKALAKA
, Eks 20:17 Musalakelake mkazi wa mnzanu
Sl 37:4 zimene mtima umalakalaka
Sl 84:2 Moyo wanga ukulakalaka
Sl 145:16 zolakalaka za chamoyo chilichonse
Aga 5:16 simudzachita zimene thupi likulakalaka
1Pe 2:11 muzipewa kulakalaka zoipa
KULAKWIRIDWA
, 1Ak 6:7 Bwanji osangolola kulakwiridwa?
KULAMBIRA MAFANO
, 1Ak 10:14 pewani kulambira mafano
KULA MWAUZIMU
, Ahe 5:14 anthu aakulu mwauzimu
Ahe 6:1 tikhale aakulu mwauzimu
KULEDZERA
, Aef 5:18 musamaledzere
KULEMEKEZA
, Afi 2:29 muziwalemekeza kwambiri
KULENGEZA
, Aro 10:10 amalengeza za chipulumutso
Ahe 10:23 kulengeza chiyembekezo
KULIMBANA
, Aef 6:12 tikulimbana ndi ziwanda
KULIMBITSA
, Afi 2:13 Mulungu amakulimbitsani
KULIRA
, Mt 26:75 kulira mopwetekedwa mtima
KULIRA MOSAMVEKA
, 1Ak 14:8 silikulira momveka
KUMBUKIRA
, Yob 14:13 mukanandibisa, nʼkudzandikumbukira
Mla 12:1 kumbukira Mlengi wako
Yes 65:17 zakale sizidzakumbukiridwanso
Lu 22:19 Muzichita zimenezi pondikumbukira
Ahe 10:32 pitirizani kukumbukira masiku akale
KUMBUTSA
, 1Ak 4:17 adzakukumbutsani mmene ndimachitira
2Pe 1:12 ndizikukumbutsani zinthu zimenezi
KUMBUYO
, Lu 9:62 nʼkumayangʼana zakumbuyo
KUMVA
, Aro 10:14 angamve popanda wolalikira?
KUMVETSA
, Aro 2:20 mumamvetsa choonadi
Ahe 5:11 mumachedwa kumvetsa zinthu
KUMWAMBA
, Sl 8:3 Ndikayangʼana kumwamba
Sl 19:1 zakumwamba zikulengeza ulemerero
Yoh 3:13 palibe anakwera kumwamba
2Ak 12:2 nʼkupita naye kumwamba kwachitatu
2Pe 3:13 kumwamba ndi dziko latsopano
KUNJA
, 1Ak 5:13 amaweruza amene ali kunja?
Akl 4:5 kuchita mwanzeru ndi anthu akunja
KUNKHA
, Le 19:9 musamachite khunkha mʼmunda
Ru 2:8 usapitenso kwina kukakunkha
KUNYALANYAZA
, 1At 4:8 sakunyalanyaza munthu
KUOMBEZA
, Nu 23:23 kuombeza maula
De 18:10 pasapezeke aliyense woombeza
KUONA
, 1Ak 2:9 amene anaonapo kapena kumva
Akl 3:22 pokhapokha akukuonani
KUONETSEDWA
, 1Ak 4:9 tikuonetsedwa kudziko
KUOPA
, Ge 9:2 zamoyo zidzapitiriza kukuopani
KUOPA YEHOVA
, Sl 19:9 Kuopa Yehova nʼkoyera
Sl 111:10 Chiyambi cha nzeru nʼkuopa Yehova
Miy 8:13 Kuopa Yehova kumatanthauza
KUPAMBANA
, 2Ak 2:14 chionetsero chonyadira kupambana
KUPANDA CHILUNGAMO
, De 32:4 sachita zopanda chilungamo
KUPANIKIZIKA
, Yes 38:14 Yehova, ine ndapanikizika
KUPATSA
, Lu 16:11 ndani angakupatseni ntchito
Mac 20:35 Kupatsa kumatichititsa kusangalala
KUPEREKA
, 1Ak 7:3 Mwamuna azipereka
1Pe 4:19 apereke moyo kwa Mlengi
KUPHA
, Yes 53:7 kumalo oti akamuphere
Yoh 16:2 amene adzakupheni adzaganiza
KUPHA MUNTHU
, Eks 20:13 Musaphe munthu
KUPHUNZITSA
, Yes 48:17 ndimakuphunzitsani kuti zikuyendereni
1Pe 5:10 adzamalizitsa kukuphunzitsani
KUPIRIRA
, Mt 24:13 amene adzapirire adzapulumuka
Lu 8:15 nʼkubereka zipatso mopirira
Lu 21:19 mukadzapirira, mudzapeza moyo
Aro 5:3 mavuto amachititsa kupirira
Aro 12:12 Muzipirira mavuto
1Ak 4:12 timapirira moleza mtima
Yak 1:4 kupirira kumalize ntchito yake
Yak 5:11 munamva za kupirira kwa Yobu
1Pe 2:20 mukamapirira chifukwa chochita zabwino
KUPITA PACHABE
, 1Ak 15:58 sizidzapita pachabe
KUPOSA
, Afi 2:3 muziona kuti ena amakuposani
1At 4:1 kuposa mmene mukuchitira
1At 4:10 kuposa mmene mukuchitira
KUPSA MTIMA
, Sl 37:8 Usapse mtima
Miy 19:19 wosachedwa kupsa mtima azilipira
Akl 3:19 musamawapsere mtima kwambiri
KUPSETSA MTIMA
, Aef 6:4 musamapsetse mtima ana anu
KUSAGANIZA
, Miy 12:18 amalankhula asanaganize
KUSALA
, Yes 58:6 kusala kudya kumene ndimafuna
Lu 18:12 ndimasala kudya kawiri pa mlungu
KUSALOWERERA ZA ENA
, 1At 4:11 Musamalowerere nkhani za ena
KUSAMVERA MALAMULO
, Mt 7:23 Chokani, osamvera malamulo inu
Mt 24:12 kuwonjezeka kwa kusamvera malamulo
Lu 22:37 mʼgulu la anthu osamvera malamulo
KUSAONEKA
, Aro 1:20 makhalidwe osaoneka
Ahe 11:27 ngati akuona Wosaonekayo
KUSINTHA MAONEKEDWE
, Mt 17:2 anaona kuti wasintha maonekedwe
KUSINTHA ZINTHU
, Miy 24:21 ofuna kusintha zinthu
Mko 10:11 wasiya mkazi wake nʼkukwatira
KUSIYANITSA
, Le 11:47 muzisiyanitsa chodetsedwa
Mki 3:18 kusiyana pakati pa wolungama
Ahe 5:14 kusiyanitsa zoyenera
KUTALI
, Mac 17:27 sali kutali ndi aliyense wa ife
KUTAMANDIDWA
, 1Mb 16:25 Yehova ndi woyenera kutamandidwa
KUTENGERANA KUKHOTI
, 1Ak 6:7 ngati mukutengerana kukhoti
KUTETEZA
, Afi 1:7 poteteza uthenga wabwino
KUTHA
, 2Ak 4:16 munthu wathu wakunja akutha
KUTHETSA BANJA
, Mki 2:16 ndimadana ndi zothetsa mabanja
KUTOPA
, Miy 25:25 kwa munthu wotopa
Yes 40:28 Iye satopa kapena kufooka
Yes 40:29 amapereka mphamvu kwa wotopa
Yes 40:31 Adzayenda koma osatopa
Yes 50:4 munthu amene watopa
Aga 6:9 tidzakolola tikapanda kutopa
Ahe 12:3 musatope nʼkutaya mtima
KUUGWIRA MTIMA
, 2Ti 2:24 wougwira mtima ena akamulakwira
KUUMA MTIMA
, Mko 3:5 chisoni chifukwa cha kuuma mtima
KUUMITSA
, De 15:7 kumuumitsira dzanja
KUVALA
, Miy 7:10 Atavala ngati hule
KUVUTIKA MAGANIZO
, Afi 2:26 [Epafurodito] akuvutika maganizo
KUWALA
, Sl 36:9 kuwala kochokera kwa inu
Sl 119:105 kuwala kounikira njira yanga
Miy 4:18 njira ya olungama ili ngati kuwala
Yes 42:6 ngati kuwala ku mitundu ya anthu
Mt 5:14 ndinu kuwala kwa dziko
Mt 5:16 muzionetsa kuwala kwanu
Yoh 8:12 ndine kuwala kwa dziko
2Ak 4:6 Kuwale kuchokera mumdima
KUWAWA
, Aro 8:22 kumva kuwawa mpaka pano
KUWODZERA
, Miy 23:21 kuwodzera kudzamuveka nsanza
KUWONGOLERA
, Yer 10:23 ulamuliro wowongolera mapazi
KUYANDIKIRA
, Yak 4:8 Yandikirani Mulungu
KUYESA
, De 13:3 Yehova akukuyesani kuti adziwe
KUYESEDWA
, Mt 6:13 kuti tisagonje tikamayesedwa
KUZAMA
, Aro 11:33 Nzeru zake nʼzozama
Aef 3:18 kumvetsa kuzama kwa choonadi
KWANIRITSA
, Yes 55:11 kukwaniritsa cholinga
Mt 5:17 ndinabwera kudzazikwaniritsa
KWANITSA
, Yob 42:2 palibe chimene simungakwanitse
KWAPULA
, Miy 13:24 amene sakwapula mwana wake
KWATIRA
, Mt 19:12 sakwatira, anabadwa choncho
Mt 22:30 akadzaukitsidwa sadzakwatira
Mt 24:38 Chigumula chisanafike ankakwatira
1Ak 7:8 osakwatira ndi akazi amasiye
1Ak 7:9 ndi bwino kukwatira kusiyana nʼkuvutika
1Ak 7:32 wosakwatira amadera nkhawa
1Ak 7:36 akwatire. Sakuchimwa
KWATIWA
, 1Ak 7:39 akwatiwe mwa Ambuye
KWERA
, Yoh 3:13 palibe anakwera kumwamba
KWEZA
, Ge 15:5 Kweza maso ako kumwamba
KWIYA
, Sl 103:8 Yehova ndi wosakwiya msanga
Miy 14:17 amene amakwiya msanga amachita
1Ak 13:5 sichikwiya, sichisunga zifukwa
Aef 4:26 Dzuwa lisalowe mudakali okwiya
Akl 3:8 Mutaye mkwiyo, mawu achipongwe
L
LAKALAKA
, Yob 14:15 Mudzalakalaka ntchito
Sl 84:2 ukulakalaka mabwalo a Yehova
Yes 26:9 ndimakulakalakani ndi mtima wonse
1Pe 1:14 siyani kutsatira zimene munkalakalaka
1Pe 2:2 muzilakalaka mkaka umene uli mʼMawu
LAKWITSA
, Yob 6:24 ndimvetse zimene ndalakwitsa
LALATA
, Aef 4:31 kupsa mtima, mkwiyo, kulalata
LALIKIDWA
, Mt 24:14 udzalalikidwa padziko lonse
LALIKIRA
, Mt 9:35 kulalikira uthenga wabwino
Aro 10:14 popanda wina kulalikira?
Akl 1:23 uthenga wabwino unalalikidwa padziko
2Ti 4:2 Lalikira mawu modzipereka
2Pe 2:5 ankalalikira za chilungamo
LALINGʼONO
, Mt 7:13 Lowani pageti lalingʼono
LAMBA
, Yes 11:5 Chilungamo chidzakhala lamba
LAMBIRA
, Mt 4:10 Yehova uyenera kumulambira
Yoh 4:24 akuyenera kumulambira
LAMULA
, Mac 5:28 Tinakulamulani mwamphamvu
LAMULIRA
, Ge 3:16 mwamuna azidzakulamulira
Sl 119:133 Musalole choipa chindilamulire
Miy 10:19 amalamulira milomo yake
Miy 16:32 amene amalamulira mkwiyo wake
Miy 29:2 woipa akamalamulira, anthu amabuula
Mla 8:9 wapweteka mnzake pomulamulira
Yes 9:7 Ulamuliro wake udzafika kutali
Da 4:17 Wamʼmwambamwamba ndi Wolamulira
Da 4:34 ulamuliro wake udzakhalapo
Mt 28:18 Ulamuliro wonse waperekedwa kwa ine
Lu 4:6 Ndikupatsani ulamuliro pa maufumu
Yoh 12:31 wolamulira wa dzikoli aponyedwa kunja
Yoh 12:42 olamulira anamukhulupirira
Yoh 14:30 wolamulira wa dziko akubwera
Mac 4:26 olamulira, alimbane ndi Yehova
Aro 6:12 uchimo uzilamulirabe ngati mfumu
Aro 13:1 azimvera olamulira akuluakulu
1Ak 6:12 kuti chinthu china chizindilamulira
1At 4:4 azidziwa kulamulira thupi lake
Tit 3:1 kumvera maboma ndi olamulira
Chv 11:15 adzalamulira monga mfumu
LAMULO
, Hab 1:4 lamulo latha mphamvu
Mt 22:40 Chilamulo chagona pa malamulo awiri
Mko 12:28 Kodi lamulo loyamba ndi liti?
Mko 12:31 Palibe lamulo lalikulu kuposa
Yoh 13:34 lamulo latsopano, muzikondana
Aro 13:8 wokonda mnzake wakwaniritsa lamulo
2Ti 2:5 kupikisana motsatira malamulo
Yak 2:8 mukutsatira lamulo lachifumu
LANDA
, Le 19:13 musamalande zinthu za aliyense
LANDIDWA
, Ahe 10:34 katundu wanu akulandidwa
LANDIRA
, Yob 2:10 tizingolandira zabwino?
Mt 5:5 ofatsa adzalandira dziko lapansi
Aro 14:1 Landirani munthu amene ali
Ahe 6:4 analandira mphatso yakumwamba
LANGA
, Miy 19:18 Langa mwana wako
Mla 8:11 ochita zoipa sanalangidwe mwamsanga
Chv 3:19 amene ndimawakonda ndimawalanga
LANGIZA
, De 8:5 Yehova wanu ankakulangizani
Owe 13:8 adzatilangize za mwana
Sl 32:8 kukulangiza njira yoyendamo
Sl 94:12 Wosangalala amene mumamulangiza
Aro 15:4 zinalembedwa kuti zitilangize
LANKHULA
, Eks 4:10 kulankhula kumandivuta
Miy 14:23 kungolankhula chabe kumasaukitsa
Yes 35:6 lilime la munthu wosalankhula
LAPA
, Lu 15:7 wochimwa amene walapa
Mac 3:19 lapani ndi kutembenuka
Mac 17:30 anthu kwina kulikonse alape
Mac 26:20 pochita zinthu zosonyeza kulapa
Aro 2:4 nʼcholinga choti ulape
2Ak 7:10 Kumva chisoni kumachititsa kulapa
Chv 16:11 Ananyoza Mulungu, ndipo sanalape
LATSOPANO
, Yoh 13:34 Ndikukupatsani lamulo latsopano
Chv 21:1 dziko lapansi latsopano
LAVULA
, Mt 26:67 anayamba kumulavulira kunkhope
LAWA
, Sl 34:8 Talawani, Yehova ndi wabwino
1Pe 2:3 ngati mutalawa nʼkuona kuti
LAZARO
, Lu 16:20 Lazaro wopemphapempha
Yoh 11:11 Mnzathu Lazaro ali mʼtulo
Yoh 11:43 Lazaro, tuluka!
LEKANITSA
, Miy 17:9 amalekanitsa mabwenzi
Mt 25:32 amalekanitsira nkhosa ndi mbuzi
LEKERERA
, 2Mf 10:16 sindilekerera zoti anthu azipikisana
Miy 29:15 mwana womulekerera
Hab 1:13 simungalekerere khalidwe loipa
Aro 9:22 analekerera moleza mtima
LEMBEDWA
, Aro 15:4 zimene zinalembedwa kalekale
LEMEDWA
, Lu 21:34 mitima yanu isalemedwe
LEMEKEZA
, Eks 20:12 Muzilemekeza bambo ndi mayi
Miy 3:9 Uzilemekeza Yehova
1Ak 16:18 anthu otere muziwalemekeza
Aef 5:33 mkazi azilemekeza mwamuna
1At 5:12 muzilemekeza amene akugwira ntchito
1Ti 5:17 azilemekezedwa kwambiri
LEMEKEZEKA
, 1Ak 1:26 si ambiri a mʼmabanja olemekezeka
2Ti 2:20 Zinthu za ntchito yolemekezeka
LEMERA
, Le 19:15 Musamakondere wolemera
Miy 10:22 Madalitso a Yehova amalemeretsa
Lu 14:12 Ukakonza chakudya usaitane olemera
2Ak 6:10 osauka koma olemeretsa anthu
1Ti 6:9 ofunitsitsa kulemera amakodwa
Chv 3:17 ukunena kuti: Ndine wolemera
LENGA
, Ge 1:1 Pachiyambi, Mulungu analenga
Sl 104:30 Mukatumiza mzimu wanu zimalengedwa
Yes 45:18 Amene sanalilenge popanda cholinga
Aro 1:20 Kuchokera pamene dziko linalengedwa
Aro 8:20 chilengedwe chinaweruzidwa
2Ak 5:17 iye ndi cholengedwa chatsopano
Akl 1:16 Kudzera mwa iye, Mulungu analenga
Chv 3:14 woyamba wa chilengedwe cha Mulungu
Chv 4:11 chifukwa munalenga zinthu zonse
LENGEZA
, Eks 9:16 dzina langa lilengezedwe
Sl 68:11 akazi amene akulengeza ndi gulu lalikulu
Lu 8:1 kulengeza uthenga wabwino
1Ak 11:26 mumakhala mukulengeza imfa
LEPHERA
, Sl 84:11 sadzalephera kupereka chabwino
Miy 3:27 Usalephere kuchitira zabwino
LEPHEREKA
, Miy 13:12 chikalephereka, mtima umadwala
LEPHERETSA
, Yes 14:27 ndani angazilepheretse?
Mko 4:19 nʼkulepheretsa mawuwo kukula
LETSA
, 1At 2:16 akuyesa kutiletsa kulalikira
LEVI
, Mki 3:3 Adzayeretsa ana a Levi
LEZA MTIMA
, Ne 9:30 Munawalezera mtima
Miy 25:15 Chifukwa cha kuleza mtima
Aro 9:22 analekerera moleza mtima
1Ak 13:4 Chikondi nʼcholeza mtima
1At 5:14 oleza mtima kwa onse
Yak 5:8 khalani oleza mtima
2Pe 3:9 Yehova akukulezerani mtima
2Pe 3:15 kuleza mtima kwa Ambuye
LIDIYA
, Mac 16:14 Lidiya ankagulitsa nsalu zapepo
LIKASA
, Eks 25:10 likasa la mtengo wa mthethe
2Sa 6:6 Uza anagwira Likasa
1Mb 15:2 Alevi okha azinyamula Likasa
LILIME
, Sl 34:13 muteteze lilime lanu
Miy 18:21 moyo zili mumphamvu ya lilime
Yes 35:6 lilime la wosalankhula lidzafuula
Yes 50:4 wandipatsa lilime la anthu
Yak 1:26 satha kulamulira lilime lake
Yak 3:8 palibe angathe kuweta lilime
LIMBA
, Yes 35:3 Limbitsani manja ofooka
Yes 35:4 Limbani mtima
Aro 15:1 Ife olimba tiziganizira anthu
Akl 2:7 chikhale cholimba
LIMBA MTIMA
, Yos 1:7 Ukhale wolimba mtima
Miy 28:1 olungama ndi olimba mtima
Mac 4:31 analankhula molimba mtima
Mac 28:15 Paulo atawaona analimba mtima
1Ak 16:13 khalani olimba mtima
2Ak 5:6 timakhala olimba mtima
Aef 6:20 ndilankhule molimba mtima
Afi 1:14 kulimba mtima polankhula mawu
1At 2:2 tinalimba mtima mothandizidwa ndi
LIMBANA
, Mac 5:38 musalimbane nawo
Mac 5:39 mukulimbana ndi Mulungu
LIMBIKITSA
, Yob 2:11 akatonthoze Yobu nʼkumulimbikitsa
Mt 5:4 achisoni adzalimbikitsidwa
Lu 22:32 ukalimbikitse abale ako
Mac 13:15 mawu olimbikitsa
Aro 1:12 ndidzalimbikitsidwe, mudzalimbikitsidwe
Aro 1:12 kapena kuti ndidzalimbikitsidwe
Aro 14:19 tiziyesetsa kulimbikitsana
Aro 15:4 Malembawa amatilimbikitsa
1Ak 8:1 koma chikondi chimalimbikitsa
1Ak 10:23 si zonse zomwe zimalimbikitsa
1Ak 14:26 kuti mulimbikitsane
1Ak 14:31 aphunzire ndi kulimbikitsidwa
Akl 3:16 Pitirizani kulimbikitsana
1At 2:11 tinkamudandaulira, kumulimbikitsa
1Ti 3:15 umalimbikitsa ndi kuteteza choonadi
Tit 1:9 kulimbikitsa anthu ndi mfundo
Ahe 10:25 tiyeni tilimbikitsane
Ahe 10:24 tilimbikitsane pa chikondi
LIMBITSA
, Yes 41:10 Ndikulimbitsa, ndikuthandiza
Mac 14:22 onsewa ankalimbitsa ophunzira
1Ak 1:8 Mulungu adzakulimbitsani
1Pe 5:10 Mulungu adzakulimbitsani
Yuda 20 muzilimbitsa chikhulupiriro chanu
LIPIRIRA
, 1At 2:6 tikanapempha kuti mutilipirire
LIPOTI
, Nu 14:36 anabweretsa lipoti loipa
Da 11:44 malipoti adzaisokoneza
LIRA
, Sl 6:6 Ndimalira, misozi imadzaza
Yes 65:19 losonyeza kuti munthu akulira
Ho 12:4 Analira komanso anachonderera
Lu 6:21 amene mukulira
Aro 12:15 muzilira ndi amene akulira
LODZA
, Nu 23:23 Palibe amene angalodze Yakobo
LOKONGOLA
, Da 11:45 phiri la Dziko Lokongola
LOLEKA
, 1Ak 6:12 Zinthu zonse ndi zololeka
LOLERA
, Aef 4:2 muzilolerana chifukwa cha chikondi
Afi 4:5 onse adziwe kuti ndinu ololera
LONDOLA
, 2Ti 1:13 mawu olondola
Tit 2:1 mfundo zolondola
LONJEZA
, De 23:21 kukwaniritsa zimene mwalonjezazo
Owe 11:30 Yefita analonjeza Yehova
1Mf 8:56 mogwirizana ndi zimene analonjeza
Sl 15:4 Sasintha zimene walonjeza
Ahe 10:23 amene watilonjeza ndi wokhulupirika
LONJEZO
, 2Ak 1:20 malonjezo a Mulungu
LOSERA
, Yow 2:28 ana anu adzalosera
LOTI
, Lu 17:32 Kumbukirani mkazi wa Loti
2Pe 2:7 anapulumutsa Loti wolungama
LOWA
, Mt 25:34 Lowani mu Ufumu anakukonzerani
LOWERERA
, 1Ti 5:13 kulowerera nkhani za eni
1Pe 4:15 akulowerera nkhani za eni
LUDZU
, Yes 49:10 sadzamva ludzu
Yes 55:1 amene mukumva ludzu
Yoh 7:37 Ngati wina akumva ludzu
LUKA
, Akl 4:14 Luka, dokotala wokondedwa
LUMA
, Aga 5:15 Koma mukapitiriza kulumana
LUMALA
, Yes 35:6 wolumala adzadumpha
Mki 1:8 Mukapereka nyama yolumala
LUMBIRA
, Ge 22:16 Ndikulumbira pali dzina langa
Mt 5:34 Musamalumbire nʼkomwe
LUMIKIZANA
, Aef 4:16 ziwalo ndi zolumikizana bwino
LUNGAMA
, Ge 15:6 anamuona kuti ndi wolungama
Sl 34:19 Mavuto a wolungama ndi ambiri
Sl 37:25 sindinaonepo wolungama atasiyidwa
Sl 72:7 wolungama zidzamuyendera bwino
Sl 141:5 Wolungama akandimenya
Miy 24:16 wolungama akhoza kugwa ka 7
Zef 2:3 Yesetsani kukhala olungama
1Pe 3:12 Maso a Yehova ali pa olungama
LUPANGA
, 1Sa 17:47 sapulumutsa ndi lupanga
Yes 2:4 adzasula malupanga awo
Mt 26:52 ogwira lupanga adzafa ndi lupanga
Aef 6:17 nyamulani lupanga la mzimu
Ahe 4:12 akuthwa kuposa lupanga
LUSO
, Eks 35:35 luso loluka nsalu ndi ulusi
Miy 22:29 munthu waluso pa ntchito yake?
Mt 25:15 Aliyense mogwirizana ndi luso lake
LUSO LA KUPHUNZITSA
, 2Ti 4:2 uzichita izi ndi luso la kuphunzitsa
M
MABALA
, Miy 23:29 mabala popanda chifukwa?
Miy 27:6 Mabala ovulazidwa ndi mnzako
Yes 53:5 chifukwa cha mabala ake tinachiritsidwa
MABERE
, Miy 5:19 Mabere ake azikukhutiritsa
MADENGU
, Mt 14:20 zinadzaza madengu 12
MADZI
, Nu 20:10 madzi mʼthanthweli?
Miy 20:5 ngati madzi akuya
Miy 25:25 ngati madzi ozizira
Yes 55:1 mudzamwe madzi
Yer 2:13 kasupe wa madzi
Yer 50:38 Madzi ake adzawonongedwa
Zek 14:8 madzi amoyo adzatuluka
Yoh 4:10 akanakupatsani madzi amoyo
Chv 7:17 akasupe a madzi a moyo
Chv 17:1 lakhala pamadzi ambiri
MAERE
, Sl 22:18 akuchita maere pa zovala zanga
MAFANIZO
, Mt 13:34 ankagwiritsa ntchito mafanizo
Mko 4:2 ankawaphunzitsa ndi mafanizo
MAFANO
, Sl 115:4 Mafano opangidwa ndi siliva
Yes 41:29 Mafano ndi opanda ntchito
1Yo 5:21 muzipewa mafano
MAFUMU
, Miy 22:29 adzaima pamaso pa mafumu
Lu 21:12 Adzakupititsani kwa mafumu
Mac 4:26 Mafumu a dziko anaima pamalo awo
Chv 1:6 nʼkutipanga kukhala mafumu
Chv 5:10 adzakhala mafumu olamulira dziko
Chv 18:3 mafumu anachita naye chiwerewere
MAFUTA
, 1Mf 17:16 mafuta amumtsuko sanathe
Mt 25:4 ochenjerawo anatenga mafuta
Mko 14:4 Nʼchifukwa chiyani akuwononga mafuta?
MAGALASI
, 2Ak 3:18 magalasi oonetsa ulemerero
MAGALETA
, Owe 4:13 magaleta okhala ndi zitsulo
2Mf 6:17 magaleta ankhondo oyaka moto
MAGANIZO
, Ge 8:21 maganizo amakhala oipa
1Mb 28:9 amazindikira maganizo a munthu
Sl 26:2 Yengani maganizo anga
Sl 139:17 maganizo anu ndi ofunika
Sl 146:4 zimene amaganiza zimatheratu
Miy 20:5 Maganizo ali ngati madzi akuya
Yes 55:8 Maganizo anga, maganizo anu
Mt 22:37 Muzikonda Yehova ndi maganizo onse
Aro 7:25 mʼmaganizo mwanga ndine kapolo
Aro 14:1 musamaweruze a maganizo osiyana
1Ak 2:16 tili ndi maganizo a Khristu
2Ak 10:5 tikugonjetsa maganizo alionse
Afi 2:5 maganizo amenenso Khristu anali nawo
Akl 2:18 maganizo amamuchititsa kudzitukumula
Chv 2:23 ndimafufuza maganizo
Chv 17:17 mogwirizana ndi maganizo ake
MAGAWO 10
, Mki 3:10 gawo limodzi pa magawo 10
MAGAZI
, Ge 9:4 musadye limodzi ndi magazi ake
Le 7:26 Musamadye magazi alionse
Le 17:11 moyo wa nyama uli mʼmagazi
Le 17:13 azithira magazi ake pansi
Sl 72:14 magazi awo ndi amtengo wapatali
Eze 3:18 ndidzakuimba mlandu wa magazi ake
Mt 9:20 matenda otaya magazi zaka 12
Mt 26:28 akuimira magazi anga a pangano
Mt 27:25 Magazi ake akhale pa ife
Mac 15:29 kupitiriza kupewa magazi
Mac 20:26 ndilibe mlandu wa magazi a anthu onse
Mac 20:28 anaugula ndi magazi a Mwana wake
Aef 1:7 tinamasulidwa ndi dipo la magazi ake
1Pe 1:19 munamasulidwa ndi magazi a Khristu
1Yo 1:7 magazi a Yesu akutiyeretsa
Chv 18:24 munapezeka magazi a aneneri
MAGOGI
, Eze 38:2 Gogi wa kudziko la Magogi
MAGULU ANKHONDO
, Chv 19:14 magulu ankhondo akumwamba
MAKALA
, Aro 12:20 udzamuunjikira makala a moto
MAKALATA A PANGANO
, Yer 32:12 makalata a pangano kwa Baruki
MAKANI
, Mac 19:9 anapitiriza kuchita makani
MAKEDONIYA
, Mac 16:9 Wolokerani ku Makedoniya
MAKHALIDWE
, Aef 4:19 sakuzindikira makhalidwe abwino
Afi 1:27 makhalidwe ogwirizana ndi uthenga
MAKIYI
, Mt 16:19 ndidzakupatsa makiyi a Ufumu
Chv 1:18 ndili ndi makiyi a imfa ndi Manda
MAKOLO
, Lu 18:29 azichimwene, makolo
Lu 21:16 makolo anu, azichimwene anu
2Ak 12:14 chidzathandize makolo awo
Aef 6:1 muzimvera makolo anu
Akl 3:20 muzimvera makolo anu pa zonse
MALAMULO
, Sl 94:20 pogwiritsa ntchito malamulo?
Aro 7:22 ndimasangalala ndi malamulo a Mulungu
MALAMULO KHUMI
, Eks 34:28 analemba Malamulo Khumi
MALANGIZO
, 1Mb 15:13 sitinatsatire malangizo ake
Miy 1:7 Zitsiru zimanyoza malangizo
Miy 3:11 usakane malangizo a Yehova
Miy 11:14 popanda malangizo, anthu amagwa
MALEMBA
, Mt 22:29 simudziwa Malemba
Lu 24:32 kutifotokozera Malemba momveka bwino
Mac 17:2 anakambirana mfundo za mʼMalemba
Mac 17:11 ankafufuza Malemba mosamala
Aro 15:4 Malembawa amatithandiza kupirira
2Ti 3:16 Malemba onse anauziridwa ndi Mulungu
MALIKO
, Akl 4:10 Maliko msuweni wa Baranaba
MALILIME
, 1Ak 13:8 kulankhula malilime, kudzatha
1Ak 14:22 malilime, chizindikiro cha osakhulupirira
MALIPIRO
, Ge 31:7 asintha malipiro anga
Yer 22:13 kuwapatsa malipiro awo
Aro 6:23 malipiro a uchimo
MALIRE
, Sl 119:96 malamulo anu alibe malire
MALIRO
, Mla 7:2 kupita kunyumba yamaliro
MALIZA
, Mac 20:24 ndimalize utumiki
MALONDA
, Mt 13:45 wamalonda amene akufunafuna ngale
Mt 22:5 anapita kumalonda ake
2Ak 2:17 sitichita nawo malonda
Yak 4:13 Tikachita malonda nʼkupeza phindu
Chv 18:3 Amalonda apadziko analemera
MALO ODYETSERA
, Yes 30:23 pamalo odyetserapo ziweto
MALO OTETEZEKA
, Sl 26:12 Phazi langa laima pamalo otetezeka
MALO OTHAWIRAKO
, Sl 9:9 Yehova malo otetezeka othawirako
MALOTO
, Mla 5:3 Maloto amabwera
MALUWA
, Yes 35:1 Dera lidzachita maluwa
Lu 12:27 Ganizirani mmene maluwa amakulira
MAMATIRA
, Yos 23:8 kumamatira Yehova Mulungu
MAMBA
, Yes 11:8 adzasewera pa una wa mamba
MAME
, De 32:2 Mawu adzatsika ngati mame
Sl 110:3 achinyamata ali ngati mame
MANA
, Eks 16:31 anachipatsa dzina lakuti mana
Yos 5:12 Mana analeka kugwa
Miy 23:6 chakudya cha munthu womana
MANASE
, 2Mb 33:13 Manase anadziwa kuti Yehova
MANDA
, Yob 14:13 mukanandibisa mʼManda
Mla 9:10 ku Manda kulibe kugwira ntchito
Ho 13:14 ndidzawawombola ku Manda
Mac 2:31 Khristu sanasiyidwe mʼManda
Chv 1:18 makiyi a imfa ndi a Manda
Chv 20:13 Manda anapereka akufa
MANDA ACHIKUMBUTSO
, Yoh 5:28 ali mʼmanda achikumbutso adzamva
MANGA
, Ge 22:9 anamanga Isaki mwana wakeyo
Sl 127:1 Yehova akapanda kumanga nyumba
Yes 61:1 Anandituma kuti ndikamange mabala
Yes 65:21 adzamanga nyumba nʼkumakhalamo
Eze 34:16 yovulala ndidzaimanga
Mt 16:19 chimene udzamanga padziko lapansi
Mt 19:6 Mulungu wachimanga pamodzi
Lu 17:28 ankadzala komanso kumanga
1Ak 3:10 aliyense asamale mmene akumangirapo
MANJA
, Yes 35:3 Limbitsani manja ofooka
MANKHUSU
, Zef 2:2 Tsiku lisanadutse ngati mankhusu
MANKHWALA
, Miy 17:22 Mtima wosangalala ndi mankhwala
Chv 3:18 mankhwala opaka mʼmaso
MANTHA
, Yob 31:34 Kodi ndinachitapo mantha?
Yob 31:34 mantha ndi gulu la anthu
Yes 41:10 Usachite mantha, chifukwa ndili nawe
Yes 44:8 musathedwe nzeru ndi mantha
Lu 21:26 Anthu adzakomoka ndi mantha
Afi 1:28 simukuchita mantha
2Ti 1:7 sanatipatse mzimu wamantha
1Yo 4:18 wokonda Mulungu sachita mantha
Chv 2:10 Usachite mantha ndi mavuto
MANYAZI
, Eza 9:6 ndikuchita manyazi kuti ndikweze
Sl 25:3 palibe adzachite manyazi
Mko 8:38 aliyense wochita manyazi ndi ine
Aro 1:16 sindichita manyazi ndi uthenga wabwino
1Ak 4:14 Sindikulemba kuti ndikuchititseni manyazi
Aef 5:4 khalidwe lochititsa manyazi
2Ti 1:8 usachite manyazi ndi ntchito yolalikira
2Ti 2:15 wosachita manyazi ndi ntchito
Ahe 11:16 Mulungu sachita manyazi kutchulidwa
1Pe 4:16 Mkhristu asachite manyazi
MAOLIVI
, Aro 11:17 mtengo wa maolivi wamʼtchire
MAONEKEDWE
, Mt 22:16 simuyangʼana maonekedwe a anthu
2Ak 10:7 potengera maonekedwe akunja
Aga 2:6 Mulungu sayangʼana maonekedwe
MAPAZI
, Yes 52:7 Mapazi obweretsa uthenga
Yer 10:23 ulamuliro wowongolera mapazi
Yoh 13:5 nʼkuyamba kusambitsa mapazi awo
Aro 16:20 aphwanya Satana pa mapazi anu
1Ak 15:27 anaika pansi pa mapazi ake
1Pe 2:21 mutsatire mapazi ake mosamala
MAPETO
, Mt 24:14 kenako mapeto adzafika
Mt 28:20 mpaka mʼnyengo ya mapeto a nthawi ino
Yoh 13:1 anawakonda mpaka pamapeto
2Ti 4:7 Ndathamanga mpaka pamapeto
MAPIKO
, Ru 2:12 wathawira mʼmapiko mwake
MAPIRI
, Ge 7:20 Madziwo anapitirira mapiriwo
MARITA
, Lu 10:41 Marita, ukuda nkhawa
MARIYA 1.
, Mko 6:3 kalipentala, mwana wa Mariya
MARIYA 2.
, Lu 10:39 Mariya ankamvetsera
Lu 10:42 Mariya wasankha chinthu chabwino
Yoh 12:3 Mariya anatenga mafuta okwera mtengo
MARIYA 3.
, Mt 27:56 Mariya wa ku Magadala
Lu 8:2 Mariya, anamutulutsa ziwanda 7
MARIYA 4.
, Mt 27:56 Mariya mayi a Yakobo
MARIYA 5.
, Mac 12:12 Mariya mayi a Yohane Maliko
MASAMBA
, Eze 47:12 masamba adzakhala mankhwala
Mt 24:32 Nthambi ikaphuka nʼkuchita masamba
MASEWERA
, Miy 10:23 kuli ngati masewera
MASIKU OTSIRIZA
, 2Ti 3:1 masiku otsiriza, nthawi yovuta
MASO
, Sl 115:5 Maso ali nawo
Miy 15:3 Maso a Yehova ali paliponse
MASOMPHENYA
, Da 10:14 masomphenyawa ndi okhudza
MASULA
, Mt 18:18 zilizonse zimene mudzamasule
Yoh 8:32 choonadi chidzakumasulani
MASULIDWA
, Aro 6:18 munamasulidwa ku uchimo
MATA
, Da 12:9 akuyenera kumatidwa mpaka mapeto
MATALENTE
, Mt 25:15 anamupatsa matalente 5
MATENDA
, Yes 53:4 ananyamula matenda athu
Mt 9:35 ankachiritsa matenda alionse
MATSENGA
, De 18:10 aliyense wochita zamatsenga
Mac 13:6 Myuda wina wamatsenga
Mac 19:19 azamatsenga anatentha mabuku
MAUFUMU
, Mt 4:8 anamuonetsa maufumu
MAVUTO
, 2Sa 22:7 Pa mavuto, ndinaitana Yehova
Yob 6:2 mavuto anga onse akanayezedwa
Yob 36:15 amapulumutsa ovutika pa mavuto
Sl 34:19 Mavuto a munthu wolungama
Sl 46:1 Thandizo pa nthawi ya mavuto
Sl 119:50 zimandilimbikitsa ndikakhala pamavuto
Sl 119:71 Zili bwino kuti ndakumana ndi mavuto
Miy 27:12 wosadziwa amakumana ndi mavuto
Mac 14:22 Tiyenera kukumana ndi mavuto ambiri
Aro 5:3 kumasangalala tikakumana ndi mavuto
Aro 8:18 mavuto amene tikukumana nawo
Aro 12:12 Muzipirira mavuto
1Ak 7:28 adzakumana ndi mavuto pa moyo
2Ak 1:8 Tinakumana ndi mavuto aakulu
2Ak 4:17 mavuto amene tikukumana nawo
2At 1:4 kulimbana ndi mavuto
Ahe 2:10 anakhala wangwiro kudzera mʼmavuto
1Pe 5:9 akukumananso ndi mavuto
MAWA
, Miy 27:1 Usadzitame ndi zimene udzachite mawa
1Ak 15:32 tidye ndi kumwa, mawa tifa
MAWU
, 1Mf 19:12 panamveka mawu achifatse
Sl 19:4 mawu awo amveka padziko
Miy 25:11 Mawu olankhulidwa nthawi yoyenera
Yes 55:11 mawu otuluka pakamwa
Lu 8:12 amabwera nʼkudzachotsa mawuwo
Yoh 1:1 ankadziwika kuti Mawu
Yoh 5:28 adzamva mawu ake
Yoh 10:27 zimamva mawu anga
Yoh 17:17 Mawu anu ndi choonadi
Mac 18:5 ntchito yolalikira mawu a Mulungu
Afi 2:16 mugwire mawu amoyo
2Ti 2:15 kufotokoza bwino mawu
Yak 1:22 muzichita zimene mawu amanena
MAWU ACHIPONGWE
, Aef 4:31 kulalata, mawu achipongwe
MAWU A MULUNGU
, Yes 40:8 mawu a Mulungu wathu
Mko 7:13 mawu a Mulungu akhale opanda pake
1At 2:13 munalandira mawu a Mulungu
Ahe 4:12 mawu a Mulungu ndi amoyo
MAWU OKOMA
, Miy 25:15 mawu okoma angathyole
MAWU OPWETEKA
, Miy 15:1 mawu opweteka amayambitsa mkwiyo
MAYESERO
, Mt 26:41 kuti musalowe mʼmayesero
Lu 22:28 mwakhalabe ndi ine mʼmayesero anga
1Ak 10:13 Palibe mayesero
Yak 1:2 mukukumana ndi mayesero
Yak 1:12 amene akupirira mayesero
MAYI
, Eks 20:12 Muzilemekeza bambo ndi mayi anu
Sl 27:10 Ngakhale bambo, mayi, atandisiya
Miy 23:22 usanyoze mayi chifukwa akalamba
Lu 8:21 Mayi ndi azichimwene anga ndi awa
Yoh 19:27 Awa akhala mayi ako
Aga 4:26 Yerusalemu wamʼmwamba, mayi athu
MAZIKO
, Lu 6:48 nʼkuyala maziko pathanthwe
Aro 15:20 ndisamange pamaziko
1Ak 3:11 angayale maziko ena
MBADWA
, Ge 3:15 chidani pakati pa mbadwa yako
Ge 22:17 ndidzachulukitsadi mbadwa zako
Yes 65:23 mbadwa za odalitsidwa ndi Yehova
Aga 3:16 kwa mbadwa yako, Khristu
Aga 3:29 ndinudi mbadwa za Abulahamu
MʼBADWO
, Mt 24:34 mʼbadwo sudzatha wonse
MBALAME
, Mt 6:26 Yangʼanitsitsani mbalame
MʼBALE
, Miy 17:17 mʼbale anabadwa kuti akuthandize
Miy 18:24 mnzako amakhala pafupi kuposa mʼbale
Mt 23:8 nonsenu ndinu abale
Mt 25:40 mmodzi wa abale anga
1Ak 5:11 aliyense wotchedwa mʼbale
1Pe 5:9 abale anu padziko lonse
MBEWU
, Lu 8:11 Mbewuzo ndi mawu a Mulungu
MBIRI
, Mla 7:1 Mbiri yabwino imaposa mafuta
MBIYA
, Aro 9:21 woumba mbiya ali ndi ufulu
MBONI
, De 19:15 mboni ziwiri kapena zitatu
Yes 43:10 Inu ndinu mboni zanga
Mt 18:16 umboni wa mboni ziwiri
Mac 1:8 mudzakhala mboni zanga
Chv 1:5 Yesu Khristu, Mboni Yokhulupirika
Chv 11:3 ndidzachititsa kuti mboni zanga
MʼBUSA
, Sl 23:1 Yehova ndi Mʼbusa wanga
Yes 40:11 adzasamalira nkhosa ngati mʼbusa
Eze 34:2 abusa akungodzidyetsa
Eze 37:24 adzakhala ndi mʼbusa mmodzi
Zek 13:7 nyamuka ubaye mʼbusa wanga
Mt 9:36 nkhosa zimene zilibe mʼbusa
Yoh 10:11 Mʼbusa wabwino amapereka moyo wake
Yoh 10:14 Ine ndine mʼbusa wabwino
Yoh 10:16 gulu limodzi mʼbusa mmodzi
Aef 4:11 ena abusa ndi aphunzitsi
MBUYE
, De 10:17 Yehova ndi Mbuye wa ambuye
Mt 7:22 Ambuye, kodi ife sitinalosere?
Mt 22:44 Yehova anauza Ambuye wanga
1Ak 7:39 kukwatiwa mwa Ambuye
MBUZI
, Le 16:8 mbuzi yotenga machimo
Mt 25:32 amalekanitsa nkhosa ndi mbuzi
MCHENGA
, Ge 22:17 mbadwa zako ngati mchenga
Chv 20:8 ochuluka ngati mchenga wakunyanja
MCHERE
, Ge 19:26 anasanduka chipilala chamchere
Mt 5:13 Inu ndinu mchere wa dziko
Akl 4:6 okoma ngati mwawathira mchere
MCHIMWENE
, Mt 13:55 azichimwene ake si Yakobo
MDANI
, Aro 12:20 ngati mdani wako ali ndi njala
MDIMA
, Yes 60:2 Mdima udzaphimba dziko
Yow 2:31 Dzuwa lidzasanduka mdima
Zef 1:15 Tsiku la mdima wochititsa mantha
Mt 4:16 okhala mumdima anaona kuwala
Yoh 3:19 anthu akukonda mdima
Aef 4:18 ali mumdima wa maganizo
1Pe 2:9 anakuitanani muchoke mumdima
MDULIDWE
, Aro 2:29 mdulidwe wochitidwa ndi mzimu
1Ak 7:19 Mdulidwe sutanthauza chilichonse
MDYEREKEZI
, Mt 25:41 moto umene anakolezera Mdyerekezi
Lu 4:6 Mdyerekezi anati ali ndi ulemerero
Lu 8:12 Mdyerekezi amadzachotsa mawuwo
Yoh 8:44 ndinu ochokera kwa Mdyerekezi
Aef 4:27 Musamupatse mpata Mdyerekezi
Aef 6:11 musagonje kwa Mdyerekezi
Yak 4:7 tsutsani Mdyerekezi, adzakuthawani
1Pe 5:8 Mdyerekezi, mkango wobangula
1Yo 3:8 awononge ntchito za Mdyerekezi
Chv 12:12 Tsoka, Mdyerekezi watsikira kwa inu
Chv 20:10 Mdyerekezi, adzaponyedwa mʼnyanja
MELEKIZEDEKI
, Ge 14:18 Melekizedeki mfumu
Sl 110:4 wansembe mofanana ndi Melekizedeki
MELITA
, Mac 28:1 chilumbacho chimatchedwa Melita
MENYA
, Yoh 19:3 ankamumenya makofi
1Ak 9:27 ndikumenya thupi langa
2Ak 6:5 pomenyedwa, kuikidwa mʼndende
MESIYA
, Da 9:25 Mesiya Mtsogoleri adzaonekere
Da 9:26 milungu 62, Mesiya adzaphedwa
Yoh 1:41 Ifetu tapeza Mesiya
Yoh 4:25 Ndikudziwa Mesiya akubwera
MFUMU
, Owe 21:25 mu Isiraeli munalibe mfumu
1Sa 23:17 ukhaladi mfumu, ndidzakhala wachiwiri
Sl 2:6 ndasankha mfumu yanga
Miy 21:1 Mtima wa mfumu uli ngati mitsinje
Yes 32:1 Mfumu idzalamulira mwachilungamo
Zek 14:9 Yehova adzakhala Mfumu ya dziko
Mt 21:5 Mfumu ikubwera itakwera bulu
Mt 27:29 Moni, Mfumu ya Ayuda!
Yoh 19:15 Tilibe mfumu koma Kaisara
1Ak 15:25 ayenera kukhala mfumu
MFUMUKAZI
, 1Mf 10:1 Mfumukazi ya ku Sheba
MFUMU YAKUMʼMWERA
, Da 11:11 mfumu yakumʼmwera idzakwiya
Da 11:40 mfumu yakumʼmwera idzakankhana
MFUMU YAKUMPOTO
, Da 11:7 kukaukira mfumu yakumpoto
Da 11:40 kukankhana ndi mfumu yakumpoto
MFUNDO YAIKULU
, Mla 12:13 mfundo yaikulu ndi yakuti:
MFUNDO ZOMVEKA
, Mac 9:22 mfundo zomveka zotsimikizira
MIKANGANO
, Miy 6:19 amayambitsa mikangano pakati pa abale
Afi 2:3 mtima wokonda mikangano
MIKANGO
, Da 6:27 wapulumutsa Danieli kwa mikango
MIKAYELI
, Da 10:13 Mikayeli mmodzi wa akalonga
Da 12:1 nthawi imeneyo Mikayeli adzaimirira
Chv 12:7 Mikayeli anamenyana ndi chinjoka
MILIRI
, Lu 21:11 kudzakhala miliri ndi njala
MILOMO
, Miy 10:19 amalamulira milomo yake
Yes 29:13 amandilemekeza ndi milomo yokha
Ahe 13:15 nsembe ya milomo yathu
MILUNGU
, Da 9:24 Pali milungu 70
MIMBA
, Aro 16:18 akapolo a mimba zawo
Afi 3:19 mulungu wawo ndi mimba zawo
MIMBULU
, Mt 7:15 ali ngati mimbulu yolusa
Lu 10:3 nkhosa pakati pa mimbulu
Mac 20:29 mimbulu yopondereza idzafika
MINA
, Lu 19:16 ndalama ya mina yapindula
MINDA YA MPESA
, Yes 65:21 adzadzala minda ya mpesa
MINGA
, Mko 15:17 chisoti chachifumu chaminga
2Ak 12:7 ndinapatsidwa minga mʼthupi
MIPANDO YACHIFUMU
, Da 7:9 mipando yachifumu inaikidwa
MIRIAMU
, Nu 12:1 Miriamu ndi Aroni ankamunena
MISALA
, Yoh 10:20 ameneyu ndi wamisala
MISECHE
, Le 19:16 nʼkumafalitsa miseche
Miy 20:19 amakonda kunena miseche
1Ti 5:13 amakondanso miseche
MISOZI
, 2Mf 20:5 ndaona misozi yako
Sl 6:6 ndimanyowetsa bedi ndi misozi
Sl 126:5 akukhetsa misozi pofesa mbewu
Mla 4:1 oponderezedwa akugwetsa misozi
Mac 20:19 ndi misozi komanso mayesero
Mac 20:31 ndikutulutsa misozi
Ahe 5:7 akugwetsa misozi
Chv 21:4 adzapukuta misozi yonse
MITAMBO
, Mla 11:4 woyangʼana mitambo sadzakolola
Mt 24:30 Mwana wa munthu akubwera pamitambo
MITENGO
, Yes 61:3 adzatchedwa mitengo ikuluikulu
Eze 47:12 mudzamera mitengo yosiyanasiyana
Chv 22:14 zipatso zamʼmitengo ya moyo
MITIMA
, Miy 17:3 Yehova amayesa mitima
Lu 12:34 mitima yanunso idzakhala komweko
Lu 21:34 mitima yanu isalemedwe
1Yo 3:20 Mulungu ndi wamkulu kuposa mitima
MITUNDU
, Ge 22:18 mitundu idzapeza madalitso
Mt 25:32 Mitundu yonse idzasonkhanitsidwa
Lu 21:24 nthawi zoikidwiratu za a mitundu
MIVI
, Sl 127:4 mivi mʼdzanja la mwamuna
MIYALA
, Eks 31:18 anapatsa Mose miyala
MIYAMBO
, Mt 15:3 chifukwa cha miyambo yanu
Mko 7:13 chifukwa cha miyambo yanu
Aga 1:14 wodzipereka pa miyambo ya makolo
MIZINDA YOTHAWIRAKO
, Nu 35:11 ikakhale mizinda yanu yothawirako
Yos 20:2 Sankhani mizinda yothawirako
MIZU
, Lu 8:13 amawalandira, koma alibe mizu
Akl 2:7 chikhulupiriro chanu chikhale ndi mizu
MKAIDI
, 2Ak 10:5 nʼkuwamanga ngati mkaidi
MKAKA
, Eks 3:8 dziko loyenda mkaka ndi uchi
Yes 60:16 udzamwa mkaka wa mitundu
Ahe 5:12 mwayambanso kufuna mkaka
1Pe 2:2 muzilakalaka mkaka wosasungunula
MKANGANO
, Miy 15:18 amaziziritsa mkangano
Miy 17:14 mkangano usanabuke, chokapo
MKANGO
, 1Sa 17:36 ndinapha mkango
Sl 91:13 Udzapondaponda mkango ndi mamba
Yes 11:7 Mkango udzadya udzu ngati ngʼombe
1Pe 5:8 Mdyerekezi akuyenda ngati mkango
Chv 5:5 Mkango wa fuko la Yuda
MKANJO
, Zek 8:23 adzagwira mkanjo wa Myuda
MKATE
, Mt 26:26 anatenga mkate
1Ak 10:17 tonse tikudya mkate umodzi
MKATI
, 2Ak 4:16 munthu wamkati watsopano
Aef 3:16 munthu wamkati akhale wamphamvu
MKAZI
, Ge 2:24 nʼkudziphatika kwa mkazi wake
Ge 3:15 pakati pa iwe ndi mkaziyo
Ge 27:46 Yakobo angatenge mkazi
1Mf 11:3 akazi ena apambali 300
Miy 5:18 uzisangalala ndi mkazi
Miy 12:4 Mkazi wamakhalidwe abwino
Miy 18:22 amene wapeza mkazi wabwino
Miy 21:19 mkazi wolongolola
Miy 31:10 ndani angapeze mkazi?
Mla 7:26 Mkazi amene ali ngati ukonde
Mla 9:9 Sangalala ndi mkazi wako
Mki 2:15 musachitire zachinyengo akazi anu
1Ak 7:2 mwamuna aliyense akhale ndi mkazi
Chv 12:1 mkazi atavala dzuwa
MKAZI WAMASIYE
, Sl 146:9 mwana wamasiye, mkazi wamasiye
Mko 12:43 mkazi wamasiye waponya zochuluka
Lu 18:3 munalinso mkazi wamasiye
MKHALAPAKATI
, 1Ti 2:5 mkhalapakati wa Mulungu ndi anthu
MKONDO
, 1Sa 18:11 Sauli anaponya mkondowo
MKULU WA ANGELO
, 1At 4:16 Mawu a mkulu wa angelo
Yuda 9 Mikayeli, mkulu wa angelo
MKWATIBWI
, Chv 21:9 mkwatibwi wa Mwanawankhosa
MKWIYO
, Miy 16:32 amalamulira mkwiyo wake
MKWIYO WA MULUNGU
, Sl 30:5 mkwiyo wa Mulungu sukhalitsa
MLALIKI
, Mac 21:8 mlaliki dzina lake Filipo
2Ti 4:5 uzigwira ntchito ya mlaliki
MLANDU
, Mac 20:26 ine ndilibe mlandu wa magazi
Aro 6:7 amene wafa sakhala ndi mlandu
Aro 8:33 Ndani adzasumira mlandu
1Ti 5:19 Usavomereze mlandu woneneza
MLANGIZI
, Miy 15:22 alangizi akachuluka zimayenda
Yes 9:6 dzina lakuti Mlangizi Wodabwitsa
MLENDO
, Eks 22:21 Musamachitire nkhanza mlendo
Nu 9:14 mlendo amene ali pakati panu
De 10:19 Inunso muzikonda mlendo
Sl 15:1 ndani angakhale mlendo mutenti yanu?
Yoh 10:5 Sizidzatsatira mlendo
MLENGI
, Mla 12:1 kumbukira Mlengi wako Wamkulu
MLINGO
, Yer 30:11 Ndidzakulanga pamlingo woyenera
MLIRI
, Eks 11:1 Patsala mliri umodzi
Chv 18:4 kulandira nawo miliri yake
MLUNGU
, 1Ak 16:2 Tsiku loyamba la mlungu
MLUZA
, Sl 139:16 pamene ndinali mluza
MMBULU
, Yes 11:6 Mmbulu udzakhala ndi nkhosa
MMISIRI
, Miy 8:30 monga mmisiri waluso
MMODZI
, 1Ak 8:6 Mulungu alipo mmodzi yekha
MʼMPHEPETE
, Le 23:22 musamachotseretu zamʼmphepete
MNENERI
, De 18:18 Ndidzawapatsa mneneri
Eze 2:5 adzadziwa kuti panali mneneri
Amo 7:14 sindinali mneneri, mwana wa mneneri
MNGELO
, 2Mf 19:35 mngelo anapha asilikali 185,000
Sl 34:7 Mngelo wa Yehova amamanga msasa
Da 3:28 anatumiza mngelo nʼkudzapulumutsa
Ho 12:4 [Yakobo] analimbana ndi mngelo
Mac 5:19 mngelo anatsegula zitseko za ndendeyo
Mac 12:11 watumiza mngelo kudzandipulumutsa
MNOFU
, Yob 33:25 Mnofu wake usalale
1Ak 15:50 mnofu, magazi sizingalowe mu Ufumu
MNYAMATA
, Yob 33:25 kuposa ali mnyamata
Sl 71:17 kuyambira ndili mnyamata
Yes 11:6 kamnyamata kadzazitsogolera
MNZAKE
, Yak 2:23 Abulahamu, mnzake wa Yehova
MNZAKO
, Miy 17:17 Mnzako weniweni amakukonda
Miy 18:24 mnzako amakhala nawe pafupi
Miy 27:6 Mabala ovulazidwa ndi mnzako
Lu 10:27 uzikonda mnzako mmene umadzikondera
MNZANGA
, Sl 55:13 Mnzanga amene ndikumudziwa
MODABWITSA
, Sl 139:14 munandipanga modabwitsa
MODYERA ZIWETO
, Lu 2:7 nʼkumugoneka modyeramo ziweto
MODZICHEPETSA
, Mik 6:8 uziyenda modzichepetsa ndi Mulungu
MODZIPEREKA
, Yes 37:32 adzachita zimenezi modzipereka
1Ti 4:15 uzizichita modzipereka kuti anthu aone
2Ti 4:2 Uzilalikira modzipereka
1Pe 5:2 mofunitsitsa monga atumiki a Mulungu
MONI
, 2Yo 10 musamupatse moni
MOONA MTIMA
, 2Ak 8:21 kusamalira moona mtima
Ahe 13:18 kuchita zonse moona mtima
MOSALEKEZA
, Da 6:16 amene ukumutumikira mosalekeza
MOSE
, Nu 12:3 Mose anali wofatsa kuposa onse
Sl 106:32 Mose sizinamuyendere bwino
Mac 7:22 Mose ankachita zinthu zazikulu
2Ak 3:7 sanathe kuyangʼanitsitsa Mose
MOTO
, Yer 20:9 moto woyaka mʼmafupa anga
Mt 25:41 kumoto wokolezedwera Mdyerekezi
1Ak 3:13 Motowo udzaonetsa ntchito ya aliyense
1At 5:19 Musazimitse moto wa mzimu
2Ti 1:6 mphatso uikolezere ngati moto
2Pe 3:7 dziko lapansi alisungira moto
MOWA
, Miy 20:1 omwa mowa amasokoneza
MOYO
, Nu 31:28 mutengepo chamoyo chimodzi
De 30:19 ndaika moyo ndi imfa
Yob 14:14 akafa, angakhalenso ndi moyo?
Sl 36:9 ndinu kasupe wa moyo
Mla 3:11 kukhala ndi moyo mpaka kalekale
Eze 18:4 Moyo wochimwa ndi umene udzafe
Da 6:26 ndi Mulungu wamoyo
Mt 22:37 moyo wanu wonse, maganizo anu onse
Lu 9:24 akufuna kupulumutsa moyo, adzautaya
Lu 20:38 Mulungu wa amoyo, onsewa ndi amoyo
Yoh 5:26 Atate ali ndi mphamvu zopereka moyo
Yoh 11:25 ndine kuuka ndi moyo
Mac 20:24 moyo wanga sindikuuona wofunika
2Ak 5:15 asakhale moyo wongodzisangalatsa
1At 4:15 ife amene tipitirize kukhala ndi moyo
Ahe 4:12 mawu a Mulungu ndi amoyo
MOYO WONSE
, Akl 3:23 muzichichita ndi moyo wanu wonse
MOYO WOSATHA
, Da 12:2 Ena adzalandira moyo wosatha
Lu 18:30 adzapeza moyo wosatha
Yoh 3:16 akhale ndi moyo wosatha
Yoh 17:3 Moyo wosatha adzaupeza
Mac 13:48 kukapeza moyo wosatha
Aro 6:23 amapereka moyo wosatha
1Ti 6:12 Gwira mwamphamvu moyo wosatha
MPAKA KALEKALE
, Ge 3:22 nʼkukhala mpaka kalekale
Sl 37:29 adzakhala mpaka kalekale
Mla 3:14 zidzakhalapo mpaka kalekale
1Pe 1:25 adzakhalapo mpaka kalekale
MPALA
, Le 21:5 Asamamete mpala mitu yawo
MPANDA
, Yos 6:5 mpanda wonse udzagwa
Eze 38:11 mʼmidzi yopanda mipanda
Lu 19:43 adzamanga mpanda
MPANDO WACHIFUMU
, Sl 45:6 mpando wachifumu mpaka kalekale
Yes 6:1 atakhala pampando wachifumu
Mt 25:31 adzakhala pampando wachifumu
Lu 1:32 adzamupatsa mpando wachifumu
MPANDO WOWERUZIRA
, Yoh 19:13 anakhala pampando woweruzira
Aro 14:10 tidzaima kumpando woweruzira
MPATUKO
, Miy 11:9 Wampatuko amawononga mnzake
Mac 28:22 gulu lampatuko amalinenera
2At 2:3 mpatuko ukuyenera kuchitika
Tit 3:10 wolimbikitsa mpatuko, usagwirizane naye
2Pe 2:1 adzayambitsa timagulu tampatuko
MPHAMVU
, Yos 1:7 uchite zinthu mwamphamvu
1Sa 30:6 ndipo anapeza mphamvu
Sl 29:11 Yehova adzapatsa anthu mphamvu
Sl 31:10 Mphamvu zanga zikuchepa
Sl 84:7 Mphamvu zidzapitiriza kuwonjezeka
Miy 17:22 akakhumudwa mphamvu zimatha
Miy 28:16 amagwiritsa ntchito mphamvu
Yes 40:29 amapereka mphamvu kwa wotopa
Yes 40:31 adzapezanso mphamvu
Zek 4:6 sipakufunika mphamvu, koma mzimu
Mko 5:30 mphamvu yatuluka mʼthupi mwake
Mko 12:30 ndi mphamvu zanu zonse
Mac 1:8 mudzakhala ndi mphamvu
1Ak 16:13 khalani ndi chikhulupiriro, amphamvu
2Ak 4:7 mphamvu yoposa yachibadwa
2Ak 12:9 mphamvu zanga, ukakhala wofooka
2Ak 12:10 mʼpamene ndimakhala wamphamvu
Afi 4:13 ndimapeza mphamvu kwa Mulungu
Chv 3:8 uli ndi mphamvu zochepa
MPHATSO
, Aro 6:23 mphatso imene Mulungu amapereka
Aro 12:6 Tili ndi mphatso zosiyanasiyana
1Ak 7:7 aliyense ali ndi mphatso
2Ak 8:12 Mphatso yochokera pansi pa mtima
Aef 4:8 anapereka amuna, akhale mphatso
Yak 1:17 Mphatso iliyonse yabwino
MPHEPO
, Mla 11:4 amene amayangʼana mphepo
Mt 7:25 Kenako chimphepo chinawomba
1Ak 9:26 sikuti ndikungomenya mphepo ayi
1Ak 14:9 mukulankhula kwa mphepo
Aef 4:14 tisamatengeketengeke ndi mphepo
Chv 7:1 atagwira mwamphamvu mphepo 4
MPHETA
, Mt 10:29 Mpheta ziwiri amazigulitsa
MPHEZI
, Mt 24:27 mphezi imangʼanimira kumʼmawa
Lu 10:18 Satana atagwa ngati mphezi
MPHONDA
, Yon 4:10 chomera cha mphondachi
MPHOTO
, Ru 2:12 Yehova akupatse mphoto
1Ak 9:24 amene amakalandira mphoto
Akl 2:18 asakulepheretseni mphoto
Akl 3:24 mphoto, cholowa chochokera kwa Yehova
Ahe 11:6 amapereka mphoto
MPHWAYI
, Miy 1:32 mphwayi zidzawawonongetsa
MPIKISANO
, Mla 9:11 amapambana pampikisano
Mac 20:24 ndimalize kuthamanga mpikisanowu
Aga 5:26 tisamayambitse mpikisano
2Ti 4:7 Ndathamanga pa mpikisanowu
MPINGO
, Sl 22:25 Ndidzakutamandani mumpingo
Sl 40:9 chilungamo mumpingo waukulu
Mt 16:18 pathanthwe ili ndidzamangapo mpingo
Mac 20:28 muwete mpingo wa Mulungu
Aro 16:5 Ndikuperekanso moni ku mpingo
MPUKUTU
, Chv 20:12 mipukutu inatambasulidwa
MPUMULO
, 2At 1:7 mudzapatsidwa mpumulo
MPWEYA
, Ge 2:7 anauzira mpweya wa moyo
Sl 146:4 Mpweya wake umachoka
Aef 2:2 wolamulira wa mpweya
MSAMPHA
, Sl 91:3 adzakupulumutsa mumsampha
Miy 29:25 Kuopa anthu ndi msampha
Lu 21:34, 35 modzidzimutsa ngati msampha
MSEWU
, Mt 7:14 msewu wake ndi wopanikiza
Mt 13:4 zinagwera mʼmbali mwa msewu
MSILIKALI
, Yer 20:11 ngati msilikali woopsa
2Ti 2:4 Msilikali sachita zamalonda
MSONKHANO
, Le 23:4 misonkhano yopatulika
MSONKHO
, Lu 20:22 nʼzololeka kuti tizipereka msonkho?
Lu 23:2 akuletsa anthu kukhoma msonkho
Aro 13:6 Nʼchifukwa chake mumakhoma misonkho
Aro 13:7 Wofuna msonkho, mʼpatseni msonkho
MTENDERE
, 1Mf 4:25 Aisiraeli ankakhala mwamtendere
Sl 29:11 adzawadalitsa powapatsa mtendere
Sl 37:11 adzasangalala ndi mtendere
Sl 72:7 padzakhala mtendere wochuluka
Sl 119:165 amakhala ndi mtendere wochuluka
Miy 17:1 kudya mkate pali mtendere
Yes 9:7 Ndipo mtendere sudzatha
Yes 32:18 adzakhala pamalo amtendere
Yes 48:18 mtendere udzakhala ngati mtsinje
Yes 54:13 mtendere wa ana ako
Yes 57:21 Oipa alibe mtendere
Yes 60:17 mtendere ukhale ngati okuyangʼanira
Yer 6:14 Kuli mtendere! Kuli mtendere!
Ho 2:18 azikhala mwamtendere
Mt 5:9 amene amabweretsa mtendere
Mt 5:24 ukakhazikitse mtendere
Mko 9:50 sungani mtendere pakati panu
Yoh 14:27 Ndikukusiyirani mtendere wanga
Mac 9:31 mpingo unakhala pamtendere
Aro 5:1 tingathe kukhala pa mtendere
Aro 8:6 kumabweretsa moyo ndi mtendere
Aro 12:18 yesetsani kukhala mwamtendere
Aro 12:18 muzikhala mwamtendere ndi anthu
Afi 4:7 mtendere wa Mulungu
1At 4:11 muzikhala mwamtendere
1At 5:3 Bata ndi mtendere!
1Pe 3:11 kumakhala mwamtendere ndi ena
Chv 6:4 kuchotsa mtendere padziko
MTENGO
, Ge 2:9 mtengo wodziwitsa chabwino
Ge 2:9 mtengo wa moyo
Sl 1:3 ngati mtengo wodzalidwa
Da 4:14 Gwetsani mtengowo mudule nthambi
Mko 15:25 anamukhomerera pamtengo
1Ak 7:23 Munagulidwa pa mtengo
Aga 3:13 wopachikidwa pamtengo
Chv 2:7 zipatso zamumtengo wa moyo
MTENGO WA MAOLIVI
, Sl 52:8 mtengo wa maolivi mʼnyumba
MTENGO WA MKUYU
, 1Mf 4:25 mtengo wa mpesa ndi wa mkuyu
Mik 4:4 pansi pa mtengo wa mkuyu
Mt 21:19 mkuyuwo unafota nthawi yomweyo
Mko 13:28 zokhudza mtengo wa mkuyu
MTENGO WA MPESA
, Mik 4:4 pansi pa mtengo wa mpesa
Yoh 15:1 mtengo wa mpesa weniweni
MTENGO WAPATALI
, Hag 2:7 zinthu zamtengo wapatali
Mt 6:26 amtengo wapatali kuposa mbalame?
1Pe 1:19 magazi amtengo wapatali
MTENGO WOZUNZIKIRAPO
, Mt 10:38 kunyamula mtengo wozunzikirapo
Lu 9:23 anyamule mtengo wozunzikirapo
MTHANDIZI
, Yoh 14:16 adzakupatsani mthandizi
Yoh 14:26 mthandizi, mzimu, adzakuphunzitsani
MTHENGA
, Mki 3:1 ndikutumiza mthenga wanga
MTHUNZI
, 1Mb 29:15 Masiku athu ali ngati mthunzi
Sl 91:1 mumthunzi wa Wamphamvuyonse
Akl 2:17 mthunzi wa zimene zinali kubwera
Yak 1:17 sasintha ngati mthunzi
MTIMA
, Ge 6:5 zofuna za mtima wawo
De 6:6 Mawu azikhala pamtima panu
1Mf 8:38 akudziwa ululu wamumtima
2Mb 16:9 odzipereka ndi mtima wonse
Eza 7:10 Ezara anakonzekeretsa mtima
Sl 34:18 ali pafupi ndi a mtima wosweka
Sl 51:10 lengani mtima wolungama
Sl 51:17 kudzimvera chisoni mumtima
Sl 51:17 simudzakana mtima wosweka
Sl 147:3 Iye amachiritsa osweka mtima
Miy 4:23 Uteteze mtima wako
Miy 14:30 Mtima wodekha, thupi lathanzi
Miy 17:22 Mtima wosangalala ndi mankhwala
Miy 17:25 amapweteketsa mtima wa mayi ake
Miy 28:26 amene amadalira mtima wake
Yes 66:2 Ndidzayangʼana wosweka mtima
Yer 17:9 Mtima ndi wopusitsa kwambiri
Yer 17:10 Ine Yehova ndimafufuza mtima
Yer 31:33 ndidzachilemba mumtima mwawo
Mt 15:19 mumtima mumachokera maganizo
Mt 22:37 Muzikonda Yehova ndi mtima wonse
Lu 24:32 tinakhudzidwa kwambiri mumtima
Mac 16:14 anatsegula mtima wake
Aro 6:17 munamvera mochokera pansi pa mtima
Aro 7:22 Mumtima mwanga ndimasangalala
Afi 2:20 ndilibe ali ndi mtima ngati wake
Ahe 3:12 nʼkukhala ndi mtima woipa
MTIMA MʼMALO
, Lu 12:19 Mtima mʼmalo, udye, umwe
MTIMA WONSE
, 1Mb 28:9 uzimutumikira ndi mtima wonse
2Mb 16:9 odzipereka ndi mtima wonse
Aef 6:6 chifuniro cha Mulungu ndi mtima wonse
MTOLO
, Mac 15:28 tisakusenzetseni mtolo wolemera
MTSIKANA
, 2Mf 5:2 anakagwirako kamtsikana
Mko 5:42 mtsikanayo anadzuka nʼkuyenda
MTSINJE
, Chv 12:16 nʼkumeza mtsinje
Chv 22:1 mtsinje wa madzi a moyo
MTSOGOLERI
, Miy 28:16 Mtsogoleri, amagwiritsa ntchito mphamvu
Mt 23:10 Mtsogoleri wanu ndi mmodzi, Khristu
MTUMIKI
, Yes 42:1 Taonani mtumiki wanga
Yes 65:13 Atumiki anga adzadya
Mko 10:43 akuyenera kukhala mtumiki
Lu 12:42 mtumiki woyangʼanira nyumba
MTUMIKI WAMKULU
, Mac 3:15 Munapha Mtumiki Wamkulu
Ahe 12:2 Mtumiki Wamkulu ndi Wokwaniritsa
MTUNDU
, Eks 19:6 mtundu wanga woyera
Sl 33:12 Wosangalala ndi mtundu
Yes 66:8 kodi mtundu ungabadwe?
Mt 21:43 Ufumu udzaperekedwa ku mtundu
Mt 24:7 Mtundu udzaukirana ndi mtundu
Mac 17:26 anapanga mitundu yonse ya anthu
1Pe 2:9 ansembe achifumu, mtundu woyera
2Pe 3:11 ganizirani za mtundu wa anthu
MUBEREKANE
, Ge 1:28 Muberekane, muchuluke
MULUNGU
, De 10:17 Yehova ndi Mulungu wa milungu
Mt 27:46 Mulungu wanga, mwandisiyiranji?
Yoh 1:18 Palibe munthu anaonapo Mulungu
Yoh 17:3 Mulungu yekhayo amene ndi woona
Yoh 20:17 Mulungu wanga ndi Mulungu wanu
1Ak 8:4 kulibe Mulungu wina
2Ak 4:4 mulungu wa nthawi ino
Aef 4:6 Mulungu mmodzi, Atate wa onse
1Yo 4:8 Mulungu ndi chikondi
MUNDA
, Ge 2:15 nʼkumuika mʼmunda wa Edeni
Mt 13:38 Munda ndi dziko
Yoh 4:35 muone mʼmindamo, mwayera
1Ak 3:9 ndinu munda wa Mulungu
MUNDA WA MPESA
, Mt 20:1 anali ndi munda wa mpesa
Mt 21:28 kukagwira ntchito mʼmunda wa mpesa
Lu 20:9 analima munda wa mpesa
MUNTHU
, Sl 8:4 munthu ndi ndani
Yak 5:17 Eliya anali munthu ngati ife
MUNTHU WOVUTIKA
, Sl 40:17 munthu wovutika, wosauka
MUSADZINAMIZE
, Aga 6:7 Musadzinamize, Mulungu sapusitsika
MUSAMAKHULUPIRIRE
, Sl 146:3 Musamakhulupirire anthu olemekezeka
MUSAMAKWIYITSE
, Akl 3:21 musamakwiyitse ana anu
MUTU
, Ge 3:15 idzaphwanya mutu wako
Da 2:32 Mutu wa chifanizirocho unali wagolide
1Ak 11:3 Mutu wa mkazi ndi mwamuna
Aef 5:23 Khristu ndi mutu wa mpingo
Aef 5:23 mwamuna ndi mutu wa mkazi
MUYEZO
, Lu 6:38 muyezo umene mukuyezera ena
MUZILANDIRANA
, Aro 15:7 muzilandirana, ngati Khristu
MVERA
, Eks 24:7 tidzachita zomwezo, tidzamumvera
1Sa 15:22 Kumvera kumaposa nsembe
1Mf 3:9 Mundipatse mtima womvera
Sl 51:12 mtima wofunitsitsa kukumverani
Mt 17:5 Mwana wanga. Muzimumvera
Lu 2:51 anapitiriza kuwamvera
Lu 10:16 akukumverani, akumveranso ine
Mac 4:19 kumvera inu mʼmalo mwa Mulungu
Mac 5:29 tiyenera kumvera Mulungu
Aro 5:19 kumvera kwa munthu mmodziyu
Aro 6:17 munamvera mochokera pansi pa mtima
Aro 13:1 azimvera olamulira akuluakulu
Aro 16:26 azimumvera mwa chikhulupiriro
Aef 6:5 Akapolo inu, muzimvera
Afi 2:8 anakhala womvera mpaka imfa
Ahe 5:8 anaphunzira kumvera
Ahe 13:17 Muzimvera amene akukutsogolerani
MVETSA
, 1Mf 3:11 ukhale womvetsa zinthu
Ne 8:8 anathandiza anthuwo kumvetsa
Yob 6:24 ndimvetse zimene ndalakwitsa
Sl 119:27 Ndithandizeni kumvetsa
Miy 3:5 luso lako lomvetsa zinthu
Miy 4:7 upezenso luso lomvetsa zinthu
Da 11:33 kuti amvetse zinthu
1Ak 14:20 pa nkhani yomvetsa
1Pe 4:4 anthu amʼdzikoli sakumvetsa
MVETSERA
, Miy 1:5 wanzeru amamvetsera
Eze 2:7 kaya akamvetsera kapena ayi
Yak 1:19 wokonzeka kumvetsera
MVULA
, Ge 7:12 chimvula chinakhuthuka masiku 40
De 11:14 ndidzakupatsaninso mvula
De 32:2 Malangizo adzagwa ngati mvula
Yes 55:10 mvula komanso sinowo
Mt 5:45 amagwetsera mvula anthu
MWALA
, Da 2:34 mwala unadulidwa kuphiri
Mt 21:42 Mwala umene omanga anaukana
Lu 19:40 miyala ingathe kufuula
MWALA WAPAKONA
, Sl 118:22 mwala wapakona wofunika
Aef 2:20 Yesu ndi mwala wapakona
MWALIRA
, Lu 8:49 Mwana wanu wamwalira
Yoh 11:25 ngakhale atamwalira, adzakhalanso
MWAMUNA
, Le 20:13 akagona ndi mwamuna
1Ak 7:2 akhale ndi mwamuna wakewake
1Ak 7:14 Mwamuna wosakhulupirira
MWANA
, Owe 13:8 zoyenera kuchita ndi mwana
Sl 2:12 Mulemekezeni mwanayo
Miy 13:24 amene sakwapula mwana wake
Miy 15:20 Mwana wanzeru amasangalatsa bambo
Miy 22:6 Phunzitsa mwana
Yer 1:7 Usanene kuti, Ndine mwana
Mt 3:17 Uyu ndi Mwana wanga wokondedwa
Lu 9:47 anatenga mwana wamngʼono
Lu 15:13 mwana wamngʼono uja
1Ak 13:11 kuganiza ngati mwana
MWANA WA DISO
, Sl 17:8 Nditetezeni ngati mwana wa diso
Zek 2:8 akukhudza mwana wa diso
MWANA WAMASIYE
, Eks 22:22 Musamazunze mwana wamasiye
Sl 68:5 Bambo wa ana amasiye
MWANA WAMNGʼONO
, Lu 9:48 zinthu ngati mwana wamngʼono
MWANA WA MUNTHU
, Da 7:13 wooneka ngati mwana wa munthu
Mt 10:23 Mwana wa munthu asanafike
Lu 21:27 adzaona Mwana wa munthu akubwera
MWANA WA NGʼOMBE
, Eks 32:4 anapanga fano la mwana wa ngʼombe
Yes 11:6 Mwana wa ngʼombe, mkango
MWANA WA NKHOSA
, 2Sa 12:3 anali ndi kamwana ka nkhosa kokha
MWANAWANKHOSA
, Yoh 1:29 Mwanawankhosa akuchotsa uchimo
MWAYI
, Yes 65:11 mulungu wa Mwayi
Afi 1:29 inu munapatsidwa mwayi
MWEZI
, Yow 2:31 mwezi udzasanduka magazi
Lu 21:25 zizindikiro padzuwa, mwezi ndi nyenyezi
MWINIWAKE
, 1Ak 6:19 mwiniwake wa inuyo si inu
MWINIWAKE WA MUNDA
, Mt 9:38 Mwiniwake wa munda atumize antchito
MYUDA
, 1Ak 9:20 Kwa Ayuda ndinakhala Myuda
MZIMU
, Nu 11:25 Anatengako gawo lina la mzimu
1Sa 16:13 mzimu wa Yehova unathandiza Davide
2Sa 23:2 Mzimu wa Yehova unalankhula
Sl 104:29 Mukachotsa mzimu wawo
Mla 12:7 mzimu udzabwerera kwa Mulungu
Yes 61:1 Mzimu wa Yehova uli pa ine
Yow 2:28 ndidzapereka mzimu wanga
Zek 4:6 koma mzimu wanga
Mt 3:16 Yohane anaona mzimu
Mt 12:31 wonyoza mzimu sadzakhululukidwa
Mt 26:41 mzimu ndi wofunitsitsa
Lu 23:46 ndikupereka mzimu wanga
Yoh 4:24 Mulungu ndi Mzimu, kulambira ndi mzimu
Yoh 16:13 mzimu wa choonadi
Aro 8:16 limodzi ndi mzimu wathu
Aro 8:26 koma mzimu umachonderera
2Ak 3:17 Yehova ndi Mzimu
Aga 5:16 motsogoleredwa ndi mzimu
Aga 5:22 mothandizidwa ndi mzimu
Aga 6:8 akutsatira mzimu wa Mulungu
1Pe 3:18 anaukitsidwa monga mzimu
MZIMU WOYERA
, Sl 51:11 musandichotsere mzimu woyera
Lu 1:35 Mzimu woyera udzakuphimba
Lu 3:22 mzimu woyera ngati nkhunda
Lu 11:13 Atate adzapereka mzimu woyera
Yoh 14:26 mzimu woyera udzakuphunzitsani
Mac 1:8 mukadzalandira mzimu woyera
Mac 2:4 anadzazidwa ndi mzimu woyera
Mac 5:32 mzimu woyera, Mulungu wapereka
Aef 4:30 musamamvetse chisoni mzimu woyera
MZINDA
, Lu 4:43 kukalengeza uthenga kumizinda ina
Ahe 11:10 mzinda wokhala ndi maziko
N
NAINI
, Lu 7:11 kupita kumzinda wa Naini
NAMA
, Miy 19:22 kusiyana nʼkukhala wonama
Akl 3:9 Musamanamizane
Tit 1:2 Mulungu amene sanganame
NAMWALI
, Mt 25:1 ndi anamwali 10
NANGULA
, Ahe 6:19 chili ngati nangula
NATANI
, 2Sa 12:7 Natani: Munthuyo ndi iweyo
NDAKATULO
, Mac 17:28 mmene andakatulo ena ananenera
NDALAMA
, Mla 7:12 ndalama zimatetezera
Mla 10:19 ndalama zimathandiza chilichonse
Lu 14:28 kukhala pansi nʼkuwerengera ndalama
1Ti 6:10 kukonda ndalama
Ahe 13:5 Musamakonde ndalama
NDEKHA
, Yoh 16:32 sindikhala ndekha
NDENDE
, Mt 25:36 Ndinali mʼndende, munadzandiona
Mac 5:18 atumwiwo anawatsekera mʼndende
Mac 5:19 anatsegula zitseko za ndendeyo
Mac 12:5 ali mʼndende, mpingo unkapemphera
Mac 16:26 maziko a ndende anagwedezeka
Ahe 13:3 Muzikumbukira ali mʼndende
Chv 2:10 apitiriza kuponya mʼndende
NDIDZAKHALA
, Eks 3:14 Ndidzakhala Amene Ndidzafune Kukhala
NDIFE
, Aro 14:8 tikafa, ndife a Yehova
NDODO
, Chv 12:5 adzakusa mitundu ndi ndodo
NDODO YACHIFUMU
, Ge 49:10 Ndodo yachifumu sidzachoka kwa Yuda
Sl 2:9 udzaiphwanya ndi ndodo yachifumu
NDUNA
, Mac 8:27 nduna ya ku Itiyopiya
NDUWIRA
, Eze 21:26 Chotsa nduwira, vula chisoti chachifumu
NEBUKADINEZARA
, Da 2:1 Nebukadinezara analota maloto
NENERA
, Miy 16:28 wonenera anzake zoipa
1Ak 4:13 Akamatinenera zoipa
Tit 2:8 ndipo asapeze chifukwa chotinenera
NENEREDWA
, 2Ak 6:8 poneneredwa zoipa
NENEZA
, Tit 1:7 wopanda chifukwa chomunenezera
Chv 12:10 woneneza abale athu waponyedwa pansi
NGALE
, Mt 7:6 kuponyera nkhumba ngale
Mt 13:45 akufunafuna ngale zabwino
NGʼAMBA
, Yow 2:13 Ngʼambani mitima yanu
NGAMILA
, Mt 19:24 kuti ngamila ilowe pakabowo
NGʼANJO
, Da 3:17 angatipulumutse mungʼanjo
NGʼOMBE
, Eks 21:28 ngʼombe yagunda mwamuna
De 25:4 Usamange ngʼombe pakamwa
Miy 7:22 kulondola mkaziyo, ngati ngʼombe
Ho 14:2 ngati ana a ngʼombe amphongo
1Ak 9:9 amangodera nkhawa ngʼombe?
NGONGOLE
, Miy 11:15 amalonjeza kuti adzapereka ngongole
Aro 1:14 ndili ndi ngongole kwa anzeru
Aro 13:8 musamakhale ndi ngongole iliyonse
NGʼUNGʼUDZA
, Nu 14:27 Aisiraeli akungʼungʼudza
1Ak 10:10 Tisakhalenso ongʼungʼudza
Afi 2:14 muzipewa kungʼungʼudza
Yuda 16 Anthu amenewa amangʼungʼudza
NINEVE
, Yon 4:11 kumvera chisoni Nineve?
NJALA
, Sl 37:19 nthawi ya njala, chakudya
Yes 65:13 adzadya, mudzakhala ndi njala
Amo 8:11 Osati njala ya chakudya kapena ludzu
Mt 24:7 Kudzakhala njala
NJENJEMERA
, Afi 2:12 kuchita mwamantha ndi kunjenjemera
NJIRA
, Miy 4:18 njira ya olungama
Miy 16:25 njira imene imaoneka
Yes 30:21 Yendani mʼnjira imeneyi
Yer 8:6 kunjira imene ambiri akuitsatira
Yow 2:7 Aliyense amayenda mʼnjira yake
Yoh 14:6 ndine njira, choonadi ndi moyo
Mac 9:2 aliyense wotsatira Njirayo
1Ak 10:13 adzapereka njira yopulumukira
Aga 6:1 kulowera njira yolakwika
NJOKA
, Ge 3:4 njokayo inauza mkaziyo kuti
Yoh 3:14 Mose anakweza njoka mʼmwamba
Chv 12:9 chinjokacho chinaponyedwa pansi
NKHANDWE
, Mt 8:20 Nkhandwe zili ndi mapanga
NKHANI
, Eks 23:1 Musafalitse nkhani yabodza
Miy 25:25 Nkhani yabwino yochokera kutali
Mac 15:32 anawakambira nkhani zambiri
NKHANZA
, Miy 11:17 wankhanza amadzibweretsera mavuto
Miy 12:10 munthu woipa ndi wankhanza
NKHATA
, 1Ak 9:25 kuti akalandire nkhata yakumutu
NKHAWA
, 1Sa 1:15 ndili ndi nkhawa kwambiri
Sl 55:22 Umutulire Yehova nkhawa zako
Sl 94:19 Nkhawa zitandichulukira munanditonthoza
Miy 12:25 Nkhawa mumtima mwa munthu
Yes 28:16 amene adzade nkhawa
Yes 41:10 Usade nkhawa, ndine Mulungu wako
Mt 6:34 Musamadere nkhawa za mawa
Mt 10:19 musadzade nkhawa kuti mudzalankhula
Mko 4:19 nkhawa za moyo wamʼnthawi ino
Lu 8:14 chifukwa chotengeka ndi nkhawa, chuma
Lu 12:25 angatalikitse moyo chifukwa cha nkhawa?
Lu 21:34 mitima yanu isalemedwe ndi nkhawa
1Ak 7:32 mukhale opanda nkhawa
1Ak 7:32 wosakwatira amadera nkhawa za Ambuye
2Ak 11:28 Ndimadera nkhawa mipingo yonse
Afi 4:6 Musamade nkhawa ndi chilichonse
1At 5:14 muzilimbikitsa amene ali ndi nkhawa
NKHONDO
, 1Sa 17:47 Yehova ndiye mwini nkhondo
2Mb 20:17 simufunikira kumenya nkhondo
Sl 46:9 Akuthetsa nkhondo padziko
Yes 2:4 sadzaphunziranso nkhondo
Ho 2:18 ndidzathetsa nkhondo mʼdzikolo
1Ak 14:8 ndani angakonzekere nkhondo?
1Ti 6:12 Menya nkhondo ya chikhulupiriro
Yuda 3 kumenya nkhondo ya chikhulupiriro
Chv 12:7 kumwamba kunabuka nkhondo
Chv 16:14 nkhondo ya tsiku lalikulu la Mulungu
NKHOSA
, Sl 100:3 Ndife nkhosa zimene akuweta
Yes 53:7 nkhosa imene akufuna kuimeta
Eze 34:12 Ndidzasamalira nkhosa zanga
Mt 25:33 Adzaika nkhosa kudzanja lamanja
Lu 12:32 Musaope kagulu ka nkhosa inu
Yoh 21:16 Weta ana a nkhosa anga
NKHOSA ZINA
, Yoh 10:16 Ndili ndi nkhosa zina zimene si zamʼkhola
NKHUKU
, Mt 23:37 nkhuku imasonkhanitsa anapiye
NKHUMBA
, Lu 8:33 nʼkukalowa munkhumbazo
Lu 15:15 kuti azikaweta nkhumba
2Pe 2:22 nkhumba imene inasambitsidwa
NKHUNDA
, Mt 3:16 mzimu ukutsika ngati nkhunda
Mt 10:16 moona mtima ngati nkhunda
NKHUNGU
, Yak 4:14 nkhungu yooneka kanthawi
NKHUNI
, Miy 26:20 Ngati palibe nkhuni
NOWA
, Ge 6:9 Nowa anayenda ndi Mulungu
Mt 24:37 mofanana ndi masiku a Nowa
NSANJA
, Ge 11:4 Tiyeni timange nsanja
Miy 18:10 Dzina la Yehova, nsanja yolimba
Lu 13:4 anthu 18 nsanja inawagwera
NSANJA YA MLONDA
, Yes 21:8 pansanja ya mlonda
NSANJE
, Sl 37:1 kuchitira nsanje anthu
Sl 73:3 ndinkachitira nsanje onyada
Sl 106:16 anayamba kuchitira nsanje Mose
Miy 6:34 nsanje imachititsa mwamuna kukwiya
Miy 14:30 nsanje imawoletsa mafupa
1Ak 13:4 Chikondi sichichita nsanje
NSEMBE
, Le 7:37 nsembe yopsereza, nsembe yambewu
1Sa 15:22 Kumvera kumaposa nsembe
2Sa 24:24 Sindingapereke nsembe osalipira
1Mb 29:9 anapereka nsembezo kwa Yehova
Sl 40:6 nsembe zina, simunazifune
Sl 51:17 Nsembe zimene amasangalala nazo
Miy 15:8 Nsembe ya woipa ndi yonyansa
Yes 1:11 Nsembe zanu zopsereza zandikwana
Ho 6:6 chikondi chokhulupirika, osati nsembe
Aro 12:1 nsembe yamoyo, yoyera
Ahe 13:15 nsembe imene tikupereka kwa Mulungu
NSEMBE YACHAKUMWA
, Afi 2:17 ngati nsembe yachakumwa
NSOMBA
, Yon 1:17 chinsomba kuti chikameze Yona
Yoh 21:11 ukonde wodzaza nsomba 153
NTCHITO
, Ne 4:6 anapitiriza kugwira ntchitoyo
Sl 104:24 Ntchito zanu ndi zochuluka
Mla 2:24 wagwira ntchito mwakhama
Yoh 6:27 Musamagwirire ntchito chakudya
Yoh 14:12 ntchito zazikulu kuposa zimenezi
Aef 4:28 azigwira ntchito molimbikira
2At 3:10 wosagwira ntchito, asadye
Ahe 9:14 ku ntchito zakufa
1Pe 1:13 mugwire ntchito mwamphamvu
NTHAKA
, Mt 13:23 inafesedwa panthaka yabwino
NTHAMBI
, Yoh 15:4 nthambi singabereke payokha
NTHAWI
, Mla 3:1 nthawi yochitira chilichonse
Mla 9:11 nthawi komanso zosayembekezereka
Yes 46:10 Kutatsala nthawi ndimaneneratu
Da 7:25 nthawi imodzi, nthawi ziwiri
Yoh 7:8 nthawi yanga sinafike
1Ak 7:29 Nthawi yotsalayi yafupika
Aef 5:16 Muzigwiritsa ntchito bwino nthawi
1Pe 4:3 nthawi imeneyo munkachita
NTHAWI YOCHEPA
, Ahe 11:25 nʼkusangalala kwa nthawi yochepa
NTHAWI YOIKIDWIRATU
, Hab 2:3 akudikira nthawi yake yoikidwiratu
Lu 21:24 nthawi zoikidwiratu za anthu a mitundu
NTHITI
, Ge 2:22 anapanga mkazi kuchokera kunthiti
NTHUMWI
, Yoh 7:29 ndine nthumwi yake
NYADA
, Miy 8:13 Ndimadana ndi kunyada
Miy 16:5 Yehova amanyansidwa ndi wonyada
Miy 16:18 Kunyada kumawononga munthu
NYADIRA
, 2At 1:4 timanyadira tikamanena za inu
NYALANYAZA
, Da 6:4 Danieli sankanyalanyaza udindo wake
1Ti 4:14 Usamanyalanyaze mphatso
NYALE
, Sl 119:105 Mawu anu ndi nyale younikira
Mt 6:22 Nyale ya thupi ndi diso
Mt 25:1 anamwali 10 anatenga nyale zawo
NYAMA
, Ge 7:2 Pa nyama zosadetsedwa utengepo 7
Le 18:23 asamagone ndi nyama
Miy 23:20 amadya nyama mosusuka
Mla 3:19 Mapeto a anthu ndi nyama ndi ofanana
NYANGA
, Da 7:7 chilombo cha 4 cha nyanga 10
Da 8:8 nyanga yaikulu inathyoledwa
NYANJA
, Eks 14:21 mphepo yamphamvu igawe nyanjayo
Yes 57:20 oipa ali ngati nyanja ya mafunde
Chv 19:20 mʼnyanja ya moto yoyaka ndi sulufule
NYANSA
, Nu 21:5 chakudya chonyansachi chatikola
NYANSIDWA
, Aro 12:9 Muzinyansidwa ndi zoipa
NYENGERERA
, Miy 7:21 Wamunyengerera ndi mawu okopa
NYENGO
, Da 2:21 amasintha nthawi ndi nyengo
Mac 1:7 kudziwa nthawi kapena nyengo
1At 5:1 za nthawi ndi nyengo
NYENYEZI
, Sl 147:4 nyenyezi iliyonse amaitchula dzina
Mt 24:29 chikadzangotha, nyenyezi zidzagwa
Chv 2:1 nyenyezi 7 mʼdzanja lamanja
NYERERE
, Miy 6:6 Pita kwa nyerere waulesi iwe
Miy 30:25 Nyerere zimasonkhanitsa chakudya
NYEZIMIRA
, Yes 14:12 Wonyezimirawe, mwana wa
NYIMBO
, Ne 12:46 nyimbo zotamanda Mulungu
Sl 98:1 Imbirani Yehova nyimbo
Mac 16:25 kutamanda Mulungu poimba nyimbo
Akl 3:16 nyimbo zauzimu zoyamikira
NYOZA
, 1Sa 17:26 kuti azinyoza asilikali
2Sa 12:14 wanyoza kwambiri Yehova
Mt 5:11 osangalala pamene akukunyozani
Mko 3:29 aliyense amene wanyoza mzimu woyera
2Pe 2:10 kulankhula zinthu zonyoza
2Pe 3:3 azidzalankhula zinthu zonyoza
NYOZEDWA
, Yes 53:3 ananyozedwa ndipo ankamupewa
NYOZEKA
, 1Ak 1:28 Mulungu anasankha zonyozeka
NYUMBA
, 2Sa 7:13 adzamangira dzina langa nyumba
Sl 27:4 ndikhale mʼnyumba ya Yehova
Sl 101:2 Ndidzayenda mʼnyumba yanga
Sl 127:1 Yehova akapanda kumanga nyumba
Yes 56:7 idzatchedwa nyumba yopemphereramo
Yes 65:21 adzamanga nyumba nʼkumakhalamo
Lu 2:49 ndiyenera kupezeka mʼnyumba
Yoh 2:16 kukhala nyumba ya malonda
Yoh 14:2 Mʼnyumba ya Atate muli malo
Mac 5:42 kunyumba ndi nyumba
Mac 7:48 sakhala mʼnyumba zomangidwa
Mac 20:20 kukuphunzitsani kunyumba ndi nyumba
2Ak 5:1 tidzalandira nyumba yamuyaya
Ahe 3:4 nyumba inamangidwa ndi winawake
NZERU
, Sl 111:10 Chiyambi cha nzeru nʼkuopa Yehova
Sl 119:98 amandichititsa kukhala wanzeru
Miy 2:6 Yehova amapereka nzeru
Miy 2:7 amawasungira nzeru zopindulitsa
Miy 3:7 Usamadzione kuti ndiwe wanzeru
Miy 3:21 Uteteze nzeru zopindulitsa
Miy 4:7 Nzeru ndi chinthu chofunika kwambiri
Miy 8:11 nzeru ndi zabwino kwambiri
Miy 9:9 wanzeru adzawonjezera nzeru
Miy 13:20 woyenda ndi anzeru adzakhala wanzeru
Miy 24:3 Nzeru zimamanga nyumba
Miy 27:11 Mwana wanga, khala wanzeru
Mla 7:12 nzeru zimateteza
Mla 10:10 nzeru zimathandiza
Mt 11:19 nzeru imatsimikizirika ndi ntchito zake
Mt 24:45 kapolo wokhulupirika ndi wanzeru
Lu 15:17 Nzeru zitamubwerera ananena kuti
Lu 16:8 amachita mwanzeru kuposa ana a kuwala
Lu 16:8 mtumiki anachita zinthu mwanzeru
Lu 21:15 nzeru zimene otsutsa sangazikane
Mac 17:18 anzeru za Epikureya ndi Sitoiki
Aro 11:33 Nzeru zake nʼzozama
1Ak 2:5 musamakhulupirire nzeru za anthu
1Ak 2:6 osati nzeru za nthawi ino
1Ak 3:19 nzeru zamʼdzikoli nʼzopusa
Aef 5:15 muziyenda ngati anthu anzeru
Akl 2:3 nzeru ndiponso kudziwa zinthu
Akl 2:8 nzeru za anthu ndi chinyengo
Yak 1:5 ngati wina akusowa nzeru
Yak 3:17 nzeru ya kumwamba ndi yamtendere
NZIKA
, Afi 3:20 ife ndife nzika zakumwamba
O
ODZICHEPETSA
, Miy 11:2 odzichepetsa ali ndi nzeru
ODZIKUZA
, Yak 4:6 Mulungu amatsutsa odzikuza
ODZIPEREKA
, Aro 10:2 umboni kuti ndi odzipereka
Tit 2:14 odzipereka pa ntchito zabwino
OFATSA
, Sl 37:11 ofatsa adzalandira dziko lapansi
Zef 2:3 Funafunani Yehova ofatsa apadziko
OFULIDWA
, Yes 56:4 wanena kwa anthu ofulidwa
OGONA AMUNA ANZAWO
, 1Ak 6:9 amuna ogona amuna anzawo
OGWIDWA NDI ZIWANDA
, Mt 8:28 amuna ogwidwa ndi ziwanda
OIPA
, Sl 37:9 anthu oipa adzaphedwa
Sl 37:10 oipa sadzakhalaponso
Miy 15:29 ali kutali ndi anthu oipa
Yes 57:21 Oipa alibe mtendere
OITANIDWA
, Mt 22:14 oitanidwa ndi ambiri
OKANA KHRISTU
, 1Yo 2:18 okana Khristu aonekera
OKHULUPIRIKA
, 1Sa 2:9 Amateteza mapazi a okhulupirika
Sl 37:28 Yehova sadzasiya okhulupirika
OKHULUPIRIRA NYENYEZI
, Mt 2:1 okhulupirira nyenyezi anabwera
OKONDERA
, Yak 2:9 mukapitiriza kukhala okondera
OLA
, Mt 24:36 tsiku ndi ola palibe akudziwa
OLAMBIRA MAFANO
, 1Ak 6:9 olambira mafano sadzalowa mu Ufumu
OLAMULIRA
, 2Pe 2:10 amene amanyoza olamulira
OLANDIRA CHOLOWA
, Aro 8:17 olandira cholowa anzake a Khristu
Aga 3:29 mbadwa, olandira cholowa
OLOSERA ZAMʼTSOGOLO
, Le 19:31 anthu olosera zamʼtsogolo
OLUMALA
, Mt 15:31 olumala akuyenda
OMASULIRA
, 1Ak 12:30 onse sangakhale omasulira
OMBEZA
, De 18:10 pasapezeke aliyense woombeza
ONA
, Mt 6:1 pamaso pa anthu kuti akuoneni
Yoh 1:18 Palibe munthu anaonapo Mulungu
Yoh 14:9 waona ine waonanso Atate
ONAMIZIRA KUTI NDI KHRISTU
, Mt 24:24 kudzabwera onamizira kuti ndi Khristu
ONEKA
, 1Sa 16:7 Usaganizire mmene akuonekera
Miy 31:30 Munthu akhoza kuoneka ngati wabwino
Yoh 7:24 Siyani kuweruza potengera maonekedwe
ONEKERA
, Aro 8:19 ulemerero udzaonekere
2At 2:6 chikuchititsa kuti panopa asaonekere
ONETSA
, Yoh 5:20 amamuonetsa zimene amachita
ONYOZEKA
, Yes 57:15 nditsitsimutse mtima wa onyozeka
OPA
, 2Mb 20:15 Musaope gulu lalikululi
Sl 23:4 Sindikuopa kanthu
Sl 56:4 ndimadalira Mulungu, sindikuopa
Sl 118:6 Yehova ali kumbali yanga, sindidzaopa
Miy 29:25 Kuopa anthu ndi msampha
Lu 12:4 musamaope amene amapha thupi
OPANDA PAKE
, Lu 17:10 akapolo opanda pake
Aef 4:17 maganizo opanda pake
OPANGA MATENTI
, Mac 18:3 onse anali opanga matenti
OPHUNZIRA
, Mt 28:19 anthu a mitundu akhale ophunzira
Yoh 8:31 Mukasunga mawu, ndinudi ophunzira
Yoh 13:35 ndinu ophunzira ngati mukukondana
OPSA
, Sl 91:5 sudzaopa choopsa chilichonse
2Ak 11:26 zoopsa mumzinda, mʼchipululu
Ahe 10:31 Kulangidwa ndi Mulungu nʼkoopsa
OPSEZA
, Miy 3:23 udzayenda popanda chokuopseza
Mik 4:4 Ndipo sipadzakhala wowaopseza
Mac 4:17 tiyeni tiwaopseze
Aef 6:9 akapolo anu, musamawaopseze
1Pe 2:23 Pamene ankazunzidwa, sanaopseze
OSAKHALITSA
, Ahe 11:13 osakhalitsa mʼdzikolo
OSAKHULUPIRIRA
, 1Ak 6:6 anthu osakhulupirira?
2Ak 6:14 Musamangidwe mʼgoli ndi osakhulupirira
OSALUNGAMA
, Mac 24:15 olungama, osalungama
1Ak 6:9 anthu osalungama sadzalowa
OSANKHIDWA
, Mt 24:22 chifukwa cha osankhidwawo, masikuwo
Mt 24:31 adzasonkhanitsa osankhidwa ake
OSAPHUNZIRA
, Mac 4:13 anali osaphunzira
OSAUKA
, 1Sa 2:8 Amachotsa osauka paphulusa
Sl 9:18 Mulungu sadzaiwala osauka
Sl 69:33 Yehova akumvetsera osauka
Miy 30:9 ndisasauke nʼkukaba
Lu 4:18 ndilengeze uthenga kwa osauka
Yoh 12:8 Osaukawo muli nawo
2Ak 6:10 osauka koma olemeretsa anthu
2Ak 8:9 anakhala wosauka
Aga 2:10 tizikumbukira osauka
OWOLOWA MANJA
, De 15:8 muzithandiza mowolowa manja
Miy 11:24 amapereka mowolowa manja
Miy 11:25 wopereka mowolowa manja
1Ti 6:18 owolowa manja, okonzeka kugawira
Yak 1:5 amapereka mowolowa manja
OYAMBA
, Mt 19:30 oyamba adzakhala omaliza
OYAMIKIRA
, Akl 3:15 sonyezani kuti ndinu oyamikira
OYENERERA
, 2At 1:5 ndinu oyenerera Ufumu
OYERA
, Eks 26:33 Malo Oyera, Malo Oyera Koposa
Le 19:2 Mukhale oyera, ndine woyera
Da 7:18 oyera adzalandira ufumu
1Pe 1:15 khalani oyera mʼmakhalidwe
Chv 4:8 Woyera, woyera ndi Yehova
P
PACHABE
, Yes 45:19 Muzindifunafuna pachabe
Yes 65:23 Sadzagwira ntchito pachabe
PACHIKA
. Onani MTENGO.
Lu 23:21 Apachikidwe ameneyo
PAFUPI
, De 10:20 muzikhala naye pafupi kwambiri
Sl 145:18 Yehova ali pafupi ndi onse
PAMBANA
, 1Ak 12:31 ndikuonetsani njira yopambana
Chv 2:7 Amene wapambana pankhondo
Chv 6:2 anapambana pankhondo yolimbana
PAMSIKA
, Mac 17:17 ankakambirana ndi anthu pamsika
PANDUKA
, Nu 20:10 tamverani anthu opanduka inu!
1Sa 15:23 kupanduka nʼchimodzimodzi kuwombeza
Miy 1:32 kupanduka kwa anthu osadziwa
PANGANO
, Ge 15:18 anachita pangano ndi Abulamu
Yer 31:31 ndidzachita pangano latsopano
Lu 22:20 Kapu iyi ikuimira pangano latsopano
Lu 22:29 Choncho ndikuchita nanu pangano
PANIKIZA
, 1Ak 7:35 osati kuti ndikupanikizeni
PARADAISO
, Lu 23:43 ndi ine mʼParadaiso
2Ak 12:4 mʼparadaisomo anamva mawu
PASIKA
, Eks 12:11 Ameneyu ndi Pasika wa Yehova
Eks 12:27 nsembe ya Pasika
1Ak 5:7 nsembe yathu ya Pasika
PATSIDWA
, Lu 12:48 amene anapatsidwa zambiri
PATSOGOLO
, Afi 3:16 mmene tapitira patsogolo
PATULIKA
, Eks 25:8 Mundipangire malo opatulika
Sl 73:17 ndinalowa mʼmalo opatulika aulemerero
PAULO
. Onaninso SAULO, 1Ak 1:12 ndine wa Paulo
PEMBEDZERA
, 1Ti 2:1 kupereka mapembedzero, Yak 5:16 Pemphero lopembedzera
PEMPHA
, Sl 2:8 Tandipempha, ndikupatsa mitundu
Sl 20:5 Yehova akwaniritse zopempha zanu
Mt 6:8 amadziwa musanamupemphe
Mt 7:7 Pitirizani kupempha, adzakupatsani
Yoh 14:13 chimene mudzapemphe mʼdzina langa
2Ak 5:20 mʼmalo mwa Khristu tikupempha
Aef 3:20 kuposa zonse zimene timapempha
Fili 9 ndichite kukupempha mwachikondi
1Yo 5:14 chilichonse chimene tingamupemphe
PEMPHERA
, 2Mf 19:15 Hezekiya anayamba kupemphera
Da 6:13 akumapemphera katatu
Mt 6:9 inu muzipemphera chonchi
Mko 1:35 Kumeneko anayamba kupemphera
Lu 5:16 ankapita kwayekha kukapemphera
Aro 8:26 sitidziwa zotchula popemphera
Aro 12:12 Muzilimbikira kupemphera
1At 5:17 Muzipemphera nthawi zonse
PEMPHERERA
, Mt 5:44 kupempherera, akukuzunzani
Mko 11:24 mukupempha ndi kuzipempherera
Mac 12:5 mpingo unkamupempherera
2At 3:1 pitirizani kutipempherera
PEMPHERO
, Sl 65:2 Inu Wakumva pemphero
Sl 141:2 Pemphero likhale ngati zofukiza
Miy 15:8 pemphero la wowongoka mtima
Miy 28:9 pemphero lake limakhala lonyansa
Yak 5:15 Pemphero lachikhulupiriro
1Pe 3:7 mapemphero asatsekerezedwe
Chv 8:4 mapemphero a oyera
PEREKA
, Eks 21:36 azipereka ngʼombe
Sl 31:5 Ndikupereka mzimu wanga
Da 11:31 zoyenera kuperekedwa nthawi zonse
Da 12:11 zoyenera kuperekedwa nthawi zonse
Mt 22:21 perekani za Kaisara kwa Kaisara
Mt 26:21 mmodzi wa inu andipereka
Aro 6:13 muwapereke kwa Mulungu
Aef 6:7 Muzitumikira ambuye modzipereka
1Yo 3:16 tiyenera kupereka moyo wathu
PEREKA CHILANGO
, 2At 1:6 Mulungu adzapereka chilango
PEREWERA
, 1Ak 13:9 ndipo tikunenera moperewera
PETULO
, Mt 14:29 Petulo anayenda pamadzi
Lu 22:54 Petulo ankawatsatira chapatali
Yoh 18:10 Simoni Petulo, anali ndi lupanga
Mac 12:5 Petulo anatsekeredwa mʼndende
PEWA
, Yes 53:3 anthu ankamupewa
PHANGA
, Mt 21:13 phanga la achifwamba
PHATIKA
, Ge 2:24 nʼkudziphatika kwa mkazi wake
PHEDWA
, Sl 44:22 ngati nkhosa zokaphedwa
PHIMBA
, Le 16:34 machimo a Aisiraeli aziphimbidwa
2Ak 3:15 imakhalabe yophimba
1Yo 2:2 anakhala nsembe yophimba
PHINDU
, Miy 15:27 wopeza phindu mwachinyengo
Mla 5:10 sakhutira ndi phindu limene amapeza
1Ak 6:12 zololeka, koma si zonse zili zaphindu
PHIRI
, Sl 24:3 angakwere kuphiri la Yehova
Yes 2:3 Tiyeni kuphiri la Yehova
Yes 11:9 Sizidzavulazana mʼphiri langa loyera
Da 2:35 phiri lalikulu linadzaza dziko lonse
PHIRI LA MAOLIVI
, Lu 22:39 anapita kuphiri la Maolivi
Mac 1:12 kuphiri la Maolivi pafupi ndi Yerusalemu
PHOMPHO
, Chv 11:7 chatuluka muphompho
Chv 17:8 chatsala pangʼono kutuluka kuphompho
Chv 20:3 anamuponyera mʼphompho
PHUNZIRA
, De 4:10 anthu kuti aphunzire
Da 12:4 adzaphunzira bukuli mokwanira
Mac 17:11 mtima wofuna kuphunzira
Afi 4:9 zimene munaphunzira, muzichita
2Ti 3:7 amaphunzira koma satha
PHUNZITSA
, Eza 7:10 aziphunzitsa malamulo
Sl 143:10 Ndiphunzitseni zimene mumafuna
Miy 9:9 Phunzitsa wolungama
Miy 22:6 Phunzitsa mwana
Yer 31:34 Munthu sadzaphunzitsanso mnzake
Mki 2:7 Wansembe ayenera kuphunzitsa
Mt 7:29 ankawaphunzitsa monga waulamuliro
Mt 15:9 amaphunzitsa malamulo
Mt 28:20 muziwaphunzitsa azisunga zonse
Yoh 7:16 Zimene ine ndimaphunzitsa
Aro 2:21 umaphunzitsa ena, bwanji sudziphunzitsa?
1Ti 2:12 Sindikulola kuti mkazi aziphunzitsa
PHUNZITSIDWA
, Yes 54:13 azidzaphunzitsidwa ndi Yehova
PHWANDO
, Yes 25:6 Phwando la zakudya, la vinyo
Aro 13:13 Tizipewa maphwando oipa
Aga 5:21 maphwando oipa
PHWANYA
, Yes 42:3 lophwanyika sadzalithyola
PILATO
, Yoh 19:6 Pilato anati: Mutengeni
PINDULITSA
, Miy 14:23 Kugwira ntchito kumapindulitsa
1Ak 10:24 zopindulitsa iyeyo
PINIHASI
, Nu 25:7 Pinihasi mwana wa Eleazara
PITA PATSOGOLO
, 1Ti 4:15 kuti ukupita patsogolo
PITIRIRA
, 1Ak 4:6 Musapitirire zinthu zolembedwa
PITITSA PADERA
, Eks 23:26 simudzapezeka mkazi wopititsa padera
PONDAPONDA
, Ahe 10:29 wapondaponda Mwana
PONDEREZA
, Sl 72:14 kuti asaponderezedwe
Mla 4:1 oponderezawo anali ndi mphamvu
Mla 7:7 kuponderezedwa kungapangitse misala
POTOZA
, 2Ak 4:2 kupotoza mawu a Mulungu
PSINJIKA
, Yes 57:15 ndimakhala ndi anthu opsinjika
PULANI
, Eks 26:30 motsatira pulani yake
1Mf 6:38 mogwirizana ndi pulani yake
Miy 15:22 Mapulani sakwaniritsidwa
Miy 19:21 mapulani ambiri mumtima
PULAWO
, Lu 9:62 Aliyense wogwira pulawo
PULUMUKA
, Yer 39:18 sudzaphedwa. Udzapulumuka
Mt 24:22 kufupikitsidwa, palibe akanapulumuka
Afi 2:12 kunjenjemera kuti adzapulumuke
PULUMUTSA
, 2Sa 22:3 mpulumutsi wanga
2Mb 20:17 mmene Yehova angakupulumutsireni
Yes 59:1 silinafupike moti nʼkulephera kupulumutsa
Mt 16:25 akufuna kupulumutsa moyo wake
Lu 19:10 kudzapulumutsa anthu osochera
Mac 4:12 palibe amene angatipulumutse
Mac 5:31 Mtumiki Wamkulu ndi Mpulumutsi
1Ti 4:16 udzadzipulumutsa komanso okumvera
2Pe 2:9 amadziwa kupulumutsa anthu
PUMA
, Da 12:13 udzapuma, pamapeto udzauka
PUNTHWA
, Yak 3:2 Paja tonsefe timapunthwa
PUNTHWITSA
, Mt 13:41 zinthu zonse zopunthwitsa
PUPULUMA
, Miy 19:2 amachita zinthu mopupuluma
PURISILA
, Mac 18:26 Purisila ndi Akula
PUSA
, Sl 14:1 wopusa amati: Kulibe Yehova
Miy 19:3 Kupusa kwa munthu
1Ak 3:19 nzeru zamʼdzikoli nʼzopusa
PUSITSA
, Yer 17:9 Mtima ndi wopusitsa kwambiri
Yer 20:7 Mwandipusitsa inu Yehova
PUSITSIKA
, Aga 6:7 Mulungu sapusitsika
PWETEKA
, Aro 9:2 mtima umandipweteka
1At 4:6 Pasapezeke wopweteka mʼbale wake
PWETEKEDWA MTIMA
, Miy 14:10 Ngati mtima ukumupweteka amadziwa
Mt 26:75 kulira mopwetekedwa mtima
R
S
SABATA
, Eks 20:8 Muzikumbukira tsiku la Sabata
Mt 12:8 Mbuye wa Sabata
Mko 2:27 Sabata linakhalako chifukwa cha munthu
Lu 14:5 itagwera mʼchitsime tsiku la Sabata
Akl 2:16 akuweruzeni chifukwa cha sabata
Ahe 4:9 mpumulo wa sabata udakalipo
SAKA
, Le 17:13 akasaka, azithira magazi pansi
SAKAZA
, Lu 15:13 ndipo anasakaza chuma
SAMALA
, Miy 14:16 wanzeru amachita mosamala
Miy 14:16 wopusa amachita zinthu mosasamala
Mac 17:11 ankafufuza Malemba mosamala
Aef 5:15 samalani, muziyenda ngati anzeru
1Ti 4:16 uzisamala ndi zimene umachita
SAMALIRA
, 1Ak 12:25 ziwalo zake zizisamalirana
1Ti 5:8 ngati sasamalira a mʼbanja lake
SAMARIYA
, 2Mf 17:6 mfumu inalanda Samariya
Lu 10:33 panafika Msamariya wina
Yoh 4:7 mayi wa mu Samariya anafika
SAMBA
, Le 15:19 wodetsedwa chifukwa akusamba
Le 18:19 usagone ndi mkazi pamene akusamba
2Mf 5:10 mukasambe maulendo 7
SAMBITSA
, Sl 51:2 Mundisambitse nʼkuchotsa cholakwa
Yoh 13:5 nʼkuyamba kusambitsa mapazi
1Ak 6:11 mwasambitsidwa kukhala oyera
SAMISONI
, Owe 13:24 anamupatsa dzina, Samisoni
SAMUELI
, 1Sa 1:20 anamupatsa dzina lakuti Samueli
1Sa 2:18 Samueli ankatumikira ali mwana
SANGAFE
, 1Ak 15:53 nʼkukhala oti sangafe
SANGALALA
, 1Mb 28:9 uzimutumikira mosangalala
1Mb 29:9 anasangalala chifukwa cha nsembe
Yob 38:7 nyenyezi zinafuula mosangalala
Sl 32:1 Wosangalala, machimo ake akhululukidwa
Sl 37:4 Uzisangalala chifukwa cha Yehova
Sl 40:8 Ndimasangalala kuchita zimene mumafuna
Sl 94:12 Wosangalala ndi amene mumamulangiza
Sl 144:15 Osangalala ndi anthu
Sl 149:4 Yehova amasangalala ndi anthu ake
Miy 8:30 Ndinkakhala wosangalala pamaso pake
Miy 8:30 ankasangalala kwambiri ndi ine
Mla 2:24 amwe ndi kusangalala
Mla 8:15 kudya, kumwa ndi kusangalala
Yes 65:13 Atumiki anga adzasangalala
Yes 65:14 Atumiki anga adzafuula mosangalala
Eze 18:32 sindisangalala ndi imfa ya aliyense
Mt 5:3 Osangalala, amazindikira zosowa zauzimu
Lu 8:13 amalandira mawuwo mosangalala
Lu 15:7 kumwamba kudzakhala chisangalalo
Yoh 16:22 kuti musiye kusangalala
Mac 5:41 atumwiwo anali osangalala
Mac 20:35 Kupatsa kumatichititsa kusangalala
Aro 5:3 kumasangalala tikakumana ndi mavuto
Aro 7:22 ndimasangalala ndi malamulo a Mulungu
Aro 12:15 Muzisangalala ndi amene akusangalala
Aro 15:13 Mulungu akuthandizeni kusangalala
2Ak 9:7 munthu amene amapereka mosangalala
Afi 3:1 kusangalala monga otsatira a Ambuye
Afi 4:4 muzisangalala chifukwa cha Ambuye
Ahe 12:2 podziwa kuti adzasangalala, anapirira
Chv 18:7 kusangalala ndi chuma mopanda manyazi
SANGALATSA
, Sl 137:6 chimene chimandisangalatsa kwambiri
Sl 147:1 Kumutamanda nʼkosangalatsa
Miy 27:11 khala wanzeru usangalatse mtima
Lu 3:22 umandisangalatsa kwambiri
Yoh 8:29 zimamusangalatsa nthawi zonse
1Ak 10:33 Ndikuyesetsa kusangalatsa anthu
Aga 1:10 ndikungofuna kusangalatsa anthu
Aef 1:5 zimene zinamusangalatsa
Aef 6:6 pongofuna kuwasangalatsa
Akl 1:10 muzimusangalatsa pa chilichonse
3Yo 4 chimandisangalatsa, akuyendabe mʼchoonadi
SANKHA
, De 30:19 musankhe moyo
Yos 24:15 sankhani amene mukufuna kumʼtumikira
Yer 1:5 usanabadwe, ndinakusankha
Afi 1:10 muzitha kusankha zofunikadi
SARA
, Ge 17:19 Sara adzakuberekera mwana
1Pe 3:6 Sara ankamutchula kuti mbuyanga
SASATITSA
, Miy 29:21 Ngati akusasatitsa kapolo
SATANA
, Yob 1:6 Satana nayenso anafika
Zek 3:2 Satana, Yehova akudzudzule
Mt 4:10 Choka Satana! Malemba amati
Mt 16:23 Pita kumbuyo kwanga, Satana
Mko 4:15 Satana amabwera nʼkudzachotsa mawu
Aro 16:20 aphwanya Satana pansi pa mapazi anu
1Ak 5:5 mupereke munthu ameneyu kwa Satana
2Ak 2:11 Satana asatichenjerere
2Ak 11:14 Satana, mngelo wa kuwala
2At 2:9 mphamvu za Satana, zizindikiro zabodza
Chv 12:9 njoka yakale, Mdyerekezi, Satana
Chv 20:2 Satana, nʼkumumanga zaka 1,000
SAULI
, 1Sa 15:11 ndinaika Sauli kukhala mfumu
SAULO
, Mac 7:58 zinaika malaya pafupi ndi Saulo
Mac 8:3 Saulo anayamba kuzunza mpingo
Mac 9:1 Saulo anapitiriza kuopseza ophunzira
Mac 9:4 Saulo, nʼchifukwa chiyani ukundizunza?
SEFUKIRA
, Lu 6:45 zosefukira mumtima
SEKA
, Ge 18:13 Nʼchifukwa chiyani Sara waseka?
Sl 2:4 Wokhala pampando kumwamba adzaseka
Miy 14:13 akuseka, mtima ukumupweteka
SENAKERIBU
, 2Mf 19:16 mawu a Senakeribu onyoza
SIKELO
, Le 19:36 Muzikhala ndi masikelo olondola
Miy 11:1 amanyasidwa ndi masikelo achinyengo
SILIVA
, Miy 2:4 kuzifunafuna ngati siliva
Eze 7:19 Siliva wawo adzamutaya
Zef 1:18 Siliva kapena golide
SILO
, Ge 49:10 mpaka Silo atabwera
SIMONI
, Mac 8:18 Simoni ataona atumwiwo
SIMUNGACHITE
, Ge 18:25 Simungachite zimenezo
SINAI
, Eks 19:20 pamwamba pa phiri la Sinai
SINKHASINKHA
, Ge 24:63 kuti akasinkhesinkhe
SINTHA
, Mki 3:6 ndine Yehova, sindisintha
2At 2:2 asinthe maganizo anu
2Ak 13:11 pitirizani kusintha maganizo
SINTHANITSA
, Mt 16:26 asinthanitse ndi moyo wake
SITEPE
, Ge 28:12 Mʼmalotowo anaona masitepe
SIYA
, De 31:8 Sadzakutayani kapena kukusiyani
1Sa 12:22 Yehova sadzasiya anthu ake
Sl 27:10 bambo anga ndi mayi anga atandisiya
Sl 37:28 Yehova sadzasiya anthu ake
Yes 1:28 amene akusiya Yehova adzatha
Mt 19:9 wasiya mkazi wake
Mt 19:29 wasiya nyumba kapena minda
Yoh 8:29 Iye sanandisiye ndekha
1Ak 7:10 mkazi asasiye mwamuna wake
Aga 6:9 tisasiye kuchita zabwino
Afi 2:7 anasiya zonse nʼkukhala kapolo
Ahe 13:5 Sindidzakusiyani kapena kukutayani
1Pe 2:23 anasiya zonse mʼmanja
SIYANITSA
, Aro 8:39 kutisiyanitsa ndi chikondi
SOCHERA
, Sl 119:176 Ndasochera ngati nkhosa yotayika
Eze 34:4 Nkhosa zosochera simunazifufuze
SOCHERETSA
, Mt 24:24 adzasocheretse ngakhale osankhidwawo
SODOMU
, Ge 19:24 ngati mvula ku Sodomu
2Pe 2:6 mizinda ya Sodomu ndi Gomora
Yuda 7 anthu amʼmizinda ya Sodomu
SODZA
, Lu 5:10 Kuyambira lero uzisodza anthu
SOLOMO
, 1Mf 4:29 anapatsa Solomo nzeru
Mt 6:29 Solomo mu ulemerero wake
SONKHANA
, Ahe 10:25 Tisasiye kusonkhana
SONKHANITSA
, Aef 1:10 kusonkhanitsa zinthu zonse
SONYEZA
, Lu 3:8 mubale zipatso zosonyeza kulapa
Mac 17:3 kusonyeza umboni wolembedwa
Aro 5:8 Mulungu akutisonyeza chikondi
2Ak 6:4 tikusonyeza mʼnjira iliyonse
SUKULU
, Yoh 7:15 popeza sanapite kusukulu
SUNGA
, Mt 28:20 muziwaphunzitsa kuti azisunga
Yoh 14:15 mudzasunga malamulo anga
SUNGA ZIFUKWA
, 1Ak 13:5 sichisunga zifukwa
SWEKA
, Miy 18:14 mtima wosweka ndani angaupirire
2Ak 11:25 Ngalawa inandiswekerapo
1Ti 1:19 chikhulupiriro chasweka ngati ngalawa
1Pe 3:7 chiwiya chosachedwa kusweka
T
TAFUNA
, Ahe 5:14 chakudya chotafuna
TALIKITSA
, Yes 54:2 Talikitsa zingwe za tenti yako
Mt 6:27 angatalikitse moyo pangʼono pokha
TAMANDA
, Sl 146:1 Moyo wanga utamande Yehova
Sl 147:1 Kuimba nyimbo zomutamanda
Sl 150:6 chilichonse chitamande Ya
Miy 27:2 Munthu wina akutamande
Miy 27:21 anthu akunena pomutamanda
Yuda 16 Amatamanda anthu kuti apeze phindu
Chv 19:1 Tamandani Ya!
TAMBALA
, Mt 26:34 tambala asanalire, undikana
TANGANIDWA
, Lu 10:40 Marita anatanganidwa
TARISI
, Yon 1:3 ananyamuka nʼkulowera ku Tarisi
TATALASI
, 2Pe 2:4 anawaponya mu Tatalasi
TAYA MTIMA
, 2Ak 4:1 tili ndi utumiki, sitikutaya mtima
2Ak 4:16 sitikutaya mtima, munthu wakunja akutha
TAYIKA
, Lu 15:24 anatayika, wapezeka
TCHIMO
, Sl 32:1 machimo ake akhululukidwa
Sl 38:18 Tchimo linkandisowetsa mtendere
Yes 1:18 machimo anu ndi ofiira
Yes 38:17 Machimo mwawaponyera kumbuyo
Yes 53:12 Ananyamula tchimo la anthu ambiri
Yer 31:34 machimo awo sindidzawakumbukiranso
Eze 33:14 nʼkusiya machimo akewo
Mko 3:29 mlandu wa tchimo losatha
Yoh 1:29 akuchotsa uchimo wa dziko
Yoh 15:22 sangakane tchimo lawo
Mac 3:19 machimo anu afafanizidwe
Aro 3:25 wosakwiya msanga, pokhululuka machimo
Aro 5:12 Uchimo unalowa mʼdziko
Aro 6:14 Uchimo usamakulamulireni
Aro 6:23 malipiro a uchimo ndi imfa
1Ti 5:24 machimo awo amadzaonekera
Yak 5:15 ngati anachita machimo
1Yo 1:7 akutiyeretsa ku machimo onse
1Yo 2:1 wina akachita tchimo
1Yo 5:17 pali tchimo losabweretsa imfa
TCHULA
, Aef 5:3 zisatchulidwe pakati panu
TEBULO
, Da 11:27 adzakhala patebulo limodzi
1Ak 10:21 muzidya patebulo la Yehova
TEMA
, Le 21:5 asamadzitemeteme thupi lawo
TEMBERERA
, Nu 23:8 Ndingathe bwanji kutemberera?
Aro 12:14 Muzidalitsa, osati kutemberera
TEMBEREREDWA
, Yoh 7:49 osadziwa Chilamulo ndi otembereredwa
TENGEKA
, Aef 4:14 tisamatengeke uku ndi uku
Ahe 2:1 tisatengeke pangʼonopangʼono
TENGERA
, Aro 12:2 Musamatengere nzeru za nthawi ino
TENTHETSANA
, Aro 1:27 nʼkumatenthetsana mwachiwawa
TENTI
, Sl 15:1 mlendo mutenti yanu?
Yes 54:2 Talikitsa zingwe za tenti
2Ak 12:9 zikhalebe ngati tenti
TERERA
, Sl 73:18 mwawaika pamalo oterera
TETEZA
, Miy 4:23 Uteteze mtima wako
Mla 7:12 nzeru zimateteza
TETEZEKA
, Miy 12:3 wotetezeka chifukwa chochita zoipa
Yes 25:4 Malo otetezeka kwa wosauka
THAMANGA
, 1Ak 9:24 Muzithamanga kuti mukalandire mphotoyo
Aga 5:7 Munkathamanga bwino
THANDIZA
, Mac 20:20 chilichonse chothandiza
1Ak 7:35 Ndikunenatu izi kuti ndikuthandizeni
Aga 6:1 kuthandiza ndi mzimu wofatsa
Aef 4:12 nʼcholinga choti athandize
2Ti 3:16 Malemba anauziridwa, ndi othandiza
THANDIZO
, Sl 46:1 Thandizo lopezeka mosavuta
THANTHWE
, De 32:4 Thanthwe, ntchito yake ndi yangwiro
Mt 7:24 anamanga nyumba yake pathanthwe
THAWA
, 1Ak 6:18 Thawani chiwerewere
THAWIRA
, Nah 1:7 amene amathawira kwa iye
THEDWA NZERU
, Yes 44:8 Ndipo musathedwe nzeru
THEKA
, Ge 18:14 pali chosatheka ndi Yehova?
2Ti 2:15 Chita chilichonse chotheka
THIRIRA
, 1Ak 3:6 Apolo anathirira
THOKOZA
, Mac 28:15 Paulo atawaona, anathokoza
1Ak 1:4 ndimathokoza Mulungu wanga
1Ti 1:12 Ndikuthokoza Khristu Yesu
THUPI
, Ge 2:24 adzakhala thupi limodzi
Mt 10:28 Musachite mantha ndi opha thupi
Mt 26:26 Mkate uwu ukuimira thupi langa
Aro 6:13 Matupi anunso muwapereke kwa Mulungu
Aro 8:5 otsatira zofuna za thupi
Aro 12:1 mupereke matupi ngati nsembe
1Ak 7:4 asakhale ndi ulamuliro pathupi lake
1Ak 12:18 Mulungu anaika ziwalo zonse za thupi
1Ak 15:44 Limakwiriridwa lili thupi la mnofu
Aga 5:19 ntchito za thupi zimaonekera
Afi 3:21 adzasintha thupi lathu lonyozekali
THYOLA
, Miy 29:1 oumitsa khosi adzathyoledwa
TIMOTEYO
, Mac 16:1 wophunzira, Timoteyo
1Ak 4:17 ndikukutumizirani Timoteyo
1Ti 1:2 Timoteyo, mwana wanga weniweni
TINGATHE
, Aga 6:10 ngati tingathe, tichitire onse zabwino
TIRIGU
, Mt 13:25 namsongole mʼmunda wa tiriguwo
TONTHOZA
, Yob 16:2 otonthoza obweretsa mavuto!
Sl 94:19 Nkhawa zitachuluka, munanditonthoza
Yes 49:13 Yehova watonthoza anthu ake
Yes 61:2 nditonthoze anthu onse amene akulira
Yer 31:15 Rakele wakana kutonthozedwa
2Ak 1:3 Mulungu amene amatitonthoza
2Ak 1:4 kutonthoza amene akuyesedwa
TONZA
, Miy 27:11 ndimuyankhe amene amanditonza
TOPA
, Yes 40:28 Iye satopa kapena kufooka
TSALA
, Mt 14:20 zinatsala madengu 12
Chv 12:17 mbadwa zimene zinatsala
TSANKHO
, Mac 10:34 Mulungu alibe tsankho
TSANZIRA
, 1Ak 11:1 Muzitsanzira ine
Aef 5:1 muzitsanzira Mulungu ngati ana ake
Ahe 13:7 tsanzirani chikhulupiriro chawo
TSATANETSATANE
, Lu 1:3 ndikulembereni mwatsatanetsatane
TSATIRA
, Mt 4:20 anasiya maukonde nʼkumutsatira
Mt 19:21 ukhale wotsatira wanga
Yoh 10:27 Nkhosa zanga zimanditsatira
Chv 14:4 amatsatira Mwanawankhosa kulikonse
TSAYA
, Mt 5:39 akakumenyani patsaya lakumanja
TSEKA
, 1Pe 2:15 kuti muwatseke pakamwa
TSIKU
, Sl 84:10 tsiku limodzi mʼmabwalo anu
Eze 4:6 tsiku limodzi, chaka chimodzi
Mt 24:36 tsiku ndi ola, palibe akudziwa
2Pe 3:8 tsiku limodzi, zaka 1,000
TSIKU LA YEHOVA
, Yow 2:1 tsiku la Yehova lili pafupi
Amo 5:18 chidzakuchitikireni pa tsiku la Yehova?
Zef 1:14 Tsiku la Yehova lili pafupi
1At 5:2 tsiku la Yehova lidzabwera ngati wakuba
2At 2:2 tsiku la Yehova lafika
2Pe 3:12 kumbukirani tsiku la Yehova
TSIKU LOBADWA
, Ge 40:20 tsiku lokumbukira kubadwa kwa Farao
Mt 14:6 tsiku lobadwa la Herode
TSIMIKIZA
, Mac 17:31 watsimikiza pomuukitsa
TSIMIKIZA MTIMA
, Aro 8:38 ndatsimikiza mtima kuti
1At 1:5 tinalalikira motsimikiza mtima
TSIRIZA
, Yes 2:2 Mʼmasiku otsiriza
TSITSI
, Mt 10:30 tsitsi lonse lamʼmutu mwanu
Lu 21:18 tsitsi lamʼmutu mwanu
1Ak 11:14 ngati mwamuna ali ndi tsitsi lalitali
TSITSIMULA
, Mt 11:28 Bwerani, ndidzakutsitsimulani
TSITSIMUTSA
, Yes 57:15 nditsitsimutse onyozeka
Mac 3:19 nyengo zotsitsimutsa zibwere
TSOGOLERA
, Sl 48:14 adzatitsogolera mpaka kalekale
Aro 12:8 Wotsogolera, azitsogolera mwakhama
1At 5:12 muzilemekeza amene amakutsogolerani
Ahe 13:7, 17 Muzikumbukira akukutsogolerani
Ahe 13:7, 17 Muzimvera amene akukutsogolerani
TSOGOLO
, Sl 73:17 ndinazindikira tsogolo lawo
Miy 24:20 woipa alibe tsogolo
TSOKA
, Miy 22:3 akaona tsoka amabisala
Yes 5:20 Tsoka amene akunena kuti
1Ak 9:16 Tsoka ngati sindilalikira
Chv 12:12 Tsoka dziko lapansi ndi nyanja
TSUTSA
, Lu 21:15 nzeru zimene otsutsa sadzazikana
Mac 17:7 akuchita zotsutsana ndi Kaisara
Aro 8:31 ndani adzatsutsana nafe?
1Ak 16:9 koma pali otsutsa ambiri
Afi 1:28 musaope amene akukutsutsani
1At 2:2 tinalimba mtima pamene ankatitsutsa
TUKWANA
, Yob 2:5 akutukwanani mʼmaso muli gwa!
Yob 2:9 Tukwanani Mulungu mufe!
Aef 5:4 zopusa, nthabwala zotukwana
Akl 3:8 pakamwa pasatuluke zotukwana
TULO
, Aro 13:11 nthawi yoti mudzuke ku tulo
TULUKANI
, Yes 52:11 tulukani, musakhudze chodetsedwa
Chv 18:4 Tulukani mwa iye anthu anga
TUMIKIRA
, Yos 24:15 amene mukufuna kumʼtumikira
1Sa 2:11 mwanayo anatsala nʼkumatumikira
1Mb 28:9 uzimutumikira ndi mtima wonse
Sl 100:2 Tumikirani Yehova mokondwera
Da 7:10 100 miliyoni ankatumikira
Mt 20:28 anabwera kudzatumikira
Aga 5:13 chizikulimbikitsani kutumikirana
1Pe 4:10 muzigwiritsa ntchito mphatso potumikirana
TUMIZA
, Yes 6:8 Kodi nditumize ndani?
U
UBATIZO
, Lu 3:3 ubatizo, chizindikiro cha kulapa
1Pe 3:21 ubatizo, ukupulumutsanso inuyo
UBWENZI
, Sl 25:14 amakhala naye pa ubwenzi
Miy 3:32 amakhala nawo pa ubwenzi
UBWEYA
, Owe 6:37 mame pa ubweya wokhawu
UCHI
, Eks 3:8 dziko loyenda mkaka ndi uchi
Miy 25:27 Si bwino kudya uchi wambiri
UCHIMO
, Ge 4:7 uchimo wakubisalira pakhomo
Aro 6:14 Uchimo usamakulamulireni
UDINDO
, Mac 1:20 Udindo wake monga woyangʼanira
UDZU
, Yes 65:25 Mkango udzadya udzu
1Ak 3:12 mitengo, udzu ndi ziputu
UFULU
, Aro 8:21 ufulu waulemerero wa ana
1Ak 9:18 ndisagwiritse ntchito molakwa ufulu
2Ak 3:17 pali mzimu, pali ufulu
1Pe 2:16 musamagwiritse ntchito ufulu
2Pe 2:19 akuwalonjeza ufulu
UFUMU
, Eks 19:6 mudzakhala ufumu wa ansembe
Da 2:44 Mulungu adzakhazikitsa ufumu
Da 7:14 anamupatsa ulamuliro, ulemu ndi ufumu
Da 7:18 oyera adzalandira ufumu
Mt 6:10 Ufumu wanu ubwere. Zofuna zanu
Mt 6:33 muziika Ufumu pamalo oyamba
Mt 21:43 Ufumu udzachotsedwa, nʼkuperekedwa
Mt 24:14 Uthenga wa Ufumu udzalalikidwa
Mt 25:34 Bwerani, lowani mu Ufumu
Lu 12:32 wavomereza kukupatsani Ufumu
Lu 22:29 ndikuchita nanu pangano la ufumu
Yoh 18:36 Ufumu wanga si wamʼdzikoli
Mac 1:6 mubwezeretsa ufumu panopa?
1Ak 15:24 adzapereka Ufumu kwa Mulungu
Aga 5:21 sadzalowa mu Ufumu wa Mulungu
Akl 1:13 nʼkutisamutsira mu ufumu
Chv 11:15 Ufumu wa dziko wakhala Ufumu
UKA
, Yoh 5:29 adzauka kuti alandire moyo
Yoh 11:24 adzauka mʼtsiku lomaliza
Yoh 11:25 Ine ndine kuuka ndi moyo
1Ak 15:13 ngati sadzauka, Khristu sanaukitsidwe
UKITSA
, Yoh 6:39 ndidzawaukitse pa tsiku lomaliza
Mac 2:24 Mulungu anamuukitsa
Mac 24:15 adzaukitsa olungama ndi osalungama
UKITSIDWA
, Mt 22:23 amati akufa sadzaukitsidwa
Mt 22:30 akadzaukitsidwa, sadzakwatira
1Pe 3:18 koma anaukitsidwa monga mzimu
UKONDE
, Lu 5:4 muponye maukonde muphe nsomba
UKWATI
, De 7:3 mgwirizano wa ukwati
Mt 22:2 mfumu inakonza phwando la ukwati
Yoh 2:1 ku Kana kunali ukwati
Ahe 13:4 Ukwati ukhale wolemekezeka
Chv 19:7 ukwati wa Mwanawankhosa
ULEMERERO
, Yoh 12:43 ankakonda ulemerero
Aro 3:23 amalephera kusonyeza ulemerero
Aro 8:18 powayerekezera ndi ulemerero
1Ak 10:31 zibweretse ulemerero kwa Mulungu
2Pe 2:10 Mulungu wawapatsa ulemerero
Chv 4:11 woyenera kulandira ulemerero
ULEMU
, Miy 5:9 usapereke ulemu kwa ena
Aro 12:10 Posonyezana ulemu
1At 5:13 Muziwasonyeza ulemu waukulu
1Ti 2:9 akazi ayenera kuvala mwaulemu
1Pe 3:2 khalidwe labwino komanso ulemu
1Pe 3:15 muziwayankha mwaulemu
ULERE
, Mt 10:8 Munalandira kwaulere
1Ak 9:18 ndikamalalikira uthenga kwaulere
Chv 22:17 madzi amoyo kwaulere
ULESI
, Miy 6:6 Pita kwa nyerere waulesi iwe
Miy 10:26 utsi umapweteka, ngati munthu waulesi
Miy 19:15 waulesi adzakhala ndi njala
Miy 19:24 waulesi amapisa dzanja lake mʼmbale
Miy 20:4 Waulesi salima nthawi yozizira
Mt 25:26 Kapolo woipa ndi waulesi
Aro 12:11 Khalani akhama osati aulesi
ULOSI
, 2Pe 1:19 mawu aulosiwa adzakwaniritsidwa
2Pe 1:20 palibe ulosi wa mʼMalemba
2Pe 1:21 ulosi sunachokere kwa anthu
ULULA
, Sl 32:5 Pamapeto pake ndinaulula tchimo
Miy 28:13 amawaulula adzachitiridwa chifundo
Mt 11:25 mwaziulula kwa ana angʼono
1Ak 2:10 Mulungu anatiululira zinthu zimenezi
Aef 3:5 sichinaululidwe kwa atumwi ndi aneneri
Yak 5:16 muululirane machimo anu poyera
ULUSI
, Nu 15:39 zizikhala ndi ulusi
UMBA
, Yes 64:8 ndife dongo, inu ndinu Wotiumba
Aro 9:21 woumba mbiya ali ndi ufulu
UMBONI
, Mt 24:14 ukhale umboni kwa anthu
Yoh 7:7 chifukwa ndimachitira umboni
Yoh 18:37 ndidzachitire umboni choonadi
Mac 10:42 kupereka umboni wokwanira
Mac 28:23 anachitira umboni mokwanira
UMITSA
, Ahe 3:13 chinyengo chisaumitse mtima
UMITSA MTIMA
, Mt 13:15 anthu aumitsa mitima
UMODZI
, Aef 4:3 Muziyesetsa kusunga umodzi
UMPHAWI
, Miy 30:8 Musandipatse umphawi
2Ak 8:2 anali pa umphawi wadzaoneni
UMUNTHU
, Aef 4:24 muvale umunthu watsopano
Akl 3:9 Vulani umunthu wakale
UNGATHE
, Miy 3:27 kuchita zabwino ngati ungathe
URIMU NDI TUMIMU
, Eks 28:30 Udzaike Urimu ndi Tumimu
USIKU
, Sl 19:2 usiku zimasonyeza nzeru zake
Aro 13:12 Usiku uli pafupi kutha ndipo masana
UTAWALEZA
, Ge 9:13 utawaleza, ukhala chizindikiro
UTHENGA
, Sl 112:7 Sadzaopa uthenga woipa
UTHENGA WABWINO
, Yes 52:7 mapazi obweretsa uthenga wabwino
Mt 24:14 Uthenga wabwino udzalalikidwa
Lu 4:43 Ndiyenera kulengeza uthenga wabwino
Aro 1:16 sindichita manyazi ndi uthenga wabwino
1Ak 9:16 ngati sindilalikira uthenga wabwino
1Ak 9:23 chifukwa cha uthenga wabwino
UTUMIKI
, Mac 20:24 ndimalize utumiki
Aro 11:13 ndimalemekeza utumiki wanga
2Ak 4:1 utumiki mogwirizana ndi chifundo
2Ak 6:3 asapezere chifukwa utumiki wathu
1Ti 1:12 anandipatsa utumiki
2Ti 4:5 uzikwaniritsa mbali zonse za utumiki
UTUMIKI WOPATULIKA
, Aro 12:1 nsembe yomwe ndi utumiki wopatulika
UZIDWA
, 1Mb 28:12 mapulani a zimene anauzidwa
UZIMU
, Mt 5:3 amazindikira zosowa zawo zauzimu
Aro 1:11 ndikupatseni mphatso yauzimu
1Ak 2:15 munthu wauzimu amafufuza
1Ak 15:44 limaukitsidwa thupi lauzimu
UZIRIDWA
, 2Ti 3:16 Malemba onse anauziridwa
UZIYA
, 2Mb 26:21 Uziya anakhala wakhate
V
VALA
, 1Ak 11:6 ngati mkazi savala kanthu kumutu
VINA
, Owe 11:34 mwana wake anabwera akuvina
VINYO
, Le 10:9 musamamwe vinyo
Sl 104:15 vinyo amasangalatsa mtima
Miy 20:1 amene amamwa vinyo wambiri
Miy 23:31 Usakopeke ndi kufiira kwa vinyo
Mla 10:19 vinyo amasangalatsa moyo
Yes 25:6 Phwando la vinyo wabwino
Ho 4:11 vinyo wakale, vinyo watsopano
Yoh 2:9 madzi amene anawasandutsa vinyowo
1Ti 5:23 uzimwa vinyo pangʼono
VOMEREZA
, Lu 23:51 sanavomereze chiwembu
Yoh 8:37 simukuvomereza zimene ndikuphunzitsa
2Ak 6:2 inoyo ndi nthawi yovomerezedwa
1Yo 1:9 tikavomereza machimo, adzatikhululukira
VOMEREZEKA
, Aef 5:10 kuti chovomerezeka nʼchiti
2Ti 2:15 usonyeze kuti ndiwe wovomerezeka
VULAZANA
, Yes 11:9 Sizidzavulazana, kuwonongana
VULAZIDWA
, Chv 13:3 unali utavulazidwa kwambiri
VUTA
, 1Yo 5:3 malamulo akewo si ovuta kuwatsatira
VUTIKA
, Aro 8:17 ngati tikuvutika naye limodzi
1Ak 12:26 ziwalo zina zonse zimavutika
Afi 1:29 mwayi wovutika chifukwa cha iye
1Pe 3:14 ngakhale mutavutika, mumasangalalabe
1Pe 4:18 wolungama angadzapulumuke movutikira
VUTO LOSAMVA
, Le 19:14 ali ndi vuto losamva
Yes 35:5 a vuto losamva adzayamba kumva
Mko 7:37 a vuto losamva akumva
VUTO LOSAONA
, Le 19:14 ali ndi vuto losaona musamamuikire
Yes 35:5 maso a anthu amene ali ndi vuto losaona
W
WAKHANDA
, 2Ti 3:15 Kuyambira uli wakhanda
WAKHATE
, Le 13:45 wakhate ankafuula
WAKUBA
, De 24:7 wakuba munthu ayenera kufa
Miy 6:30 Anthu sanyoza wakuba
Miy 29:24 wakuba amadzibweretsera mavuto
Mt 24:43 nthawi imene wakuba angabwere
1At 5:2 ngati wakuba usiku
WAKUFA
, Lu 15:24 mwana wangayu anali wakufa
WAMASIKU AMBIRI
, Da 7:9 Wamasiku Ambiri anakhala pampando
WAMBIRI
, Sl 72:16 padzakhala tirigu wambiri
WAMKULU
, Yoh 14:28 Atate ndi wamkulu kuposa ine
1Yo 3:20 ndi wamkulu kuposa mitima yathu
WAMʼMWAMBAMWAMBA
, Sl 83:18 Yehova, Wamʼmwambamwamba
Da 4:17 Wamʼmwambamwamba ndi Wolamulira
WAMNGʼONO
, Yes 60:22 Wamngʼono adzasanduka 1,000
Mko 10:20 kuyambira ndili wamngʼono
1Ti 4:12 poona kuti ndiwe wamngʼono
WANGWIRO
, Ahe 2:10 anakhala wangwiro
WANSEMBE
, Sl 110:4 wansembe mpaka kalekale
Ho 4:6 asamanditumikire ngati wansembe
Mki 2:7 Wansembe ayenera kuphunzitsa
WANTCHITO
, Lu 10:7 wantchito ayenera kulandira malipiro
WENIWENI
, 1Ti 6:19 agwire moyo weniweniwo
WERENGA
, De 17:19 aziliwerenga masiku onse
Mac 8:30 mukumvetsa zimene mukuwerengazo?
WERENGERA
, Lu 14:28 nʼkuwerengera ndalama
WERUZA
, Yes 26:9 mukaweruza dziko lapansi
Mt 7:2 mmene mumaweruzira ena
Lu 6:37 siyani kuweruza, simudzaweruzidwa
Lu 22:30 kuweruza mafuko 12
Yoh 5:22 wapereka udindo woweruza
Mac 17:31 tsiku limene akufuna kudzaweruza
Aro 14:4 kuti uweruze wantchito wa mnzako?
1Ak 6:2 oyerawo adzaweruza dziko
2Ak 1:9 taweruzidwa kuti tiphedwe
Yak 4:12 ndiwe ndani kuti uziweruza mnzako?
WETA
, Mac 20:28 muwete mpingo wa Mulungu
1Pe 5:2 Wetani gulu la nkhosa
WILO
, Eze 1:16 wilo lina lili pakati pa linzake
WINDO
, Mac 20:9 Utiko anakhala pawindo
WOBADWA YEKHA
, Yoh 1:18 mulungu wobadwa yekha
Yoh 3:16 anapereka Mwana wobadwa yekha
WODETSEDWA
, Le 13:45 nʼkumafuula kuti, wodetsedwa!
WODZIDALIRA
, Miy 14:16 wopusa amakhala wodzidalira
WOFUNDA
, Chv 3:16 chifukwa choti ndiwe wofunda
WOIPA
, Miy 15:8 Nsembe ya munthu woipa
Miy 29:2 munthu woipa akamalamulira
Yes 26:10 munthu woipa atachitiridwa zabwino
1Yo 5:19 lili mʼmanja mwa woipayo
WOKHOMETSA MSONKHO
, Mt 18:17 akhale ngati wokhometsa msonkho
Lu 18:11 Ndine wosiyana ndi wokhometsa msonkho
WOKHULUPIRIKA
, 2Sa 22:26 wokhulupirika, mumamuchitira
Sl 16:10 Simudzalola wokhulupirika aone dzenje
WOKOMA MTIMA
, Eks 34:6 Mulungu wachifundo, wokoma mtima
WOKONDEDWA
, Da 9:23 wokondedwa kwambiri
WOLA
, Aef 4:29 Mawu owola asamatuluke pakamwa
WOLANKHULA NDI MIZIMU
, De 18:11 wofunsira kwa wolankhula ndi mizimu
WOLEMEKEZEKA
, Mac 24:3 Wolemekezeka a Felike
WOMBOLA
, Sl 49:7 Palibe angawombole mʼbale
Ho 13:14 Ine ndidzawombola anthu
WOMVETSA CHISONI
, Aro 7:24 Munthu womvetsa chisoni ine!
WONONGA
, Eze 21:27 Ine ndidzawononga
Aro 14:20 Siyani kuwononga ntchito ya Mulungu
2Pe 3:7 kuwononga anthu osaopa Mulungu
Chv 11:18 muwononge amene akuwononga dziko
WONONGEKA
, 1Ak 15:42 limene limaukitsidwa silingawonongeke
WONYOZEKA
, 1Sa 2:8 Amadzutsa wonyozeka
Sl 41:1 moganizira munthu wonyozeka
WOONA
, Yoh 17:3 Mulungu yekhayo woona
WOPANDA NTCHITO
, Sl 119:141 wopanda ntchito ndi wonyozeka
WOPANDA NZERU
, Lu 12:20 Wopanda nzeru iwe
WOPEREKA MALAMULO
, Yak 4:12 Wopereka Malamulo alipo mmodzi
WOPHA ANTHU
, Yoh 8:44 wopha anthu kuchokera pachiyambi
WOPHA MNZAKE
, Nu 35:6 wopha mnzake azikathawirako
WOSACHEDWA KUKWIYA
, Miy 21:19 mkazi wosachedwa kukwiya
WOSACHIMWA
, Yob 14:4 angabereke munthu wosachimwa?
WOSADZIWA ZINTHU
, Sl 19:7 zimapatsa nzeru wosadziwa zinthu
Miy 22:3 Munthu wosadziwa zinthu
WOSAKA MBALAME
, Sl 91:3 mumsampha wa wosaka mbalame
WOSAKHULUPIRIRA
, 1Ak 7:12 mkazi wosakhulupirira
WOSALONGOSOKA
, 1At 5:14 muzichenjeza wosalongosoka
2At 3:6 muzipewa mʼbale wosalongosoka
WOSAMVERA
, Yoh 3:36 Wosamvera Mwanayo
WOSAMVERA MALAMULO
, 2At 2:3 wosamvera malamulo akuonekera
WOSAUGWIRA MTIMA
, Miy 14:29 wosaugwira mtima amasonyeza
WOSAYAMIKA
, Miy 29:21 adzakhala wosayamika
WOWERUZA
, Yes 33:22 Yehova ndi Woweruza wathu
Lu 18:2 woweruza wosaopa Mulungu
WOYAMBA
, Mko 9:35 woyamba ayenera kukhala wotsiriza
WOYAMBA KUBADWA
, Eks 11:5 woyamba kubadwa ku Iguputo adzafa
Akl 1:15 woyamba kubadwa wa chilengedwe
WOYANGʼANIRA
, 1Ti 3:1 akuyesetsa kuti akhale woyangʼanira
1Pe 2:25 mʼbusa ndi woyangʼanira miyoyo
Y
YA
, Eks 15:2 Ya, mphamvu ndi nyonga zanga
Yes 12:2 Ya, ndi mphamvu zanga
YABWINO
, Lu 4:13 mpaka nthawi ina yabwino
YAKA
, Aro 12:11 Yakani ndi mzimu
YAKOBO 1.
, Ge 32:24 kulimbana ndi Yakobo
YAKOBO 2.
, Lu 6:16 Yudasi mwana wa Yakobo
YAKOBO 3.
, Mac 12:2 anapha Yakobo
YAKOBO 4.
, Mko 15:40 Mariya mayi a Yakobo
YAKOBO 5.
, Mt 13:55 azichimwene ake si Yakobo?
Mac 15:13 Atamaliza, Yakobo anayankha
1Ak 15:7 anaonekera kwa Yakobo
Yak 1:1 Yakobo, kapolo wa Mulungu
YAMBA
, Zek 4:10 munayamba kumanga ndi zochepa
YAMBITSA
, Sl 94:20 akuyambitsa mavuto
YAMIKA
, Sl 92:1 Ndi bwino kuyamika inu
Aef 5:20 Nthawi zonse muziyamika Mulungu
YAMIKANI
, Yoh 11:41 Atate, ndikukuyamikani
YAMIKIRA
, Sl 27:4 ndiyangʼane kachisi moyamikira
Sl 95:2 pamaso pake moyamikira
1Ak 11:2 Ndikukuyamikirani, mukundikumbukira
YAMWITSA
, 1At 2:7 mmene mayi woyamwitsa
YANDIKIRA
, Sl 73:28 kuyandikira kwa Mulungu
YANGʼANIRA
, Ge 1:28 Muyangʼanirenso nsomba
Yes 60:17 mtendere kuti ukhale okuyangʼanira
Yoh 17:12 ndinali nawo, ndinkawayangʼanira
Mac 20:28 mzimu wakuikani kuti muziliyangʼanira
Mac 20:28 Muzidziyangʼanira nokha
1Pe 5:2 Monga oyangʼanira, muzigwira ntchito
YANGWIRO
, De 32:4 ntchito yake ndi yangwiro
YANKHA
, Miy 15:1 Kuyankha modekha kumabweza mkwiyo
Miy 15:28 wolungama amaganizira asanayankhe
Miy 18:13 akayankhira nkhani asanaimvetsetse
Yes 65:24 asanandiitane, ine ndidzayankha
Aro 14:12 aliyense wa ife adzayankha
Akl 4:6 mudziwe mmene mungayankhire
YANKHO
, Miy 15:23 amasangalala akapereka yankho
YAPADERA
, 2Ti 3:1 nthawi yapadera ndi yovuta
YEFITA
, Owe 11:30 Yefita analonjeza Yehova
YEHOSAFATI
, 2Mb 20:3 Yehosafati anachita mantha
YEHOVA
, Eks 3:15 Yehova ndi dzina langa
Eks 5:2 Yehova ndani? sindikumudziwa Yehova
Eks 6:3 dzina lakuti Yehova, sindinadzidziwikitse
Eks 20:7 dzina la Yehova molakwika
De 6:5 Muzikonda Yehova ndi mtima wonse
De 7:9 Yehova ndi woona, wokhulupirika
Sl 83:18 dzina lanu ndinu Yehova
Yes 42:8 Dzina langa ndine Yehova
Ho 12:5 Yehova wa magulu ankhondo
Mki 3:6 ndine Yehova, sindisintha
Mko 12:29 Yehova ndi mmodzi
YEMBEKEZA
, Sl 37:7 umuyembekezere moleza mtima
Mik 7:7 Ndidzayembekezera moleza mtima
Aro 8:25 zimene tikuyembekezera
YEMBEKEZERA
, Eks 21:22 avulaza mkazi woyembekezera
Miy 13:12 umayembekezera chikalephereka
Hab 2:3 atachedwa uziwayembekezerabe
Lu 3:15 anthu ankayembekezera Khristu
Lu 21:26 adzakomoka chifukwa choyembekezera
1At 5:3 mkazi woyembekezera
YENDA
, Ge 33:14 kuyenda kwa ziwetozi, anawa
De 8:16 mʼtsogolo zidzakuyendereni bwino
2Mb 16:9 Maso a Yehova akuyendayenda
Sl 1:3 zimene amachita zimamuyendera
Yes 48:17 kuti zinthu zikuyendereni bwino
Yes 53:6 Tonsefe tikungoyendayenda
Mik 6:8 uziyenda modzichepetsa
Yoh 6:19 Yesu akuyenda panyanja
YENERA
, Mt 10:37 ine ndi wosayenera
Lu 15:19 Si inenso woyenera kutchulidwa
Mac 5:41 anawaona kuti ndi oyenera
Mac 13:46 osayenera moyo wosatha
1Ak 9:27 ndisakhale wosayenera
1Ak 11:27 kumwa za mʼkapu mosayenera
1Ak 14:40 zonse zizichitika moyenera
1Ak 15:23 pa nthawi yoyenera
2Ak 3:5 oyenera kugwira ntchitoyi
Ahe 11:38 osayenera kukhala mʼdziko
Chv 4:11 Ndinu woyenera, inu Yehova
YENERERA
, Eks 18:21 usankhepo amuna oyenerera
Eze 21:27 amene ali woyenerera mwalamulo
Mt 10:11 muzifufuza woyenerera
Aga 6:1 amene ndi oyenerera mwauzimu
2Ti 2:2 oyenerera kuphunzitsa ena
YENGA
, Da 11:35 ntchito yoyenga ichitike
Zek 13:9 ndidzawayenga ngati siliva
Mki 3:3 adzakhala ngati woyenga zitsulo
YERA
, Yes 1:18 machimo adzayera kwambiri
Hab 1:13 Maso anu ndi oyera kwambiri
Zef 3:9 chikhale chilankhulo choyera
Mt 5:8 Osangalala ndi oyera mtima
Yoh 15:3 ndinu oyera kale chifukwa cha mawu
Ahe 12:14 Muziyesetsa kukhala oyera
YEREKEZERA
, Yes 46:5 mungandiyerekezere ndi ndani?
Aga 6:4 osati modziyerekezera ndi wina
YEREMIYA
, Yer 38:6 iwo anagwira Yeremiya
YERETSA
, 1Mf 9:3 Ndayeretsa nyumba wamangayi
Sl 51:2 Ndiyeretseni ku tchimo langa
Eze 36:23 Ndidzayeretsadi dzina langa
Da 12:10 Anthu ambiri adzadziyeretsa
Lu 11:2 dzina lanu liyeretsedwe
2Ak 7:1 tidziyeretse, tichotse choipitsa
Chv 7:14 mikanjo yawo nʼkuiyeretsa mʼmagazi
YERUSALEMU
, Yos 18:28 Yebusi, kutanthauza Yerusalemu
Da 9:25 Yerusalemu amangidwenso
Mt 23:37 Yerusalemu, wopha aneneri
Lu 2:41 ankakonda kupita ku Yerusalemu
Lu 21:20 mukadzaona atazungulira Yerusalemu
Lu 21:24 Anthu adzapondaponda Yerusalemu
Mac 5:28 mwadzaza Yerusalemu yense
Mac 15:2 atumwi ndi akulu ku Yerusalemu
Aga 4:26 Yerusalemu wamʼmwamba
Ahe 12:22 mwafika ku Yerusalemu wakumwamba
Chv 3:12 Yerusalemu Watsopano akutsika
Chv 21:2 Yerusalemu Watsopano ngati mkwatibwi
YESA
, Miy 27:21 munthu amayesedwa
Mki 3:10 Ndiyeseni pa nkhani imeneyi
Lu 8:13 nthawi yoyesedwa ikafika
Mac 5:9 kuti muyese mzimu wa Yehova?
1Ak 10:9 Tisamamuyesenso Yehova
Aga 6:4 aliyense ayese zochita zake
1Ti 3:10 ayesedwe ngati ali oyenerera
Yak 1:3 chikhulupiriro pamene mukuyesedwa
YESETSA
, Lu 13:24 Yesetsani kuti mulowe pakhomo
Aro 12:9 nʼkumayesetsa kuchita zabwino
Aro 14:19 tiziyesetsa kukhala mwamtendere
YESU
, Mt 1:21 udzamupatse dzina lakuti Yesu
YEZEBELI
, 1Mf 21:23 Agalu adzamudya Yezebeli
Chv 2:20 ukulekerera Yezebeli
YEZEDWA
, Da 5:27 mwayezedwa pasikelo
YOBU
, Yob 1:9 Kodi Yobu amangoopa Mulungu?
Yak 5:11 Munamva za kupirira kwa Yobu
YOHANE 1.
, Mt 21:25 ubatizo wa Yohane unachokera kuti?
Mko 1:9 Yesu anabatizidwa ndi Yohane
YOHANE 2.
, Yoh 1:42 Simoni mwana wa Yohane
YOHANE 3.
, Mt 4:21 ndi mchimwene wake Yohane
YONA
, Yon 2:1 Yona anapemphera
YONATANI
, 1Sa 18:3 Yonatani ndi Davide anachita pangano
1Sa 23:16 Yonatani anathandiza Davide
YORODANO
, Yos 3:13 madzi a mu Yorodano aima
2Mf 5:10 mukasambe maulendo 7 mu Yorodano
YOSEFE
, Ge 39:23 Yehova anali ndi Yosefe
Lu 4:22 Kodi si mwana wa Yosefe?
YOSIYA
, 2Mf 22:1 Yosiya analamulira zaka 31
YOSWA
, Eks 33:11 Yoswa mwana wa Nuni
YUDA
, Ge 49:10 Ndodo yachifumu sidzachoka kwa Yuda
YUDASI
, Mt 27:3 Yudasi anakabweza ndalama 30
Z
ZABWINO
, Yes 26:10 woipa atachitiridwa zabwino
ZACHABECHABE
, Mla 1:2 zonse nʼzachabechabe
ZAKALE
, Yes 65:17 zakale sizidzakumbukiridwanso
ZAKEYU
, Lu 19:2 munthu wina dzina lake Zakeyu
ZAKUDYA ZABWINO
, Da 1:5 aziwapatsa zakudya zabwino
ZAKUFA
, Akl 3:5 ziwalo za thupi zakufa
ZAMBIRI
, 1Ak 15:58 muzikhala ndi zochita zambiri
ZAMTENGO WAPATALI
, Miy 3:9 zinthu zamtengo wapatali
ZATSOPANO
, Yes 42:9 ndikulengeza zatsopano
Mac 17:21 kumvetsera nkhani zatsopano
Chv 21:5 zimene ndikupanga ndi zatsopano
ZAZIKULU
, Aef 3:20 kuchita zazikulu kwambiri
ZEDEKIYA
, Yer 52:11 inachititsa khungu Zedekiya
ZEKARIYA 1.
, Lu 11:51 magazi a Zekariya
ZEKARIYA 2.
, Eza 5:1 Zekariya mdzukulu wa Ido
ZEKARIYA 3.
, Lu 1:5 wansembe dzina lake Zekariya
ZEMBA
, Yuda 4 alowa mozemba pakati panu
ZENGEREZA
, Yer 48:10 Munthu wozengereza
ZEU
, Mac 14:12 anayamba kumutchula kuti Zeu
ZIDA
, 2Ak 10:4 Zida zomenyera nkhondoyi
Aef 6:13 nyamulani zida zonse
ZIDA ZANKHONDO
, Aef 6:11 Valani zida zankhondo
ZIDZAKUYENDERA
, 1Mf 2:3 zidzakuyendera bwino
ZIKHALE MOMWEMO
, De 27:15 azidzayankha kuti, Zikhale momwemo!
ZIKONDWERERO
, Le 23:4 Zikondwerero za Yehova
ZIKUMBUTSO
, Sl 119:24 Ndimakonda zikumbutso
ZIKUYENDERENI
, 2Mb 20:20 zinthu zikuyendereni bwino
ZILAKOLAKO
, Aro 1:26 zilakolako zosalamulirika
ZILANKHULO
, Zek 8:23 ochokera mʼzilankhulo zonse
Mac 2:4 ankalankhula zilankhulo zosiyanasiyana
ZILIZONSE
, Afi 4:8 zinthu zilizonse zoona,
ZILOMBO
, Le 26:6 Ndidzachotsa zilombo zoopsa
Eze 34:25 ndidzachotsa zilombo zolusa mʼdzikomo
Da 7:3 zilombo 4 zinatuluka mʼnyanjayo
Ho 2:18 pangano ndi zilombo zakutchire
ZIMENE MUNGATHE
, 2Pe 3:14 yesetsani kuchita zimene mungathe
ZINDIKIRA
, 1Mf 8:47 nʼkuzindikira kulakwa kwawo
Sl 119:99 Ndine wozindikira kuposa aphunzitsi
Miy 19:11 Kuzindikira kumabweza mkwiyo
Da 12:3 Anthu ozindikira adzawala
Mt 24:15 wowerenga adzazindikire
ZINTHU
, Yes 61:6 zinthu zochokera kumitundu
1Ak 2:10 mzimu umafufuza zinthu zozama
Aga 6:2 Pitirizani kunyamulirana zinthu zolemera
Aef 1:18 zinthu zabwino zimene walonjeza
ZINYALALA
, 1Ak 4:13 tikuonedwa ngati zinyalala
Afi 3:8 ndimaziona ngati mulu wa zinyalala
ZIPATSO
, Ge 3:3 zipatso za mtengo wapakati
Mt 7:20 mudzawazindikira ndi zipatso
Mt 21:43 mtundu wobereka zipatso
Lu 8:15 nʼkubereka zipatso mopirira
Yoh 15:2 ibereke zipatso zambiri
Yoh 15:8 kubereka zipatso zambiri
ZIPATSO ZOYAMBIRIRA
, Aro 8:23 zipatso zoyambirira zomwe ndi mzimu
ZIPHASO
, Mt 17:25 amalandira ndalama za ziphaso
ZIPILALA
, Aga 2:9 anali ngati zipilala
ZIPINDA
, Yes 26:20 mukalowe mʼzipinda zamkati
ZIPUMI
, Eze 9:4 ulembe chizindikiro pazipumi
ZITSANZO
, 1Ak 10:6 zimenezi ndi zitsanzo kwa ife
ZITSEKO
, Yoh 20:19 anakhoma zitseko
ZIVOMEREZI
, Lu 21:11 Kudzachitika zivomerezi
ZIWALA
, Yes 40:22 ali ngati ziwala
Yow 1:4 zimene ziwala zowononga zinasiya
ZIWALO
, 1Ak 12:18 Mulungu anaika ziwalo za thupi
ZIWANDA
, 1Ak 10:20 amazipereka kwa ziwanda
1Ak 10:21 kudya patebulo la ziwanda
Aef 6:12 tikulimbana ndi ziwanda
Yak 2:19 ziwanda zimakhulupirira, zimanjenjemera
ZIWETO
, Miy 12:10 Wolungama amasamalira ziweto
ZIYONI
, Sl 2:6 mfumu ikulamulira ku Ziyoni
Sl 48:2 Phiri la Ziyoni
Yes 66:8 Ziyoni anabereka ana aamuna
Chv 14:1 ataimirira paphiri la Ziyoni
ZIZIKUYENDERA
, Yos 1:8 Ukamatero, zizikuyendera
ZIZINDIKIRO
, Lu 21:25 padzakhala zizindikiro
2At 2:9 zizindikiro zabodza, zodabwitsa
ZIZINDIKIRO PAKHUNGU
, Le 19:28 musamadzilembe zizindikiro pakhungu
ZOCHITIKA
, 1Ak 7:31 zochitika zapadzikoli zikusintha
ZODALIRIKA
, Sl 19:7 Zikumbutso za Yehova ndi zodalirika
ZOFIIRA
, Ge 25:30 ndigawireko mphodza zofiira
ZOFUFUMITSA
, Mt 13:33 Ufumu uli ngati zofufumitsa
1Ak 5:6 zofufumitsa zapangʼono zimafufumitsa
ZOFUNIKA
, Mt 23:23 zinthu zofunika za mʼChilamulo
Afi 1:10 zinthu zofunikadi kwambiri
ZOIPA
, De 23:13 muzikwirira zoipazo
1At 5:22 Muzipewa zoipa
ZOKONZEDWERATU
, Yes 65:11 mulungu wa Zokonzedweratu
ZOLAKWA
, Sl 40:12 Zolakwa zanga ndi zochuluka
Sl 130:3 mumayangʼanitsitsa zolakwa
Yes 53:5 chifukwa cha zolakwa zathu
Mt 6:12 Mutikhululukire zolakwa zathu
ZOLEMBEDWA
, 1Ak 4:6 Musapitirire zolembedwa
ZOLINGA
, Miy 16:2 Yehova amafufuza zolinga
ZOLUMIKIZANA
, Aef 4:16 ziwalo zolumikizana bwino
ZONYANSA
, Aro 1:24 kuti achite zonyansa
Aro 1:27 amuna okhaokha kuchitirana zonyansa
ZOONA
, Sl 15:2 kulankhula zoona mumtima mwake
Aef 4:25 aliyense wa inu azilankhula zoona
ZOOPSA
, Miy 3:25 Sudzaopa zoopsa zilizonse
ZOPANDA
, Afi 3:7 ndikuziona kuti nʼzopanda phindu
ZOPANDA PAKE
, Mt 15:9 Chilichonse amachita ndi chopanda pake
Lu 24:11 zinkaoneka ngati zopanda pake
ZOPANDA UMBONI
, 1Ti 1:4 nkhani zopanda umboni
ZOPEREKA
, 2Mb 31:10 anabweretsa zopereka
ZOSANGALATSA
, Lu 8:14 zosangalatsa za moyo
ZOSAONEKA
, 2Ak 4:18 zosaoneka, osati zooneka
ZOSATHEKA
, Mt 19:26 Kwa anthu nʼzosatheka
ZOSAYEMBEKEZEREKA
, Mla 9:11 zinthu zosayembekezereka
ZOSOKONEZA
, 1Ak 7:35 popanda zosokoneza
ZOSOWA
, Aro 12:13 mogwirizana ndi zosowa
ZOTOPETSA
, Mki 1:13 Koma ndiye nʼzotopetsa
ZOUNIKIRA
, Afi 2:15 mukuwala ngati zounikira
ZOVALA
, Ge 3:21 anawapangira zovala zazitali
ZOWAKOMERA
, 2Ti 4:3 zowakomera mʼkhutu
ZOZIKIKA
, 2Ak 10:4 zinthu zozikika molimba
ZUNGULIRA
, Yes 40:22 pamwamba pa dziko lozungulira
ZUNGUZA
, Yoh 6:60 Mawu amenewa ndi ozunguza
ZUNZA
, Sl 119:86 akundizunza popanda chifukwa
Yoh 15:20 Ngati anazunza ine
Mac 22:4 Ndinkazunza otsatira Njira
Aro 12:14 muzidalitsa amene akukuzunzani
1Ak 4:12 akamatizunza, timapirira
ZUNZIDWA
, Mt 5:10 azunzidwa chifukwa cha chilungamo
Mt 13:21 kuzunzidwa chifukwa cha mawuwo
Mko 4:17 kuvutitsidwa kapena kuzunzidwa
Mko 10:30 ana ndi minda, adzazunzidwa
2Ak 4:9 Timazunzidwa, Mulungu samatisiya
1Pe 2:19 akuzunzidwa, Mulungu amasangalala naye
ZUNZIKA
, Lu 21:25 anthu a mitundu ina adzazunzika
0-9
10
, Ge 18:32 chifukwa cha 10 amenewo
Chv 5:11 chinali 10 sauzande
12
, Mko 3:14 12, anawapatsa dzina lakuti atumwi
24
, Chv 4:4 mipando yachifumu 24, akulu 24
70
, Sl 90:10 Masiku a moyo amangokwana zaka 70
Da 9:2 Yerusalemu adzakhala bwinja zaka 70
Da 9:24 Pali milungu 70 imene yaikidwa
Lu 10:1 Ambuye anasankha anthu 70 nʼkuwatumiza
77
, Mt 18:22 osati maulendo 7 okha ayi, koma 77
100
, Mt 13:8 inabereka zipatso 100
Mt 18:12 nkhosa 100 ndipo imodzi nʼkusochera
Mko 10:30 kuwirikiza maulendo 100 mʼnthawi ino
300
, Owe 7:7 Ndidzakupulumutsani ndi amuna 300
500
, 1Ak 15:6 anaonekeranso kwa abale oposa 500
666
, Chv 13:18 Nambala yake ndi 666
1,000
, Sl 91:7 Anthu 1,000 adzagwa
Yes 60:22 adzasanduka anthu 1,000
2Pe 3:8 zaka 1,000 zili ngati tsiku limodzi
Chv 20:2 nʼkumumanga kwa zaka 1,000
Chv 20:4 analamulira ndi Khristu kwa zaka 1,000
4,000
, Mko 8:20 mitanda 7 nʼkudyetsa amuna 4,000
5,000
, Mt 14:21 anadya anali amuna 5,000
144,000
, Chv 7:4 anadindidwa chidindo, 144,000
Chv 14:3 144,000 anagulidwa padziko lapansi
185,000
, 2Mf 19:35 mngelo anapha asilikali 185,000