Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Kalozera wa Mawu a MʼBaibulo

A

ABBA

, Aro 8:15 timafuula kuti: Abba, Atate!

ABELE

, Ge 4:8 Kaini anamenya Abele nʼkumupha

Mt 23:35 Kuyambira magazi a Abele wolungama

ABIGAYELI

, 1Sa 25:3 Abigayeli anali wanzeru

ABULAHAMU

, Ge 21:12 anauza Abulahamu kuti mumvere

2Mb 20:7 Abulahamu, bwenzi lanu

Mt 22:32 Mulungu wa Abulahamu, Mulungu wa

Aro 4:3 Abulahamu anakhulupirira Yehova

ABWERERANE

, 1Ak 7:11 asakwatiwe,abwererane

ACHIBALE

, Mac 10:24 atasonkhanitsa achibale

ACHIFWAMBA

, Lu 10:36 anakumana ndi achifwamba

ACHIKULIRE

, Aef 4:13 tidzakhala anthu achikulire

ACHINYAMATA

, Sl 110:3 Gulu la achinyamata

ADAMU

, Ge 5:5 Adamu anakhala ndi moyo zaka 930

1Ak 15:22 anthu onse amafa chifukwa cha Adamu

1Ak 15:45 Adamu womalizira anakhala mzimu

1Ti 2:14 Adamu sanapusitsidwe, koma mkaziyo

ADANI

, Sl 110:2 Pita pakati pa adani ako

Mt 5:44 Pitirizani kukonda adani anu

Mt 10:36 adani adzakhala a mʼbanja lake

ADYO

, Nu 11:5 Tikukumbukira adyo

ADZADZIWA KUTI NDINE YEHOVA

, Eks 7:5 Aiguputo adzadziwa kuti ndine Yehova

Eze 39:7 a mitundu adzadziwa kuti ndine Yehova

ADZITAME

, 1Ak 1:31 adzitame mwa Yehova

AGOGO

, 1Ti 5:4 Azibwezera kwa agogo awo

AKANI

, Yos 7:1 Akani anatenga zina mwa zinthu

AKAZI

, De 31:12 amuna, akazi, ana ndi alendo

1Mf 11:3 akazi olemekezeka 700

Miy 31:3 Usamapereke mphamvu kwa akazi

1Ak 9:5 ufulu woyenda ndi akazi athu

Aef 5:22 Akazi azigonjera amuna awo

Aef 5:28 amuna azikonda akazi awo

AKAZI AMASIYE

, Yak 1:27 Kusamalira ana ndi akazi amasiye

AKHRISTU

, Mac 11:26 anayamba kutchedwa Akhristu

AKUBA

, Mt 6:20 kumene akuba sangathyole

1Ak 6:10 akuba sadzalowa mu Ufumu

AKUFA

, Mla 9:5 akufa sadziwa chilichonse

Lu 20:38 Mulungu wa amoyo, osati akufa

Aef 2:1 munali akufa mʼmachimo anu

1At 4:16 amene anafa mwa Khristu

Chv 14:13 akufa ali ogwirizana ndi Ambuye

AKULA

, Mac 18:2 anapeza Myuda dzina lake Akula

AKULU

, Tit 1:5 uike akulu mumzinda

AKULUAKULU

, Aro 13:1 azimvera olamulira akuluakulu

1Ak 14:20 khalani anthu akuluakulu

ALEFA

, Chv 1:8 ndine Alefa ndi Omega

ALEVI

, Eks 32:26 Alevi onse anapita kwa Mose

Nu 3:12 Aleviwo adzakhala anga

2Mb 35:3 anauza Alevi, alangizi a Aisiraeli onse

ALIBE

, Yak 2:15 mʼbale kapena mlongo alibe zovala

ALIPODI

, Yoh 7:28 amene anandituma alipodi

AMBUYE

, Mt 6:24 sangatumikire ambuye awiri

1Ak 8:5 milungu yambiri ndi ambuye ambiri

Akl 4:1 inunso muli ndi Ambuye kumwamba

AMBUYE WAMKULU KOPOSA

, Sl 73:28 Yehova Ambuye Wamkulu Koposa

Mac 4:24 Ambuye Wamkulu, inu munapanga

AME

, 1Ak 14:16 anganene bwanji Ame?

2Ak 1:20 kudzeranso mwa iye, Ame amanenedwa

AMUNA

, Aef 5:25 Amuna, pitirizani kukonda akazi anu

Akl 3:18 akazi, muzigonjera amuna anu

ANA

, Ge 6:2 ana a Mulungu woona anatenga akazi

De 31:12 Sonkhanitsani anthu, ana ndi alendo

1Sa 8:3 Ana akewa sanatsatire chitsanzo chake

Yob 38:7 ana a Mulungu anayamba kufuula

Sl 8:2 mʼkamwa mwa ana ndi mwa makanda

Yes 54:13 Ana ako azidzaphunzitsidwa

Yes 66:8 Ziyoni anabereka ana aamuna

Mt 11:16 ngati ana aangʼono mʼmisika

Mt 18:3 nʼkukhala ngati ana aangʼono

Mt 19:14 Asiyeni anawo ndipo musawaletse

Lu 10:21 zimenezi mwaziulula kwa ana

Aro 8:14 ndi anadi a Mulungu

Aro 8:21 ufulu waulemerero wa ana a Mulungu

1Ak 7:14 ana anu sakanakhala oyera

1Ak 14:20 Koma khalani ana pa zoipa

2Ak 12:14 si udindo wa ana kusunga chuma

Aef 6:1 Ana inu, muzimvera makolo anu

1Yo 3:2 tsopano ndife ana a Mulungu

ANA AAKAZI

, Yow 2:28 ana aamuna ndi ana aakazi adzalosera

Mac 21:9 ana aakazi 4 osakwatiwa

2Ak 6:18 ana anga aamuna ndi aakazi

ANA AMASIYE

, Yak 1:27 Kusamalira ana amasiye

ANA A NKHOSA

, Yes 40:11 adzasonkhanitsa ana a nkhosa

Yoh 21:15 Dyetsa ana a nkhosa anga

ANEFILI

, Ge 6:4 padziko lapansi panali Anefili

ANENERI

, 1Mf 18:4 Obadiya anabisa aneneri 100

Amo 3:7 Asanaulule chinsinsi kwa aneneri

Mac 10:43 Aneneri amachitira umboni

ANENERI ABODZA

, Mt 7:15 Chenjerani ndi aneneri abodza

Mt 24:11 Kudzakhala aneneri abodza

Mko 13:22 kudzabwera aneneri abodza

ANGELO

, Ge 28:12 angelo akukwera ndi kutsika

Yob 4:18 angelo ake amawapezera zifukwa

Mt 13:41 adzatumiza angelo ake

Mt 22:30 adzakhala ngati angelo akumwamba

Mt 24:31 angelo adzasonkhanitsa osankhidwa ake

1Ak 4:9 tili mʼbwalo lamasewera kwa angelo

1Ak 6:3 simukudziwa kuti tidzaweruza angelo?

Ahe 13:2 anachereza angelo mosadziwa

1Pe 1:12 Angelo amafunitsitsa atamvetsa

Yuda 6 angelo amene anasiya utumiki

ANGWIRO

, Mt 5:48 Choncho khalani angwiro

ANNA

, Lu 2:36, 37 mneneri wamkazi, Anna

ANSEMBE

, Mik 3:11 Ansembe ake amaphunzitsa

Mac 6:7 ansembe anakhala okhulupirira

Ahe 2:17 mkulu wa ansembe wachifundo

1Pe 2:9 ansembe achifumu, mtundu woyera

Chv 20:6 ansembe a Mulungu adzalamulira

ANTCHITO ANZAKE

, 1Ak 3:9 antchito anzake a Mulungu

ANTHU

, 1At 2:14 kuvutitsidwa ndi anthu akwanu

ANTHU ANZERU

, Lu 10:21 anthu anzeru mwawabisira

ANTHU WAMBA

, Mac 4:13 osaphunzira ndiponso anthu wamba

ANYAMATA

, Miy 20:29 Ulemerero wa anyamata

ANZAKE

, Miy 14:20 amakhala ndi anzake ambiri

Yoh 15:13 wapereka moyo chifukwa cha anzake

ANZANGA

, Yoh 15:14 mukhala anzanga

ANZANU

, Lu 16:9 Pezani anzanu ndi chuma chosalungama

ANZERU

, Yes 5:21 amadziona ngati anzeru

Mt 11:25 anthu anzeru ndi ozindikira mwawabisira

1Ak 1:26 anthu amawaona kuti ndi anzeru

APHUNZITSI

, Sl 119:99 kuposa aphunzitsi anga

Aef 4:11 kuti akhale abusa ndi aphunzitsi

APOLO

, Mac 18:24 Apolo, ankalankhula mwaluso

APOZI

, Miy 25:11 maapozi agolide mʼmbale zasiliva

ARAMAGEDO

, Chv 16:16 mʼChiheberi, Aramagedo

ARARATI

, Ge 8:4 chinaima pamapiri a Ararati

AREKABU

, Yer 35:5 vinyo pamaso pa Arekabu

AREOPAGI

, Mac 17:22 anaima mʼbwalo la Areopagi

ASADYE

, 2At 3:10 osagwira ntchito, asadye

ASODZI A ANTHU

, Mt 4:19 ndikusandutsani asodzi a anthu

ATATE

, Yes 9:6 dzina lakuti Atate Wamuyaya

Mt 6:9 Atate wathu wakumwamba

Mt 23:9 musamatchule aliyense kuti atate

Lu 2:49 ndiyenera kupezeka mʼnyumba ya Atate

Yoh 5:20 Atate amamuonetsa zonse

Yoh 10:30 Ine ndi Atate ndife amodzi

Yoh 14:6 Palibe amafika kwa Atate osadzera

Yoh 14:9 Amene waona ine waona Atate

Yoh 14:28 Atate ndi wamkulu kuposa ine

Yoh 14:28 ndikupita kwa Atate wanga

ATEMI

, Mac 19:34 Wamkulu ndi Atemi

ATUMIKI

, 1Ak 4:2 chofunika kwa atumiki

2Ak 3:6 oyenera kukhala atumiki

2Ak 6:4 tikusonyeza kuti ndife atumiki a Mulungu

ATUMIKI APAKACHISI

, Eza 8:20 panali atumiki apakachisi

ATUMIKI OTHANDIZA

, 1Ti 3:8 atumiki othandiza akhale

ATUMWI

, Mt 10:2 Mayina a atumwi 12 ndi awa

Mac 15:6 atumwi ndi akulu anasonkhana

1Ak 15:9 ndine wamngʼono kwambiri pa atumwi

2Ak 11:5 atumwi anu apamwambawo

AWIRIAWIRI

, Lu 10:1 nʼkuwatumiza awiriawiri

AYUDA

, Aro 3:29 kodi ndi Mulungu wa Ayuda okha?

B

BAALA

, Yer 19:5 ngati nsembe kwa Baala

BABELE

, Ge 11:9 unatchedwa Babele

BABULO

, Yer 51:6 Tulukani mʼBabulo nʼkuthawa

Yer 51:30 Asilikali a ku Babulo asiya kumenya

Yer 51:37 Babulo adzakhala milu yamiyala

Chv 17:5 Babulo Wamkulu, mayi wa mahule

Chv 18:2 Wagwa! Babulo Wamkulu wagwa

BADWA

, Yob 14:1 Munthu wobadwa kwa mkazi

Sl 51:5 Ndinabadwa ndili wochimwa

1Pe 1:3 anachititsa kuti tibadwenso mwatsopano

BALAMU

, Nu 22:28 bulu analankhula kwa Balamu

BAMBO

, Ge 2:24 adzasiya bambo ndi mayi ake

Sl 2:7 Lero, ine ndakhala bambo ako

Sl 89:26 Inu ndinu Bambo anga

Sl 103:13 Mofanana ndi bambo wachifundo

Lu 15:20 bambo anathamanga nʼkumukumbatira

BANJA

, 1Ak 7:25 amene sali pabanja

1Ak 7:38 amene sanalowe mʼbanja wachita bwino

Aef 2:19 ndinu a mʼbanja la Mulungu

Aef 3:15 amapangitsa banja kukhala ndi dzina

BARANABA

, Mac 9:27 Baranaba anamuthandiza

BARUKI

, Yer 45:2 Ponena za iwe Baruki, Yehova

BATI-SEBA

, 2Sa 11:3 Bati-seba, mkazi wa Uriya

BATIZA

, Mt 3:13 kwa Yohane kuti amubatize

Mt 28:19 Muziwabatiza mʼdzina la Atate

Mac 2:41 amene analandira mawu anabatizidwa

Mac 8:36 Chikundiletsa kubatizidwa nʼchiyani?

Aro 6:4 tinabatizidwa mu imfa yake

BAYA

, Zek 12:10 adzayangʼana amene anamubaya

BELISAZARA

, Da 5:1 Belisazara anakonza phwando

BEREKA

, Eks 23:26 mkazi wosabereka

De 7:14 sipadzapezeka chiweto chosabereka

Yes 54:1 mkazi amene sunaberekepo mwana

Yes 66:7 anabereka asanayambe kumva zowawa

BETELEHEMU

, Mik 5:2 Iwe Betelehemu Efurata

BETELI

, Ge 28:19 anawapatsa dzina lakuti Beteli

BEZALELI

, Eks 31:2 Inetu ndasankha Bezaleli

BISA

, Miy 28:13 Wobisa machimo sizidzamuyendera

BISIKA

, Sl 91:1 mʼmalo obisika a Wamʼmwambamwamba

BODZA

, Sl 101:7 wabodza sadzaima pamaso panga

Mt 26:59 ankafunafuna umboni wabodza

Yoh 8:44 Mdyerekezi, tate wake wa bodza

2At 2:11 kuti azikhulupirira bodza

BUKU

, Eks 32:33 ndimufufute mʼbuku langa

Yos 1:8 Buku la Chilamulo ili lisachoke

Mla 12:12 adzapitirizabe kulemba mabuku ambiri

Mki 3:16 Buku la chikumbutso linalembedwa

Mac 19:19 anasonkhanitsa mabuku nʼkuwatentha

Chv 20:15 dzina silinalembedwe mʼbuku la moyo

BULU

, Nu 22:28 anachititsa bulu kulankhula

Zek 9:9 mfumu ikubwera itakwera bulu

BUNTHWA

, Mla 10:10 Ngati nkhwangwa yabunthwa

BUULA

, Eks 2:24 Mulungu anamva kubuula

Yes 35:10 chisoni ndi kubuula zidzachoka

Eze 9:4 akuusa moyo komanso kubuula

Aro 8:22 chilengedwe chonse chikubuula

BWALO LA MILANDU

, Da 7:10 Bwalo la milandu linayamba kuzenga

BWANA

, Aro 14:4 udindo wa bwana kumuweruza

BWENZI

, 2Mb 20:7 Abulahamu, bwenzi lanu

Miy 16:28 amalekanitsa mabwenzi

Yak 4:4 akufuna kukhala bwenzi la dziko

BWERA

, Yes 55:1 bwerani mudzamwe madzi

Mac 1:11 adzabwera mʼnjira yofanana

Chv 22:17 amene wamva anene kuti, Bwera!

BWEREKA

, Sl 37:21 woipa amabwereka osabweza

Miy 22:7 wobwereka amakhala kapolo

BWERERA

, Yow 2:12 bwererani ndi mtima wonse

Mki 3:7 Bwererani ndipo ndidzabwerera kwa inu

Aga 4:9 kubwerera ku mfundo zamʼdzikoli

Ahe 10:39 obwerera kupita kuchiwonongeko

BWEZA

, Sl 37:21 woipa amabwereka osabweza

BWEZERA

, De 32:35 Kubwezera ndi kwanga

Sl 116:12 Yehova ndidzamubwezera chiyani

Miy 20:22 Ndidzabwezera choipa

Aro 12:19 Okondedwa, musamabwezere zoipa

Aro 12:19 Malemba amati: Kubwezera ndi kwanga

2At 1:8 adzabwezera chilango

BWINO

, Ge 1:31 zonse zinali zabwino

Ge 3:5 Mudzadziwa zabwino ndi zoipa

De 10:13 kuti zinthu zikuyendereni bwino

Mt 25:21 Wachita bwino kwambiri

Aro 5:7 angalimbe mtima kufera munthu wabwino

Aro 7:19 Zinthu zabwino zimene ndimafuna

Aga 6:10 tiyeni tichitire onse zabwino

C

CHACHINGʼONO

, Lu 16:10 wokhulupirika pa chachingʼono

CHAKA

, Nu 14:34 tsiku limodzi kuwerengera chaka

CHAKA CHA UFULU

, Le 25:10 Chizikhala Chaka cha Ufulu

CHAKHUMI

, Ne 10:38 magawo 10 a chakhumicho

CHAKUDYA

, Ne 9:15 chakudya chochokera kumwamba

Sl 37:25 ana ake akupemphapempha chakudya

Sl 145:15 Mumazipatsa chakudya

Yes 55:2 polipirira zinthu zimene si chakudya

Mt 4:4 sangakhale ndi moyo ndi chakudya

Mt 6:11 Mutipatse chakudya chimene tikufunikira

Mt 24:45 chakudya pa nthawi yoyenera

Yoh 4:34 Chakudya, kuchita zofuna zanu

Yoh 6:27 chakudya chomwe chimawonongeka

Yoh 6:35 Ine ndine chakudya chopatsa moyo

Mac 14:17 Anadzaza mitima yanu ndi chakudya

1Ak 8:13 ngati chakudya chikukhumudwitsa

CHAKUDYA CHAMADZULO

, 1Ak 11:20 Chakudya Chamadzulo cha Ambuye

CHAKUKHOSI

, Le 19:18 musasunge chakukhosi

CHALA

, Eks 8:19 Chimenechi ndi chala cha Mulungu!

Eks 31:18 yolembedwa ndi chala cha Mulungu

CHAMOYO

, Sl 150:6 Chamoyo chitamande Ya

CHANGWIRO

, Sl 19:7 Chilamulo cha Yehova ndi changwiro

CHEDWA

, Yes 46:13 chipulumutso sichidzachedwa

Hab 2:3 Ngakhale atachedwa uziwayembekezera

Hab 2:3 masomphenyawa sadzachedwa

Lu 12:45 Mbuye wanga akuchedwa kubwera

2Pe 3:9 Yehova sakuchedwa kukwaniritsa

CHEMWALI

, De 27:22 wogona ndi mchemwali wake

CHENJERA

, Miy 12:23 wochenjera amabisa

Miy 14:15 wochenjera amaganizira zotsatira

Miy 22:3 wochenjera akaona tsoka amabisala

Mt 10:16 muzichita zinthu mochenjera ngati njoka

CHENJEZA

, Eze 3:17 ukuyenera kuwachenjeza

Eze 33:9 ukachenjeza munthu woipa

1Ak 10:11 zinalembedwa kuti zitichenjeze

CHENJEZO

, Eze 33:4 koma osamvera chenjezolo

CHEPA

, Zek 4:10 munayamba ndi zinthu zochepa

CHEREZA

, Aro 12:13 Khalani ochereza

Tit 1:7, 8 akhale wochereza alendo

Ahe 13:2 Musaiwale kuchereza alendo

1Pe 4:9 Muzicherezana popanda kudandaula

3Yo 8 ndi udindo wathu kuwachereza

CHEZA

, Ge 19:14 ankangoona ngati akunena zocheza

Miy 26:19 Inetu ndimangochita zocheza

CHEZERA

, Mac 15:36 tikachezere abale, tikawaone

CHIBADWA

, Le 18:23 nʼzosemphana ndi chibadwa

Aro 1:26 akazi anasiya njira yachibadwa

Aro 1:27 Amunanso anasiya njira yachibadwa

Yuda 7 mʼnjira imene si yachibadwa

CHIDA

, Yes 54:17 Chida chilichonse sichidzapambana

CHIDAKWA

, Miy 23:21 chidakwa chidzasauka

1Ak 5:11 musamagwirizane ndi chidakwa

1Ak 6:10 zidakwa sizidzalowa mu Ufumu

CHIDANI

, Ge 3:15 Ndidzaika chidani

Aef 4:31 Chidani chachikulu, kupsa mtima

CHIDINDO

, Nym 8:6 pamtima pako ngati chidindo

2Ak 1:22 watidinda chidindo chake

2Ak 1:22 Chidindo chimenechi ndi mzimu woyera

Aef 1:13 ndi mzimu woyera anakuikani chidindo

Chv 7:3 mpaka titadinda chidindo pazipumi

CHIFANIZIRO

, Ge 1:26 munthu mʼchifaniziro chathu

Eks 20:4 Musadzipangire chifaniziro

Da 2:31 mukuona chifaniziro chachikulu

CHIFUKWA

, Mla 7:25 chifukwa chake zinthu zimachitika

Aro 13:5 chifukwa chabwino choti muzigonjera

CHIFUKWA CHOMVEKA

, Aro 1:20 alibenso chifukwa chomveka

CHIFUNDO

, De 4:31 Yehova ndi Mulungu wachifundo

1Mb 21:13 chifundo chake nʼchachikulu

Ne 9:19 simunawasiye chifukwa cha chifundo

Sl 78:38 ankawamvera chifundo

Miy 28:13 adzachitiridwa chifundo

Yes 55:7 abwerere, adzamuchitira chifundo

Mt 5:7 Osangalala ndi anthu achifundo

Mt 9:13 Ndikufuna chifundo, osati nsembe

Mt 20:34 Yesu atagwidwa ndi chifundo

Lu 6:36 achifundo mofanana ndi Atate wanu

Yak 2:13 Chifundo chimaposa chiweruzo

Yak 5:11 Yehova ndi wachikondi, wachifundo

1Yo 3:17 koma osamusonyeza chifundo

CHIFUNDO CHACHIKULU

, 2Ak 1:3 Bambo wachifundo chachikulu

Akl 3:12 valani chifundo chachikulu

CHIFUNIRO

, Mac 21:14 Chifuniro cha Yehova chichitike

Aro 12:2 muzindikire chifuniro cha Mulungu

Ahe 13:21 muchite chifuniro chake

CHIFUWA

, Yes 40:11 adzawanyamulira pachifuwa

CHIGOLOLO

, Eks 20:14 Musachite chigololo

Mt 5:28 wachita naye kale chigololo mumtima

Mt 19:9 nʼkukwatira wina wachita chigololo

1Ak 6:9 achigololo sadzalowa mu Ufumu

CHIGUMULA

, Ge 9:11 sizidzawonongedwanso ndi chigumula

Mt 24:38 Chigumula chisanafike, ankadya

2Pe 2:5 anabweretsa chigumula padziko

CHIHEMA

, Yos 18:1 chihema chokumanako

Sl 78:60 anasiya chihema cha ku Silo

Sl 84:1 ndimakonda chihema chanu

Chv 21:3 Taonani! Chihema cha Mulungu

CHIKHULUPIRIRO

, Sl 27:13 kukhala ndi chikhulupiriro

Lu 17:6 chikhulupiriro chofanana ndi kanjere

Lu 18:8 akadzafika, adzapezadi chikhulupiriro?

Aro 1:17 chifukwa cha chikhulupiriro chake

Aro 4:20 chikhulupiriro chinamupatsa mphamvu

2Ak 4:13 tili ndi chikhulupiriro, tikulankhula

2Ak 5:7 tikuyenda ndi chikhulupiriro

Aga 6:10 abale ndi alongo athu mʼchikhulupiriro

Aef 4:5 chikhulupiriro chimodzi, ubatizo umodzi

2At 3:2 si onse ali ndi chikhulupiriro

2At 3:4 tili ndi chikhulupiriro mwa inu

2Ti 1:5 chikhulupiriro chopanda chinyengo

Ahe 11:1 Chikhulupiriro ndi kusakayikira

Ahe 11:6 popanda chikhulupiriro nʼzosatheka

Yak 2:26 chikhulupiriro chopanda ntchito

1Pe 1:7 Chikhulupiriro chanu chayesedwa

CHIKOLE

, Miy 17:18 amalonjeza kuti akhala chikole

Aef 1:14 chikole chotsimikizira

CHIKONDI

, Nym 8:6 chikondi sichigonja

Mt 24:12 chikondi cha ambiri chidzazirala

Yoh 15:13 Palibe amene ali ndi chikondi kuposa

Aro 8:39 kutisiyanitsa ndi chikondi cha Mulungu

Aro 13:10 chikondi chimakwaniritsa lamulo

1Ak 8:1 chikondi chimalimbikitsa

1Ak 13:2 ngati ndilibe chikondi, zilibe ntchito

1Ak 13:8 Chikondi sichitha

1Ak 13:13 Koma chachikulu ndi chikondi

1Ak 16:14 Zonse muzizichita mwachikondi

Akl 3:14 chikondi chimagwirizanitsa mwamphamvu

1At 2:7 tinakusonyezani chikondi

1Pe 4:8 chikondi chimakwirira machimo

1Yo 4:8 Mulungu ndi chikondi

Chv 2:4 kusonyeza chikondi ngati poyamba

CHIKONDI CHACHIKULU

, Yak 5:11 Yehova ndi wachikondi chachikulu

CHIKONDI CHOKHULUPIRIKA

, Eks 34:6 Yehova, wachikondi chokhulupirika

Sl 13:5 ndakhulupirira chikondi chokhulupirika

Sl 136:1-26 Chikondi chokhulupirika chidzakhalapo

Ho 6:6 chikondi chokhulupirika, osati nsembe

CHIKUMBUMTIMA

, 1Pe 3:16 Muzikhala ndi chikumbumtima chabwino

1Pe 3:21 kupempha chikumbumtima chabwino

1Ti 4:2 chikumbumtima chili ngati chipsera

Aro 2:15 chikumbumtima chimawachitira umboni

Aro 13:5 chifukwanso cha chikumbumtima chanu

1Ak 8:12 nʼkumavulaza chikumbumtima chawo

CHILAKOLAKO

, Aef 2:3 motsatira zilakolako za thupi

Akl 3:5 chilakolako chosalamulirika

1At 4:5 chilakolako chosalamulirika chogonana

2Ti 2:22 thawa zilakolako za unyamata

Yak 1:14 amayesedwa ndi chilakolako

1Yo 2:16 thupi limalakalaka, maso amalakalaka

CHILALA

, Yer 17:8 pa chilala sadzada nkhawa

CHILAMULO

, Sl 19:7 Chilamulo cha Yehova ndi changwiro

Sl 40:8 chilamulo chanu chili mumtima mwanga

Sl 119:97 Ndimakonda kwambiri chilamulo chanu!

Yer 31:33 Ndidzaika chilamulo changa mwa iwo

Aro 10:4 Khristu ndi kutha kwa Chilamulo

Aga 3:24 Chilamulo chinatitsogolera kwa Khristu

Aga 6:2 mukukwaniritsa chilamulo cha Khristu

CHILANGO

, Miy 23:13 usalephere kumupatsa chilango

1Ak 11:29 akudzibweretsera chilango

Ahe 12:11 palibe chilango chosangalatsa

CHILANKHULO

, Ge 11:7 nʼkukasokoneza chilankhulo

Zef 3:9 ndidzasintha chilankhulo cha anthu

Chv 7:9 chilankhulo chilichonse

CHILEMA

, Le 22:21 nyama yopanda chilema

CHILIMWE

, Mt 24:32 chilimwe chili pafupi

CHILUNGAMO

, Yob 34:12 sakhotetsa chilungamo

Yob 40:8 Kodi ndine wopanda chilungamo?

Sl 37:28 Yehova amakonda chilungamo

Sl 45:7 Unkakonda chilungamo

Miy 29:4 Mfumu ikamachita zachilungamo

Mla 5:8 Ukaona zopanda chilungamo usadabwe

Yes 26:9 amaphunzira zokhudza chilungamo

Yes 32:1 Mfumu idzalamulira mwachilungamo

Yes 32:1 adzalamulira mwachilungamo

Yes 60:17 chilungamo chikhale okupatsa ntchito

Mik 6:8 kuti uzichita chilungamo

Lu 18:7 kuti chilungamo chachitika?

Mac 28:4 Chilungamo sichinamulole

Aro 9:14 Mulungu alibe chilungamo? Ayi ndithu

2Pe 3:13 mmenemo mudzakhala chilungamo

CHIMAKE

, 1Ak 7:36 pachimake pa unyamata

CHIMANJAMANJA

, De 16:16 kukaonekera chimanjamanja

CHIMBALANGONDO

, 1Sa 17:37 mʼkamwa mwa chimbalangondo

Yes 11:7 Ngʼombe ndi chimbalangondo

CHIMWA

, Ge 39:9 nʼkuchimwira Mulungu?

2Sa 12:13 Ndachimwira Yehova

1Mf 8:46 Anthu anu akakuchimwirani

Sl 1:5 ochimwa sadzapezekanso

Mt 18:15 ngati mʼbale wako wachimwa

Lu 15:7 munthu wochimwa amene walapa

Lu 18:13 ndikomereni mtima wochimwa ine

Yoh 9:31 Mulungu samvetsera ochimwa

Aro 3:23 onse ndi ochimwa ndipo amalephera

Aro 5:8 pamene tinali ochimwa, Khristu anatifera

Yak 4:17 koma sakuchichita, akuchimwa

CHIMWEMWE

, Ne 8:10 chimwemwe chimene Yehova amapereka

1At 1:6 chimwemwe cha mzimu woyera

1Ti 1:11 Mulungu wachimwemwe

CHIMWITSA

, Mt 5:29 diso limakuchimwitsa

CHINGALAWA

, Ge 6:14 Upange chingalawa

CHINGWE

, Mla 4:12 chopotedwa ndi zingwe zitatu

Yes 54:2 Talikitsa zingwe za tenti yako

CHINGWE CHA NYALE

, Yes 42:3 chingwe cha nyale sadzachizimitsa

CHINSINSI

, Miy 11:13 amasunga chinsinsi

Miy 20:19 amayendayenda nʼkumaulula zinsinsi

Miy 25:9 usaulule zachinsinsi zimene unauzidwa

Amo 3:7 Asanaulule chinsinsi chake kwa aneneri

Afi 4:12 ndaphunzira chinsinsi chokhala wokhuta

CHINSINSI CHOPATULIKA

, Aro 16:25 chinsinsi chopatulika chakhala chobisika

Aef 3:4 kuzindikira chinsinsi chopatulika

CHINTHU CHONYANSA

, Mt 24:15 mukadzaona chinthu chonyansa

CHINTHU CHOSEKETSA

, Yer 20:7 Ndakhala chinthu choseketsa

CHINYENGO

, Sl 34:13 milomo isalankhule chinyengo

Miy 15:27 wopeza phindu mwachinyengo

Da 6:4 Danieli sankachita zachinyengo

Mki 2:15 musachitire zachinyengo akazi anu

Aro 16:18 amagwiritsa ntchito mawu achinyengo

Aga 2:4 abale achinyengo analowa

Aef 4:25 tayani chinyengo, lankhulani zoona

2Pe 2:3 azidzagwiritsa ntchito mawu achinyengo

CHIONETSERO

, 1Ak 4:9 waika atumwi pachionetsero

CHIPEWA

, Aef 6:17 valani chipewa cha chipulumutso

CHIPHAMASO

, Miy 3:32 amanyansidwa ndi wachiphamaso

Miy 26:28 pakamwa polankhula mwachiphamaso

Miy 29:5 woyamikira mnzake mwachiphamaso

Aro 12:9 Chikondi chisakhale chachiphamaso

CHIPHUPHU

, Mla 7:7 chiphuphu chimawononga

CHIPILALA

, Ge 19:26 anasanduka chipilala

Eks 13:22 Chipilala cha mtambo sichinkachoka

CHIPONGWE

, Lu 18:32 akamuchitira chipongwe

Lu 22:63 anamuchitira zachipongwe, kumumenya

1Pe 2:23 sanabwezere zachipongwe

CHIPULULU

, Yes 35:1 Dera lachipululu lidzakondwa

Yes 35:6 mʼdera lachipululu mudzayenda mitsinje

Yes 35:6 Mʼchipululu mudzatumphuka madzi

Yes 41:18 Chipululu ndidzachisandutsa dambo

CHIPULUMUTSO

, Est 4:14 chipulumutso chidzachokera kwina

Sl 3:8 Chipulumutso chimachokera kwa Yehova

Lu 21:28 chipulumutso chanu chikuyandikira

Aro 13:11 chipulumutso chathu chili pafupi

Chv 7:10 Chipulumutso chachokera kwa Mulungu

CHIPUMI

, Eze 3:9 chipumi chikhale ngati mwala

CHIRITSA

, 2Mb 36:16 chiyembekezo cha kuchiritsidwa

Sl 147:3 Iye amachiritsa anthu osweka mtima

Miy 12:18 lilime la anzeru limachiritsa

Lu 4:23 Wochiritsa iwe, dzichiritse wekha

Lu 9:11 anachiritsa ofunika kuchiritsidwa

Lu 10:9 muzichiritsanso odwala

Mac 5:16 Ndipo onsewo ankachiritsidwa

Chv 22:2 Masamba ochiritsira anthu

CHISAUTSO

, Mt 24:21 kudzakhala chisautso chachikulu

Chv 7:14 atuluka mʼchisautso chachikulu

CHISHANGO

, Sl 84:11 Yehova ndi chishango

Aef 6:16 chishango chachikulu chachikhulupiriro

CHISOKONEZO

, 1Ak 14:33 Mulungu si wachisokonezo

CHISONI

, Sl 31:10 ndi wodzaza ndi chisoni

Sl 34:18 amapulumutsa odzimvera chisoni

Sl 38:6 ndili wachisoni tsiku lonse

Sl 51:17 kudzimvera chisoni mumtima

Sl 78:41 ankachititsa kuti amve chisoni

Sl 90:10 zodzaza ndi mavuto komanso chisoni

Mla 7:3 Ndi bwino kumva chisoni

Yes 51:11 chisoni ndi kulira zidzachoka

Mt 5:4 Osangalala ndi amene akumva chisoni

Mt 9:36 Ataona anthu, anawamvera chisoni

1Ak 15:19 ndife omvetsa chisoni

2Ak 2:7 angakhale ndi chisoni chopitirira malire

2Ak 7:9 Popeza munamva chisoni

Aef 4:30 musamamvetse chisoni mzimu woyera

1At 4:13 musakhale ndi chisoni chofanana

Ahe 4:15 amene sangatimvere chisoni

CHISOTI

, Miy 12:4 Mkazi wabwino ndi chisoti

Mt 27:29 analuka chisoti chachifumu chaminga

CHISWE

, Aro 16:4 anaika miyoyo yawo pachiswe

CHITA

, Eks 19:8 tidzachita zomwezo

Mla 12:13 zimene munthu akuyenera kuchita

Aro 7:15 zimene ndimafuna kuchita, sindizichita

2At 3:14 musiye kuchitira naye zinthu limodzi

1Yo 3:6 chizolowezi chochita tchimo

CHITETEZO

, Sl 18:2 Yehova ndi malo anga achitetezo

Yes 32:17 chilungamo chidzabweretsa chitetezo

Zef 3:12 adzapeza chitetezo mʼdzina la Yehova

Afi 3:1 Kubwereza kulemba ndi chitetezo

CHITIKA

, Yes 46:10 zimene zidzachitike

Yes 55:11 zimene ndinawatumizira zidzachitikadi

CHITIRA UMBONI

, Le 5:1 akachitire umboni za tchimolo

CHITITSA

, 1Sa 22:22 ndachititsa kuti anthu aphedwe

CHITSA

, Yes 11:1 idzaphuka pachitsa cha Jese

Da 4:15 musiye chitsa ndi mizu yake

CHITSAMBA

, Mac 7:30 anaonekera pachitsamba

CHITSANZO

, Yoh 13:15 ndakupatsani chitsanzo

2Ak 4:2 takhala chitsanzo chabwino

1Ti 4:12 ukhale chitsanzo kwa okhulupirika

2Ti 1:13 chitsanzo cha mawu olondola

Ahe 8:5 wapanga zonse motsatira chitsanzo

Yak 5:10 tengerani chitsanzo cha aneneri

1Pe 2:21 Khristu anakusiyirani chitsanzo

1Pe 5:3 chitsanzo chabwino kwa nkhosa

CHITSIME

, Miy 5:15 Imwa madzi amʼchitsime chako

CHITSIRU

, Miy 22:15 Uchitsiru umakhazikika

CHITSOTSO

, Mt 7:3 kachitsotso mʼdiso

CHITSULO

, Miy 27:17 Chitsulo chimanola chitsulo

Yes 60:17 Mʼmalo mwa chitsulo ndidzabweretsa

Da 2:43 chitsulo sichingasakanikirane ndi dongo

CHIWANDA

, Mac 16:16 chiwanda cholosera

CHIWAWA

, Ge 6:11 dziko linadzaza ndi chiwawa

Sl 5:6 Yehova amadana ndi anthu achiwawa

Sl 11:5 amene amakonda chiwawa

Sl 72:14 kuchitiridwa zachiwawa

CHIWEREWERE

, Mt 15:19 maganizo a chiwerewere

Mac 15:20 apewe chiwerewere ndi magazi

1Ak 5:9 musiye kugwirizana ndi achiwerewere

1Ak 6:9 Achiwerewere sadzalowa mu Ufumu

1Ak 6:18 Thawani chiwerewere

1Ak 10:8 tisamachite chiwerewere

Aga 5:19 ntchito za thupi ndi chiwerewere

Aef 5:3 Nkhani zachiwerewere zisatchulidwe

Akl 3:5 ziwalo zikhale zakufa ku chiwerewere

1At 4:3 Mulungu akufuna muzipewa chiwerewere

CHIWERUZO

, 1Pe 4:17 chiweruzo chiyambira panyumba yake

CHIWIYA

, Mac 9:15 ameneyu ndi chiwiya changa

CHIWOMBANKHANGA

, Yes 40:31 adzauluka ngati chiwombankhanga

CHIWONONGEKO

, Mt 25:46 kupita kuchiwonongeko

2At 1:9 chilango cha chiwonongeko chamuyaya

CHIYAMBI

, Mt 24:8 chiyambi cha mavuto aakulu

Mt 25:34 kuchokera pachiyambi cha dziko

CHIYEMBEKEZO

, Sl 146:5 chiyembekezo chake chili mwa Yehova

Aro 8:24 sichikhalanso chiyembekezo

Aro 12:12 Kondwerani ndi chiyembekezo

Aro 15:4 tikhale ndi chiyembekezo

Aef 1:18 chiyembekezo chimene wakupatsani

Aef 2:12 Munalibe chiyembekezo

Ahe 6:19 Chiyembekezo chili ngati nangula

CHIZINDIKIRO

, Eze 9:4 ulembe chizindikiro pazipumi

Mt 24:3 chizindikiro cha kukhalapo kwanu

Mt 24:30 chizindikiro cha Mwana wa munthu

2At 3:14 muikeni chizindikiro, osachita naye zinthu

Chv 13:17 kupatulapo ngati ali ndi chizindikirocho

CHOBISIKA

, Lu 8:17 palibe chobisika

CHODZITETEZERA PACHIFUWA

, Aef 6:14 mutavala chodzitetezera pachifuwa

CHOIPA

, Sl 101:3 Sindidzayangʼana choipa

Aro 12:17 Musamabwezere choipa pa choipa

CHOKA

, Yer 23:5 yochokera mʼbanja la Davide

1Ak 7:15 wosakhulupirirayo wasankha kuchoka

CHOLEMERA

, Ahe 12:1 titaye cholemera chilichonse

CHOLINGA

, Miy 16:4 chikwaniritse cholinga

Aro 8:28 mogwirizana ndi cholinga chake

Aro 9:11 Mulungu anasonyeza cholinga chake

Aef 3:11 nʼzogwirizana ndi cholinga chamuyaya

CHOLOWA

, Nu 18:20 ndine gawo ndi cholowa chako

Sl 127:3 Ana ndi cholowa

Mlr 3:24 Yehova ndi cholowa changa

1Pe 1:4 cholowa chosadetsedwa, chosasuluka

CHONDERERA

, Aro 8:34 amatilankhulira mochonderera

Ahe 5:7 anapereka mapemphero ochonderera

CHOONADI

, Sl 119:160 Mawu anu ndi choonadi

Miy 23:23 Gula choonadi ndipo usachigulitse

Yoh 4:24 kulambira ndi mzimu komanso choonadi

Yoh 8:32 Mudzadziwa choonadi, chidzakumasulani

Yoh 14:6 Ine ndine njira, choonadi ndi moyo

Yoh 16:13 mzimu wa choonadi, adzakutsogolerani

Yoh 17:17 Ayeretseni ndi choonadi

Yoh 18:38 Pilato anati: Choonadi nʼchiyani?

2Ak 13:8 sitingachite chotsutsana ndi choonadi

2Pe 1:12 ndinu olimba mʼchoonadi

3Yo 4 ana anga akuyendabe mʼchoonadi

CHOTSA

, 1Ak 5:13 Mʼchotseni munthu woipayo

CHULUKA

, Sl 40:12 Zolakwa zanga ndi zochuluka

Lu 12:15 atakhala ndi zochuluka chotani

Yoh 10:10 zikhale ndi moyo wochuluka

CHUMA

, Eks 19:5 mudzakhaladi chuma chapadera

Sl 62:10 Ngati chuma chanu chachuluka

Miy 2:4 kuzifufuza ngati chuma chobisika

Miy 10:2 Chuma chopeza pochita zoipa

Miy 11:4 Chuma chidzakhala chopanda phindu

Miy 11:28 Munthu amene amadalira chuma

Miy 18:11 Chuma cha munthu wolemera

Miy 30:8 Musandipatse umphawi kapena chuma

Mla 5:10 wokonda chuma sakhutira

Yer 9:23 wachuma asadzitame

Eze 28:5 unadzikuza chifukwa cha chuma

Mt 6:21 kumene kuli chuma chako

Mt 6:24 kutumikira Mulungu ndi Chuma

Mt 13:22 chinyengo champhamvu cha chuma

Mt 13:44 uli ngati chuma chobisika

Lu 6:45 amatulutsa zabwino mʼchuma chabwino

Lu 12:33 chuma chosatha kumwamba

Lu 14:33 akulephera kusiya chuma chake

Lu 16:9 Pezani anzanu ndi chuma chosalungama

2Ak 4:7 tili ndi chuma mʼziwiya zadothi

1Ti 6:17 achuma asakhale odzikweza

Ahe 10:34 chuma chabwino kwambiri

D

DALA

, Ahe 10:26 Ngati tikuchita machimo mwadala

DALAKIMA

, Lu 15:8 zokwana madalakima 10

DALIRA

, Sl 56:11 ndimadalira Mulungu; Sindikuopa

2Ak 1:9 tisamadzidalire, tizidalira Mulungu

Sl 62:8 Muzimudalira nthawi zonse

Miy 3:5 usamadalire luso lako

Miy 3:26 uzidzadalira kwambiri Yehova

Miy 28:26 wodalira mtima wake ndi wopusa

Aro 9:11 cholinga chidzadalira amene amaitana

1Pe 4:11 modalira mphamvu ya Mulungu

DALIRIKA

, Sl 33:4 chimene amachita ndi chodalirika

DALITSA

, Ge 1:28 Mulungu anawadalitsa

Ge 32:26 Sindikusiya mpaka utandidalitsa

Nu 6:24 Yehova akudalitseni

Owe 5:24 Mkazi wodalitsika kwambiri ndi Yaeli

Lu 6:28 kudalitsa amene akukutembererani

Yoh 12:13 Wodalitsidwa ndi amene akubwera

Aro 12:14 Pitirizani kudalitsa anthu

DALITSO

, De 30:19 ndaika dalitso ndi temberero

Miy 10:22 Madalitso a Yehova amalemeretsa

Mki 3:10 ngati sindikukhuthulirani madalitso

DAMA

. Onani CHIWEREWERE.

DANA

, Le 19:17 Usamadane ndi mʼbale wako

Sl 45:7 unkadana ndi zoipa

Sl 97:10 okonda Yehova, muzidana ndi zoipa

Miy 6:16 zinthu 6 zimene Yehova amadana nazo

Miy 8:13 kumatanthauza kudana ndi zoipa

Amo 5:15 Muzidana ndi choipa

Mt 24:9 adzadana nanu

Lu 6:27 amene akudana nanu

Yoh 7:7 Dziko limadana ndi ine

Yoh 15:25 Anadana nane popanda chifukwa

1Yo 3:15 amadana ndi mʼbale wake

DANDAULA

, Akl 3:13 chodandaulira za mnzake

Yuda 16 amakonda kungʼungʼudza, kudandaula

DANDAULIRA

, Aro 12:1 ndikukudandaulirani

DANDAULO

, Aro 8:26 madandaulo amene sitingawafotokoze

DAVIDE

, 1Sa 16:13 Samueli anadzoza Davide

Lu 1:32 mpando wachifumu wa Davide

Mac 2:34 Davide sanapite kumwamba

DAZI

, Le 13:40 Mwamuna akayamba dazi

2Mf 2:23 Choka kuno wadazi iwe!

DEKHA

, Miy 17:27 wozindikira amakhala wodekha

2Ti 2:24 ayenera kukhala wodekha

1Pe 3:4 atavala mtima wodekha

DERA

, Aro 15:23 sindinafikeko mʼmadera amenewa

DETSA

, Eze 39:7 Sindidzalolanso kuti lidetsedwe

DIKIRA

, 1Ak 7:5 ngati mwagwirizana kudikira

DINA

, Ge 34:1 Dina ankakonda kukacheza

DINARI

, Lu 7:41 ngongole ya madinari 500

DIPO

, Sl 49:7 kumuperekera dipo kwa Mulungu

Mt 20:28 kudzapereka moyo wake dipo

Aro 8:23 kutimasula ndi dipo

DISO

, Mt 5:38 Diso kulipira diso

Mt 6:22 diso likuyangʼana chimodzi

1Ak 12:21 Diso silingauze dzanja

1Ak 15:52 mʼkuphethira kwa diso

DOKOTALA

, Lu 5:31 abwino safunikira dokotala

DONGO

, Yes 45:9 Kodi dongo lingafunse woumba?

Yes 64:8 ndife dongo, inu ndinu Wotiumba

Da 2:42 chitsulo chosakanikirana ndi dongo

DONGOSOLO

, 1Ak 14:40 moyenera ndi mwadongosolo

Aef 1:10 akakhazikitse dongosolo

1Ti 3:2 wochita zinthu mwadongosolo

DORIKA

, Mac 9:36 wophunzira dzina lake Dorika

DOTHI

, Ge 2:7 anamuumba kuchokera kudothi

DWALA

, Sl 41:3 pamene akudwala pabedi lake

Yes 33:24 adzanene kuti: Ine ndikudwala

Yak 5:14 pali akudwala pakati panu?

DYERA

, Lu 12:15 chenjerani ndi dyera

1Ak 5:11 musiye kugwirizana ndi wadyera

1Ak 6:10 adyera sadzalowa mu Ufumu

Akl 3:5 dyera ndi kulambira mafano

DYERA MASUKU PAMUTU

, 2Ak 7:2 sitinadyere masuku pamutu

DYETSA

, Yoh 21:17 Yesu anati: Dyetsa ana a nkhosa

DZALA

, Mla 11:6 Dzala mbewu zako

Yes 65:22 sadzadzala kuti ena adye

1Ak 3:6 ndinadzala, Apolo anathirira

DZANJA

, Sl 145:16 Mumatambasula dzanja lanu

Yes 41:10 Ndikugwira mwamphamvu ndi dzanja

Zek 14:13 adzagwira dzanja la mnzake

Mt 6:3 dzanja lako lamanzere

Yoh 12:38 dzanja la Yehova laonetsedwa

DZANZI

, Sl 143:4 mtima wanga wachita dzanzi

DZAZA

, Ge 1:28 mudzaze dziko lapansi

DZENJE

, Miy 26:27 Amene akukumba dzenje

Da 6:7 mʼdzenje la mikango

Mt 15:14 onse awiri adzagwera mʼdzenje

DZIDZIMUTSA

, Lu 21:34 lingadzakufikireni modzidzimutsa

DZIKO

, Ge 1:28 mudzaze dziko lapansi

Eks 9:29 dziko lapansi ndi la Yehova

Yob 38:4 maziko a dziko lapansi

Sl 37:11 adzalandira dziko lapansi

Sl 37:29 adzalandira dziko lapansi

Sl 104:5 dziko silidzasunthidwa

Sl 115:16 dziko analipereka kwa anthu

Miy 2:21 owongoka mtima adzakhala padziko

Yes 45:18 anaumba dziko lapansi

Yes 66:8 dziko lingabadwe tsiku limodzi?

Mt 5:5 ofatsa adzalandira dziko

Lu 9:25 zonse zamʼdzikoli

Yoh 15:19 simuli mbali ya dziko

Yoh 17:16 Iwo sali mbali ya dziko

1Ak 2:14 wokonda zinthu zamʼdziko

1Ak 3:3 mukuganiza ngati anthu amʼdzikoli

1Yo 2:15 Musamakonde dziko

1Yo 2:17 dzikoli likupita

DZINA

, Ge 11:4 tidzipangire dzina kuti titchuke

Eks 3:13 nʼkundifunsa kuti, Dzina lake ndani?

Eks 3:15 Dzina langa ndi limeneli

Eks 9:16 dzina langa lilengezedwe

Eks 20:7 wogwiritsa ntchito dzina molakwika

1Sa 17:45 ndikubwera mʼdzina la Yehova

1Mb 29:13 kutamanda dzina lanu lokongola

Sl 9:10 odziwa dzina adzakukhulupirirani

Sl 79:9 Chifukwa cha dzina lanu

Miy 18:10 Dzina la Yehova ndi nsanja yolimba

Miy 22:1 Ndi bwino kusankha dzina labwino

Yer 23:27 anthu anga aiwale dzina langa

Eze 39:25 ndidzateteza dzina langa loyera

Mki 1:11 dzina langa lidzakwezeka

Mki 3:16 amene ankaganizira za dzina lake

Mt 6:9 dzina lanu liyeretsedwe

Yoh 12:28 Atate lemekezani dzina lanu

Yoh 14:14 Ngati mutapempha mʼdzina langa

Yoh 17:26 ndachititsa kuti adziwe dzina lanu

Mac 4:12 palibe dzina lina padziko lapansi

Mac 15:14 anthu odziwika ndi dzina lake

Aro 10:13 woitana pa dzina la Yehova

Afi 2:9 anamupatsa dzina loposa lililonse

DZIWA

, Miy 14:15 amene sadziwa zambiri

Mla 7:14 asamadziwe chilichonse

Yes 11:9 lidzadzaza ndi odziwa Yehova

Yer 31:34 Mumʼdziwe Yehova, adzandidziwa

Ho 4:6 Popeza akana kundidziwa

1Ak 9:26 osadziwa kumene ndikupita

2Ak 2:11 tikudziwa bwino ziwembu zake

1Ti 1:13 ndinkachita zinthu mosadziwa

DZIWA MOLONDOLA

, Aro 10:2 koma sakumudziwa molondola

Akl 3:10 mukudziwa Mulungu molondola

1Ti 2:4 adziwe choonadi molondola

DZIWIDWA

, Aga 4:9 mwadziwidwa ndi Mulungu

DZIWIKA

, 2Ak 6:9 ngati osadziwika koma odziwika

DZOZA

, 1Sa 16:13 Samueli anadzoza Davide

Sl 2:2 Mafumu akulimbana ndi wodzozedwa

Sl 105:15 Musakhudze odzozedwa anga

Yes 61:1 Yehova anandidzoza kuti ndilengeze

DZUDZULA

, Sl 141:5 Akandidzudzula wandidzoza mafuta

Miy 3:11 usanyansidwe ndi kudzudzula

Miy 27:5 Kudzudzula mosabisa mawu

Miy 29:1 amaumitsa khosi podzudzulidwa

Mla 7:5 kumvetsera wanzeru akamakudzudzula

1Ti 5:1 Usadzudzule mokalipa wachikulire

DZUTSA

, Yoh 11:11 ndikupita kukamudzutsa

DZUWA

, Yos 10:12 Dzuwa, ima pamwamba

Mt 24:29 dzuwa lidzachita mdima

Mac 2:20 Dzuwa lidzasanduka mdima

E

EDENI

, Ge 2:8 anadzala munda ku Edeni

EFESO

, 1Ak 15:32 zilombo ku Efeso

ELI

, 1Sa 1:3 ana a Eli anali ansembe

ELIYA

, Yak 5:17 Eliya anali ngati ife tomwe

EODIYA

, Afi 4:2 Ndikudandaulira Eodiya

ESAU

, Ge 25:34 Esau ananyoza ukulu wake

Ahe 12:16 wosayamikira ngati Esau

EZARA

, Eza 7:11 Ezara wokopera Malemba

F

FAFANIZA

, Mac 3:19 machimo anu afafanizidwe

FANO

, Da 3:18 sitilambira fano lagolide

FATSA

, 1Ak 4:13 timayankha mofatsa

Akl 3:12 valani kufatsa komanso kuleza mtima

1Pe 3:4 mtima wodekha komanso wofatsa

FESA

, Sl 126:5 akukhetsa misozi pofesa

Aga 6:7 chimene munthu wafesa

FIIRA

, Yes 1:18 machimo anu ndi ofiira kwambiri

FILIPO

, Mac 8:26 mngelo analankhula kwa Filipo

Mac 21:8 mlaliki wina dzina lake Filipo

FOOKA

, Miy 24:10 Ukafooka pa nthawi ya mavuto

Aro 14:1 chikhulupiriro chofooka

Aro 15:1 chikhulupiriro chofooka

1Ak 1:27 anasankha zinthu zofooka

2Ak 12:10 ndimasangalala ndi kufooka

1At 3:3 chikhulupiriro chafooka

1At 5:14 muzithandiza ofooka

FOTOKOZA

, Ne 8:8 kuchifotokoza momveka bwino

Yoh 1:18 anafotokoza za Mulungu

Mac 17:3 ankafotokoza ndi kusonyeza umboni

FUFUZA

, De 13:14 muzifufuza mosamala

Sl 26:2 Ndifufuzeni, inu Yehova

Miy 21:2 Yehova amafufuza mitima

Miy 25:2 ulemerero wa mafumu ndi kufufuza nkhani

Lu 15:8 kusesa mʼnyumba nʼkuifufuza

1Ak 11:28 Munthu azidzifufuza kaye

1At 5:21 Muzifufuza zonse, nʼkugwira zabwino

1Pe 1:10 anafufuza za chipulumutso

1Yo 4:1 muzifufuza mawu ouziridwawo

FUKO

, Ge 49:28 mafuko 12 a Isiraeli

FULUMIRA

, Miy 29:20 ofulumira kulankhula

Yes 60:22 zichitike mofulumira

Yak 1:19 asamafulumire kukwiya

FUMBI

, Ge 3:19 ndiwe fumbi, udzabwerera

Sl 103:14 Amakumbukira kuti ndife fumbi

Yes 40:15 amawaona ngati fumbi pasikelo

FUNA

, De 10:12 akufuna muzichita chiyani?

1Mb 29:17 ndapereka mwakufuna kwanga

Yob 23:12 zimene amafuna kuti ndichite

Sl 40:8 kuchita zimene mumafuna

Sl 143:10 Ndiphunzitseni zimene mumafuna 

Mik 6:8 Yehova akufuna uzichita chiyani?

Mt 6:10 Zofuna zanu zichitike padziko

Mt 7:21 zimene Atate wanga amafuna

Lu 22:42 osati zofuna zanga

Yoh 4:23 Atate akufuna anthu ngati amenewo

Yoh 6:38 osati zofuna zanga

Aro 7:18 Chifukwa ndimafuna kuchita zabwino

1Ak 12:18 anaika ziwalo mmene anafunira

1Ak 13:5 sichisamala zofuna zake zokha

Afi 2:4 muziganiziranso zofuna za ena

Afi 2:13 mtima wofuna kuchita zinthu

Afi 2:21 akungoganizira zofuna zawo

1At 4:3 Mulungu akufuna mukhale oyera

1Pe 5:7 chifukwa amakufunirani zabwino

1Yo 2:17 wochita zimene Mulungu amafuna

1Yo 5:14 mogwirizana ndi zimene amafuna

FUNAFUNA

, 1Mb 28:9 Ukamufunafuna, udzamupeza

Sl 119:176 Ndifunefuneni ine mtumiki wanu

Yes 55:6 Funafunani Yehova

Eze 34:11 ndidzafunafuna nkhosa zanga

Zef 2:3 Funafunani Yehova, inu ofatsa

Mac 17:27 anthuwo afunefune Mulungu

Akl 3:1 pitirizani kufunafuna zakumwamba

FUNIKA

, Aga 6:3 akudziona kuti ndi wofunika

FUNIKIRA

, Mt 6:32 mumafunikira zonsezi

FUNITSITSA

, Eks 35:5 mtima wofunitsitsa

Eks 35:21 wa mtima wofunitsitsa anabweretsa

Sl 51:12 mtima wofunitsitsa kukumverani

Sl 110:3 adzadzipereka mofunitsitsa

Aro 1:15 ndikufunitsitsa kudzalalikira

Afi 1:8 ndikufunitsitsa nditakuonani

1Pe 1:12 Angelo amafunitsitsa atamvetsa

FUPA

, Ge 2:23 uyu ndi fupa la mafupa anga

2Mf 13:21 Mtembowo utakhudza mafupa a Elisa

Sl 34:20 Amateteza mafupa a wolungama

Miy 25:15 mawu okoma akhoza kuthyola fupa

Yer 20:9 moto umene watsekeredwa mʼmafupa

Yoh 19:36 Sadzathyola fupa lake

G

GABIRIELI

, Lu 1:19 Gabirieli, pamaso pa Mulungu

GALASI

, 1Ak 13:12 galasi losaoneka bwino

Yak 1:23 kudziyangʼanira nkhope pagalasi

GALU

, Miy 26:17 wogwira makutu a galu

Mla 9:4 galu wamoyo ali bwino

2Pe 2:22 Galu wabwerera kumasanzi

GAMALIYELI

, Mac 22:3 kuphunzitsidwa ndi Gamaliyeli

GANIZA

, Yob 6:3 ndalankhula mosaganiza bwino

Miy 15:28 amaganiza asanayankhe

Aef 4:23 atsopano pa kaganizidwe kanu

GANIZIRA

, Sl 8:4 munthu ndani kuti muzimuganizira?

Sl 41:1 moganizira wonyozeka

Mt 24:44 pa ola limene simukuliganizira

Aro 8:6 kuganizira za thupi kumabweretsa imfa

Aro 12:3 musamadziganizire kuposa mmene

Aro 15:1 olimba aziganizira ofooka

Afi 3:19 amangoganizira zapadziko lapansi

Akl 3:2 Pitirizani kuganizira zinthu zakumwamba

GANIZIRA MOZAMA

, Sl 19:14 ndimaganizira mozama

Sl 77:12 Ndidzaganizira mozama za ntchito zanu

GAWANA

, Aro 12:13 Gawanani ndi oyera

GAWO

, Da 12:13 udzauka kuti ulandire gawo

GEHAZI

, 2Mf 5:20 Gehazi anati, ndimʼthamangira

GEHENA

, Mt 10:28 kuwononga zonse ziwiri mʼGehena

GETI

, Mt 7:13 Lowani pageti lalingʼono

GIBIYONI

, Yos 9:3 anthu a ku Gibiyoni anamva

GIDIYONI

, Owe 7:20 Yehova ndi Gidiyoni!

GOGODA

, Mt 7:7 Pitirizani kugogoda

GOLI

, 1Mf 12:14 anakusenzetsani goli lolemera

Mt 11:30 goli langa ndi losavuta kunyamula

2Ak 6:14 Musamangidwe mʼgoli ndi osakhulupirira

GOLIDE

, Eze 7:19 golide sadzawapulumutsa

Da 3:1 Nebukadinezara anapanga fano lagolide

GOLIYATI

, 1Sa 17:4 ngwazi dzina lake Goliyati

GOLOGOTA

, Yoh 19:17 ankatchulidwa kuti Gologota

GOMORA

, Ge 19:24 sulufule ndi moto ku Gomora

GONA

, Miy 6:10 Ukapitiriza kugona pangʼono

2Ak 6:5 kusagona tulo ndiponso kukhala osadya

2Ak 11:27 Nthawi zambiri usiku sindinkagona

1At 5:6 tisapitirize kugona ngati ena onse

Ahe 13:4 pogona pa okwatirana posadetsedwa

GONJERA

, Ahe 13:17 ndipo muziwagonjera

1Pe 2:13 pogonjera ulamuliro uliwonse

GONJETSA

, Yer 1:19 Koma sadzakugonjetsa

Yoh 16:33 limbani mtima. Ine ndaligonjetsa dziko

Aro 8:37 tikugonjetsa zinthu zonsezi

Aro 12:21 pitirizani kugonjetsa choipa

GULA

, 1Ak 7:23 Munagulidwa pa mtengo wokwera

Chv 5:9 ndi magazi anu munagula anthu

GULU

, Eks 23:2 Musamachite zoipa pongotsatira gulu

Ahe 12:1 tazunguliridwa ndi gulu lalikulu la mboni

1Pe 2:17 Muzikonda gulu lonse la abale

GULU LACHIWAWA

, Mac 17:5 gulu lachiwawa mumzinda

GULU LANKHONDO

, Zek 4:6 sipakufunika gulu lankhondo koma mzimu

GUWA LANSEMBE

, Ge 8:20 Nowa, guwa lansembe

Eks 27:1 Upange guwa lansembe lamatabwa

Mt 5:24 patsogolo pa guwa lansembe

Mac 17:23 guwa lansembe la Mulungu Wosadziwika

GWEDEZA

, Hag 2:7 Ndigwedeza mitundu yonse

GWETSA

, 2Ak 10:4 zimatha kugwetsa zinthu zozikika

GWIRA

, Afi 2:16 mugwire mawu amoyo

GWIRA NTCHITO

, Yoh 5:17 Atate akugwirabe ntchito

1At 2:9 Tinkagwira ntchito usiku ndi masana

GWIRITSA NTCHITO MOLAKWA

, 1Ak 9:18 ndisagwiritse ntchito molakwa ufulu

GWIRITSIRA

, Sl 90:12 tingagwiritsire ntchito moyo

1Ak 7:31 Amene amagwiritsira ntchito

GWIRIZANA

, Sl 133:1 akakhala mogwirizana

Zef 3:9 Nʼkumamutumikira mogwirizana

Mac 15:25 Choncho tonse tagwirizana

Aro 3:25 anthu agwirizanenso ndi Mulungu

1Ak 1:10 nonse muzilankhula mogwirizana

1Ak 5:9 musiye kugwirizana ndi achiwerewere

1Ak 7:5 pokhapokha ngati mwagwirizana

1Ak 15:33 Kugwirizana ndi anthu oipa

Aga 5:25 kuchita mogwirizana ndi mzimuwo

Aef 4:1 muzichita zinthu mogwirizana

Aef 4:13 mpaka tidzakhale ogwirizana

Afi 2:2 ndinu ogwirizana kwambiri

Akl 1:10 mukhale ndi khalidwe logwirizana

GWIRIZANITSA

, Aro 5:10 ngati tinagwirizanitsidwa

Aro 8:28 amagwirizanitsa zochita zake zonse

2Ak 5:19 Mulungu ankagwirizanitsa dziko ndi iyeyo

Aef 4:3 chomangira chotigwirizanitsa

Akl 3:14 chikondi chimagwirizanitsa

H

HANANIYA

, Mac 5:1 Hananiya ndi Safira

HATCHI

, Chv 6:2 hatchi yoyera

Chv 19:11 ndinaona hatchi yoyera

HEZEKIYA

, 2Mf 19:15 Hezekiya anapemphera

HULE

, Miy 7:10 Atavala ngati hule

Lu 15:30 anawononga chuma ndi mahule

1Ak 6:16 amene wagonana ndi hule

Chv 17:1 chiweruzo cha hule lalikulu

Chv 17:16 zidzadana ndi hulelo

I

IGUPUTO

, Mt 2:15 atuluke mu Iguputo

IKA

, Lu 22:37 anaikidwa mʼgulu la osamvera

IMA

, Yob 37:14 Imani ndi kuganizira mozama

1Ak 10:12 amene akuganiza waima bwinobwino

IMBA

, 1Mb 15:16 asankhe abale awo oimba

Sl 96:1 Imbirani Yehova

Mt 26:30 atamaliza kuimba nyimbo

Aef 5:19 Muziimba nyimbo zotamanda

IMFA

, Ru 1:17 kupatulapo imfa

Sl 89:48 Kodi pali amene sadzafa?

Yes 25:8 adzameza imfa kwamuyaya

Eze 18:32 sindisangalala ndi imfa

Ho 13:14 Imfa, mphamvu yako ili kuti?

Yoh 8:51 wosunga mawu, sadzaona imfa

Aro 5:12 imfayo inafalikira kwa onse

Aro 6:23 malipiro a uchimo ndi imfa

1Ak 15:26 Imfa, idzawonongedwa

1At 4:13 amene akugona mu imfa

Ahe 2:9 Yesu analawa imfa

Ahe 2:15 ukapolo chifukwa choopa imfa

Chv 21:4 imfa sidzakhalaponso

IMFA YACHIWIRI

, Chv 2:11 sadzakhudzidwa ndi imfa yachiwiri

Chv 20:6 Imfa yachiwiri ilibe ulamuliro

Chv 20:14 Nyanja yamoto ikuimira imfa yachiwiri

IMVI

, Miy 16:31 Imvi ndi chisoti cha ulemerero

IMWA

, Mt 20:22 Kodi mungamwe?

INDE

, Mt 5:37 mukati Inde akhaledi inde

INOKI

, Ge 5:24 Inoki anayenda ndi Mulungu

IPA

, Ge 3:5 Mudzadziwa zabwino ndi zoipa

Yes 5:20 akunena kuti chabwino nʼchoipa

Aro 7:19 koma zoipa zimene sindifuna kuchita

IPITSA

, 2Ak 7:1 tidziyeretse ku choipitsa thupi

ISAKI

, Ge 22:9 anamanga Isaki mwana wake

ISIRAELI

, Ge 35:10 dzina lako likhala Isiraeli

Sl 135:4 Wasankha Isiraeli kukhala chuma

Aga 6:16 Isiraeli wa Mulungu akhale ndi mtendere

ITANA

, Aro 10:13 woitana pa dzina la Yehova

Aef 4:1 muzichita zinthu mogwirizana ndi kuitana

IWALA

, De 4:23 musaiwale pangano

Sl 119:141 sindinaiwale malamulo anu

Yes 49:15 mayi angaiwale mwana?

Afi 3:13 Ndikuiwala zinthu zakumbuyo

Ahe 6:10 kuti angaiwale ntchito yanu

J

JESE

, 1Sa 17:12 Jese anali ndi ana 8

Yes 11:1 Nthambi idzaphuka pachitsa cha Jese

K

KACHISI

. Onaninso NYUMBA, Sl 11:4 Yehova ali mʼkachisi

Sl 27:4 ndiyangʼane kachisi wake

Yer 7:4 kachisi wa Yehova

Eze 41:13 anayeza kachisi nʼkupeza kuti

Mki 3:1 adzabwera kukachisi wake

Mt 21:12 analowa mʼkachisi nʼkuthamangitsa

Yoh 2:19 Gwetsani kachisiyu

Mac 17:24 sakhala mu akachisi opangidwa

1Ak 3:16 ndinu kachisi wa Mulungu

KAGULU KA NKHOSA

, Lu 12:32 Musaope, kagulu ka nkhosa

KAINI

, 1Yo 3:12 Kaini, anapha mʼbale wake

KAISARA

, Mt 22:17 kupereka msonkho kwa Kaisara

Mko 12:17 Perekani za Kaisara kwa Kaisara

Yoh 19:12 ndiye kuti si inu mnzake wa Kaisara

Yoh 19:15 Tilibe mfumu ina koma Kaisara

Mac 25:11 Ndikuchita apilo kwa Kaisara

KAKAMIZA

, Mac 26:11 kuwakakamiza kuti asiye

KALAMBA

, Sl 71:9 Musanditaye pamene ndakalamba

Sl 92:14 Ngakhale atakalamba zidzawayendera

KALATA

, De 24:1 kalata yothetsera ukwati

Mt 19:7 azipereka kalata yothetsera ukwati

KALEBE

, Nu 13:30 Kalebe anawakhazika mtima pansi

Nu 14:24 Kalebe anali wosiyana ndi ena

KALIPENTALA

, Mko 6:3 Kodi iyeyu si kalipentala?

KALONGA

, Sl 45:16 akhale akalonga padziko

Yes 9:6 Kalonga Wamtendere

Yes 32:1 akalonga adzalamuliranso

Da 10:13 kalonga wa ufumu wa Perisiya

KAMBIRANA

, Miy 15:22 ngati anthu sakambirana

Mac 17:2 anakambirana mfundo za mʼMalemba

KAMBUKU

, Yes 11:6 kambuku adzagona ndi mbuzi

Da 7:6 chilombo chooneka ngati kambuku

KAMWA

, De 25:4 Usamange ngʼombe pakamwa

Sl 8:2 ochokera mʼkamwa mwa ana

Ho 14:2 tidzakutamandani ndi pakamwa pathu

Aro 10:10 ndi pakamwa pake amalengeza

Yak 3:10 Pakamwa pomwepo, mawu otamanda

KANA

, Yer 8:9 Iwo akana mawu a Yehova

Yoh 2:1 ku Kana kunali ukwati

KANGANA

, Mac 15:39 anakangana koopsa

2Ti 2:24 Kapolo sakangana ndi anthu

KANIZA

, 1Ak 7:5 Musamakanizane

KANJERE KA MPIRU

, Lu 13:19 ngati kanjere ka mpiru

KANTHAWI

, Yes 26:20 Mukabisale kwa kanthawi

2Ak 4:17 mavuto ndi akanthawi

KAPHUNZITSIDWE

, Mt 7:28 ndi kaphunzitsidwe kake

KAPOLO

, Miy 22:7 kapolo wa wobwereketsa

Mt 24:45 kapolo wokhulupirika

Mt 25:21 ndiwe kapolo wabwino

Lu 17:10 Ife ndi akapolo opanda pake

Yoh 8:34 ndi kapolo wa tchimo

1Ak 7:23 siyani kukhala akapolo a anthu

KAPU

, Lu 22:20 Kapu ikuimira pangano latsopano

Lu 22:42 ndichotsereni kapu iyi

1Ak 11:25 chimodzimodzi ndi kapu

KASUPE

, Sl 36:9 Inu ndinu kasupe wa moyo

Yer 2:13 kasupe wa madzi amoyo

KATATU

, De 16:16 katatu pa chaka

KATUNDU

, Sl 38:4 zolakwa, katundu wolemera

Sl 68:19 Yehova amanyamula katundu wathu

Yes 60:5 Katundu wa anthu adzabwera

Lu 11:46 mumasenzetsa anthu katundu

Aga 6:5 kunyamula katundu wake

Ahe 10:34 katundu wanu akulandidwa

Chv 2:24 Sindikusenzetsani katundu wolemera

KAYIKA

, 1Mf 18:21 Kodi mukayikakayika mpaka liti?

Yak 1:8 ndi wokayikakayika, amasinthasintha

KAYIKIRA

, Mt 21:21 ngati simukukayikira

Aro 4:21 sankakayikira kuti ali ndi mphamvu

Aro 15:14 Abale anga, ine sindikukayikira

Akl 4:12 musamakayikire ngakhale pangʼono

Yak 1:6 azipempha, asamakayikire

Yuda 22 anthu amene amakayikira

KAZEMBE

, 2Ak 5:20 akazembe mʼmalo mwa Khristu

KEFA

, 1Ak 15:5 anaonekera kwa Kefa kenako atumwi

Aga 2:11 Kefa atabwera ku Antiokeya

KERUBI

, Ge 3:24 anamuthamangitsa nʼkuika akerubi

Eze 28:14 kuti ukhale kerubi wodzozedwa

KHALA

, Eks 3:14 Ndidzakhala Amene Ndidzafune Kukhala

Sl 110:1 Khala kudzanja langa lamanja

Yes 45:18 analiumba kuti anthu akhalemo

Lu 22:28 inu ndi amene mwakhalabe

Aro 8:15 munalandira mzimu wakuti mukhale ana

1Ak 9:22 Ndakhala zinthu zonse

Aga 6:16 lamulo la mmene tiyenera kukhalira

1Pe 2:12 Mukhale ndi khalidwe labwino

1Yo 2:17 adzakhala mpaka kalekale

KHALA CHETE

, Sl 4:4 ndipo mukhale chete

Sl 32:3 ndinakhala chete osaulula machimo

Mla 3:7 Nthawi yokhala chete

Yes 53:7 imene yangokhala chete

KHALANI MASO

, Mt 26:41 Khalani maso, mupitirize

Lu 21:36 Choncho khalani maso

1Ak 16:13 Khalani maso, khalani ndi chikhulupiriro

1Pe 4:7 khalani maso, muzipemphera

Chv 16:15 Wosangalala amene akukhalabe maso

KHALANI OLIMBA

, 1Ak 15:58 abale, khalani olimba

1Ak 16:13 khalani olimba mʼchikhulupiriro

KHALIDWE

, Miy 31:29 akazi amakhalidwe abwino

Aga 5:22 makhalidwe a mzimu woyera

1Pe 3:1 akopeke ndi khalidwe lanu

1Pe 3:16 chifukwa cha khalidwe lanu labwino

KHALIDWE LOPANDA MANYAZI

, Aga 5:19 chiwerewere, khalidwe lopanda manyazi

2Pe 2:7 ankavutika ndi khalidwe lopanda manyazi

Yuda 4 chochitira khalidwe lopanda manyazi

KHALIDWE LOYENERA

, Aro 13:13 tikhale ndi khalidwe loyenera

KHAMA

, Miy 10:4 wogwira mwakhama adzalemera

Miy 12:27 khama ndi chuma cha munthu

Miy 21:5 Mapulani a munthu wakhama

Mac 5:42 kuphunzitsa mwakhama

Aro 12:11 Khalani akhama osati aulesi

Ahe 6:11 kusonyeza khama lapoyamba

2Pe 1:5 yesetsani mwakhama

KHAMU LALIKULU

, Chv 7:9 khamu lalikulu la anthu

KHATE

, Nu 12:10 Miriamu anagwidwa ndi khate

Lu 5:12 munthu wakhate thupi lonse

KHOKA

, Mt 13:47 Ufumu uli ngati khoka

KHOLA

, Yoh 10:16 nkhosa zimene si zamʼkhola ili

KHOMA

, Da 5:5 kulemba pakhoma lapulasitala

Yow 2:7 Amakwera khoma ngati asilikali

KHOMEREZA

, De 6:7 muziwakhomereza mwa ana

KHOMO

, 1Ak 16:9 khomo la utumiki landitsegukira

Chv 3:20 Ndaima pakhomo, ndikugogoda

KHOTA

, Mla 1:15 chokhota sichingawongoledwe

KHOTI

, Mko 13:9 Anthu adzakutengerani kumakhoti

1Ak 6:6 azitengera mʼbale wake kukhoti

KHOTI LALIKULU LA AYUDA

, Mac 5:41 anachoka pa Khoti Lalikulu la Ayuda

KHRISTU

, Mt 16:16 Khristu, Mwana wa Mulungu

Lu 24:26 kuti Khristu amve zowawa

Yoh 17:3 Yesu Khristu, amene munamutuma

Mac 18:28 posonyeza kuti Yesu ndiyedi Khristu

1Ak 11:3 mutu wa Khristu ndi Mulungu

KHUDZA

, Miy 6:29 wokhudza mkaziyo adzalangidwa

Yes 52:11 musakhudze chodetsedwa

Mt 8:3 nʼkumukhudza ndipo anati: Ndikufuna

2Ak 6:17 Musakhudze chinthu chodetsedwa

KHULULUKA

, Ne 9:17 wokonzeka kukhululuka

Miy 17:9 amene amakhululuka zolakwa

Yes 55:7 adzamukhululukira ndi mtima wonse

KHULULUKIDWA

, Mt 26:28 machimo awo akhululukidwe

KHULULUKIRA

, Sl 25:11 Mundikhululukire tchimo

Sl 103:3 amakukhululukira zolakwa

Mt 6:14 Mukamakhululukira anthu

Mt 18:21 ndizimukhululukira kangati

Akl 3:13 Yehova anakukhululukirani

KHULUPIRIKA

, Eks 18:21 oopa Mulungu, okhulupirika

1Mb 29:17 mumakonda okhulupirika

Yob 27:5 sindidzasiya kukhala wokhulupirika

Sl 25:21 Kukhala wokhulupirika kunditeteze

Sl 26:11 ndidzachita mokhulupirika

Sl 101:2 ndi mtima wokhulupirika

Lu 16:10 wokhulupirika pa chachingʼono

Tit 2:10 akhale okhulupirika pa chilichonse

KHULUPIRIRA

, Sl 9:10 anthu adzakukhulupirirani

Sl 84:12 Wosangalala amakukhulupirirani

Miy 3:5 Uzikhulupirira Yehova ndi mtima wonse

Yer 17:5 wokhulupirira munthu

Yoh 3:16 womukhulupirira asawonongedwe

Yoh 20:29 Osangalala amakhulupirira

2At 2:12 chifukwa sanakhulupirire choonadi

KHUMUDWA

, Sl 119:165 Palibe chingawakhumudwitse

Aro 5:5 Chiyembekezo sichitikhumudwitsa

Aro 9:33 wokhulupirira sadzakhumudwa

Akl 3:21 asakhale okhumudwa

KHUMUDWITSA

, Sl 78:40 ndipo ankamukhumudwitsa

Lu 17:2 akhumudwitse mmodzi wa tiana

Aro 14:13 chimene chingakhumudwitse

1Ak 8:13 chikukhumudwitsa mʼbale wanga

1Ak 10:32 Muzipewa kukhumudwitsa Ayuda

Afi 1:10 osakhumudwitsa ena

KHUNGU

, Ge 19:11 anachititsa khungu amuna

Mt 15:14 Iwo ndi atsogoleri akhungu

2Ak 4:4 mulungu wa nthawi ino wachititsa khungu

KHUNYU

, Mt 4:24 akhunyu ndi akufa ziwalo

KHUTHULA

, Sl 62:8 Mukhuthulireni zamumtima

KHUTIRA

, Afi 4:11 ndaphunzira kukhala wokhutira

1Ti 6:8 tizikhala okhutira ndi zinthu zimenezi

2Ti 3:14 unakhulupirira pambuyo pokhutira

KISI

, Lu 22:48 ukupereka Mwana wa munthu ndi kisi?

KIYI

, Lu 11:52 munalanda kiyi yowathandiza

KOKA

, Yoh 6:44 pokhapokha Atate atamukoka

KOKOMEZA

, 1Ak 2:1 sindinkalankhula mokokomeza

KOLOLA

, Mla 11:4 woyangʼana mitambo sadzakolola

Ho 8:7 adzakolola mphepo yamkuntho

Mt 9:37 zinthu zambiri zofunika kukolola

2Ak 9:6 wodzala moumira adzakolola zochepa

Aga 6:7 adzakololanso chomwecho

Aga 6:9 tidzakolola tikapanda kutopa

KOMETSERA

, Tit 2:10 kuti azikometsera

KONDA

, Le 19:18 Uzikonda mnzako

De 6:5 Muzikonda Yehova ndi mtima wonse

Sl 1:2 amakonda chilamulo cha Yehova

Mt 10:37 amakonda kwambiri bambo kapena mayi

Mt 22:37 Muzikonda Yehova

Mko 10:21 Yesu anamukonda

Yoh 3:16 Mulungu anakonda dziko

Yoh 12:25 amene amakonda moyo akuuwononga

Yoh 13:1 anawakonda mpaka pamapeto

Yoh 13:34 kuti muzikondana

Yoh 14:15 Ngati mumandikonda, mudzasunga

Yoh 21:17 Simoni, kodi umandikonda kwambiri?

Aro 13:8 ngongole, kupatulapo kukondana

2Ak 2:8 mumutsimikizire kuti mumamukonda

Aga 2:20 Mwana wa Mulungu anandikonda

Aef 5:29 amalidyetsa ndi kulikonda

Akl 3:19 pitirizani kukonda akazi anu

1Ti 6:4 amakonda kukangana ndi kutsutsana

1Yo 2:15 Musamakonde dziko kapena

1Yo 3:18 tisamakondane ndi mawu okha

1Yo 4:10 anatikonda, osati ifeyo tinamukonda

1Yo 4:20 wosakonda mʼbale, sangakonde Mulungu

1Yo 5:3 Kukonda Mulungu kumatanthauza

Yuda 21 Mulungu azikukondani

Chv 3:19 amene ndimawakonda, ndimawadzudzula

KONDA ABALE

, Aro 12:10 Pokonda abale, chikondi

KONDEDWA

, Mt 3:17 Mwana wanga wokondedwa

KONDERA

, De 10:17 amene sakondera munthu

KONDWA

, Sl 100:2 Tumikirani Yehova mokondwera

Aro 12:12 Kondwerani chifukwa cha chiyembekezo

KONDWERETSA

, Aro 15:1 kumangodzikondweretsa

Aro 15:2 aziyesetsa kukondweretsa mnzake

Aro 15:3 sankachita zinthu zodzikondweretsa

1Ak 7:33 angakondweretsere mkazi wake

KONELIYO

, Mac 10:24 Koneliyo anasonkhanitsa

KONGOLA

, Miy 6:25 Usasirire kukongola kwake

Miy 19:11 kumamʼchititsa kukhala wokongola

Miy 31:30 kukongola sikungachedwe kutha

Eze 28:17 unadzikweza chifukwa cha kukongola

KONGOZA

, Miy 19:17 akukongoza Yehova

Lu 6:35 kukongoza popanda chiwongoladzanja

KONZA

, Yoh 14:2 ndikupita kukakukonzerani malo

KONZEKA

, Mt 24:44 khalani okonzeka

1Pe 3:15 okonzeka kuyankha aliyense

KONZEKERA

, Aro 13:14 musamakonzekere kuchita

Aef 6:15 pokonzekera kulengeza uthenga

KOPA

, Aro 16:18 amagwiritsa ntchito mawu okopa

1Ak 2:4 mawu anga sanali okopa

2Ak 5:11 tikupitiriza kukopa anthu

KOPERA

, De 17:18 ayenera kukopera Chilamulo

KORA

, Nu 26:11 ana a Kora sanafe

Yuda 11 polankhula moukira ngati Kora

KORESI

, Eza 6:3 Koresi anaika lamulo

Yes 45:1 wodzozedwa wake Koresi, wamugwira

KOTULUKIRA DZUWA

, Yes 41:2 kuchokera kotulukira dzuwa

KUBA

, Eks 20:15 Musabe

Le 19:13 Musamabere anzanu

Miy 30:9 Ndiponso ndisasauke nʼkukaba

Aef 4:28 wakuba asiye kubako

KUBEREDWA

, 1Ak 6:7 Bwanji osalola kuberedwa?

KUBEREKA ZIPATSO

, 2Pe 1:8 zidzakuthandizani kubereka zipatso

KUCHITA ZOYENERA

, Yob 1:8 amachita zoyenera

KUDYA

, 1Ak 5:11 ngakhale kudya naye, ayi

KUDZICHEPETSA

, De 8:2 akuphunzitseni kudzichepetsa

Miy 15:33 umabwera ndi kudzichepetsa

Zek 9:9 Ndi yodzichepetsa, inakwera bulu

Mt 18:4 amene adzadzichepetse ngati mwana

Yak 4:6 odzichepetsa amawakomera mtima

Yak 4:10 Dzichepetseni pamaso pa Yehova

1Pe 5:6 dzichepetseni pamaso pa Mulungu

KUDZIKANA

, Mt 16:24 adzikane yekha

KUDZIKONGOLETSA

, 1Pe 3:3 Kudzikongoletsa kusakhale kwa kunja

KUDZIKUZA

, De 17:12 amene adzachite zinthu modzikuza

1Sa 15:23 kuchita zinthu modzikuza

Sl 19:13 mundiletse kuchita zinthu modzikuza

Aro 12:16 Musamaganize modzikuza

KUDZIKWEZA

, Miy 11:2 Kudzikweza kukafika

KUDZILETSA

, 1Ak 7:5 mukalephera kudziletsa

Aga 5:22, 23 chikhulupiriro, kufatsa ndi kudziletsa

KUDZIONETSERA

, 1Yo 2:16 kudzionetsera ndi zimene ali nazo

KUDZIPATULA

, Miy 18:1 aliyense wodzipatula

KUDZIPEREKA

, Eks 34:14 azidzipereka kwa iye yekha

Eks 36:2 amene anadzipereka mofunitsitsa

Sl 69:9 Kudzipereka panyumba yanu

Nym 8:6 kudzipereka ndi mtima wonse

2Ak 12:15 ndidzadzipereka ndi mtima wonse

KUDZIPEREKA KWA MULUNGU

, 1Ti 4:7 ukhalebe wodzipereka kwa Mulungu

1Ti 4:8 kudzipereka kwa Mulungu nʼkothandiza

1Ti 6:6 kukhala wodzipereka kwa Mulungu

2Ti 3:12 moyo wodzipereka kwa Mulungu

KUDZIWA ZINTHU

, Miy 1:7 chiyambi cha kudziwa zinthu

Miy 2:10 kudziwa zinthu kukakhala kosangalatsa

Miy 24:5 wodziwa zinthu amawonjezera mphamvu

Yes 5:13 ku ukapolo chifukwa chosadziwa zinthu

Da 12:4 adzadziwa zinthu zambiri zoona

Lu 11:52 kiyi yowathandiza kudziwa zinthu

1Ak 8:1 Kudziwa zinthu kumachititsa kudzikuza

KUDZIYESA

, 2Ak 13:5 Pitirizani kudziyesa

KUFA

, Ge 3:4 simudzafa ayi

Yob 14:14 Munthu akafa, angakhalenso ndi moyo?

Yoh 11:26 amene amandikhulupirira sadzafa

Aro 14:8 tikafa, timafera Yehova

2Ak 5:15 wosangalatsa amene anawafera

KUFANANA

, 2Ak 8:14 kuti pakhale kufanana

Afi 2:6 akhale wofanana ndi Mulungu

KUFA ZIWALO

, Lu 5:24 anauza wakufa ziwalo

KUGANIZA BWINO

, Miy 1:4 wachinyamata aziganiza bwino

KUGANIZIRA MOZAMA

, Yos 1:8 Uziliwerenga ndi kuganizira mozama

Sl 1:2 amawerenga ndi kuganizira mozama

KUGAWANIKA

, 1Ak 1:10 pasakhale kugawanika

KUGAWANITSA

, Mt 10:35 Ndinabwera kudzagawanitsa

Aro 16:17 musamale ndi ogawanitsa

KUGWA

, Miy 24:16 wolungama angagwe maulendo 7

Mla 4:10 ngati mmodzi atagwa

1Ak 10:12 asamale kuti asagwe

KUGWA ULESI

, 2Mb 15:7 musagwe ulesi

KUGWIRA NJAKATA

, Afi 1:23 Ndagwira njakata ndisankhe chiti

KUGWIRA NTCHITO

, Aro 12:4 ziwalo sizigwira ntchito yofanana

Aef 4:16 chikamagwira ntchito yake

KUIPA

, 2At 2:7 kuipa kwayamba kugwira ntchito

KUKANA

, Miy 30:9 ndisakhute nʼkukukanani

Mko 14:30 undikana katatu

Tit 1:16 amamukana ndi zochita

KUKHALAPO

, Mt 24:3 chizindikiro cha kukhalapo kwanu

Mt 24:37 kukhalapo kwa Mwana wa munthu

2Pe 3:4 kukhalapo kolonjezedwa kuli kuti?

KUKHALA WATSOPANO

, Aro 12:2 khalani watsopano posintha maganizo

KUKHAZIKITSA MWALAMULO

, Afi 1:7 kukhazikitsa mwalamulo uthenga wabwino

KUKHULUPIRIKA

, Mik 6:8 uzichita chilungamo, uzikukhulupirika

Hab 2:4 chifukwa cha kukhulupirika

1Ak 4:2 chofunika kwa atumiki ndi kukhulupirika

1Ak 10:13 Mulungu ndi wokhulupirika

Chv 2:10 Sonyeza kukhulupirika mpaka imfa

KUKHULUPIRIRA MIZIMU

, Aga 5:20 kulambira mafano, kukhulupirira mizimu

KUKOMA MTIMA

, Miy 11:17 wokoma mtima zimamuyendera

Miy 31:26 lamulo la kukoma mtima lili palilime

Mt 16:22 Dzikomereni mtima Ambuye

Mac 28:2 Anthu anatisonyeza kukoma mtima

KUKOMA MTIMA KWAKUKULU

, Yoh 1:17 kukoma mtima kwakukulu mwa Yesu

1Ak 15:10 kukoma mtima kwakukulu kumene

2Ak 6:1 musalandire kukoma mtima kwakukulu

2Ak 12:9 Kukoma mtima kwakukulu nʼkokwanira

KUKONZEKA

, 2Ti 3:17 wokonzeka mokwanira

KULA

, Sl 37:25 Ndinali mwana, tsopano ndakula

KULAKALAKA

, Eks 20:17 Musalakelake mkazi wa mnzanu

Sl 37:4 zimene mtima umalakalaka

Sl 84:2 Moyo wanga ukulakalaka

Sl 145:16 zolakalaka za chamoyo chilichonse

Aga 5:16 simudzachita zimene thupi likulakalaka

1Pe 2:11 muzipewa kulakalaka zoipa

KULAKWIRIDWA

, 1Ak 6:7 Bwanji osangolola kulakwiridwa?

KULAMBIRA MAFANO

, 1Ak 10:14 pewani kulambira mafano

KULA MWAUZIMU

, Ahe 5:14 anthu aakulu mwauzimu

Ahe 6:1 tikhale aakulu mwauzimu

KULEDZERA

, Aef 5:18 musamaledzere

KULEMEKEZA

, Afi 2:29 muziwalemekeza kwambiri

KULENGEZA

, Aro 10:10 amalengeza za chipulumutso

Ahe 10:23 kulengeza chiyembekezo

KULIMBANA

, Aef 6:12 tikulimbana ndi ziwanda

KULIMBITSA

, Afi 2:13 Mulungu amakulimbitsani

KULIRA

, Mt 26:75 kulira mopwetekedwa mtima

KULIRA MOSAMVEKA

, 1Ak 14:8 silikulira momveka

KUMBUKIRA

, Yob 14:13 mukanandibisa, nʼkudzandikumbukira

Mla 12:1 kumbukira Mlengi wako

Yes 65:17 zakale sizidzakumbukiridwanso

Lu 22:19 Muzichita zimenezi pondikumbukira

Ahe 10:32 pitirizani kukumbukira masiku akale

KUMBUTSA

, 1Ak 4:17 adzakukumbutsani mmene ndimachitira

2Pe 1:12 ndizikukumbutsani zinthu zimenezi

KUMBUYO

, Lu 9:62 nʼkumayangʼana zakumbuyo

KUMVA

, Aro 10:14 angamve popanda wolalikira?

KUMVETSA

, Aro 2:20 mumamvetsa choonadi

Ahe 5:11 mumachedwa kumvetsa zinthu

KUMWAMBA

, Sl 8:3 Ndikayangʼana kumwamba

Sl 19:1 zakumwamba zikulengeza ulemerero

Yoh 3:13 palibe anakwera kumwamba

2Ak 12:2 nʼkupita naye kumwamba kwachitatu

2Pe 3:13 kumwamba ndi dziko latsopano

KUNJA

, 1Ak 5:13 amaweruza amene ali kunja?

Akl 4:5 kuchita mwanzeru ndi anthu akunja

KUNKHA

, Le 19:9 musamachite khunkha mʼmunda

Ru 2:8 usapitenso kwina kukakunkha

KUNYALANYAZA

, 1At 4:8 sakunyalanyaza munthu

KUOMBEZA

, Nu 23:23 kuombeza maula

De 18:10 pasapezeke aliyense woombeza

KUONA

, 1Ak 2:9 amene anaonapo kapena kumva

Akl 3:22 pokhapokha akukuonani

KUONETSEDWA

, 1Ak 4:9 tikuonetsedwa kudziko

KUOPA

, Ge 9:2 zamoyo zidzapitiriza kukuopani

KUOPA YEHOVA

, Sl 19:9 Kuopa Yehova nʼkoyera

Sl 111:10 Chiyambi cha nzeru nʼkuopa Yehova

Miy 8:13 Kuopa Yehova kumatanthauza

KUPAMBANA

, 2Ak 2:14 chionetsero chonyadira kupambana

KUPANDA CHILUNGAMO

, De 32:4 sachita zopanda chilungamo

KUPANIKIZIKA

, Yes 38:14 Yehova, ine ndapanikizika

KUPATSA

, Lu 16:11 ndani angakupatseni ntchito

Mac 20:35 Kupatsa kumatichititsa kusangalala

KUPEREKA

, 1Ak 7:3 Mwamuna azipereka

1Pe 4:19 apereke moyo kwa Mlengi

KUPHA

, Yes 53:7 kumalo oti akamuphere

Yoh 16:2 amene adzakupheni adzaganiza

KUPHA MUNTHU

, Eks 20:13 Musaphe munthu

KUPHUNZITSA

, Yes 48:17 ndimakuphunzitsani kuti zikuyendereni

1Pe 5:10 adzamalizitsa kukuphunzitsani

KUPIRIRA

, Mt 24:13 amene adzapirire adzapulumuka

Lu 8:15 nʼkubereka zipatso mopirira

Lu 21:19 mukadzapirira, mudzapeza moyo

Aro 5:3 mavuto amachititsa kupirira

Aro 12:12 Muzipirira mavuto

1Ak 4:12 timapirira moleza mtima

Yak 1:4 kupirira kumalize ntchito yake

Yak 5:11 munamva za kupirira kwa Yobu

1Pe 2:20 mukamapirira chifukwa chochita zabwino

KUPITA PACHABE

, 1Ak 15:58 sizidzapita pachabe

KUPOSA

, Afi 2:3 muziona kuti ena amakuposani

1At 4:1 kuposa mmene mukuchitira

1At 4:10 kuposa mmene mukuchitira

KUPSA MTIMA

, Sl 37:8 Usapse mtima

Miy 19:19 wosachedwa kupsa mtima azilipira

Akl 3:19 musamawapsere mtima kwambiri

KUPSETSA MTIMA

, Aef 6:4 musamapsetse mtima ana anu

KUSAGANIZA

, Miy 12:18 amalankhula asanaganize

KUSALA

, Yes 58:6 kusala kudya kumene ndimafuna

Lu 18:12 ndimasala kudya kawiri pa mlungu

KUSALOWERERA ZA ENA

, 1At 4:11 Musamalowerere nkhani za ena

KUSAMVERA MALAMULO

, Mt 7:23 Chokani, osamvera malamulo inu

Mt 24:12 kuwonjezeka kwa kusamvera malamulo

Lu 22:37 mʼgulu la anthu osamvera malamulo

KUSAONEKA

, Aro 1:20 makhalidwe osaoneka

Ahe 11:27 ngati akuona Wosaonekayo

KUSINTHA MAONEKEDWE

, Mt 17:2 anaona kuti wasintha maonekedwe

KUSINTHA ZINTHU

, Miy 24:21 ofuna kusintha zinthu

Mko 10:11 wasiya mkazi wake nʼkukwatira

KUSIYANITSA

, Le 11:47 muzisiyanitsa chodetsedwa

Mki 3:18 kusiyana pakati pa wolungama

Ahe 5:14 kusiyanitsa zoyenera

KUTALI

, Mac 17:27 sali kutali ndi aliyense wa ife

KUTAMANDIDWA

, 1Mb 16:25 Yehova ndi woyenera kutamandidwa

KUTENGERANA KUKHOTI

, 1Ak 6:7 ngati mukutengerana kukhoti

KUTETEZA

, Afi 1:7 poteteza uthenga wabwino

KUTHA

, 2Ak 4:16 munthu wathu wakunja akutha

KUTHETSA BANJA

, Mki 2:16 ndimadana ndi zothetsa mabanja

KUTOPA

, Miy 25:25 kwa munthu wotopa

Yes 40:28 Iye satopa kapena kufooka

Yes 40:29 amapereka mphamvu kwa wotopa

Yes 40:31 Adzayenda koma osatopa

Yes 50:4 munthu amene watopa

Aga 6:9 tidzakolola tikapanda kutopa

Ahe 12:3 musatope nʼkutaya mtima

KUUGWIRA MTIMA

, 2Ti 2:24 wougwira mtima ena akamulakwira

KUUMA MTIMA

, Mko 3:5 chisoni chifukwa cha kuuma mtima

KUUMITSA

, De 15:7 kumuumitsira dzanja

KUVALA

, Miy 7:10 Atavala ngati hule

KUVUTIKA MAGANIZO

, Afi 2:26 [Epafurodito] akuvutika maganizo

KUWALA

, Sl 36:9 kuwala kochokera kwa inu

Sl 119:105 kuwala kounikira njira yanga

Miy 4:18 njira ya olungama ili ngati kuwala

Yes 42:6 ngati kuwala ku mitundu ya anthu

Mt 5:14 ndinu kuwala kwa dziko

Mt 5:16 muzionetsa kuwala kwanu

Yoh 8:12 ndine kuwala kwa dziko

2Ak 4:6 Kuwale kuchokera mumdima

KUWAWA

, Aro 8:22 kumva kuwawa mpaka pano

KUWODZERA

, Miy 23:21 kuwodzera kudzamuveka nsanza

KUWONGOLERA

, Yer 10:23 ulamuliro wowongolera mapazi

KUYANDIKIRA

, Yak 4:8 Yandikirani Mulungu

KUYESA

, De 13:3 Yehova akukuyesani kuti adziwe

KUYESEDWA

, Mt 6:13 kuti tisagonje tikamayesedwa

KUZAMA

, Aro 11:33 Nzeru zake nʼzozama

Aef 3:18 kumvetsa kuzama kwa choonadi

KWANIRITSA

, Yes 55:11 kukwaniritsa cholinga

Mt 5:17 ndinabwera kudzazikwaniritsa

KWANITSA

, Yob 42:2 palibe chimene simungakwanitse

KWAPULA

, Miy 13:24 amene sakwapula mwana wake

KWATIRA

, Mt 19:12 sakwatira, anabadwa choncho

Mt 22:30 akadzaukitsidwa sadzakwatira

Mt 24:38 Chigumula chisanafike ankakwatira

1Ak 7:8 osakwatira ndi akazi amasiye

1Ak 7:9 ndi bwino kukwatira kusiyana nʼkuvutika

1Ak 7:32 wosakwatira amadera nkhawa

1Ak 7:36 akwatire. Sakuchimwa

KWATIWA

, 1Ak 7:39 akwatiwe mwa Ambuye

KWERA

, Yoh 3:13 palibe anakwera kumwamba

KWEZA

, Ge 15:5 Kweza maso ako kumwamba

KWIYA

, Sl 103:8 Yehova ndi wosakwiya msanga

Miy 14:17 amene amakwiya msanga amachita

1Ak 13:5 sichikwiya, sichisunga zifukwa

Aef 4:26 Dzuwa lisalowe mudakali okwiya

Akl 3:8 Mutaye mkwiyo, mawu achipongwe

L

LAKALAKA

, Yob 14:15 Mudzalakalaka ntchito

Sl 84:2 ukulakalaka mabwalo a Yehova

Yes 26:9 ndimakulakalakani ndi mtima wonse

1Pe 1:14 siyani kutsatira zimene munkalakalaka

1Pe 2:2 muzilakalaka mkaka umene uli mʼMawu

LAKWITSA

, Yob 6:24 ndimvetse zimene ndalakwitsa

LALATA

, Aef 4:31 kupsa mtima, mkwiyo, kulalata

LALIKIDWA

, Mt 24:14 udzalalikidwa padziko lonse

LALIKIRA

, Mt 9:35 kulalikira uthenga wabwino

Aro 10:14 popanda wina kulalikira?

Akl 1:23 uthenga wabwino unalalikidwa padziko

2Ti 4:2 Lalikira mawu modzipereka

2Pe 2:5 ankalalikira za chilungamo

LALINGʼONO

, Mt 7:13 Lowani pageti lalingʼono

LAMBA

, Yes 11:5 Chilungamo chidzakhala lamba

LAMBIRA

, Mt 4:10 Yehova uyenera kumulambira

Yoh 4:24 akuyenera kumulambira

LAMULA

, Mac 5:28 Tinakulamulani mwamphamvu

LAMULIRA

, Ge 3:16 mwamuna azidzakulamulira

Sl 119:133 Musalole choipa chindilamulire

Miy 10:19 amalamulira milomo yake

Miy 16:32 amene amalamulira mkwiyo wake

Miy 29:2 woipa akamalamulira, anthu amabuula

Mla 8:9 wapweteka mnzake pomulamulira

Yes 9:7 Ulamuliro wake udzafika kutali

Da 4:17 Wamʼmwambamwamba ndi Wolamulira

Da 4:34 ulamuliro wake udzakhalapo

Mt 28:18 Ulamuliro wonse waperekedwa kwa ine

Lu 4:6 Ndikupatsani ulamuliro pa maufumu

Yoh 12:31 wolamulira wa dzikoli aponyedwa kunja

Yoh 12:42 olamulira anamukhulupirira

Yoh 14:30 wolamulira wa dziko akubwera

Mac 4:26 olamulira, alimbane ndi Yehova

Aro 6:12 uchimo uzilamulirabe ngati mfumu

Aro 13:1 azimvera olamulira akuluakulu

1Ak 6:12 kuti chinthu china chizindilamulira

1At 4:4 azidziwa kulamulira thupi lake

Tit 3:1 kumvera maboma ndi olamulira

Chv 11:15 adzalamulira monga mfumu

LAMULO

, Hab 1:4 lamulo latha mphamvu

Mt 22:40 Chilamulo chagona pa malamulo awiri

Mko 12:28 Kodi lamulo loyamba ndi liti?

Mko 12:31 Palibe lamulo lalikulu kuposa

Yoh 13:34 lamulo latsopano, muzikondana

Aro 13:8 wokonda mnzake wakwaniritsa lamulo

2Ti 2:5 kupikisana motsatira malamulo

Yak 2:8 mukutsatira lamulo lachifumu

LANDA

, Le 19:13 musamalande zinthu za aliyense

LANDIDWA

, Ahe 10:34 katundu wanu akulandidwa

LANDIRA

, Yob 2:10 tizingolandira zabwino?

Mt 5:5 ofatsa adzalandira dziko lapansi

Aro 14:1 Landirani munthu amene ali

Ahe 6:4 analandira mphatso yakumwamba

LANGA

, Miy 19:18 Langa mwana wako

Mla 8:11 ochita zoipa sanalangidwe mwamsanga

Chv 3:19 amene ndimawakonda ndimawalanga

LANGIZA

, De 8:5 Yehova wanu ankakulangizani

Owe 13:8 adzatilangize za mwana

Sl 32:8 kukulangiza njira yoyendamo

Sl 94:12 Wosangalala amene mumamulangiza

Aro 15:4 zinalembedwa kuti zitilangize

LANKHULA

, Eks 4:10 kulankhula kumandivuta

Miy 14:23 kungolankhula chabe kumasaukitsa

Yes 35:6 lilime la munthu wosalankhula

LAPA

, Lu 15:7 wochimwa amene walapa

Mac 3:19 lapani ndi kutembenuka

Mac 17:30 anthu kwina kulikonse alape

Mac 26:20 pochita zinthu zosonyeza kulapa

Aro 2:4 nʼcholinga choti ulape

2Ak 7:10 Kumva chisoni kumachititsa kulapa

Chv 16:11 Ananyoza Mulungu, ndipo sanalape

LATSOPANO

, Yoh 13:34 Ndikukupatsani lamulo latsopano

Chv 21:1 dziko lapansi latsopano

LAVULA

, Mt 26:67 anayamba kumulavulira kunkhope

LAWA

, Sl 34:8 Talawani, Yehova ndi wabwino

1Pe 2:3 ngati mutalawa nʼkuona kuti

LAZARO

, Lu 16:20 Lazaro wopemphapempha

Yoh 11:11 Mnzathu Lazaro ali mʼtulo

Yoh 11:43 Lazaro, tuluka!

LEKANITSA

, Miy 17:9 amalekanitsa mabwenzi

Mt 25:32 amalekanitsira nkhosa ndi mbuzi

LEKERERA

, 2Mf 10:16 sindilekerera zoti anthu azipikisana

Miy 29:15 mwana womulekerera

Hab 1:13 simungalekerere khalidwe loipa

Aro 9:22 analekerera moleza mtima

LEMBEDWA

, Aro 15:4 zimene zinalembedwa kalekale

LEMEDWA

, Lu 21:34 mitima yanu isalemedwe

LEMEKEZA

, Eks 20:12 Muzilemekeza bambo ndi mayi

Miy 3:9 Uzilemekeza Yehova

1Ak 16:18 anthu otere muziwalemekeza

Aef 5:33 mkazi azilemekeza mwamuna

1At 5:12 muzilemekeza amene akugwira ntchito

1Ti 5:17 azilemekezedwa kwambiri

LEMEKEZEKA

, 1Ak 1:26 si ambiri a mʼmabanja olemekezeka

2Ti 2:20 Zinthu za ntchito yolemekezeka

LEMERA

, Le 19:15 Musamakondere wolemera

Miy 10:22 Madalitso a Yehova amalemeretsa

Lu 14:12 Ukakonza chakudya usaitane olemera

2Ak 6:10 osauka koma olemeretsa anthu

1Ti 6:9 ofunitsitsa kulemera amakodwa

Chv 3:17 ukunena kuti: Ndine wolemera

LENGA

, Ge 1:1 Pachiyambi, Mulungu analenga

Sl 104:30 Mukatumiza mzimu wanu zimalengedwa

Yes 45:18 Amene sanalilenge popanda cholinga

Aro 1:20 Kuchokera pamene dziko linalengedwa

Aro 8:20 chilengedwe chinaweruzidwa

2Ak 5:17 iye ndi cholengedwa chatsopano

Akl 1:16 Kudzera mwa iye, Mulungu analenga

Chv 3:14 woyamba wa chilengedwe cha Mulungu

Chv 4:11 chifukwa munalenga zinthu zonse

LENGEZA

, Eks 9:16 dzina langa lilengezedwe

Sl 68:11 akazi amene akulengeza ndi gulu lalikulu

Lu 8:1 kulengeza uthenga wabwino

1Ak 11:26 mumakhala mukulengeza imfa

LEPHERA

, Sl 84:11 sadzalephera kupereka chabwino

Miy 3:27 Usalephere kuchitira zabwino

LEPHEREKA

, Miy 13:12 chikalephereka, mtima umadwala

LEPHERETSA

, Yes 14:27 ndani angazilepheretse?

Mko 4:19 nʼkulepheretsa mawuwo kukula

LETSA

, 1At 2:16 akuyesa kutiletsa kulalikira

LEVI

, Mki 3:3 Adzayeretsa ana a Levi

LEZA MTIMA

, Ne 9:30 Munawalezera mtima

Miy 25:15 Chifukwa cha kuleza mtima

Aro 9:22 analekerera moleza mtima

1Ak 13:4 Chikondi nʼcholeza mtima

1At 5:14 oleza mtima kwa onse

Yak 5:8 khalani oleza mtima

2Pe 3:9 Yehova akukulezerani mtima

2Pe 3:15 kuleza mtima kwa Ambuye

LIDIYA

, Mac 16:14 Lidiya ankagulitsa nsalu zapepo

LIKASA

, Eks 25:10 likasa la mtengo wa mthethe

2Sa 6:6 Uza anagwira Likasa

1Mb 15:2 Alevi okha azinyamula Likasa

LILIME

, Sl 34:13 muteteze lilime lanu

Miy 18:21 moyo zili mumphamvu ya lilime

Yes 35:6 lilime la wosalankhula lidzafuula

Yes 50:4 wandipatsa lilime la anthu

Yak 1:26 satha kulamulira lilime lake

Yak 3:8 palibe angathe kuweta lilime

LIMBA

, Yes 35:3 Limbitsani manja ofooka

Yes 35:4 Limbani mtima

Aro 15:1 Ife olimba tiziganizira anthu

Akl 2:7 chikhale cholimba

LIMBA MTIMA

, Yos 1:7 Ukhale wolimba mtima

Miy 28:1 olungama ndi olimba mtima

Mac 4:31 analankhula molimba mtima

Mac 28:15 Paulo atawaona analimba mtima

1Ak 16:13 khalani olimba mtima

2Ak 5:6 timakhala olimba mtima

Aef 6:20 ndilankhule molimba mtima

Afi 1:14 kulimba mtima polankhula mawu

1At 2:2 tinalimba mtima mothandizidwa ndi

LIMBANA

, Mac 5:38 musalimbane nawo

Mac 5:39 mukulimbana ndi Mulungu

LIMBIKITSA

, Yob 2:11 akatonthoze Yobu nʼkumulimbikitsa

Mt 5:4 achisoni adzalimbikitsidwa

Lu 22:32 ukalimbikitse abale ako

Mac 13:15 mawu olimbikitsa

Aro 1:12 ndidzalimbikitsidwe, mudzalimbikitsidwe

Aro 1:12 kapena kuti ndidzalimbikitsidwe

Aro 14:19 tiziyesetsa kulimbikitsana

Aro 15:4 Malembawa amatilimbikitsa

1Ak 8:1 koma chikondi chimalimbikitsa

1Ak 10:23 si zonse zomwe zimalimbikitsa

1Ak 14:26 kuti mulimbikitsane

1Ak 14:31 aphunzire ndi kulimbikitsidwa

Akl 3:16 Pitirizani kulimbikitsana

1At 2:11 tinkamudandaulira, kumulimbikitsa

1Ti 3:15 umalimbikitsa ndi kuteteza choonadi

Tit 1:9 kulimbikitsa anthu ndi mfundo

Ahe 10:25 tiyeni tilimbikitsane

Ahe 10:24 tilimbikitsane pa chikondi

LIMBITSA

, Yes 41:10 Ndikulimbitsa, ndikuthandiza

Mac 14:22 onsewa ankalimbitsa ophunzira

1Ak 1:8 Mulungu adzakulimbitsani

1Pe 5:10 Mulungu adzakulimbitsani

Yuda 20 muzilimbitsa chikhulupiriro chanu

LIPIRIRA

, 1At 2:6 tikanapempha kuti mutilipirire

LIPOTI

, Nu 14:36 anabweretsa lipoti loipa

Da 11:44 malipoti adzaisokoneza

LIRA

, Sl 6:6 Ndimalira, misozi imadzaza

Yes 65:19 losonyeza kuti munthu akulira

Ho 12:4 Analira komanso anachonderera

Lu 6:21 amene mukulira

Aro 12:15 muzilira ndi amene akulira

LODZA

, Nu 23:23 Palibe amene angalodze Yakobo

LOKONGOLA

, Da 11:45 phiri la Dziko Lokongola

LOLEKA

, 1Ak 6:12 Zinthu zonse ndi zololeka

LOLERA

, Aef 4:2 muzilolerana chifukwa cha chikondi

Afi 4:5 onse adziwe kuti ndinu ololera

LONDOLA

, 2Ti 1:13 mawu olondola

Tit 2:1 mfundo zolondola

LONJEZA

, De 23:21 kukwaniritsa zimene mwalonjezazo

Owe 11:30 Yefita analonjeza Yehova

1Mf 8:56 mogwirizana ndi zimene analonjeza

Sl 15:4 Sasintha zimene walonjeza

Ahe 10:23 amene watilonjeza ndi wokhulupirika

LONJEZO

, 2Ak 1:20 malonjezo a Mulungu

LOSERA

, Yow 2:28 ana anu adzalosera

LOTI

, Lu 17:32 Kumbukirani mkazi wa Loti

2Pe 2:7 anapulumutsa Loti wolungama

LOWA

, Mt 25:34 Lowani mu Ufumu anakukonzerani

LOWERERA

, 1Ti 5:13 kulowerera nkhani za eni

1Pe 4:15 akulowerera nkhani za eni

LUDZU

, Yes 49:10 sadzamva ludzu

Yes 55:1 amene mukumva ludzu

Yoh 7:37 Ngati wina akumva ludzu

LUKA

, Akl 4:14 Luka, dokotala wokondedwa

LUMA

, Aga 5:15 Koma mukapitiriza kulumana

LUMALA

, Yes 35:6 wolumala adzadumpha

Mki 1:8 Mukapereka nyama yolumala

LUMBIRA

, Ge 22:16 Ndikulumbira pali dzina langa

Mt 5:34 Musamalumbire nʼkomwe

LUMIKIZANA

, Aef 4:16 ziwalo ndi zolumikizana bwino

LUNGAMA

, Ge 15:6 anamuona kuti ndi wolungama

Sl 34:19 Mavuto a wolungama ndi ambiri

Sl 37:25 sindinaonepo wolungama atasiyidwa

Sl 72:7 wolungama zidzamuyendera bwino

Sl 141:5 Wolungama akandimenya

Miy 24:16 wolungama akhoza kugwa ka 7

Zef 2:3 Yesetsani kukhala olungama

1Pe 3:12 Maso a Yehova ali pa olungama

LUPANGA

, 1Sa 17:47 sapulumutsa ndi lupanga

Yes 2:4 adzasula malupanga awo

Mt 26:52 ogwira lupanga adzafa ndi lupanga

Aef 6:17 nyamulani lupanga la mzimu

Ahe 4:12 akuthwa kuposa lupanga

LUSO

, Eks 35:35 luso loluka nsalu ndi ulusi

Miy 22:29 munthu waluso pa ntchito yake?

Mt 25:15 Aliyense mogwirizana ndi luso lake

LUSO LA KUPHUNZITSA

, 2Ti 4:2 uzichita izi ndi luso la kuphunzitsa

M

MABALA

, Miy 23:29 mabala popanda chifukwa?

Miy 27:6 Mabala ovulazidwa ndi mnzako

Yes 53:5 chifukwa cha mabala ake tinachiritsidwa

MABERE

, Miy 5:19 Mabere ake azikukhutiritsa

MADENGU

, Mt 14:20 zinadzaza madengu 12

MADZI

, Nu 20:10 madzi mʼthanthweli?

Miy 20:5 ngati madzi akuya

Miy 25:25 ngati madzi ozizira

Yes 55:1 mudzamwe madzi

Yer 2:13 kasupe wa madzi

Yer 50:38 Madzi ake adzawonongedwa

Zek 14:8 madzi amoyo adzatuluka

Yoh 4:10 akanakupatsani madzi amoyo

Chv 7:17 akasupe a madzi a moyo

Chv 17:1 lakhala pamadzi ambiri

MAERE

, Sl 22:18 akuchita maere pa zovala zanga

MAFANIZO

, Mt 13:34 ankagwiritsa ntchito mafanizo

Mko 4:2 ankawaphunzitsa ndi mafanizo

MAFANO

, Sl 115:4 Mafano opangidwa ndi siliva

Yes 41:29 Mafano ndi opanda ntchito

1Yo 5:21 muzipewa mafano

MAFUMU

, Miy 22:29 adzaima pamaso pa mafumu

Lu 21:12 Adzakupititsani kwa mafumu

Mac 4:26 Mafumu a dziko anaima pamalo awo

Chv 1:6 nʼkutipanga kukhala mafumu

Chv 5:10 adzakhala mafumu olamulira dziko

Chv 18:3 mafumu anachita naye chiwerewere

MAFUTA

, 1Mf 17:16 mafuta amumtsuko sanathe

Mt 25:4 ochenjerawo anatenga mafuta

Mko 14:4 Nʼchifukwa chiyani akuwononga mafuta?

MAGALASI

, 2Ak 3:18 magalasi oonetsa ulemerero

MAGALETA

, Owe 4:13 magaleta okhala ndi zitsulo

2Mf 6:17 magaleta ankhondo oyaka moto

MAGANIZO

, Ge 8:21 maganizo amakhala oipa

1Mb 28:9 amazindikira maganizo a munthu

Sl 26:2 Yengani maganizo anga

Sl 139:17 maganizo anu ndi ofunika

Sl 146:4 zimene amaganiza zimatheratu

Miy 20:5 Maganizo ali ngati madzi akuya

Yes 55:8 Maganizo anga, maganizo anu

Mt 22:37 Muzikonda Yehova ndi maganizo onse

Aro 7:25 mʼmaganizo mwanga ndine kapolo

Aro 14:1 musamaweruze a maganizo osiyana

1Ak 2:16 tili ndi maganizo a Khristu

2Ak 10:5 tikugonjetsa maganizo alionse

Afi 2:5 maganizo amenenso Khristu anali nawo

Akl 2:18 maganizo amamuchititsa kudzitukumula

Chv 2:23 ndimafufuza maganizo

Chv 17:17 mogwirizana ndi maganizo ake

MAGAWO 10

, Mki 3:10 gawo limodzi pa magawo 10

MAGAZI

, Ge 9:4 musadye limodzi ndi magazi ake

Le 7:26 Musamadye magazi alionse

Le 17:11 moyo wa nyama uli mʼmagazi

Le 17:13 azithira magazi ake pansi

Sl 72:14 magazi awo ndi amtengo wapatali

Eze 3:18 ndidzakuimba mlandu wa magazi ake

Mt 9:20 matenda otaya magazi zaka 12

Mt 26:28 akuimira magazi anga a pangano

Mt 27:25 Magazi ake akhale pa ife

Mac 15:29 kupitiriza kupewa magazi

Mac 20:26 ndilibe mlandu wa magazi a anthu onse

Mac 20:28 anaugula ndi magazi a Mwana wake

Aef 1:7 tinamasulidwa ndi dipo la magazi ake

1Pe 1:19 munamasulidwa ndi magazi a Khristu

1Yo 1:7 magazi a Yesu akutiyeretsa

Chv 18:24 munapezeka magazi a aneneri

MAGOGI

, Eze 38:2 Gogi wa kudziko la Magogi

MAGULU ANKHONDO

, Chv 19:14 magulu ankhondo akumwamba

MAKALA

, Aro 12:20 udzamuunjikira makala a moto

MAKALATA A PANGANO

, Yer 32:12 makalata a pangano kwa Baruki

MAKANI

, Mac 19:9 anapitiriza kuchita makani

MAKEDONIYA

, Mac 16:9 Wolokerani ku Makedoniya

MAKHALIDWE

, Aef 4:19 sakuzindikira makhalidwe abwino

Afi 1:27 makhalidwe ogwirizana ndi uthenga

MAKIYI

, Mt 16:19 ndidzakupatsa makiyi a Ufumu

Chv 1:18 ndili ndi makiyi a imfa ndi Manda

MAKOLO

, Lu 18:29 azichimwene, makolo

Lu 21:16 makolo anu, azichimwene anu

2Ak 12:14 chidzathandize makolo awo

Aef 6:1 muzimvera makolo anu

Akl 3:20 muzimvera makolo anu pa zonse

MALAMULO

, Sl 94:20 pogwiritsa ntchito malamulo?

Aro 7:22 ndimasangalala ndi malamulo a Mulungu

MALAMULO KHUMI

, Eks 34:28 analemba Malamulo Khumi

MALANGIZO

, 1Mb 15:13 sitinatsatire malangizo ake

Miy 1:7 Zitsiru zimanyoza malangizo

Miy 3:11 usakane malangizo a Yehova

Miy 11:14 popanda malangizo, anthu amagwa

MALEMBA

, Mt 22:29 simudziwa Malemba

Lu 24:32 kutifotokozera Malemba momveka bwino

Mac 17:2 anakambirana mfundo za mʼMalemba

Mac 17:11 ankafufuza Malemba mosamala

Aro 15:4 Malembawa amatithandiza kupirira

2Ti 3:16 Malemba onse anauziridwa ndi Mulungu

MALIKO

, Akl 4:10 Maliko msuweni wa Baranaba

MALILIME

, 1Ak 13:8 kulankhula malilime, kudzatha

1Ak 14:22 malilime, chizindikiro cha osakhulupirira

MALIPIRO

, Ge 31:7 asintha malipiro anga

Yer 22:13 kuwapatsa malipiro awo

Aro 6:23 malipiro a uchimo

MALIRE

, Sl 119:96 malamulo anu alibe malire

MALIRO

, Mla 7:2 kupita kunyumba yamaliro

MALIZA

, Mac 20:24 ndimalize utumiki

MALONDA

, Mt 13:45 wamalonda amene akufunafuna ngale

Mt 22:5 anapita kumalonda ake

2Ak 2:17 sitichita nawo malonda

Yak 4:13 Tikachita malonda nʼkupeza phindu

Chv 18:3 Amalonda apadziko analemera

MALO ODYETSERA

, Yes 30:23 pamalo odyetserapo ziweto

MALO OTETEZEKA

, Sl 26:12 Phazi langa laima pamalo otetezeka

MALO OTHAWIRAKO

, Sl 9:9 Yehova malo otetezeka othawirako

MALOTO

, Mla 5:3 Maloto amabwera

MALUWA

, Yes 35:1 Dera lidzachita maluwa

Lu 12:27 Ganizirani mmene maluwa amakulira

MAMATIRA

, Yos 23:8 kumamatira Yehova Mulungu

MAMBA

, Yes 11:8 adzasewera pa una wa mamba

MAME

, De 32:2 Mawu adzatsika ngati mame

Sl 110:3 achinyamata ali ngati mame

MANA

, Eks 16:31 anachipatsa dzina lakuti mana

Yos 5:12 Mana analeka kugwa

Miy 23:6 chakudya cha munthu womana

MANASE

, 2Mb 33:13 Manase anadziwa kuti Yehova

MANDA

, Yob 14:13 mukanandibisa mʼManda

Mla 9:10 ku Manda kulibe kugwira ntchito

Ho 13:14 ndidzawawombola ku Manda

Mac 2:31 Khristu sanasiyidwe mʼManda

Chv 1:18 makiyi a imfa ndi a Manda

Chv 20:13 Manda anapereka akufa

MANDA ACHIKUMBUTSO

, Yoh 5:28 ali mʼmanda achikumbutso adzamva

MANGA

, Ge 22:9 anamanga Isaki mwana wakeyo

Sl 127:1 Yehova akapanda kumanga nyumba

Yes 61:1 Anandituma kuti ndikamange mabala

Yes 65:21 adzamanga nyumba nʼkumakhalamo

Eze 34:16 yovulala ndidzaimanga

Mt 16:19 chimene udzamanga padziko lapansi

Mt 19:6 Mulungu wachimanga pamodzi

Lu 17:28 ankadzala komanso kumanga

1Ak 3:10 aliyense asamale mmene akumangirapo

MANJA

, Yes 35:3 Limbitsani manja ofooka

MANKHUSU

, Zef 2:2 Tsiku lisanadutse ngati mankhusu

MANKHWALA

, Miy 17:22 Mtima wosangalala ndi mankhwala

Chv 3:18 mankhwala opaka mʼmaso

MANTHA

, Yob 31:34 Kodi ndinachitapo mantha?

Yob 31:34 mantha ndi gulu la anthu

Yes 41:10 Usachite mantha, chifukwa ndili nawe

Yes 44:8 musathedwe nzeru ndi mantha

Lu 21:26 Anthu adzakomoka ndi mantha

Afi 1:28 simukuchita mantha

2Ti 1:7 sanatipatse mzimu wamantha

1Yo 4:18 wokonda Mulungu sachita mantha

Chv 2:10 Usachite mantha ndi mavuto

MANYAZI

, Eza 9:6 ndikuchita manyazi kuti ndikweze

Sl 25:3 palibe adzachite manyazi

Mko 8:38 aliyense wochita manyazi ndi ine

Aro 1:16 sindichita manyazi ndi uthenga wabwino

1Ak 4:14 Sindikulemba kuti ndikuchititseni manyazi

Aef 5:4 khalidwe lochititsa manyazi

2Ti 1:8 usachite manyazi ndi ntchito yolalikira

2Ti 2:15 wosachita manyazi ndi ntchito

Ahe 11:16 Mulungu sachita manyazi kutchulidwa

1Pe 4:16 Mkhristu asachite manyazi

MAOLIVI

, Aro 11:17 mtengo wa maolivi wamʼtchire

MAONEKEDWE

, Mt 22:16 simuyangʼana maonekedwe a anthu

2Ak 10:7 potengera maonekedwe akunja

Aga 2:6 Mulungu sayangʼana maonekedwe

MAPAZI

, Yes 52:7 Mapazi obweretsa uthenga

Yer 10:23 ulamuliro wowongolera mapazi

Yoh 13:5 nʼkuyamba kusambitsa mapazi awo

Aro 16:20 aphwanya Satana pa mapazi anu

1Ak 15:27 anaika pansi pa mapazi ake

1Pe 2:21 mutsatire mapazi ake mosamala

MAPETO

, Mt 24:14 kenako mapeto adzafika

Mt 28:20 mpaka mʼnyengo ya mapeto a nthawi ino

Yoh 13:1 anawakonda mpaka pamapeto

2Ti 4:7 Ndathamanga mpaka pamapeto

MAPIKO

, Ru 2:12 wathawira mʼmapiko mwake

MAPIRI

, Ge 7:20 Madziwo anapitirira mapiriwo

MARITA

, Lu 10:41 Marita, ukuda nkhawa

MARIYA 1.

, Mko 6:3 kalipentala, mwana wa Mariya

MARIYA 2.

, Lu 10:39 Mariya ankamvetsera

Lu 10:42 Mariya wasankha chinthu chabwino

Yoh 12:3 Mariya anatenga mafuta okwera mtengo

MARIYA 3.

, Mt 27:56 Mariya wa ku Magadala

Lu 8:2 Mariya, anamutulutsa ziwanda 7

MARIYA 4.

, Mt 27:56 Mariya mayi a Yakobo

MARIYA 5.

, Mac 12:12 Mariya mayi a Yohane Maliko

MASAMBA

, Eze 47:12 masamba adzakhala mankhwala

Mt 24:32 Nthambi ikaphuka nʼkuchita masamba

MASEWERA

, Miy 10:23 kuli ngati masewera

MASIKU OTSIRIZA

, 2Ti 3:1 masiku otsiriza, nthawi yovuta

MASO

, Sl 115:5 Maso ali nawo

Miy 15:3 Maso a Yehova ali paliponse

MASOMPHENYA

, Da 10:14 masomphenyawa ndi okhudza

MASULA

, Mt 18:18 zilizonse zimene mudzamasule

Yoh 8:32 choonadi chidzakumasulani

MASULIDWA

, Aro 6:18 munamasulidwa ku uchimo

MATA

, Da 12:9 akuyenera kumatidwa mpaka mapeto

MATALENTE

, Mt 25:15 anamupatsa matalente 5

MATENDA

, Yes 53:4 ananyamula matenda athu

Mt 9:35 ankachiritsa matenda alionse

MATSENGA

, De 18:10 aliyense wochita zamatsenga

Mac 13:6 Myuda wina wamatsenga

Mac 19:19 azamatsenga anatentha mabuku

MAUFUMU

, Mt 4:8 anamuonetsa maufumu

MAVUTO

, 2Sa 22:7 Pa mavuto, ndinaitana Yehova

Yob 6:2 mavuto anga onse akanayezedwa

Yob 36:15 amapulumutsa ovutika pa mavuto

Sl 34:19 Mavuto a munthu wolungama

Sl 46:1 Thandizo pa nthawi ya mavuto

Sl 119:50 zimandilimbikitsa ndikakhala pamavuto

Sl 119:71 Zili bwino kuti ndakumana ndi mavuto

Miy 27:12 wosadziwa amakumana ndi mavuto

Mac 14:22 Tiyenera kukumana ndi mavuto ambiri

Aro 5:3 kumasangalala tikakumana ndi mavuto

Aro 8:18 mavuto amene tikukumana nawo

Aro 12:12 Muzipirira mavuto

1Ak 7:28 adzakumana ndi mavuto pa moyo

2Ak 1:8 Tinakumana ndi mavuto aakulu

2Ak 4:17 mavuto amene tikukumana nawo

2At 1:4 kulimbana ndi mavuto

Ahe 2:10 anakhala wangwiro kudzera mʼmavuto

1Pe 5:9 akukumananso ndi mavuto

MAWA

, Miy 27:1 Usadzitame ndi zimene udzachite mawa

1Ak 15:32 tidye ndi kumwa, mawa tifa

MAWU

, 1Mf 19:12 panamveka mawu achifatse

Sl 19:4 mawu awo amveka padziko

Miy 25:11 Mawu olankhulidwa nthawi yoyenera

Yes 55:11 mawu otuluka pakamwa

Lu 8:12 amabwera nʼkudzachotsa mawuwo

Yoh 1:1 ankadziwika kuti Mawu

Yoh 5:28 adzamva mawu ake

Yoh 10:27 zimamva mawu anga

Yoh 17:17 Mawu anu ndi choonadi

Mac 18:5 ntchito yolalikira mawu a Mulungu

Afi 2:16 mugwire mawu amoyo

2Ti 2:15 kufotokoza bwino mawu

Yak 1:22 muzichita zimene mawu amanena

MAWU ACHIPONGWE

, Aef 4:31 kulalata, mawu achipongwe

MAWU A MULUNGU

, Yes 40:8 mawu a Mulungu wathu

Mko 7:13 mawu a Mulungu akhale opanda pake

1At 2:13 munalandira mawu a Mulungu

Ahe 4:12 mawu a Mulungu ndi amoyo

MAWU OKOMA

, Miy 25:15 mawu okoma angathyole

MAWU OPWETEKA

, Miy 15:1 mawu opweteka amayambitsa mkwiyo

MAYESERO

, Mt 26:41 kuti musalowe mʼmayesero

Lu 22:28 mwakhalabe ndi ine mʼmayesero anga

1Ak 10:13 Palibe mayesero

Yak 1:2 mukukumana ndi mayesero

Yak 1:12 amene akupirira mayesero

MAYI

, Eks 20:12 Muzilemekeza bambo ndi mayi anu

Sl 27:10 Ngakhale bambo, mayi, atandisiya

Miy 23:22 usanyoze mayi chifukwa akalamba

Lu 8:21 Mayi ndi azichimwene anga ndi awa

Yoh 19:27 Awa akhala mayi ako

Aga 4:26 Yerusalemu wamʼmwamba, mayi athu

MAZIKO

, Lu 6:48 nʼkuyala maziko pathanthwe

Aro 15:20 ndisamange pamaziko

1Ak 3:11 angayale maziko ena

MBADWA

, Ge 3:15 chidani pakati pa mbadwa yako

Ge 22:17 ndidzachulukitsadi mbadwa zako

Yes 65:23 mbadwa za odalitsidwa ndi Yehova

Aga 3:16 kwa mbadwa yako, Khristu

Aga 3:29 ndinudi mbadwa za Abulahamu

MʼBADWO

, Mt 24:34 mʼbadwo sudzatha wonse

MBALAME

, Mt 6:26 Yangʼanitsitsani mbalame

MʼBALE

, Miy 17:17 mʼbale anabadwa kuti akuthandize

Miy 18:24 mnzako amakhala pafupi kuposa mʼbale

Mt 23:8 nonsenu ndinu abale

Mt 25:40 mmodzi wa abale anga

1Ak 5:11 aliyense wotchedwa mʼbale

1Pe 5:9 abale anu padziko lonse

MBEWU

, Lu 8:11 Mbewuzo ndi mawu a Mulungu

MBIRI

, Mla 7:1 Mbiri yabwino imaposa mafuta

MBIYA

, Aro 9:21 woumba mbiya ali ndi ufulu

MBONI

, De 19:15 mboni ziwiri kapena zitatu

Yes 43:10 Inu ndinu mboni zanga

Mt 18:16 umboni wa mboni ziwiri

Mac 1:8 mudzakhala mboni zanga

Chv 1:5 Yesu Khristu, Mboni Yokhulupirika

Chv 11:3 ndidzachititsa kuti mboni zanga

MʼBUSA

, Sl 23:1 Yehova ndi Mʼbusa wanga

Yes 40:11 adzasamalira nkhosa ngati mʼbusa

Eze 34:2 abusa akungodzidyetsa

Eze 37:24 adzakhala ndi mʼbusa mmodzi

Zek 13:7 nyamuka ubaye mʼbusa wanga

Mt 9:36 nkhosa zimene zilibe mʼbusa

Yoh 10:11 Mʼbusa wabwino amapereka moyo wake

Yoh 10:14 Ine ndine mʼbusa wabwino

Yoh 10:16 gulu limodzi mʼbusa mmodzi

Aef 4:11 ena abusa ndi aphunzitsi

MBUYE

, De 10:17 Yehova ndi Mbuye wa ambuye

Mt 7:22 Ambuye, kodi ife sitinalosere?

Mt 22:44 Yehova anauza Ambuye wanga

1Ak 7:39 kukwatiwa mwa Ambuye

MBUZI

, Le 16:8 mbuzi yotenga machimo

Mt 25:32 amalekanitsa nkhosa ndi mbuzi

MCHENGA

, Ge 22:17 mbadwa zako ngati mchenga

Chv 20:8 ochuluka ngati mchenga wakunyanja

MCHERE

, Ge 19:26 anasanduka chipilala chamchere

Mt 5:13 Inu ndinu mchere wa dziko

Akl 4:6 okoma ngati mwawathira mchere

MCHIMWENE

, Mt 13:55 azichimwene ake si Yakobo

MDANI

, Aro 12:20 ngati mdani wako ali ndi njala

MDIMA

, Yes 60:2 Mdima udzaphimba dziko

Yow 2:31 Dzuwa lidzasanduka mdima

Zef 1:15 Tsiku la mdima wochititsa mantha

Mt 4:16 okhala mumdima anaona kuwala

Yoh 3:19 anthu akukonda mdima

Aef 4:18 ali mumdima wa maganizo

1Pe 2:9 anakuitanani muchoke mumdima

MDULIDWE

, Aro 2:29 mdulidwe wochitidwa ndi mzimu

1Ak 7:19 Mdulidwe sutanthauza chilichonse

MDYEREKEZI

, Mt 25:41 moto umene anakolezera Mdyerekezi

Lu 4:6 Mdyerekezi anati ali ndi ulemerero

Lu 8:12 Mdyerekezi amadzachotsa mawuwo

Yoh 8:44 ndinu ochokera kwa Mdyerekezi

Aef 4:27 Musamupatse mpata Mdyerekezi

Aef 6:11 musagonje kwa Mdyerekezi

Yak 4:7 tsutsani Mdyerekezi, adzakuthawani

1Pe 5:8 Mdyerekezi, mkango wobangula

1Yo 3:8 awononge ntchito za Mdyerekezi

Chv 12:12 Tsoka, Mdyerekezi watsikira kwa inu

Chv 20:10 Mdyerekezi, adzaponyedwa mʼnyanja

MELEKIZEDEKI

, Ge 14:18 Melekizedeki mfumu

Sl 110:4 wansembe mofanana ndi Melekizedeki

MELITA

, Mac 28:1 chilumbacho chimatchedwa Melita

MENYA

, Yoh 19:3 ankamumenya makofi

1Ak 9:27 ndikumenya thupi langa

2Ak 6:5 pomenyedwa, kuikidwa mʼndende

MESIYA

, Da 9:25 Mesiya Mtsogoleri adzaonekere

Da 9:26 milungu 62, Mesiya adzaphedwa

Yoh 1:41 Ifetu tapeza Mesiya

Yoh 4:25 Ndikudziwa Mesiya akubwera

MFUMU

, Owe 21:25 mu Isiraeli munalibe mfumu

1Sa 23:17 ukhaladi mfumu, ndidzakhala wachiwiri

Sl 2:6 ndasankha mfumu yanga

Miy 21:1 Mtima wa mfumu uli ngati mitsinje

Yes 32:1 Mfumu idzalamulira mwachilungamo

Zek 14:9 Yehova adzakhala Mfumu ya dziko

Mt 21:5 Mfumu ikubwera itakwera bulu

Mt 27:29 Moni, Mfumu ya Ayuda!

Yoh 19:15 Tilibe mfumu koma Kaisara

1Ak 15:25 ayenera kukhala mfumu

MFUMUKAZI

, 1Mf 10:1 Mfumukazi ya ku Sheba

MFUMU YAKUMʼMWERA

, Da 11:11 mfumu yakumʼmwera idzakwiya

Da 11:40 mfumu yakumʼmwera idzakankhana

MFUMU YAKUMPOTO

, Da 11:7 kukaukira mfumu yakumpoto

Da 11:40 kukankhana ndi mfumu yakumpoto

MFUNDO YAIKULU

, Mla 12:13 mfundo yaikulu ndi yakuti:

MFUNDO ZOMVEKA

, Mac 9:22 mfundo zomveka zotsimikizira

MIKANGANO

, Miy 6:19 amayambitsa mikangano pakati pa abale

Afi 2:3 mtima wokonda mikangano

MIKANGO

, Da 6:27 wapulumutsa Danieli kwa mikango

MIKAYELI

, Da 10:13 Mikayeli mmodzi wa akalonga

Da 12:1 nthawi imeneyo Mikayeli adzaimirira

Chv 12:7 Mikayeli anamenyana ndi chinjoka

MILIRI

, Lu 21:11 kudzakhala miliri ndi njala

MILOMO

, Miy 10:19 amalamulira milomo yake

Yes 29:13 amandilemekeza ndi milomo yokha

Ahe 13:15 nsembe ya milomo yathu

MILUNGU

, Da 9:24 Pali milungu 70

MIMBA

, Aro 16:18 akapolo a mimba zawo

Afi 3:19 mulungu wawo ndi mimba zawo

MIMBULU

, Mt 7:15 ali ngati mimbulu yolusa

Lu 10:3 nkhosa pakati pa mimbulu

Mac 20:29 mimbulu yopondereza idzafika

MINA

, Lu 19:16 ndalama ya mina yapindula

MINDA YA MPESA

, Yes 65:21 adzadzala minda ya mpesa

MINGA

, Mko 15:17 chisoti chachifumu chaminga

2Ak 12:7 ndinapatsidwa minga mʼthupi

MIPANDO YACHIFUMU

, Da 7:9 mipando yachifumu inaikidwa

MIRIAMU

, Nu 12:1 Miriamu ndi Aroni ankamunena

MISALA

, Yoh 10:20 ameneyu ndi wamisala

MISECHE

, Le 19:16 nʼkumafalitsa miseche

Miy 20:19 amakonda kunena miseche

1Ti 5:13 amakondanso miseche

MISOZI

, 2Mf 20:5 ndaona misozi yako

Sl 6:6 ndimanyowetsa bedi ndi misozi

Sl 126:5 akukhetsa misozi pofesa mbewu

Mla 4:1 oponderezedwa akugwetsa misozi

Mac 20:19 ndi misozi komanso mayesero

Mac 20:31 ndikutulutsa misozi

Ahe 5:7 akugwetsa misozi

Chv 21:4 adzapukuta misozi yonse

MITAMBO

, Mla 11:4 woyangʼana mitambo sadzakolola

Mt 24:30 Mwana wa munthu akubwera pamitambo

MITENGO

, Yes 61:3 adzatchedwa mitengo ikuluikulu

Eze 47:12 mudzamera mitengo yosiyanasiyana

Chv 22:14 zipatso zamʼmitengo ya moyo

MITIMA

, Miy 17:3 Yehova amayesa mitima

Lu 12:34 mitima yanunso idzakhala komweko

Lu 21:34 mitima yanu isalemedwe

1Yo 3:20 Mulungu ndi wamkulu kuposa mitima

MITUNDU

, Ge 22:18 mitundu idzapeza madalitso

Mt 25:32 Mitundu yonse idzasonkhanitsidwa

Lu 21:24 nthawi zoikidwiratu za a mitundu

MIVI

, Sl 127:4 mivi mʼdzanja la mwamuna

MIYALA

, Eks 31:18 anapatsa Mose miyala

MIYAMBO

, Mt 15:3 chifukwa cha miyambo yanu

Mko 7:13 chifukwa cha miyambo yanu

Aga 1:14 wodzipereka pa miyambo ya makolo

MIZINDA YOTHAWIRAKO

, Nu 35:11 ikakhale mizinda yanu yothawirako

Yos 20:2 Sankhani mizinda yothawirako

MIZU

, Lu 8:13 amawalandira, koma alibe mizu

Akl 2:7 chikhulupiriro chanu chikhale ndi mizu

MKAIDI

, 2Ak 10:5 nʼkuwamanga ngati mkaidi

MKAKA

, Eks 3:8 dziko loyenda mkaka ndi uchi

Yes 60:16 udzamwa mkaka wa mitundu

Ahe 5:12 mwayambanso kufuna mkaka

1Pe 2:2 muzilakalaka mkaka wosasungunula

MKANGANO

, Miy 15:18 amaziziritsa mkangano

Miy 17:14 mkangano usanabuke, chokapo

MKANGO

, 1Sa 17:36 ndinapha mkango

Sl 91:13 Udzapondaponda mkango ndi mamba

Yes 11:7 Mkango udzadya udzu ngati ngʼombe

1Pe 5:8 Mdyerekezi akuyenda ngati mkango

Chv 5:5 Mkango wa fuko la Yuda

MKANJO

, Zek 8:23 adzagwira mkanjo wa Myuda

MKATE

, Mt 26:26 anatenga mkate

1Ak 10:17 tonse tikudya mkate umodzi

MKATI

, 2Ak 4:16 munthu wamkati watsopano

Aef 3:16 munthu wamkati akhale wamphamvu

MKAZI

, Ge 2:24 nʼkudziphatika kwa mkazi wake

Ge 3:15 pakati pa iwe ndi mkaziyo

Ge 27:46 Yakobo angatenge mkazi

1Mf 11:3 akazi ena apambali 300

Miy 5:18 uzisangalala ndi mkazi

Miy 12:4 Mkazi wamakhalidwe abwino

Miy 18:22 amene wapeza mkazi wabwino

Miy 21:19 mkazi wolongolola

Miy 31:10 ndani angapeze mkazi?

Mla 7:26 Mkazi amene ali ngati ukonde

Mla 9:9 Sangalala ndi mkazi wako

Mki 2:15 musachitire zachinyengo akazi anu

1Ak 7:2 mwamuna aliyense akhale ndi mkazi

Chv 12:1 mkazi atavala dzuwa

MKAZI WAMASIYE

, Sl 146:9 mwana wamasiye, mkazi wamasiye

Mko 12:43 mkazi wamasiye waponya zochuluka

Lu 18:3 munalinso mkazi wamasiye

MKHALAPAKATI

, 1Ti 2:5 mkhalapakati wa Mulungu ndi anthu

MKONDO

, 1Sa 18:11 Sauli anaponya mkondowo

MKULU WA ANGELO

, 1At 4:16 Mawu a mkulu wa angelo

Yuda 9 Mikayeli, mkulu wa angelo

MKWATIBWI

, Chv 21:9 mkwatibwi wa Mwanawankhosa

MKWIYO

, Miy 16:32 amalamulira mkwiyo wake

MKWIYO WA MULUNGU

, Sl 30:5 mkwiyo wa Mulungu sukhalitsa

MLALIKI

, Mac 21:8 mlaliki dzina lake Filipo

2Ti 4:5 uzigwira ntchito ya mlaliki

MLANDU

, Mac 20:26 ine ndilibe mlandu wa magazi

Aro 6:7 amene wafa sakhala ndi mlandu

Aro 8:33 Ndani adzasumira mlandu

1Ti 5:19 Usavomereze mlandu woneneza

MLANGIZI

, Miy 15:22 alangizi akachuluka zimayenda

Yes 9:6 dzina lakuti Mlangizi Wodabwitsa

MLENDO

, Eks 22:21 Musamachitire nkhanza mlendo

Nu 9:14 mlendo amene ali pakati panu

De 10:19 Inunso muzikonda mlendo

Sl 15:1 ndani angakhale mlendo mutenti yanu?

Yoh 10:5 Sizidzatsatira mlendo

MLENGI

, Mla 12:1 kumbukira Mlengi wako Wamkulu

MLINGO

, Yer 30:11 Ndidzakulanga pamlingo woyenera

MLIRI

, Eks 11:1 Patsala mliri umodzi

Chv 18:4 kulandira nawo miliri yake

MLUNGU

, 1Ak 16:2 Tsiku loyamba la mlungu

MLUZA

, Sl 139:16 pamene ndinali mluza

MMBULU

, Yes 11:6 Mmbulu udzakhala ndi nkhosa

MMISIRI

, Miy 8:30 monga mmisiri waluso

MMODZI

, 1Ak 8:6 Mulungu alipo mmodzi yekha

MʼMPHEPETE

, Le 23:22 musamachotseretu zamʼmphepete

MNENERI

, De 18:18 Ndidzawapatsa mneneri

Eze 2:5 adzadziwa kuti panali mneneri

Amo 7:14 sindinali mneneri, mwana wa mneneri

MNGELO

, 2Mf 19:35 mngelo anapha asilikali 185,000

Sl 34:7 Mngelo wa Yehova amamanga msasa

Da 3:28 anatumiza mngelo nʼkudzapulumutsa

Ho 12:4 [Yakobo] analimbana ndi mngelo

Mac 5:19 mngelo anatsegula zitseko za ndendeyo

Mac 12:11 watumiza mngelo kudzandipulumutsa

MNOFU

, Yob 33:25 Mnofu wake usalale

1Ak 15:50 mnofu, magazi sizingalowe mu Ufumu

MNYAMATA

, Yob 33:25 kuposa ali mnyamata

Sl 71:17 kuyambira ndili mnyamata

Yes 11:6 kamnyamata kadzazitsogolera

MNZAKE

, Yak 2:23 Abulahamu, mnzake wa Yehova

MNZAKO

, Miy 17:17 Mnzako weniweni amakukonda

Miy 18:24 mnzako amakhala nawe pafupi

Miy 27:6 Mabala ovulazidwa ndi mnzako

Lu 10:27 uzikonda mnzako mmene umadzikondera

MNZANGA

, Sl 55:13 Mnzanga amene ndikumudziwa

MODABWITSA

, Sl 139:14 munandipanga modabwitsa

MODYERA ZIWETO

, Lu 2:7 nʼkumugoneka modyeramo ziweto

MODZICHEPETSA

, Mik 6:8 uziyenda modzichepetsa ndi Mulungu

MODZIPEREKA

, Yes 37:32 adzachita zimenezi modzipereka

1Ti 4:15 uzizichita modzipereka kuti anthu aone

2Ti 4:2 Uzilalikira modzipereka

1Pe 5:2 mofunitsitsa monga atumiki a Mulungu

MONI

, 2Yo 10 musamupatse moni

MOONA MTIMA

, 2Ak 8:21 kusamalira moona mtima

Ahe 13:18 kuchita zonse moona mtima

MOSALEKEZA

, Da 6:16 amene ukumutumikira mosalekeza

MOSE

, Nu 12:3 Mose anali wofatsa kuposa onse

Sl 106:32 Mose sizinamuyendere bwino

Mac 7:22 Mose ankachita zinthu zazikulu

2Ak 3:7 sanathe kuyangʼanitsitsa Mose

MOTO

, Yer 20:9 moto woyaka mʼmafupa anga

Mt 25:41 kumoto wokolezedwera Mdyerekezi

1Ak 3:13 Motowo udzaonetsa ntchito ya aliyense

1At 5:19 Musazimitse moto wa mzimu

2Ti 1:6 mphatso uikolezere ngati moto

2Pe 3:7 dziko lapansi alisungira moto

MOWA

, Miy 20:1 omwa mowa amasokoneza

MOYO

, Nu 31:28 mutengepo chamoyo chimodzi

De 30:19 ndaika moyo ndi imfa

Yob 14:14 akafa, angakhalenso ndi moyo?

Sl 36:9 ndinu kasupe wa moyo

Mla 3:11 kukhala ndi moyo mpaka kalekale

Eze 18:4 Moyo wochimwa ndi umene udzafe

Da 6:26 ndi Mulungu wamoyo

Mt 22:37 moyo wanu wonse, maganizo anu onse

Lu 9:24 akufuna kupulumutsa moyo, adzautaya

Lu 20:38 Mulungu wa amoyo, onsewa ndi amoyo

Yoh 5:26 Atate ali ndi mphamvu zopereka moyo

Yoh 11:25 ndine kuuka ndi moyo

Mac 20:24 moyo wanga sindikuuona wofunika

2Ak 5:15 asakhale moyo wongodzisangalatsa

1At 4:15 ife amene tipitirize kukhala ndi moyo

Ahe 4:12 mawu a Mulungu ndi amoyo

MOYO WONSE

, Akl 3:23 muzichichita ndi moyo wanu wonse

MOYO WOSATHA

, Da 12:2 Ena adzalandira moyo wosatha

Lu 18:30 adzapeza moyo wosatha

Yoh 3:16 akhale ndi moyo wosatha

Yoh 17:3 Moyo wosatha adzaupeza

Mac 13:48 kukapeza moyo wosatha

Aro 6:23 amapereka moyo wosatha

1Ti 6:12 Gwira mwamphamvu moyo wosatha

MPAKA KALEKALE

, Ge 3:22 nʼkukhala mpaka kalekale

Sl 37:29 adzakhala mpaka kalekale

Mla 3:14 zidzakhalapo mpaka kalekale

1Pe 1:25 adzakhalapo mpaka kalekale

MPALA

, Le 21:5 Asamamete mpala mitu yawo

MPANDA

, Yos 6:5 mpanda wonse udzagwa

Eze 38:11 mʼmidzi yopanda mipanda

Lu 19:43 adzamanga mpanda

MPANDO WACHIFUMU

, Sl 45:6 mpando wachifumu mpaka kalekale

Yes 6:1 atakhala pampando wachifumu

Mt 25:31 adzakhala pampando wachifumu

Lu 1:32 adzamupatsa mpando wachifumu

MPANDO WOWERUZIRA

, Yoh 19:13 anakhala pampando woweruzira

Aro 14:10 tidzaima kumpando woweruzira

MPATUKO

, Miy 11:9 Wampatuko amawononga mnzake

Mac 28:22 gulu lampatuko amalinenera

2At 2:3 mpatuko ukuyenera kuchitika

Tit 3:10 wolimbikitsa mpatuko, usagwirizane naye

2Pe 2:1 adzayambitsa timagulu tampatuko

MPHAMVU

, Yos 1:7 uchite zinthu mwamphamvu

1Sa 30:6 ndipo anapeza mphamvu

Sl 29:11 Yehova adzapatsa anthu mphamvu

Sl 31:10 Mphamvu zanga zikuchepa

Sl 84:7 Mphamvu zidzapitiriza kuwonjezeka

Miy 17:22 akakhumudwa mphamvu zimatha

Miy 28:16 amagwiritsa ntchito mphamvu

Yes 40:29 amapereka mphamvu kwa wotopa

Yes 40:31 adzapezanso mphamvu

Zek 4:6 sipakufunika mphamvu, koma mzimu

Mko 5:30 mphamvu yatuluka mʼthupi mwake

Mko 12:30 ndi mphamvu zanu zonse

Mac 1:8 mudzakhala ndi mphamvu

1Ak 16:13 khalani ndi chikhulupiriro, amphamvu

2Ak 4:7 mphamvu yoposa yachibadwa

2Ak 12:9 mphamvu zanga, ukakhala wofooka

2Ak 12:10 mʼpamene ndimakhala wamphamvu

Afi 4:13 ndimapeza mphamvu kwa Mulungu

Chv 3:8 uli ndi mphamvu zochepa

MPHATSO

, Aro 6:23 mphatso imene Mulungu amapereka

Aro 12:6 Tili ndi mphatso zosiyanasiyana

1Ak 7:7 aliyense ali ndi mphatso

2Ak 8:12 Mphatso yochokera pansi pa mtima

Aef 4:8 anapereka amuna, akhale mphatso

Yak 1:17 Mphatso iliyonse yabwino

MPHEPO

, Mla 11:4 amene amayangʼana mphepo

Mt 7:25 Kenako chimphepo chinawomba

1Ak 9:26 sikuti ndikungomenya mphepo ayi

1Ak 14:9 mukulankhula kwa mphepo

Aef 4:14 tisamatengeketengeke ndi mphepo

Chv 7:1 atagwira mwamphamvu mphepo 4

MPHETA

, Mt 10:29 Mpheta ziwiri amazigulitsa

MPHEZI

, Mt 24:27 mphezi imangʼanimira kumʼmawa

Lu 10:18 Satana atagwa ngati mphezi

MPHONDA

, Yon 4:10 chomera cha mphondachi

MPHOTO

, Ru 2:12 Yehova akupatse mphoto

1Ak 9:24 amene amakalandira mphoto

Akl 2:18 asakulepheretseni mphoto

Akl 3:24 mphoto, cholowa chochokera kwa Yehova

Ahe 11:6 amapereka mphoto

MPHWAYI

, Miy 1:32 mphwayi zidzawawonongetsa

MPIKISANO

, Mla 9:11 amapambana pampikisano

Mac 20:24 ndimalize kuthamanga mpikisanowu

Aga 5:26 tisamayambitse mpikisano

2Ti 4:7 Ndathamanga pa mpikisanowu

MPINGO

, Sl 22:25 Ndidzakutamandani mumpingo

Sl 40:9 chilungamo mumpingo waukulu

Mt 16:18 pathanthwe ili ndidzamangapo mpingo

Mac 20:28 muwete mpingo wa Mulungu

Aro 16:5 Ndikuperekanso moni ku mpingo

MPUKUTU

, Chv 20:12 mipukutu inatambasulidwa

MPUMULO

, 2At 1:7 mudzapatsidwa mpumulo

MPWEYA

, Ge 2:7 anauzira mpweya wa moyo

Sl 146:4 Mpweya wake umachoka

Aef 2:2 wolamulira wa mpweya

MSAMPHA

, Sl 91:3 adzakupulumutsa mumsampha

Miy 29:25 Kuopa anthu ndi msampha

Lu 21:34, 35 modzidzimutsa ngati msampha

MSEWU

, Mt 7:14 msewu wake ndi wopanikiza

Mt 13:4 zinagwera mʼmbali mwa msewu

MSILIKALI

, Yer 20:11 ngati msilikali woopsa

2Ti 2:4 Msilikali sachita zamalonda

MSONKHANO

, Le 23:4 misonkhano yopatulika

MSONKHO

, Lu 20:22 nʼzololeka kuti tizipereka msonkho?

Lu 23:2 akuletsa anthu kukhoma msonkho

Aro 13:6 Nʼchifukwa chake mumakhoma misonkho

Aro 13:7 Wofuna msonkho, mʼpatseni msonkho

MTENDERE

, 1Mf 4:25 Aisiraeli ankakhala mwamtendere

Sl 29:11 adzawadalitsa powapatsa mtendere

Sl 37:11 adzasangalala ndi mtendere

Sl 72:7 padzakhala mtendere wochuluka

Sl 119:165 amakhala ndi mtendere wochuluka

Miy 17:1 kudya mkate pali mtendere

Yes 9:7 Ndipo mtendere sudzatha

Yes 32:18 adzakhala pamalo amtendere

Yes 48:18 mtendere udzakhala ngati mtsinje

Yes 54:13 mtendere wa ana ako

Yes 57:21 Oipa alibe mtendere

Yes 60:17 mtendere ukhale ngati okuyangʼanira

Yer 6:14 Kuli mtendere! Kuli mtendere!

Ho 2:18 azikhala mwamtendere

Mt 5:9 amene amabweretsa mtendere

Mt 5:24 ukakhazikitse mtendere

Mko 9:50 sungani mtendere pakati panu

Yoh 14:27 Ndikukusiyirani mtendere wanga

Mac 9:31 mpingo unakhala pamtendere

Aro 5:1 tingathe kukhala pa mtendere

Aro 8:6 kumabweretsa moyo ndi mtendere

Aro 12:18 yesetsani kukhala mwamtendere

Aro 12:18 muzikhala mwamtendere ndi anthu

Afi 4:7 mtendere wa Mulungu

1At 4:11 muzikhala mwamtendere

1At 5:3 Bata ndi mtendere!

1Pe 3:11 kumakhala mwamtendere ndi ena

Chv 6:4 kuchotsa mtendere padziko

MTENGO

, Ge 2:9 mtengo wodziwitsa chabwino

Ge 2:9 mtengo wa moyo

Sl 1:3 ngati mtengo wodzalidwa

Da 4:14 Gwetsani mtengowo mudule nthambi

Mko 15:25 anamukhomerera pamtengo

1Ak 7:23 Munagulidwa pa mtengo

Aga 3:13 wopachikidwa pamtengo

Chv 2:7 zipatso zamumtengo wa moyo

MTENGO WA MAOLIVI

, Sl 52:8 mtengo wa maolivi mʼnyumba

MTENGO WA MKUYU

, 1Mf 4:25 mtengo wa mpesa ndi wa mkuyu

Mik 4:4 pansi pa mtengo wa mkuyu

Mt 21:19 mkuyuwo unafota nthawi yomweyo

Mko 13:28 zokhudza mtengo wa mkuyu

MTENGO WA MPESA

, Mik 4:4 pansi pa mtengo wa mpesa

Yoh 15:1 mtengo wa mpesa weniweni

MTENGO WAPATALI

, Hag 2:7 zinthu zamtengo wapatali

Mt 6:26 amtengo wapatali kuposa mbalame?

1Pe 1:19 magazi amtengo wapatali

MTENGO WOZUNZIKIRAPO

, Mt 10:38 kunyamula mtengo wozunzikirapo

Lu 9:23 anyamule mtengo wozunzikirapo

MTHANDIZI

, Yoh 14:16 adzakupatsani mthandizi

Yoh 14:26 mthandizi, mzimu, adzakuphunzitsani

MTHENGA

, Mki 3:1 ndikutumiza mthenga wanga

MTHUNZI

, 1Mb 29:15 Masiku athu ali ngati mthunzi

Sl 91:1 mumthunzi wa Wamphamvuyonse

Akl 2:17 mthunzi wa zimene zinali kubwera

Yak 1:17 sasintha ngati mthunzi

MTIMA

, Ge 6:5 zofuna za mtima wawo

De 6:6 Mawu azikhala pamtima panu

1Mf 8:38 akudziwa ululu wamumtima

2Mb 16:9 odzipereka ndi mtima wonse

Eza 7:10 Ezara anakonzekeretsa mtima

Sl 34:18 ali pafupi ndi a mtima wosweka

Sl 51:10 lengani mtima wolungama

Sl 51:17 kudzimvera chisoni mumtima

Sl 51:17 simudzakana mtima wosweka

Sl 147:3 Iye amachiritsa osweka mtima

Miy 4:23 Uteteze mtima wako

Miy 14:30 Mtima wodekha, thupi lathanzi

Miy 17:22 Mtima wosangalala ndi mankhwala

Miy 17:25 amapweteketsa mtima wa mayi ake

Miy 28:26 amene amadalira mtima wake

Yes 66:2 Ndidzayangʼana wosweka mtima

Yer 17:9 Mtima ndi wopusitsa kwambiri

Yer 17:10 Ine Yehova ndimafufuza mtima

Yer 31:33 ndidzachilemba mumtima mwawo

Mt 15:19 mumtima mumachokera maganizo

Mt 22:37 Muzikonda Yehova ndi mtima wonse

Lu 24:32 tinakhudzidwa kwambiri mumtima

Mac 16:14 anatsegula mtima wake

Aro 6:17 munamvera mochokera pansi pa mtima

Aro 7:22 Mumtima mwanga ndimasangalala

Afi 2:20 ndilibe ali ndi mtima ngati wake

Ahe 3:12 nʼkukhala ndi mtima woipa

MTIMA MʼMALO

, Lu 12:19 Mtima mʼmalo, udye, umwe

MTIMA WONSE

, 1Mb 28:9 uzimutumikira ndi mtima wonse

2Mb 16:9 odzipereka ndi mtima wonse

Aef 6:6 chifuniro cha Mulungu ndi mtima wonse

MTOLO

, Mac 15:28 tisakusenzetseni mtolo wolemera

MTSIKANA

, 2Mf 5:2 anakagwirako kamtsikana

Mko 5:42 mtsikanayo anadzuka nʼkuyenda

MTSINJE

, Chv 12:16 nʼkumeza mtsinje

Chv 22:1 mtsinje wa madzi a moyo

MTSOGOLERI

, Miy 28:16 Mtsogoleri, amagwiritsa ntchito mphamvu

Mt 23:10 Mtsogoleri wanu ndi mmodzi, Khristu

MTUMIKI

, Yes 42:1 Taonani mtumiki wanga

Yes 65:13 Atumiki anga adzadya

Mko 10:43 akuyenera kukhala mtumiki

Lu 12:42 mtumiki woyangʼanira nyumba

MTUMIKI WAMKULU

, Mac 3:15 Munapha Mtumiki Wamkulu

Ahe 12:2 Mtumiki Wamkulu ndi Wokwaniritsa

MTUNDU

, Eks 19:6 mtundu wanga woyera

Sl 33:12 Wosangalala ndi mtundu

Yes 66:8 kodi mtundu ungabadwe?

Mt 21:43 Ufumu udzaperekedwa ku mtundu

Mt 24:7 Mtundu udzaukirana ndi mtundu

Mac 17:26 anapanga mitundu yonse ya anthu

1Pe 2:9 ansembe achifumu, mtundu woyera

2Pe 3:11 ganizirani za mtundu wa anthu

MUBEREKANE

, Ge 1:28 Muberekane, muchuluke

MULUNGU

, De 10:17 Yehova ndi Mulungu wa milungu

Mt 27:46 Mulungu wanga, mwandisiyiranji?

Yoh 1:18 Palibe munthu anaonapo Mulungu

Yoh 17:3 Mulungu yekhayo amene ndi woona

Yoh 20:17 Mulungu wanga ndi Mulungu wanu

1Ak 8:4 kulibe Mulungu wina

2Ak 4:4 mulungu wa nthawi ino

Aef 4:6 Mulungu mmodzi, Atate wa onse

1Yo 4:8 Mulungu ndi chikondi

MUNDA

, Ge 2:15 nʼkumuika mʼmunda wa Edeni

Mt 13:38 Munda ndi dziko

Yoh 4:35 muone mʼmindamo, mwayera

1Ak 3:9 ndinu munda wa Mulungu

MUNDA WA MPESA

, Mt 20:1 anali ndi munda wa mpesa

Mt 21:28 kukagwira ntchito mʼmunda wa mpesa

Lu 20:9 analima munda wa mpesa

MUNTHU

, Sl 8:4 munthu ndi ndani

Yak 5:17 Eliya anali munthu ngati ife

MUNTHU WOVUTIKA

, Sl 40:17 munthu wovutika, wosauka

MUSADZINAMIZE

, Aga 6:7 Musadzinamize, Mulungu sapusitsika

MUSAMAKHULUPIRIRE

, Sl 146:3 Musamakhulupirire anthu olemekezeka

MUSAMAKWIYITSE

, Akl 3:21 musamakwiyitse ana anu

MUTU

, Ge 3:15 idzaphwanya mutu wako

Da 2:32 Mutu wa chifanizirocho unali wagolide

1Ak 11:3 Mutu wa mkazi ndi mwamuna

Aef 5:23 Khristu ndi mutu wa mpingo

Aef 5:23 mwamuna ndi mutu wa mkazi

MUYEZO

, Lu 6:38 muyezo umene mukuyezera ena

MUZILANDIRANA

, Aro 15:7 muzilandirana, ngati Khristu

MVERA

, Eks 24:7 tidzachita zomwezo, tidzamumvera

1Sa 15:22 Kumvera kumaposa nsembe

1Mf 3:9 Mundipatse mtima womvera

Sl 51:12 mtima wofunitsitsa kukumverani

Mt 17:5 Mwana wanga. Muzimumvera

Lu 2:51 anapitiriza kuwamvera

Lu 10:16 akukumverani, akumveranso ine

Mac 4:19 kumvera inu mʼmalo mwa Mulungu

Mac 5:29 tiyenera kumvera Mulungu

Aro 5:19 kumvera kwa munthu mmodziyu

Aro 6:17 munamvera mochokera pansi pa mtima

Aro 13:1 azimvera olamulira akuluakulu

Aro 16:26 azimumvera mwa chikhulupiriro

Aef 6:5 Akapolo inu, muzimvera

Afi 2:8 anakhala womvera mpaka imfa

Ahe 5:8 anaphunzira kumvera

Ahe 13:17 Muzimvera amene akukutsogolerani

MVETSA

, 1Mf 3:11 ukhale womvetsa zinthu

Ne 8:8 anathandiza anthuwo kumvetsa

Yob 6:24 ndimvetse zimene ndalakwitsa

Sl 119:27 Ndithandizeni kumvetsa

Miy 3:5 luso lako lomvetsa zinthu

Miy 4:7 upezenso luso lomvetsa zinthu

Da 11:33 kuti amvetse zinthu

1Ak 14:20 pa nkhani yomvetsa

1Pe 4:4 anthu amʼdzikoli sakumvetsa

MVETSERA

, Miy 1:5 wanzeru amamvetsera

Eze 2:7 kaya akamvetsera kapena ayi

Yak 1:19 wokonzeka kumvetsera

MVULA

, Ge 7:12 chimvula chinakhuthuka masiku 40

De 11:14 ndidzakupatsaninso mvula

De 32:2 Malangizo adzagwa ngati mvula

Yes 55:10 mvula komanso sinowo

Mt 5:45 amagwetsera mvula anthu

MWALA

, Da 2:34 mwala unadulidwa kuphiri

Mt 21:42 Mwala umene omanga anaukana

Lu 19:40 miyala ingathe kufuula

MWALA WAPAKONA

, Sl 118:22 mwala wapakona wofunika

Aef 2:20 Yesu ndi mwala wapakona

MWALIRA

, Lu 8:49 Mwana wanu wamwalira

Yoh 11:25 ngakhale atamwalira, adzakhalanso

MWAMUNA

, Le 20:13 akagona ndi mwamuna

1Ak 7:2 akhale ndi mwamuna wakewake

1Ak 7:14 Mwamuna wosakhulupirira

MWANA

, Owe 13:8 zoyenera kuchita ndi mwana

Sl 2:12 Mulemekezeni mwanayo

Miy 13:24 amene sakwapula mwana wake

Miy 15:20 Mwana wanzeru amasangalatsa bambo

Miy 22:6 Phunzitsa mwana

Yer 1:7 Usanene kuti, Ndine mwana

Mt 3:17 Uyu ndi Mwana wanga wokondedwa

Lu 9:47 anatenga mwana wamngʼono

Lu 15:13 mwana wamngʼono uja

1Ak 13:11 kuganiza ngati mwana

MWANA WA DISO

, Sl 17:8 Nditetezeni ngati mwana wa diso

Zek 2:8 akukhudza mwana wa diso

MWANA WAMASIYE

, Eks 22:22 Musamazunze mwana wamasiye

Sl 68:5 Bambo wa ana amasiye

MWANA WAMNGʼONO

, Lu 9:48 zinthu ngati mwana wamngʼono

MWANA WA MUNTHU

, Da 7:13 wooneka ngati mwana wa munthu

Mt 10:23 Mwana wa munthu asanafike

Lu 21:27 adzaona Mwana wa munthu akubwera

MWANA WA NGʼOMBE

, Eks 32:4 anapanga fano la mwana wa ngʼombe

Yes 11:6 Mwana wa ngʼombe, mkango

MWANA WA NKHOSA

, 2Sa 12:3 anali ndi kamwana ka nkhosa kokha

MWANAWANKHOSA

, Yoh 1:29 Mwanawankhosa akuchotsa uchimo

MWAYI

, Yes 65:11 mulungu wa Mwayi

Afi 1:29 inu munapatsidwa mwayi

MWEZI

, Yow 2:31 mwezi udzasanduka magazi

Lu 21:25 zizindikiro padzuwa, mwezi ndi nyenyezi

MWINIWAKE

, 1Ak 6:19 mwiniwake wa inuyo si inu

MWINIWAKE WA MUNDA

, Mt 9:38 Mwiniwake wa munda atumize antchito

MYUDA

, 1Ak 9:20 Kwa Ayuda ndinakhala Myuda

MZIMU

, Nu 11:25 Anatengako gawo lina la mzimu

1Sa 16:13 mzimu wa Yehova unathandiza Davide

2Sa 23:2 Mzimu wa Yehova unalankhula

Sl 104:29 Mukachotsa mzimu wawo

Mla 12:7 mzimu udzabwerera kwa Mulungu

Yes 61:1 Mzimu wa Yehova uli pa ine

Yow 2:28 ndidzapereka mzimu wanga

Zek 4:6 koma mzimu wanga

Mt 3:16 Yohane anaona mzimu

Mt 12:31 wonyoza mzimu sadzakhululukidwa

Mt 26:41 mzimu ndi wofunitsitsa

Lu 23:46 ndikupereka mzimu wanga

Yoh 4:24 Mulungu ndi Mzimu, kulambira ndi mzimu

Yoh 16:13 mzimu wa choonadi

Aro 8:16 limodzi ndi mzimu wathu

Aro 8:26 koma mzimu umachonderera

2Ak 3:17 Yehova ndi Mzimu

Aga 5:16 motsogoleredwa ndi mzimu

Aga 5:22 mothandizidwa ndi mzimu

Aga 6:8 akutsatira mzimu wa Mulungu

1Pe 3:18 anaukitsidwa monga mzimu

MZIMU WOYERA

, Sl 51:11 musandichotsere mzimu woyera

Lu 1:35 Mzimu woyera udzakuphimba

Lu 3:22 mzimu woyera ngati nkhunda

Lu 11:13 Atate adzapereka mzimu woyera

Yoh 14:26 mzimu woyera udzakuphunzitsani

Mac 1:8 mukadzalandira mzimu woyera

Mac 2:4 anadzazidwa ndi mzimu woyera

Mac 5:32 mzimu woyera, Mulungu wapereka

Aef 4:30 musamamvetse chisoni mzimu woyera

MZINDA

, Lu 4:43 kukalengeza uthenga kumizinda ina

Ahe 11:10 mzinda wokhala ndi maziko

N

NAINI

, Lu 7:11 kupita kumzinda wa Naini

NAMA

, Miy 19:22 kusiyana nʼkukhala wonama

Akl 3:9 Musamanamizane

Tit 1:2 Mulungu amene sanganame

NAMWALI

, Mt 25:1 ndi anamwali 10

NANGULA

, Ahe 6:19 chili ngati nangula

NATANI

, 2Sa 12:7 Natani: Munthuyo ndi iweyo

NDAKATULO

, Mac 17:28 mmene andakatulo ena ananenera

NDALAMA

, Mla 7:12 ndalama zimatetezera

Mla 10:19 ndalama zimathandiza chilichonse

Lu 14:28 kukhala pansi nʼkuwerengera ndalama

1Ti 6:10 kukonda ndalama

Ahe 13:5 Musamakonde ndalama

NDEKHA

, Yoh 16:32 sindikhala ndekha

NDENDE

, Mt 25:36 Ndinali mʼndende, munadzandiona

Mac 5:18 atumwiwo anawatsekera mʼndende

Mac 5:19 anatsegula zitseko za ndendeyo

Mac 12:5 ali mʼndende, mpingo unkapemphera

Mac 16:26 maziko a ndende anagwedezeka

Ahe 13:3 Muzikumbukira ali mʼndende

Chv 2:10 apitiriza kuponya mʼndende

NDIDZAKHALA

, Eks 3:14 Ndidzakhala Amene Ndidzafune Kukhala

NDIFE

, Aro 14:8 tikafa, ndife a Yehova

NDODO

, Chv 12:5 adzakusa mitundu ndi ndodo

NDODO YACHIFUMU

, Ge 49:10 Ndodo yachifumu sidzachoka kwa Yuda

Sl 2:9 udzaiphwanya ndi ndodo yachifumu

NDUNA

, Mac 8:27 nduna ya ku Itiyopiya

NDUWIRA

, Eze 21:26 Chotsa nduwira, vula chisoti chachifumu

NEBUKADINEZARA

, Da 2:1 Nebukadinezara analota maloto

NENERA

, Miy 16:28 wonenera anzake zoipa

1Ak 4:13 Akamatinenera zoipa

Tit 2:8 ndipo asapeze chifukwa chotinenera

NENEREDWA

, 2Ak 6:8 poneneredwa zoipa

NENEZA

, Tit 1:7 wopanda chifukwa chomunenezera

Chv 12:10 woneneza abale athu waponyedwa pansi

NGALE

, Mt 7:6 kuponyera nkhumba ngale

Mt 13:45 akufunafuna ngale zabwino

NGʼAMBA

, Yow 2:13 Ngʼambani mitima yanu

NGAMILA

, Mt 19:24 kuti ngamila ilowe pakabowo

NGʼANJO

, Da 3:17 angatipulumutse mungʼanjo

NGʼOMBE

, Eks 21:28 ngʼombe yagunda mwamuna

De 25:4 Usamange ngʼombe pakamwa

Miy 7:22 kulondola mkaziyo, ngati ngʼombe

Ho 14:2 ngati ana a ngʼombe amphongo

1Ak 9:9 amangodera nkhawa ngʼombe?

NGONGOLE

, Miy 11:15 amalonjeza kuti adzapereka ngongole

Aro 1:14 ndili ndi ngongole kwa anzeru

Aro 13:8 musamakhale ndi ngongole iliyonse

NGʼUNGʼUDZA

, Nu 14:27 Aisiraeli akungʼungʼudza

1Ak 10:10 Tisakhalenso ongʼungʼudza

Afi 2:14 muzipewa kungʼungʼudza

Yuda 16 Anthu amenewa amangʼungʼudza

NINEVE

, Yon 4:11 kumvera chisoni Nineve?

NJALA

, Sl 37:19 nthawi ya njala, chakudya

Yes 65:13 adzadya, mudzakhala ndi njala

Amo 8:11 Osati njala ya chakudya kapena ludzu

Mt 24:7 Kudzakhala njala

NJENJEMERA

, Afi 2:12 kuchita mwamantha ndi kunjenjemera

NJIRA

, Miy 4:18 njira ya olungama

Miy 16:25 njira imene imaoneka

Yes 30:21 Yendani mʼnjira imeneyi

Yer 8:6 kunjira imene ambiri akuitsatira

Yow 2:7 Aliyense amayenda mʼnjira yake

Yoh 14:6 ndine njira, choonadi ndi moyo

Mac 9:2 aliyense wotsatira Njirayo

1Ak 10:13 adzapereka njira yopulumukira

Aga 6:1 kulowera njira yolakwika

NJOKA

, Ge 3:4 njokayo inauza mkaziyo kuti

Yoh 3:14 Mose anakweza njoka mʼmwamba

Chv 12:9 chinjokacho chinaponyedwa pansi

NKHANDWE

, Mt 8:20 Nkhandwe zili ndi mapanga

NKHANI

, Eks 23:1 Musafalitse nkhani yabodza

Miy 25:25 Nkhani yabwino yochokera kutali

Mac 15:32 anawakambira nkhani zambiri

NKHANZA

, Miy 11:17 wankhanza amadzibweretsera mavuto

Miy 12:10 munthu woipa ndi wankhanza

NKHATA

, 1Ak 9:25 kuti akalandire nkhata yakumutu

NKHAWA

, 1Sa 1:15 ndili ndi nkhawa kwambiri

Sl 55:22 Umutulire Yehova nkhawa zako

Sl 94:19 Nkhawa zitandichulukira munanditonthoza

Miy 12:25 Nkhawa mumtima mwa munthu

Yes 28:16 amene adzade nkhawa

Yes 41:10 Usade nkhawa, ndine Mulungu wako

Mt 6:34 Musamadere nkhawa za mawa

Mt 10:19 musadzade nkhawa kuti mudzalankhula

Mko 4:19 nkhawa za moyo wamʼnthawi ino

Lu 8:14 chifukwa chotengeka ndi nkhawa, chuma

Lu 12:25 angatalikitse moyo chifukwa cha nkhawa?

Lu 21:34 mitima yanu isalemedwe ndi nkhawa

1Ak 7:32 mukhale opanda nkhawa

1Ak 7:32 wosakwatira amadera nkhawa za Ambuye

2Ak 11:28 Ndimadera nkhawa mipingo yonse

Afi 4:6 Musamade nkhawa ndi chilichonse

1At 5:14 muzilimbikitsa amene ali ndi nkhawa

NKHONDO

, 1Sa 17:47 Yehova ndiye mwini nkhondo

2Mb 20:17 simufunikira kumenya nkhondo

Sl 46:9 Akuthetsa nkhondo padziko

Yes 2:4 sadzaphunziranso nkhondo

Ho 2:18 ndidzathetsa nkhondo mʼdzikolo

1Ak 14:8 ndani angakonzekere nkhondo?

1Ti 6:12 Menya nkhondo ya chikhulupiriro

Yuda 3 kumenya nkhondo ya chikhulupiriro

Chv 12:7 kumwamba kunabuka nkhondo

Chv 16:14 nkhondo ya tsiku lalikulu la Mulungu

NKHOSA

, Sl 100:3 Ndife nkhosa zimene akuweta

Yes 53:7 nkhosa imene akufuna kuimeta

Eze 34:12 Ndidzasamalira nkhosa zanga

Mt 25:33 Adzaika nkhosa kudzanja lamanja

Lu 12:32 Musaope kagulu ka nkhosa inu

Yoh 21:16 Weta ana a nkhosa anga

NKHOSA ZINA

, Yoh 10:16 Ndili ndi nkhosa zina zimene si zamʼkhola

NKHUKU

, Mt 23:37 nkhuku imasonkhanitsa anapiye

NKHUMBA

, Lu 8:33 nʼkukalowa munkhumbazo

Lu 15:15 kuti azikaweta nkhumba

2Pe 2:22 nkhumba imene inasambitsidwa

NKHUNDA

, Mt 3:16 mzimu ukutsika ngati nkhunda

Mt 10:16 moona mtima ngati nkhunda

NKHUNGU

, Yak 4:14 nkhungu yooneka kanthawi

NKHUNI

, Miy 26:20 Ngati palibe nkhuni

NOWA

, Ge 6:9 Nowa anayenda ndi Mulungu

Mt 24:37 mofanana ndi masiku a Nowa

NSANJA

, Ge 11:4 Tiyeni timange nsanja

Miy 18:10 Dzina la Yehova, nsanja yolimba

Lu 13:4 anthu 18 nsanja inawagwera

NSANJA YA MLONDA

, Yes 21:8 pansanja ya mlonda

NSANJE

, Sl 37:1 kuchitira nsanje anthu

Sl 73:3 ndinkachitira nsanje onyada

Sl 106:16 anayamba kuchitira nsanje Mose

Miy 6:34 nsanje imachititsa mwamuna kukwiya

Miy 14:30 nsanje imawoletsa mafupa

1Ak 13:4 Chikondi sichichita nsanje

NSEMBE

, Le 7:37 nsembe yopsereza, nsembe yambewu

1Sa 15:22 Kumvera kumaposa nsembe

2Sa 24:24 Sindingapereke nsembe osalipira

1Mb 29:9 anapereka nsembezo kwa Yehova

Sl 40:6 nsembe zina, simunazifune

Sl 51:17 Nsembe zimene amasangalala nazo

Miy 15:8 Nsembe ya woipa ndi yonyansa

Yes 1:11 Nsembe zanu zopsereza zandikwana

Ho 6:6 chikondi chokhulupirika, osati nsembe

Aro 12:1 nsembe yamoyo, yoyera

Ahe 13:15 nsembe imene tikupereka kwa Mulungu

NSEMBE YACHAKUMWA

, Afi 2:17 ngati nsembe yachakumwa

NSOMBA

, Yon 1:17 chinsomba kuti chikameze Yona

Yoh 21:11 ukonde wodzaza nsomba 153

NTCHITO

, Ne 4:6 anapitiriza kugwira ntchitoyo

Sl 104:24 Ntchito zanu ndi zochuluka

Mla 2:24 wagwira ntchito mwakhama

Yoh 6:27 Musamagwirire ntchito chakudya

Yoh 14:12 ntchito zazikulu kuposa zimenezi

Aef 4:28 azigwira ntchito molimbikira

2At 3:10 wosagwira ntchito, asadye

Ahe 9:14 ku ntchito zakufa

1Pe 1:13 mugwire ntchito mwamphamvu

NTHAKA

, Mt 13:23 inafesedwa panthaka yabwino

NTHAMBI

, Yoh 15:4 nthambi singabereke payokha

NTHAWI

, Mla 3:1 nthawi yochitira chilichonse

Mla 9:11 nthawi komanso zosayembekezereka

Yes 46:10 Kutatsala nthawi ndimaneneratu

Da 7:25 nthawi imodzi, nthawi ziwiri

Yoh 7:8 nthawi yanga sinafike

1Ak 7:29 Nthawi yotsalayi yafupika

Aef 5:16 Muzigwiritsa ntchito bwino nthawi

1Pe 4:3 nthawi imeneyo munkachita

NTHAWI YOCHEPA

, Ahe 11:25 nʼkusangalala kwa nthawi yochepa

NTHAWI YOIKIDWIRATU

, Hab 2:3 akudikira nthawi yake yoikidwiratu

Lu 21:24 nthawi zoikidwiratu za anthu a mitundu

NTHITI

, Ge 2:22 anapanga mkazi kuchokera kunthiti

NTHUMWI

, Yoh 7:29 ndine nthumwi yake

NYADA

, Miy 8:13 Ndimadana ndi kunyada

Miy 16:5 Yehova amanyansidwa ndi wonyada

Miy 16:18 Kunyada kumawononga munthu

NYADIRA

, 2At 1:4 timanyadira tikamanena za inu

NYALANYAZA

, Da 6:4 Danieli sankanyalanyaza udindo wake

1Ti 4:14 Usamanyalanyaze mphatso

NYALE

, Sl 119:105 Mawu anu ndi nyale younikira

Mt 6:22 Nyale ya thupi ndi diso

Mt 25:1 anamwali 10 anatenga nyale zawo

NYAMA

, Ge 7:2 Pa nyama zosadetsedwa utengepo 7

Le 18:23 asamagone ndi nyama

Miy 23:20 amadya nyama mosusuka

Mla 3:19 Mapeto a anthu ndi nyama ndi ofanana

NYANGA

, Da 7:7 chilombo cha 4 cha nyanga 10

Da 8:8 nyanga yaikulu inathyoledwa

NYANJA

, Eks 14:21 mphepo yamphamvu igawe nyanjayo

Yes 57:20 oipa ali ngati nyanja ya mafunde

Chv 19:20 mʼnyanja ya moto yoyaka ndi sulufule

NYANSA

, Nu 21:5 chakudya chonyansachi chatikola

NYANSIDWA

, Aro 12:9 Muzinyansidwa ndi zoipa

NYENGERERA

, Miy 7:21 Wamunyengerera ndi mawu okopa

NYENGO

, Da 2:21 amasintha nthawi ndi nyengo

Mac 1:7 kudziwa nthawi kapena nyengo

1At 5:1 za nthawi ndi nyengo

NYENYEZI

, Sl 147:4 nyenyezi iliyonse amaitchula dzina

Mt 24:29 chikadzangotha, nyenyezi zidzagwa

Chv 2:1 nyenyezi 7 mʼdzanja lamanja

NYERERE

, Miy 6:6 Pita kwa nyerere waulesi iwe

Miy 30:25 Nyerere zimasonkhanitsa chakudya

NYEZIMIRA

, Yes 14:12 Wonyezimirawe, mwana wa

NYIMBO

, Ne 12:46 nyimbo zotamanda Mulungu

Sl 98:1 Imbirani Yehova nyimbo

Mac 16:25 kutamanda Mulungu poimba nyimbo

Akl 3:16 nyimbo zauzimu zoyamikira

NYOZA

, 1Sa 17:26 kuti azinyoza asilikali

2Sa 12:14 wanyoza kwambiri Yehova

Mt 5:11 osangalala pamene akukunyozani

Mko 3:29 aliyense amene wanyoza mzimu woyera

2Pe 2:10 kulankhula zinthu zonyoza

2Pe 3:3 azidzalankhula zinthu zonyoza

NYOZEDWA

, Yes 53:3 ananyozedwa ndipo ankamupewa

NYOZEKA

, 1Ak 1:28 Mulungu anasankha zonyozeka

NYUMBA

, 2Sa 7:13 adzamangira dzina langa nyumba

Sl 27:4 ndikhale mʼnyumba ya Yehova

Sl 101:2 Ndidzayenda mʼnyumba yanga

Sl 127:1 Yehova akapanda kumanga nyumba

Yes 56:7 idzatchedwa nyumba yopemphereramo

Yes 65:21 adzamanga nyumba nʼkumakhalamo

Lu 2:49 ndiyenera kupezeka mʼnyumba

Yoh 2:16 kukhala nyumba ya malonda

Yoh 14:2 Mʼnyumba ya Atate muli malo

Mac 5:42 kunyumba ndi nyumba

Mac 7:48 sakhala mʼnyumba zomangidwa

Mac 20:20 kukuphunzitsani kunyumba ndi nyumba

2Ak 5:1 tidzalandira nyumba yamuyaya

Ahe 3:4 nyumba inamangidwa ndi winawake

NZERU

, Sl 111:10 Chiyambi cha nzeru nʼkuopa Yehova

Sl 119:98 amandichititsa kukhala wanzeru

Miy 2:6 Yehova amapereka nzeru

Miy 2:7 amawasungira nzeru zopindulitsa

Miy 3:7 Usamadzione kuti ndiwe wanzeru

Miy 3:21 Uteteze nzeru zopindulitsa

Miy 4:7 Nzeru ndi chinthu chofunika kwambiri

Miy 8:11 nzeru ndi zabwino kwambiri

Miy 9:9 wanzeru adzawonjezera nzeru

Miy 13:20 woyenda ndi anzeru adzakhala wanzeru

Miy 24:3 Nzeru zimamanga nyumba

Miy 27:11 Mwana wanga, khala wanzeru

Mla 7:12 nzeru zimateteza

Mla 10:10 nzeru zimathandiza

Mt 11:19 nzeru imatsimikizirika ndi ntchito zake

Mt 24:45 kapolo wokhulupirika ndi wanzeru

Lu 15:17 Nzeru zitamubwerera ananena kuti

Lu 16:8 amachita mwanzeru kuposa ana a kuwala

Lu 16:8 mtumiki anachita zinthu mwanzeru

Lu 21:15 nzeru zimene otsutsa sangazikane

Mac 17:18 anzeru za Epikureya ndi Sitoiki

Aro 11:33 Nzeru zake nʼzozama

1Ak 2:5 musamakhulupirire nzeru za anthu

1Ak 2:6 osati nzeru za nthawi ino

1Ak 3:19 nzeru zamʼdzikoli nʼzopusa

Aef 5:15 muziyenda ngati anthu anzeru

Akl 2:3 nzeru ndiponso kudziwa zinthu

Akl 2:8 nzeru za anthu ndi chinyengo

Yak 1:5 ngati wina akusowa nzeru

Yak 3:17 nzeru ya kumwamba ndi yamtendere

NZIKA

, Afi 3:20 ife ndife nzika zakumwamba

O

ODZICHEPETSA

, Miy 11:2 odzichepetsa ali ndi nzeru

ODZIKUZA

, Yak 4:6 Mulungu amatsutsa odzikuza

ODZIPEREKA

, Aro 10:2 umboni kuti ndi odzipereka

Tit 2:14 odzipereka pa ntchito zabwino

OFATSA

, Sl 37:11 ofatsa adzalandira dziko lapansi

Zef 2:3 Funafunani Yehova ofatsa apadziko

OFULIDWA

, Yes 56:4 wanena kwa anthu ofulidwa

OGONA AMUNA ANZAWO

, 1Ak 6:9 amuna ogona amuna anzawo

OGWIDWA NDI ZIWANDA

, Mt 8:28 amuna ogwidwa ndi ziwanda

OIPA

, Sl 37:9 anthu oipa adzaphedwa

Sl 37:10 oipa sadzakhalaponso

Miy 15:29 ali kutali ndi anthu oipa

Yes 57:21 Oipa alibe mtendere

OITANIDWA

, Mt 22:14 oitanidwa ndi ambiri

OKANA KHRISTU

, 1Yo 2:18 okana Khristu aonekera

OKHULUPIRIKA

, 1Sa 2:9 Amateteza mapazi a okhulupirika

Sl 37:28 Yehova sadzasiya okhulupirika

OKHULUPIRIRA NYENYEZI

, Mt 2:1 okhulupirira nyenyezi anabwera

OKONDERA

, Yak 2:9 mukapitiriza kukhala okondera

OLA

, Mt 24:36 tsiku ndi ola palibe akudziwa

OLAMBIRA MAFANO

, 1Ak 6:9 olambira mafano sadzalowa mu Ufumu

OLAMULIRA

, 2Pe 2:10 amene amanyoza olamulira

OLANDIRA CHOLOWA

, Aro 8:17 olandira cholowa anzake a Khristu

Aga 3:29 mbadwa, olandira cholowa

OLOSERA ZAMʼTSOGOLO

, Le 19:31 anthu olosera zamʼtsogolo

OLUMALA

, Mt 15:31 olumala akuyenda

OMASULIRA

, 1Ak 12:30 onse sangakhale omasulira

OMBEZA

, De 18:10 pasapezeke aliyense woombeza

ONA

, Mt 6:1 pamaso pa anthu kuti akuoneni

Yoh 1:18 Palibe munthu anaonapo Mulungu

Yoh 14:9 waona ine waonanso Atate

ONAMIZIRA KUTI NDI KHRISTU

, Mt 24:24 kudzabwera onamizira kuti ndi Khristu

ONEKA

, 1Sa 16:7 Usaganizire mmene akuonekera

Miy 31:30 Munthu akhoza kuoneka ngati wabwino

Yoh 7:24 Siyani kuweruza potengera maonekedwe

ONEKERA

, Aro 8:19 ulemerero udzaonekere

2At 2:6 chikuchititsa kuti panopa asaonekere

ONETSA

, Yoh 5:20 amamuonetsa zimene amachita

ONYOZEKA

, Yes 57:15 nditsitsimutse mtima wa onyozeka

OPA

, 2Mb 20:15 Musaope gulu lalikululi

Sl 23:4 Sindikuopa kanthu

Sl 56:4 ndimadalira Mulungu, sindikuopa

Sl 118:6 Yehova ali kumbali yanga, sindidzaopa

Miy 29:25 Kuopa anthu ndi msampha

Lu 12:4 musamaope amene amapha thupi

OPANDA PAKE

, Lu 17:10 akapolo opanda pake

Aef 4:17 maganizo opanda pake

OPANGA MATENTI

, Mac 18:3 onse anali opanga matenti

OPHUNZIRA

, Mt 28:19 anthu a mitundu akhale ophunzira

Yoh 8:31 Mukasunga mawu, ndinudi ophunzira

Yoh 13:35 ndinu ophunzira ngati mukukondana

OPSA

, Sl 91:5 sudzaopa choopsa chilichonse

2Ak 11:26 zoopsa mumzinda, mʼchipululu

Ahe 10:31 Kulangidwa ndi Mulungu nʼkoopsa

OPSEZA

, Miy 3:23 udzayenda popanda chokuopseza

Mik 4:4 Ndipo sipadzakhala wowaopseza

Mac 4:17 tiyeni tiwaopseze

Aef 6:9 akapolo anu, musamawaopseze

1Pe 2:23 Pamene ankazunzidwa, sanaopseze

OSAKHALITSA

, Ahe 11:13 osakhalitsa mʼdzikolo

OSAKHULUPIRIRA

, 1Ak 6:6 anthu osakhulupirira?

2Ak 6:14 Musamangidwe mʼgoli ndi osakhulupirira

OSALUNGAMA

, Mac 24:15 olungama, osalungama

1Ak 6:9 anthu osalungama sadzalowa

OSANKHIDWA

, Mt 24:22 chifukwa cha osankhidwawo, masikuwo

Mt 24:31 adzasonkhanitsa osankhidwa ake

OSAPHUNZIRA

, Mac 4:13 anali osaphunzira

OSAUKA

, 1Sa 2:8 Amachotsa osauka paphulusa

Sl 9:18 Mulungu sadzaiwala osauka

Sl 69:33 Yehova akumvetsera osauka

Miy 30:9 ndisasauke nʼkukaba

Lu 4:18 ndilengeze uthenga kwa osauka

Yoh 12:8 Osaukawo muli nawo

2Ak 6:10 osauka koma olemeretsa anthu

2Ak 8:9 anakhala wosauka

Aga 2:10 tizikumbukira osauka

OWOLOWA MANJA

, De 15:8 muzithandiza mowolowa manja

Miy 11:24 amapereka mowolowa manja

Miy 11:25 wopereka mowolowa manja

1Ti 6:18 owolowa manja, okonzeka kugawira

Yak 1:5 amapereka mowolowa manja

OYAMBA

, Mt 19:30 oyamba adzakhala omaliza

OYAMIKIRA

, Akl 3:15 sonyezani kuti ndinu oyamikira

OYENERERA

, 2At 1:5 ndinu oyenerera Ufumu

OYERA

, Eks 26:33 Malo Oyera, Malo Oyera Koposa

Le 19:2 Mukhale oyera, ndine woyera

Da 7:18 oyera adzalandira ufumu

1Pe 1:15 khalani oyera mʼmakhalidwe

Chv 4:8 Woyera, woyera ndi Yehova

P

PACHABE

, Yes 45:19 Muzindifunafuna pachabe

Yes 65:23 Sadzagwira ntchito pachabe

PACHIKA

. Onani MTENGO.

Lu 23:21 Apachikidwe ameneyo

PAFUPI

, De 10:20 muzikhala naye pafupi kwambiri

Sl 145:18 Yehova ali pafupi ndi onse

PAMBANA

, 1Ak 12:31 ndikuonetsani njira yopambana

Chv 2:7 Amene wapambana pankhondo

Chv 6:2 anapambana pankhondo yolimbana

PAMSIKA

, Mac 17:17 ankakambirana ndi anthu pamsika

PANDUKA

, Nu 20:10 tamverani anthu opanduka inu!

1Sa 15:23 kupanduka nʼchimodzimodzi kuwombeza

Miy 1:32 kupanduka kwa anthu osadziwa

PANGANO

, Ge 15:18 anachita pangano ndi Abulamu

Yer 31:31 ndidzachita pangano latsopano

Lu 22:20 Kapu iyi ikuimira pangano latsopano

Lu 22:29 Choncho ndikuchita nanu pangano

PANIKIZA

, 1Ak 7:35 osati kuti ndikupanikizeni

PARADAISO

, Lu 23:43 ndi ine mʼParadaiso

2Ak 12:4 mʼparadaisomo anamva mawu

PASIKA

, Eks 12:11 Ameneyu ndi Pasika wa Yehova

Eks 12:27 nsembe ya Pasika

1Ak 5:7 nsembe yathu ya Pasika

PATSIDWA

, Lu 12:48 amene anapatsidwa zambiri

PATSOGOLO

, Afi 3:16 mmene tapitira patsogolo

PATULIKA

, Eks 25:8 Mundipangire malo opatulika

Sl 73:17 ndinalowa mʼmalo opatulika aulemerero

PAULO

. Onaninso SAULO, 1Ak 1:12 ndine wa Paulo

PEMBEDZERA

, 1Ti 2:1 kupereka mapembedzero, Yak 5:16 Pemphero lopembedzera

PEMPHA

, Sl 2:8 Tandipempha, ndikupatsa mitundu

Sl 20:5 Yehova akwaniritse zopempha zanu

Mt 6:8 amadziwa musanamupemphe

Mt 7:7 Pitirizani kupempha, adzakupatsani

Yoh 14:13 chimene mudzapemphe mʼdzina langa

2Ak 5:20 mʼmalo mwa Khristu tikupempha

Aef 3:20 kuposa zonse zimene timapempha

Fili 9 ndichite kukupempha mwachikondi

1Yo 5:14 chilichonse chimene tingamupemphe

PEMPHERA

, 2Mf 19:15 Hezekiya anayamba kupemphera

Da 6:13 akumapemphera katatu

Mt 6:9 inu muzipemphera chonchi

Mko 1:35 Kumeneko anayamba kupemphera

Lu 5:16 ankapita kwayekha kukapemphera

Aro 8:26 sitidziwa zotchula popemphera

Aro 12:12 Muzilimbikira kupemphera

1At 5:17 Muzipemphera nthawi zonse

PEMPHERERA

, Mt 5:44 kupempherera, akukuzunzani

Mko 11:24 mukupempha ndi kuzipempherera

Mac 12:5 mpingo unkamupempherera

2At 3:1 pitirizani kutipempherera

PEMPHERO

, Sl 65:2 Inu Wakumva pemphero

Sl 141:2 Pemphero likhale ngati zofukiza

Miy 15:8 pemphero la wowongoka mtima

Miy 28:9 pemphero lake limakhala lonyansa

Yak 5:15 Pemphero lachikhulupiriro

1Pe 3:7 mapemphero asatsekerezedwe

Chv 8:4 mapemphero a oyera

PEREKA

, Eks 21:36 azipereka ngʼombe

Sl 31:5 Ndikupereka mzimu wanga

Da 11:31 zoyenera kuperekedwa nthawi zonse

Da 12:11 zoyenera kuperekedwa nthawi zonse

Mt 22:21 perekani za Kaisara kwa Kaisara

Mt 26:21 mmodzi wa inu andipereka

Aro 6:13 muwapereke kwa Mulungu

Aef 6:7 Muzitumikira ambuye modzipereka

1Yo 3:16 tiyenera kupereka moyo wathu

PEREKA CHILANGO

, 2At 1:6 Mulungu adzapereka chilango

PEREWERA

, 1Ak 13:9 ndipo tikunenera moperewera

PETULO

, Mt 14:29 Petulo anayenda pamadzi

Lu 22:54 Petulo ankawatsatira chapatali

Yoh 18:10 Simoni Petulo, anali ndi lupanga

Mac 12:5 Petulo anatsekeredwa mʼndende

PEWA

, Yes 53:3 anthu ankamupewa

PHANGA

, Mt 21:13 phanga la achifwamba

PHATIKA

, Ge 2:24 nʼkudziphatika kwa mkazi wake

PHEDWA

, Sl 44:22 ngati nkhosa zokaphedwa

PHIMBA

, Le 16:34 machimo a Aisiraeli aziphimbidwa

2Ak 3:15 imakhalabe yophimba

1Yo 2:2 anakhala nsembe yophimba

PHINDU

, Miy 15:27 wopeza phindu mwachinyengo

Mla 5:10 sakhutira ndi phindu limene amapeza

1Ak 6:12 zololeka, koma si zonse zili zaphindu

PHIRI

, Sl 24:3 angakwere kuphiri la Yehova

Yes 2:3 Tiyeni kuphiri la Yehova

Yes 11:9 Sizidzavulazana mʼphiri langa loyera

Da 2:35 phiri lalikulu linadzaza dziko lonse

PHIRI LA MAOLIVI

, Lu 22:39 anapita kuphiri la Maolivi

Mac 1:12 kuphiri la Maolivi pafupi ndi Yerusalemu

PHOMPHO

, Chv 11:7 chatuluka muphompho

Chv 17:8 chatsala pangʼono kutuluka kuphompho

Chv 20:3 anamuponyera mʼphompho

PHUNZIRA

, De 4:10 anthu kuti aphunzire

Da 12:4 adzaphunzira bukuli mokwanira

Mac 17:11 mtima wofuna kuphunzira

Afi 4:9 zimene munaphunzira, muzichita

2Ti 3:7 amaphunzira koma satha

PHUNZITSA

, Eza 7:10 aziphunzitsa malamulo

Sl 143:10 Ndiphunzitseni zimene mumafuna

Miy 9:9 Phunzitsa wolungama

Miy 22:6 Phunzitsa mwana

Yer 31:34 Munthu sadzaphunzitsanso mnzake

Mki 2:7 Wansembe ayenera kuphunzitsa

Mt 7:29 ankawaphunzitsa monga waulamuliro

Mt 15:9 amaphunzitsa malamulo

Mt 28:20 muziwaphunzitsa azisunga zonse

Yoh 7:16 Zimene ine ndimaphunzitsa

Aro 2:21 umaphunzitsa ena, bwanji sudziphunzitsa?

1Ti 2:12 Sindikulola kuti mkazi aziphunzitsa

PHUNZITSIDWA

, Yes 54:13 azidzaphunzitsidwa ndi Yehova

PHWANDO

, Yes 25:6 Phwando la zakudya, la vinyo

Aro 13:13 Tizipewa maphwando oipa

Aga 5:21 maphwando oipa

PHWANYA

, Yes 42:3 lophwanyika sadzalithyola

PILATO

, Yoh 19:6 Pilato anati: Mutengeni

PINDULITSA

, Miy 14:23 Kugwira ntchito kumapindulitsa

1Ak 10:24 zopindulitsa iyeyo

PINIHASI

, Nu 25:7 Pinihasi mwana wa Eleazara

PITA PATSOGOLO

, 1Ti 4:15 kuti ukupita patsogolo

PITIRIRA

, 1Ak 4:6 Musapitirire zinthu zolembedwa

PITITSA PADERA

, Eks 23:26 simudzapezeka mkazi wopititsa padera

PONDAPONDA

, Ahe 10:29 wapondaponda Mwana

PONDEREZA

, Sl 72:14 kuti asaponderezedwe

Mla 4:1 oponderezawo anali ndi mphamvu

Mla 7:7 kuponderezedwa kungapangitse misala

POTOZA

, 2Ak 4:2 kupotoza mawu a Mulungu

PSINJIKA

, Yes 57:15 ndimakhala ndi anthu opsinjika

PULANI

, Eks 26:30 motsatira pulani yake

1Mf 6:38 mogwirizana ndi pulani yake

Miy 15:22 Mapulani sakwaniritsidwa

Miy 19:21 mapulani ambiri mumtima

PULAWO

, Lu 9:62 Aliyense wogwira pulawo

PULUMUKA

, Yer 39:18 sudzaphedwa. Udzapulumuka

Mt 24:22 kufupikitsidwa, palibe akanapulumuka

Afi 2:12 kunjenjemera kuti adzapulumuke

PULUMUTSA

, 2Sa 22:3 mpulumutsi wanga

2Mb 20:17 mmene Yehova angakupulumutsireni

Yes 59:1 silinafupike moti nʼkulephera kupulumutsa

Mt 16:25 akufuna kupulumutsa moyo wake

Lu 19:10 kudzapulumutsa anthu osochera

Mac 4:12 palibe amene angatipulumutse

Mac 5:31 Mtumiki Wamkulu ndi Mpulumutsi

1Ti 4:16 udzadzipulumutsa komanso okumvera

2Pe 2:9 amadziwa kupulumutsa anthu

PUMA

, Da 12:13 udzapuma, pamapeto udzauka

PUNTHWA

, Yak 3:2 Paja tonsefe timapunthwa

PUNTHWITSA

, Mt 13:41 zinthu zonse zopunthwitsa

PUPULUMA

, Miy 19:2 amachita zinthu mopupuluma

PURISILA

, Mac 18:26 Purisila ndi Akula

PUSA

, Sl 14:1 wopusa amati: Kulibe Yehova

Miy 19:3 Kupusa kwa munthu

1Ak 3:19 nzeru zamʼdzikoli nʼzopusa

PUSITSA

, Yer 17:9 Mtima ndi wopusitsa kwambiri

Yer 20:7 Mwandipusitsa inu Yehova

PUSITSIKA

, Aga 6:7 Mulungu sapusitsika

PWETEKA

, Aro 9:2 mtima umandipweteka

1At 4:6 Pasapezeke wopweteka mʼbale wake

PWETEKEDWA MTIMA

, Miy 14:10 Ngati mtima ukumupweteka amadziwa

Mt 26:75 kulira mopwetekedwa mtima

R

RABEKA

, Ge 26:7 Rabeka anali wokongola

RAKELE

, Ge 29:18 zaka 7, kuti mudzandipatse Rakele

Yer 31:15 Rakele akulirira ana ake

S

SABATA

, Eks 20:8 Muzikumbukira tsiku la Sabata

Mt 12:8 Mbuye wa Sabata

Mko 2:27 Sabata linakhalako chifukwa cha munthu

Lu 14:5 itagwera mʼchitsime tsiku la Sabata

Akl 2:16 akuweruzeni chifukwa cha sabata

Ahe 4:9 mpumulo wa sabata udakalipo

SAKA

, Le 17:13 akasaka, azithira magazi pansi

SAKAZA

, Lu 15:13 ndipo anasakaza chuma

SAMALA

, Miy 14:16 wanzeru amachita mosamala

Miy 14:16 wopusa amachita zinthu mosasamala

Mac 17:11 ankafufuza Malemba mosamala

Aef 5:15 samalani, muziyenda ngati anzeru

1Ti 4:16 uzisamala ndi zimene umachita

SAMALIRA

, 1Ak 12:25 ziwalo zake zizisamalirana

1Ti 5:8 ngati sasamalira a mʼbanja lake

SAMARIYA

, 2Mf 17:6 mfumu inalanda Samariya

Lu 10:33 panafika Msamariya wina

Yoh 4:7 mayi wa mu Samariya anafika

SAMBA

, Le 15:19 wodetsedwa chifukwa akusamba

Le 18:19 usagone ndi mkazi pamene akusamba

2Mf 5:10 mukasambe maulendo 7

SAMBITSA

, Sl 51:2 Mundisambitse nʼkuchotsa cholakwa

Yoh 13:5 nʼkuyamba kusambitsa mapazi

1Ak 6:11 mwasambitsidwa kukhala oyera

SAMISONI

, Owe 13:24 anamupatsa dzina, Samisoni

SAMUELI

, 1Sa 1:20 anamupatsa dzina lakuti Samueli

1Sa 2:18 Samueli ankatumikira ali mwana

SANGAFE

, 1Ak 15:53 nʼkukhala oti sangafe

SANGALALA

, 1Mb 28:9 uzimutumikira mosangalala

1Mb 29:9 anasangalala chifukwa cha nsembe

Yob 38:7 nyenyezi zinafuula mosangalala

Sl 32:1 Wosangalala, machimo ake akhululukidwa

Sl 37:4 Uzisangalala chifukwa cha Yehova

Sl 40:8 Ndimasangalala kuchita zimene mumafuna

Sl 94:12 Wosangalala ndi amene mumamulangiza

Sl 144:15 Osangalala ndi anthu

Sl 149:4 Yehova amasangalala ndi anthu ake

Miy 8:30 Ndinkakhala wosangalala pamaso pake

Miy 8:30 ankasangalala kwambiri ndi ine

Mla 2:24 amwe ndi kusangalala

Mla 8:15 kudya, kumwa ndi kusangalala

Yes 65:13 Atumiki anga adzasangalala

Yes 65:14 Atumiki anga adzafuula mosangalala

Eze 18:32 sindisangalala ndi imfa ya aliyense

Mt 5:3 Osangalala, amazindikira zosowa zauzimu

Lu 8:13 amalandira mawuwo mosangalala

Lu 15:7 kumwamba kudzakhala chisangalalo

Yoh 16:22 kuti musiye kusangalala

Mac 5:41 atumwiwo anali osangalala

Mac 20:35 Kupatsa kumatichititsa kusangalala

Aro 5:3 kumasangalala tikakumana ndi mavuto

Aro 7:22 ndimasangalala ndi malamulo a Mulungu

Aro 12:15 Muzisangalala ndi amene akusangalala

Aro 15:13 Mulungu akuthandizeni kusangalala

2Ak 9:7 munthu amene amapereka mosangalala

Afi 3:1 kusangalala monga otsatira a Ambuye

Afi 4:4 muzisangalala chifukwa cha Ambuye

Ahe 12:2 podziwa kuti adzasangalala, anapirira

Chv 18:7 kusangalala ndi chuma mopanda manyazi

SANGALATSA

, Sl 137:6 chimene chimandisangalatsa kwambiri

Sl 147:1 Kumutamanda nʼkosangalatsa

Miy 27:11 khala wanzeru usangalatse mtima

Lu 3:22 umandisangalatsa kwambiri

Yoh 8:29 zimamusangalatsa nthawi zonse

1Ak 10:33 Ndikuyesetsa kusangalatsa anthu

Aga 1:10 ndikungofuna kusangalatsa anthu

Aef 1:5 zimene zinamusangalatsa

Aef 6:6 pongofuna kuwasangalatsa

Akl 1:10 muzimusangalatsa pa chilichonse

3Yo 4 chimandisangalatsa, akuyendabe mʼchoonadi

SANKHA

, De 30:19 musankhe moyo

Yos 24:15 sankhani amene mukufuna kumʼtumikira

Yer 1:5 usanabadwe, ndinakusankha

Afi 1:10 muzitha kusankha zofunikadi

SARA

, Ge 17:19 Sara adzakuberekera mwana

1Pe 3:6 Sara ankamutchula kuti mbuyanga

SASATITSA

, Miy 29:21 Ngati akusasatitsa kapolo

SATANA

, Yob 1:6 Satana nayenso anafika

Zek 3:2 Satana, Yehova akudzudzule

Mt 4:10 Choka Satana! Malemba amati

Mt 16:23 Pita kumbuyo kwanga, Satana

Mko 4:15 Satana amabwera nʼkudzachotsa mawu

Aro 16:20 aphwanya Satana pansi pa mapazi anu

1Ak 5:5 mupereke munthu ameneyu kwa Satana

2Ak 2:11 Satana asatichenjerere

2Ak 11:14 Satana, mngelo wa kuwala

2At 2:9 mphamvu za Satana, zizindikiro zabodza

Chv 12:9 njoka yakale, Mdyerekezi, Satana

Chv 20:2 Satana, nʼkumumanga zaka 1,000

SAULI

, 1Sa 15:11 ndinaika Sauli kukhala mfumu

SAULO

, Mac 7:58 zinaika malaya pafupi ndi Saulo

Mac 8:3 Saulo anayamba kuzunza mpingo

Mac 9:1 Saulo anapitiriza kuopseza ophunzira

Mac 9:4 Saulo, nʼchifukwa chiyani ukundizunza?

SEFUKIRA

, Lu 6:45 zosefukira mumtima

SEKA

, Ge 18:13 Nʼchifukwa chiyani Sara waseka?

Sl 2:4 Wokhala pampando kumwamba adzaseka

Miy 14:13 akuseka, mtima ukumupweteka

SENAKERIBU

, 2Mf 19:16 mawu a Senakeribu onyoza

SIKELO

, Le 19:36 Muzikhala ndi masikelo olondola

Miy 11:1 amanyasidwa ndi masikelo achinyengo

SILIVA

, Miy 2:4 kuzifunafuna ngati siliva

Eze 7:19 Siliva wawo adzamutaya

Zef 1:18 Siliva kapena golide

SILO

, Ge 49:10 mpaka Silo atabwera

SIMONI

, Mac 8:18 Simoni ataona atumwiwo

SIMUNGACHITE

, Ge 18:25 Simungachite zimenezo

SINAI

, Eks 19:20 pamwamba pa phiri la Sinai

SINKHASINKHA

, Ge 24:63 kuti akasinkhesinkhe

SINTHA

, Mki 3:6 ndine Yehova, sindisintha

2At 2:2 asinthe maganizo anu

2Ak 13:11 pitirizani kusintha maganizo

SINTHANITSA

, Mt 16:26 asinthanitse ndi moyo wake

SITEPE

, Ge 28:12 Mʼmalotowo anaona masitepe

SIYA

, De 31:8 Sadzakutayani kapena kukusiyani

1Sa 12:22 Yehova sadzasiya anthu ake

Sl 27:10 bambo anga ndi mayi anga atandisiya

Sl 37:28 Yehova sadzasiya anthu ake

Yes 1:28 amene akusiya Yehova adzatha

Mt 19:9 wasiya mkazi wake

Mt 19:29 wasiya nyumba kapena minda

Yoh 8:29 Iye sanandisiye ndekha

1Ak 7:10 mkazi asasiye mwamuna wake

Aga 6:9 tisasiye kuchita zabwino

Afi 2:7 anasiya zonse nʼkukhala kapolo

Ahe 13:5 Sindidzakusiyani kapena kukutayani

1Pe 2:23 anasiya zonse mʼmanja

SIYANITSA

, Aro 8:39 kutisiyanitsa ndi chikondi

SOCHERA

, Sl 119:176 Ndasochera ngati nkhosa yotayika

Eze 34:4 Nkhosa zosochera simunazifufuze

SOCHERETSA

, Mt 24:24 adzasocheretse ngakhale osankhidwawo

SODOMU

, Ge 19:24 ngati mvula ku Sodomu

2Pe 2:6 mizinda ya Sodomu ndi Gomora

Yuda 7 anthu amʼmizinda ya Sodomu

SODZA

, Lu 5:10 Kuyambira lero uzisodza anthu

SOLOMO

, 1Mf 4:29 anapatsa Solomo nzeru

Mt 6:29 Solomo mu ulemerero wake

SONKHANA

, Ahe 10:25 Tisasiye kusonkhana

SONKHANITSA

, Aef 1:10 kusonkhanitsa zinthu zonse

SONYEZA

, Lu 3:8 mubale zipatso zosonyeza kulapa

Mac 17:3 kusonyeza umboni wolembedwa

Aro 5:8 Mulungu akutisonyeza chikondi

2Ak 6:4 tikusonyeza mʼnjira iliyonse

SUKULU

, Yoh 7:15 popeza sanapite kusukulu

SUNGA

, Mt 28:20 muziwaphunzitsa kuti azisunga

Yoh 14:15 mudzasunga malamulo anga

SUNGA ZIFUKWA

, 1Ak 13:5 sichisunga zifukwa

SWEKA

, Miy 18:14 mtima wosweka ndani angaupirire

2Ak 11:25 Ngalawa inandiswekerapo

1Ti 1:19 chikhulupiriro chasweka ngati ngalawa

1Pe 3:7 chiwiya chosachedwa kusweka

T

TAFUNA

, Ahe 5:14 chakudya chotafuna

TALIKITSA

, Yes 54:2 Talikitsa zingwe za tenti yako

Mt 6:27 angatalikitse moyo pangʼono pokha

TAMANDA

, Sl 146:1 Moyo wanga utamande Yehova

Sl 147:1 Kuimba nyimbo zomutamanda

Sl 150:6 chilichonse chitamande Ya

Miy 27:2 Munthu wina akutamande

Miy 27:21 anthu akunena pomutamanda

Yuda 16 Amatamanda anthu kuti apeze phindu

Chv 19:1 Tamandani Ya!

TAMBALA

, Mt 26:34 tambala asanalire, undikana

TANGANIDWA

, Lu 10:40 Marita anatanganidwa

TARISI

, Yon 1:3 ananyamuka nʼkulowera ku Tarisi

TATALASI

, 2Pe 2:4 anawaponya mu Tatalasi

TAYA MTIMA

, 2Ak 4:1 tili ndi utumiki, sitikutaya mtima

2Ak 4:16 sitikutaya mtima, munthu wakunja akutha

TAYIKA

, Lu 15:24 anatayika, wapezeka

TCHIMO

, Sl 32:1 machimo ake akhululukidwa

Sl 38:18 Tchimo linkandisowetsa mtendere

Yes 1:18 machimo anu ndi ofiira

Yes 38:17 Machimo mwawaponyera kumbuyo

Yes 53:12 Ananyamula tchimo la anthu ambiri

Yer 31:34 machimo awo sindidzawakumbukiranso

Eze 33:14 nʼkusiya machimo akewo

Mko 3:29 mlandu wa tchimo losatha

Yoh 1:29 akuchotsa uchimo wa dziko

Yoh 15:22 sangakane tchimo lawo

Mac 3:19 machimo anu afafanizidwe

Aro 3:25 wosakwiya msanga, pokhululuka machimo

Aro 5:12 Uchimo unalowa mʼdziko

Aro 6:14 Uchimo usamakulamulireni

Aro 6:23 malipiro a uchimo ndi imfa

1Ti 5:24 machimo awo amadzaonekera

Yak 5:15 ngati anachita machimo

1Yo 1:7 akutiyeretsa ku machimo onse

1Yo 2:1 wina akachita tchimo

1Yo 5:17 pali tchimo losabweretsa imfa

TCHULA

, Aef 5:3 zisatchulidwe pakati panu

TEBULO

, Da 11:27 adzakhala patebulo limodzi

1Ak 10:21 muzidya patebulo la Yehova

TEMA

, Le 21:5 asamadzitemeteme thupi lawo

TEMBERERA

, Nu 23:8 Ndingathe bwanji kutemberera?

Aro 12:14 Muzidalitsa, osati kutemberera

TEMBEREREDWA

, Yoh 7:49 osadziwa Chilamulo ndi otembereredwa

TENGEKA

, Aef 4:14 tisamatengeke uku ndi uku

Ahe 2:1 tisatengeke pangʼonopangʼono

TENGERA

, Aro 12:2 Musamatengere nzeru za nthawi ino

TENTHETSANA

, Aro 1:27 nʼkumatenthetsana mwachiwawa

TENTI

, Sl 15:1 mlendo mutenti yanu?

Yes 54:2 Talikitsa zingwe za tenti

2Ak 12:9 zikhalebe ngati tenti

TERERA

, Sl 73:18 mwawaika pamalo oterera

TETEZA

, Miy 4:23 Uteteze mtima wako

Mla 7:12 nzeru zimateteza

TETEZEKA

, Miy 12:3 wotetezeka chifukwa chochita zoipa

Yes 25:4 Malo otetezeka kwa wosauka

THAMANGA

, 1Ak 9:24 Muzithamanga kuti mukalandire mphotoyo

Aga 5:7 Munkathamanga bwino

THANDIZA

, Mac 20:20 chilichonse chothandiza

1Ak 7:35 Ndikunenatu izi kuti ndikuthandizeni

Aga 6:1 kuthandiza ndi mzimu wofatsa

Aef 4:12 nʼcholinga choti athandize

2Ti 3:16 Malemba anauziridwa, ndi othandiza

THANDIZO

, Sl 46:1 Thandizo lopezeka mosavuta

THANTHWE

, De 32:4 Thanthwe, ntchito yake ndi yangwiro

Mt 7:24 anamanga nyumba yake pathanthwe

THAWA

, 1Ak 6:18 Thawani chiwerewere

THAWIRA

, Nah 1:7 amene amathawira kwa iye

THEDWA NZERU

, Yes 44:8 Ndipo musathedwe nzeru

THEKA

, Ge 18:14 pali chosatheka ndi Yehova?

2Ti 2:15 Chita chilichonse chotheka

THIRIRA

, 1Ak 3:6 Apolo anathirira

THOKOZA

, Mac 28:15 Paulo atawaona, anathokoza

1Ak 1:4 ndimathokoza Mulungu wanga

1Ti 1:12 Ndikuthokoza Khristu Yesu

THUPI

, Ge 2:24 adzakhala thupi limodzi

Mt 10:28 Musachite mantha ndi opha thupi

Mt 26:26 Mkate uwu ukuimira thupi langa

Aro 6:13 Matupi anunso muwapereke kwa Mulungu

Aro 8:5 otsatira zofuna za thupi

Aro 12:1 mupereke matupi ngati nsembe

1Ak 7:4 asakhale ndi ulamuliro pathupi lake

1Ak 12:18 Mulungu anaika ziwalo zonse za thupi

1Ak 15:44 Limakwiriridwa lili thupi la mnofu

Aga 5:19 ntchito za thupi zimaonekera

Afi 3:21 adzasintha thupi lathu lonyozekali

THYOLA

, Miy 29:1 oumitsa khosi adzathyoledwa

TIMOTEYO

, Mac 16:1 wophunzira, Timoteyo

1Ak 4:17 ndikukutumizirani Timoteyo

1Ti 1:2 Timoteyo, mwana wanga weniweni

TINGATHE

, Aga 6:10 ngati tingathe, tichitire onse zabwino

TIRIGU

, Mt 13:25 namsongole mʼmunda wa tiriguwo

TONTHOZA

, Yob 16:2 otonthoza obweretsa mavuto!

Sl 94:19 Nkhawa zitachuluka, munanditonthoza

Yes 49:13 Yehova watonthoza anthu ake

Yes 61:2 nditonthoze anthu onse amene akulira

Yer 31:15 Rakele wakana kutonthozedwa

2Ak 1:3 Mulungu amene amatitonthoza

2Ak 1:4 kutonthoza amene akuyesedwa

TONZA

, Miy 27:11 ndimuyankhe amene amanditonza

TOPA

, Yes 40:28 Iye satopa kapena kufooka

TSALA

, Mt 14:20 zinatsala madengu 12

Chv 12:17 mbadwa zimene zinatsala

TSANKHO

, Mac 10:34 Mulungu alibe tsankho

TSANZIRA

, 1Ak 11:1 Muzitsanzira ine

Aef 5:1 muzitsanzira Mulungu ngati ana ake

Ahe 13:7 tsanzirani chikhulupiriro chawo

TSATANETSATANE

, Lu 1:3 ndikulembereni mwatsatanetsatane

TSATIRA

, Mt 4:20 anasiya maukonde nʼkumutsatira

Mt 19:21 ukhale wotsatira wanga

Yoh 10:27 Nkhosa zanga zimanditsatira

Chv 14:4 amatsatira Mwanawankhosa kulikonse

TSAYA

, Mt 5:39 akakumenyani patsaya lakumanja

TSEKA

, 1Pe 2:15 kuti muwatseke pakamwa

TSIKU

, Sl 84:10 tsiku limodzi mʼmabwalo anu

Eze 4:6 tsiku limodzi, chaka chimodzi

Mt 24:36 tsiku ndi ola, palibe akudziwa

2Pe 3:8 tsiku limodzi, zaka 1,000

TSIKU LA YEHOVA

, Yow 2:1 tsiku la Yehova lili pafupi

Amo 5:18 chidzakuchitikireni pa tsiku la Yehova?

Zef 1:14 Tsiku la Yehova lili pafupi

1At 5:2 tsiku la Yehova lidzabwera ngati wakuba

2At 2:2 tsiku la Yehova lafika

2Pe 3:12 kumbukirani tsiku la Yehova

TSIKU LOBADWA

, Ge 40:20 tsiku lokumbukira kubadwa kwa Farao

Mt 14:6 tsiku lobadwa la Herode

TSIMIKIZA

, Mac 17:31 watsimikiza pomuukitsa

TSIMIKIZA MTIMA

, Aro 8:38 ndatsimikiza mtima kuti

1At 1:5 tinalalikira motsimikiza mtima

TSIRIZA

, Yes 2:2 Mʼmasiku otsiriza

TSITSI

, Mt 10:30 tsitsi lonse lamʼmutu mwanu

Lu 21:18 tsitsi lamʼmutu mwanu

1Ak 11:14 ngati mwamuna ali ndi tsitsi lalitali

TSITSIMULA

, Mt 11:28 Bwerani, ndidzakutsitsimulani

TSITSIMUTSA

, Yes 57:15 nditsitsimutse onyozeka

Mac 3:19 nyengo zotsitsimutsa zibwere

TSOGOLERA

, Sl 48:14 adzatitsogolera mpaka kalekale

Aro 12:8 Wotsogolera, azitsogolera mwakhama

1At 5:12 muzilemekeza amene amakutsogolerani

Ahe 13:7, 17 Muzikumbukira akukutsogolerani

Ahe 13:7, 17 Muzimvera amene akukutsogolerani

TSOGOLO

, Sl 73:17 ndinazindikira tsogolo lawo

Miy 24:20 woipa alibe tsogolo

TSOKA

, Miy 22:3 akaona tsoka amabisala

Yes 5:20 Tsoka amene akunena kuti

1Ak 9:16 Tsoka ngati sindilalikira

Chv 12:12 Tsoka dziko lapansi ndi nyanja

TSUTSA

, Lu 21:15 nzeru zimene otsutsa sadzazikana

Mac 17:7 akuchita zotsutsana ndi Kaisara

Aro 8:31 ndani adzatsutsana nafe?

1Ak 16:9 koma pali otsutsa ambiri

Afi 1:28 musaope amene akukutsutsani

1At 2:2 tinalimba mtima pamene ankatitsutsa

TUKWANA

, Yob 2:5 akutukwanani mʼmaso muli gwa!

Yob 2:9 Tukwanani Mulungu mufe!

Aef 5:4 zopusa, nthabwala zotukwana

Akl 3:8 pakamwa pasatuluke zotukwana

TULO

, Aro 13:11 nthawi yoti mudzuke ku tulo

TULUKANI

, Yes 52:11 tulukani, musakhudze chodetsedwa

Chv 18:4 Tulukani mwa iye anthu anga

TUMIKIRA

, Yos 24:15 amene mukufuna kumʼtumikira

1Sa 2:11 mwanayo anatsala nʼkumatumikira

1Mb 28:9 uzimutumikira ndi mtima wonse

Sl 100:2 Tumikirani Yehova mokondwera

Da 7:10 100 miliyoni ankatumikira

Mt 20:28 anabwera kudzatumikira

Aga 5:13 chizikulimbikitsani kutumikirana

1Pe 4:10 muzigwiritsa ntchito mphatso potumikirana

TUMIZA

, Yes 6:8 Kodi nditumize ndani?

U

UBATIZO

, Lu 3:3 ubatizo, chizindikiro cha kulapa

1Pe 3:21 ubatizo, ukupulumutsanso inuyo

UBWENZI

, Sl 25:14 amakhala naye pa ubwenzi

Miy 3:32 amakhala nawo pa ubwenzi

UBWEYA

, Owe 6:37 mame pa ubweya wokhawu

UCHI

, Eks 3:8 dziko loyenda mkaka ndi uchi

Miy 25:27 Si bwino kudya uchi wambiri

UCHIMO

, Ge 4:7 uchimo wakubisalira pakhomo

Aro 6:14 Uchimo usamakulamulireni

UDINDO

, Mac 1:20 Udindo wake monga woyangʼanira

UDZU

, Yes 65:25 Mkango udzadya udzu

1Ak 3:12 mitengo, udzu ndi ziputu

UFULU

, Aro 8:21 ufulu waulemerero wa ana

1Ak 9:18 ndisagwiritse ntchito molakwa ufulu

2Ak 3:17 pali mzimu, pali ufulu

1Pe 2:16 musamagwiritse ntchito ufulu

2Pe 2:19 akuwalonjeza ufulu

UFUMU

, Eks 19:6 mudzakhala ufumu wa ansembe

Da 2:44 Mulungu adzakhazikitsa ufumu

Da 7:14 anamupatsa ulamuliro, ulemu ndi ufumu

Da 7:18 oyera adzalandira ufumu

Mt 6:10 Ufumu wanu ubwere. Zofuna zanu

Mt 6:33 muziika Ufumu pamalo oyamba

Mt 21:43 Ufumu udzachotsedwa, nʼkuperekedwa

Mt 24:14 Uthenga wa Ufumu udzalalikidwa

Mt 25:34 Bwerani, lowani mu Ufumu

Lu 12:32 wavomereza kukupatsani Ufumu

Lu 22:29 ndikuchita nanu pangano la ufumu

Yoh 18:36 Ufumu wanga si wamʼdzikoli

Mac 1:6 mubwezeretsa ufumu panopa?

1Ak 15:24 adzapereka Ufumu kwa Mulungu

Aga 5:21 sadzalowa mu Ufumu wa Mulungu

Akl 1:13 nʼkutisamutsira mu ufumu

Chv 11:15 Ufumu wa dziko wakhala Ufumu

UKA

, Yoh 5:29 adzauka kuti alandire moyo

Yoh 11:24 adzauka mʼtsiku lomaliza

Yoh 11:25 Ine ndine kuuka ndi moyo

1Ak 15:13 ngati sadzauka, Khristu sanaukitsidwe

UKITSA

, Yoh 6:39 ndidzawaukitse pa tsiku lomaliza

Mac 2:24 Mulungu anamuukitsa

Mac 24:15 adzaukitsa olungama ndi osalungama

UKITSIDWA

, Mt 22:23 amati akufa sadzaukitsidwa

Mt 22:30 akadzaukitsidwa, sadzakwatira

1Pe 3:18 koma anaukitsidwa monga mzimu

UKONDE

, Lu 5:4 muponye maukonde muphe nsomba

UKWATI

, De 7:3 mgwirizano wa ukwati

Mt 22:2 mfumu inakonza phwando la ukwati

Yoh 2:1 ku Kana kunali ukwati

Ahe 13:4 Ukwati ukhale wolemekezeka

Chv 19:7 ukwati wa Mwanawankhosa

ULEMERERO

, Yoh 12:43 ankakonda ulemerero

Aro 3:23 amalephera kusonyeza ulemerero

Aro 8:18 powayerekezera ndi ulemerero

1Ak 10:31 zibweretse ulemerero kwa Mulungu

2Pe 2:10 Mulungu wawapatsa ulemerero

Chv 4:11 woyenera kulandira ulemerero

ULEMU

, Miy 5:9 usapereke ulemu kwa ena

Aro 12:10 Posonyezana ulemu

1At 5:13 Muziwasonyeza ulemu waukulu

1Ti 2:9 akazi ayenera kuvala mwaulemu

1Pe 3:2 khalidwe labwino komanso ulemu

1Pe 3:15 muziwayankha mwaulemu

ULERE

, Mt 10:8 Munalandira kwaulere

1Ak 9:18 ndikamalalikira uthenga kwaulere

Chv 22:17 madzi amoyo kwaulere

ULESI

, Miy 6:6 Pita kwa nyerere waulesi iwe

Miy 10:26 utsi umapweteka, ngati munthu waulesi

Miy 19:15 waulesi adzakhala ndi njala

Miy 19:24 waulesi amapisa dzanja lake mʼmbale

Miy 20:4 Waulesi salima nthawi yozizira

Mt 25:26 Kapolo woipa ndi waulesi

Aro 12:11 Khalani akhama osati aulesi

ULOSI

, 2Pe 1:19 mawu aulosiwa adzakwaniritsidwa

2Pe 1:20 palibe ulosi wa mʼMalemba

2Pe 1:21 ulosi sunachokere kwa anthu

ULULA

, Sl 32:5 Pamapeto pake ndinaulula tchimo

Miy 28:13 amawaulula adzachitiridwa chifundo

Mt 11:25 mwaziulula kwa ana angʼono

1Ak 2:10 Mulungu anatiululira zinthu zimenezi

Aef 3:5 sichinaululidwe kwa atumwi ndi aneneri

Yak 5:16 muululirane machimo anu poyera

ULUSI

, Nu 15:39 zizikhala ndi ulusi

UMBA

, Yes 64:8 ndife dongo, inu ndinu Wotiumba

Aro 9:21 woumba mbiya ali ndi ufulu

UMBONI

, Mt 24:14 ukhale umboni kwa anthu

Yoh 7:7 chifukwa ndimachitira umboni

Yoh 18:37 ndidzachitire umboni choonadi

Mac 10:42 kupereka umboni wokwanira

Mac 28:23 anachitira umboni mokwanira

UMITSA

, Ahe 3:13 chinyengo chisaumitse mtima

UMITSA MTIMA

, Mt 13:15 anthu aumitsa mitima

UMODZI

, Aef 4:3 Muziyesetsa kusunga umodzi

UMPHAWI

, Miy 30:8 Musandipatse umphawi

2Ak 8:2 anali pa umphawi wadzaoneni

UMUNTHU

, Aef 4:24 muvale umunthu watsopano

Akl 3:9 Vulani umunthu wakale

UNGATHE

, Miy 3:27 kuchita zabwino ngati ungathe

URIMU NDI TUMIMU

, Eks 28:30 Udzaike Urimu ndi Tumimu

USIKU

, Sl 19:2 usiku zimasonyeza nzeru zake

Aro 13:12 Usiku uli pafupi kutha ndipo masana

UTAWALEZA

, Ge 9:13 utawaleza, ukhala chizindikiro

UTHENGA

, Sl 112:7 Sadzaopa uthenga woipa

UTHENGA WABWINO

, Yes 52:7 mapazi obweretsa uthenga wabwino

Mt 24:14 Uthenga wabwino udzalalikidwa

Lu 4:43 Ndiyenera kulengeza uthenga wabwino

Aro 1:16 sindichita manyazi ndi uthenga wabwino

1Ak 9:16 ngati sindilalikira uthenga wabwino

1Ak 9:23 chifukwa cha uthenga wabwino

UTUMIKI

, Mac 20:24 ndimalize utumiki

Aro 11:13 ndimalemekeza utumiki wanga

2Ak 4:1 utumiki mogwirizana ndi chifundo

2Ak 6:3 asapezere chifukwa utumiki wathu

1Ti 1:12 anandipatsa utumiki

2Ti 4:5 uzikwaniritsa mbali zonse za utumiki

UTUMIKI WOPATULIKA

, Aro 12:1 nsembe yomwe ndi utumiki wopatulika

UZIDWA

, 1Mb 28:12 mapulani a zimene anauzidwa

UZIMU

, Mt 5:3 amazindikira zosowa zawo zauzimu

Aro 1:11 ndikupatseni mphatso yauzimu

1Ak 2:15 munthu wauzimu amafufuza

1Ak 15:44 limaukitsidwa thupi lauzimu

UZIRIDWA

, 2Ti 3:16 Malemba onse anauziridwa

UZIYA

, 2Mb 26:21 Uziya anakhala wakhate

V

VALA

, 1Ak 11:6 ngati mkazi savala kanthu kumutu

VINA

, Owe 11:34 mwana wake anabwera akuvina

VINYO

, Le 10:9 musamamwe vinyo

Sl 104:15 vinyo amasangalatsa mtima

Miy 20:1 amene amamwa vinyo wambiri

Miy 23:31 Usakopeke ndi kufiira kwa vinyo

Mla 10:19 vinyo amasangalatsa moyo

Yes 25:6 Phwando la vinyo wabwino

Ho 4:11 vinyo wakale, vinyo watsopano

Yoh 2:9 madzi amene anawasandutsa vinyowo

1Ti 5:23 uzimwa vinyo pangʼono

VOMEREZA

, Lu 23:51 sanavomereze chiwembu

Yoh 8:37 simukuvomereza zimene ndikuphunzitsa

2Ak 6:2 inoyo ndi nthawi yovomerezedwa

1Yo 1:9 tikavomereza machimo, adzatikhululukira

VOMEREZEKA

, Aef 5:10 kuti chovomerezeka nʼchiti

2Ti 2:15 usonyeze kuti ndiwe wovomerezeka

VULAZANA

, Yes 11:9 Sizidzavulazana, kuwonongana

VULAZIDWA

, Chv 13:3 unali utavulazidwa kwambiri

VUTA

, 1Yo 5:3 malamulo akewo si ovuta kuwatsatira

VUTIKA

, Aro 8:17 ngati tikuvutika naye limodzi

1Ak 12:26 ziwalo zina zonse zimavutika

Afi 1:29 mwayi wovutika chifukwa cha iye

1Pe 3:14 ngakhale mutavutika, mumasangalalabe

1Pe 4:18 wolungama angadzapulumuke movutikira

VUTO LOSAMVA

, Le 19:14 ali ndi vuto losamva

Yes 35:5 a vuto losamva adzayamba kumva

Mko 7:37 a vuto losamva akumva

VUTO LOSAONA

, Le 19:14 ali ndi vuto losaona musamamuikire

Yes 35:5 maso a anthu amene ali ndi vuto losaona

W

WAKHANDA

, 2Ti 3:15 Kuyambira uli wakhanda

WAKHATE

, Le 13:45 wakhate ankafuula

WAKUBA

, De 24:7 wakuba munthu ayenera kufa

Miy 6:30 Anthu sanyoza wakuba

Miy 29:24 wakuba amadzibweretsera mavuto

Mt 24:43 nthawi imene wakuba angabwere

1At 5:2 ngati wakuba usiku

WAKUFA

, Lu 15:24 mwana wangayu anali wakufa

WAMASIKU AMBIRI

, Da 7:9 Wamasiku Ambiri anakhala pampando

WAMBIRI

, Sl 72:16 padzakhala tirigu wambiri

WAMKULU

, Yoh 14:28 Atate ndi wamkulu kuposa ine

1Yo 3:20 ndi wamkulu kuposa mitima yathu

WAMʼMWAMBAMWAMBA

, Sl 83:18 Yehova, Wamʼmwambamwamba

Da 4:17 Wamʼmwambamwamba ndi Wolamulira

WAMNGʼONO

, Yes 60:22 Wamngʼono adzasanduka 1,000

Mko 10:20 kuyambira ndili wamngʼono

1Ti 4:12 poona kuti ndiwe wamngʼono

WANGWIRO

, Ahe 2:10 anakhala wangwiro

WANSEMBE

, Sl 110:4 wansembe mpaka kalekale

Ho 4:6 asamanditumikire ngati wansembe

Mki 2:7 Wansembe ayenera kuphunzitsa

WANTCHITO

, Lu 10:7 wantchito ayenera kulandira malipiro

WENIWENI

, 1Ti 6:19 agwire moyo weniweniwo

WERENGA

, De 17:19 aziliwerenga masiku onse

Mac 8:30 mukumvetsa zimene mukuwerengazo?

WERENGERA

, Lu 14:28 nʼkuwerengera ndalama

WERUZA

, Yes 26:9 mukaweruza dziko lapansi

Mt 7:2 mmene mumaweruzira ena

Lu 6:37 siyani kuweruza, simudzaweruzidwa

Lu 22:30 kuweruza mafuko 12

Yoh 5:22 wapereka udindo woweruza

Mac 17:31 tsiku limene akufuna kudzaweruza

Aro 14:4 kuti uweruze wantchito wa mnzako?

1Ak 6:2 oyerawo adzaweruza dziko

2Ak 1:9 taweruzidwa kuti tiphedwe

Yak 4:12 ndiwe ndani kuti uziweruza mnzako?

WETA

, Mac 20:28 muwete mpingo wa Mulungu

1Pe 5:2 Wetani gulu la nkhosa

WILO

, Eze 1:16 wilo lina lili pakati pa linzake

WINDO

, Mac 20:9 Utiko anakhala pawindo

WOBADWA YEKHA

, Yoh 1:18 mulungu wobadwa yekha

Yoh 3:16 anapereka Mwana wobadwa yekha

WODETSEDWA

, Le 13:45 nʼkumafuula kuti, wodetsedwa!

WODZIDALIRA

, Miy 14:16 wopusa amakhala wodzidalira

WOFUNDA

, Chv 3:16 chifukwa choti ndiwe wofunda

WOIPA

, Miy 15:8 Nsembe ya munthu woipa

Miy 29:2 munthu woipa akamalamulira

Yes 26:10 munthu woipa atachitiridwa zabwino

1Yo 5:19 lili mʼmanja mwa woipayo

WOKHOMETSA MSONKHO

, Mt 18:17 akhale ngati wokhometsa msonkho

Lu 18:11 Ndine wosiyana ndi wokhometsa msonkho

WOKHULUPIRIKA

, 2Sa 22:26 wokhulupirika, mumamuchitira

Sl 16:10 Simudzalola wokhulupirika aone dzenje

WOKOMA MTIMA

, Eks 34:6 Mulungu wachifundo, wokoma mtima

WOKONDEDWA

, Da 9:23 wokondedwa kwambiri

WOLA

, Aef 4:29 Mawu owola asamatuluke pakamwa

WOLANKHULA NDI MIZIMU

, De 18:11 wofunsira kwa wolankhula ndi mizimu

WOLEMEKEZEKA

, Mac 24:3 Wolemekezeka a Felike

WOMBOLA

, Sl 49:7 Palibe angawombole mʼbale

Ho 13:14 Ine ndidzawombola anthu

WOMVETSA CHISONI

, Aro 7:24 Munthu womvetsa chisoni ine!

WONONGA

, Eze 21:27 Ine ndidzawononga

Aro 14:20 Siyani kuwononga ntchito ya Mulungu

2Pe 3:7 kuwononga anthu osaopa Mulungu

Chv 11:18 muwononge amene akuwononga dziko

WONONGEKA

, 1Ak 15:42 limene limaukitsidwa silingawonongeke

WONYOZEKA

, 1Sa 2:8 Amadzutsa wonyozeka

Sl 41:1 moganizira munthu wonyozeka

WOONA

, Yoh 17:3 Mulungu yekhayo woona

WOPANDA NTCHITO

, Sl 119:141 wopanda ntchito ndi wonyozeka

WOPANDA NZERU

, Lu 12:20 Wopanda nzeru iwe

WOPEREKA MALAMULO

, Yak 4:12 Wopereka Malamulo alipo mmodzi

WOPHA ANTHU

, Yoh 8:44 wopha anthu kuchokera pachiyambi

WOPHA MNZAKE

, Nu 35:6 wopha mnzake azikathawirako

WOSACHEDWA KUKWIYA

, Miy 21:19 mkazi wosachedwa kukwiya

WOSACHIMWA

, Yob 14:4 angabereke munthu wosachimwa?

WOSADZIWA ZINTHU

, Sl 19:7 zimapatsa nzeru wosadziwa zinthu

Miy 22:3 Munthu wosadziwa zinthu

WOSAKA MBALAME

, Sl 91:3 mumsampha wa wosaka mbalame

WOSAKHULUPIRIRA

, 1Ak 7:12 mkazi wosakhulupirira

WOSALONGOSOKA

, 1At 5:14 muzichenjeza wosalongosoka

2At 3:6 muzipewa mʼbale wosalongosoka

WOSAMVERA

, Yoh 3:36 Wosamvera Mwanayo

WOSAMVERA MALAMULO

, 2At 2:3 wosamvera malamulo akuonekera

WOSAUGWIRA MTIMA

, Miy 14:29 wosaugwira mtima amasonyeza

WOSAYAMIKA

, Miy 29:21 adzakhala wosayamika

WOWERUZA

, Yes 33:22 Yehova ndi Woweruza wathu

Lu 18:2 woweruza wosaopa Mulungu

WOYAMBA

, Mko 9:35 woyamba ayenera kukhala wotsiriza

WOYAMBA KUBADWA

, Eks 11:5 woyamba kubadwa ku Iguputo adzafa

Akl 1:15 woyamba kubadwa wa chilengedwe

WOYANGʼANIRA

, 1Ti 3:1 akuyesetsa kuti akhale woyangʼanira

1Pe 2:25 mʼbusa ndi woyangʼanira miyoyo

Y

YA

, Eks 15:2 Ya, mphamvu ndi nyonga zanga

Yes 12:2 Ya, ndi mphamvu zanga

YABWINO

, Lu 4:13 mpaka nthawi ina yabwino

YAKA

, Aro 12:11 Yakani ndi mzimu

YAKOBO 1.

, Ge 32:24 kulimbana ndi Yakobo

YAKOBO 2.

, Lu 6:16 Yudasi mwana wa Yakobo

YAKOBO 3.

, Mac 12:2 anapha Yakobo

YAKOBO 4.

, Mko 15:40 Mariya mayi a Yakobo

YAKOBO 5.

, Mt 13:55 azichimwene ake si Yakobo?

Mac 15:13 Atamaliza, Yakobo anayankha

1Ak 15:7 anaonekera kwa Yakobo

Yak 1:1 Yakobo, kapolo wa Mulungu

YAMBA

, Zek 4:10 munayamba kumanga ndi zochepa

YAMBITSA

, Sl 94:20 akuyambitsa mavuto

YAMIKA

, Sl 92:1 Ndi bwino kuyamika inu

Aef 5:20 Nthawi zonse muziyamika Mulungu

YAMIKANI

, Yoh 11:41 Atate, ndikukuyamikani

YAMIKIRA

, Sl 27:4 ndiyangʼane kachisi moyamikira

Sl 95:2 pamaso pake moyamikira

1Ak 11:2 Ndikukuyamikirani, mukundikumbukira

YAMWITSA

, 1At 2:7 mmene mayi woyamwitsa

YANDIKIRA

, Sl 73:28 kuyandikira kwa Mulungu

YANGʼANIRA

, Ge 1:28 Muyangʼanirenso nsomba

Yes 60:17 mtendere kuti ukhale okuyangʼanira

Yoh 17:12 ndinali nawo, ndinkawayangʼanira

Mac 20:28 mzimu wakuikani kuti muziliyangʼanira

Mac 20:28 Muzidziyangʼanira nokha

1Pe 5:2 Monga oyangʼanira, muzigwira ntchito

YANGWIRO

, De 32:4 ntchito yake ndi yangwiro

YANKHA

, Miy 15:1 Kuyankha modekha kumabweza mkwiyo

Miy 15:28 wolungama amaganizira asanayankhe

Miy 18:13 akayankhira nkhani asanaimvetsetse

Yes 65:24 asanandiitane, ine ndidzayankha

Aro 14:12 aliyense wa ife adzayankha

Akl 4:6 mudziwe mmene mungayankhire

YANKHO

, Miy 15:23 amasangalala akapereka yankho

YAPADERA

, 2Ti 3:1 nthawi yapadera ndi yovuta

YEFITA

, Owe 11:30 Yefita analonjeza Yehova

YEHOSAFATI

, 2Mb 20:3 Yehosafati anachita mantha

YEHOVA

, Eks 3:15 Yehova ndi dzina langa

Eks 5:2 Yehova ndani? sindikumudziwa Yehova

Eks 6:3 dzina lakuti Yehova, sindinadzidziwikitse

Eks 20:7 dzina la Yehova molakwika

De 6:5 Muzikonda Yehova ndi mtima wonse

De 7:9 Yehova ndi woona, wokhulupirika

Sl 83:18 dzina lanu ndinu Yehova

Yes 42:8 Dzina langa ndine Yehova

Ho 12:5 Yehova wa magulu ankhondo

Mki 3:6 ndine Yehova, sindisintha

Mko 12:29 Yehova ndi mmodzi

YEMBEKEZA

, Sl 37:7 umuyembekezere moleza mtima

Mik 7:7 Ndidzayembekezera moleza mtima

Aro 8:25 zimene tikuyembekezera

YEMBEKEZERA

, Eks 21:22 avulaza mkazi woyembekezera

Miy 13:12 umayembekezera chikalephereka

Hab 2:3 atachedwa uziwayembekezerabe

Lu 3:15 anthu ankayembekezera Khristu

Lu 21:26 adzakomoka chifukwa choyembekezera

1At 5:3 mkazi woyembekezera

YENDA

, Ge 33:14 kuyenda kwa ziwetozi, anawa

De 8:16 mʼtsogolo zidzakuyendereni bwino

2Mb 16:9 Maso a Yehova akuyendayenda

Sl 1:3 zimene amachita zimamuyendera

Yes 48:17 kuti zinthu zikuyendereni bwino

Yes 53:6 Tonsefe tikungoyendayenda

Mik 6:8 uziyenda modzichepetsa

Yoh 6:19 Yesu akuyenda panyanja

YENERA

, Mt 10:37 ine ndi wosayenera

Lu 15:19 Si inenso woyenera kutchulidwa

Mac 5:41 anawaona kuti ndi oyenera

Mac 13:46 osayenera moyo wosatha

1Ak 9:27 ndisakhale wosayenera

1Ak 11:27 kumwa za mʼkapu mosayenera

1Ak 14:40 zonse zizichitika moyenera

1Ak 15:23 pa nthawi yoyenera

2Ak 3:5 oyenera kugwira ntchitoyi

Ahe 11:38 osayenera kukhala mʼdziko

Chv 4:11 Ndinu woyenera, inu Yehova

YENERERA

, Eks 18:21 usankhepo amuna oyenerera

Eze 21:27 amene ali woyenerera mwalamulo

Mt 10:11 muzifufuza woyenerera

Aga 6:1 amene ndi oyenerera mwauzimu

2Ti 2:2 oyenerera kuphunzitsa ena

YENGA

, Da 11:35 ntchito yoyenga ichitike

Zek 13:9 ndidzawayenga ngati siliva

Mki 3:3 adzakhala ngati woyenga zitsulo

YERA

, Yes 1:18 machimo adzayera kwambiri

Hab 1:13 Maso anu ndi oyera kwambiri

Zef 3:9 chikhale chilankhulo choyera

Mt 5:8 Osangalala ndi oyera mtima

Yoh 15:3 ndinu oyera kale chifukwa cha mawu

Ahe 12:14 Muziyesetsa kukhala oyera

YEREKEZERA

, Yes 46:5 mungandiyerekezere ndi ndani?

Aga 6:4 osati modziyerekezera ndi wina

YEREMIYA

, Yer 38:6 iwo anagwira Yeremiya

YERETSA

, 1Mf 9:3 Ndayeretsa nyumba wamangayi

Sl 51:2 Ndiyeretseni ku tchimo langa

Eze 36:23 Ndidzayeretsadi dzina langa

Da 12:10 Anthu ambiri adzadziyeretsa

Lu 11:2 dzina lanu liyeretsedwe

2Ak 7:1 tidziyeretse, tichotse choipitsa

Chv 7:14 mikanjo yawo nʼkuiyeretsa mʼmagazi

YERUSALEMU

, Yos 18:28 Yebusi, kutanthauza Yerusalemu

Da 9:25 Yerusalemu amangidwenso

Mt 23:37 Yerusalemu, wopha aneneri

Lu 2:41 ankakonda kupita ku Yerusalemu

Lu 21:20 mukadzaona atazungulira Yerusalemu

Lu 21:24 Anthu adzapondaponda Yerusalemu

Mac 5:28 mwadzaza Yerusalemu yense

Mac 15:2 atumwi ndi akulu ku Yerusalemu

Aga 4:26 Yerusalemu wamʼmwamba

Ahe 12:22 mwafika ku Yerusalemu wakumwamba

Chv 3:12 Yerusalemu Watsopano akutsika

Chv 21:2 Yerusalemu Watsopano ngati mkwatibwi

YESA

, Miy 27:21 munthu amayesedwa

Mki 3:10 Ndiyeseni pa nkhani imeneyi

Lu 8:13 nthawi yoyesedwa ikafika

Mac 5:9 kuti muyese mzimu wa Yehova?

1Ak 10:9 Tisamamuyesenso Yehova

Aga 6:4 aliyense ayese zochita zake

1Ti 3:10 ayesedwe ngati ali oyenerera

Yak 1:3 chikhulupiriro pamene mukuyesedwa

YESETSA

, Lu 13:24 Yesetsani kuti mulowe pakhomo

Aro 12:9 nʼkumayesetsa kuchita zabwino

Aro 14:19 tiziyesetsa kukhala mwamtendere

YESU

, Mt 1:21 udzamupatse dzina lakuti Yesu

YEZEBELI

, 1Mf 21:23 Agalu adzamudya Yezebeli

Chv 2:20 ukulekerera Yezebeli

YEZEDWA

, Da 5:27 mwayezedwa pasikelo

YOBU

, Yob 1:9 Kodi Yobu amangoopa Mulungu?

Yak 5:11 Munamva za kupirira kwa Yobu

YOHANE 1.

, Mt 21:25 ubatizo wa Yohane unachokera kuti?

Mko 1:9 Yesu anabatizidwa ndi Yohane

YOHANE 2.

, Yoh 1:42 Simoni mwana wa Yohane

YOHANE 3.

, Mt 4:21 ndi mchimwene wake Yohane

YONA

, Yon 2:1 Yona anapemphera

YONATANI

, 1Sa 18:3 Yonatani ndi Davide anachita pangano

1Sa 23:16 Yonatani anathandiza Davide

YORODANO

, Yos 3:13 madzi a mu Yorodano aima

2Mf 5:10 mukasambe maulendo 7 mu Yorodano

YOSEFE

, Ge 39:23 Yehova anali ndi Yosefe

Lu 4:22 Kodi si mwana wa Yosefe?

YOSIYA

, 2Mf 22:1 Yosiya analamulira zaka 31

YOSWA

, Eks 33:11 Yoswa mwana wa Nuni

YUDA

, Ge 49:10 Ndodo yachifumu sidzachoka kwa Yuda

YUDASI

, Mt 27:3 Yudasi anakabweza ndalama 30

Z

ZABWINO

, Yes 26:10 woipa atachitiridwa zabwino

ZACHABECHABE

, Mla 1:2 zonse nʼzachabechabe

ZAKALE

, Yes 65:17 zakale sizidzakumbukiridwanso

ZAKEYU

, Lu 19:2 munthu wina dzina lake Zakeyu

ZAKUDYA ZABWINO

, Da 1:5 aziwapatsa zakudya zabwino

ZAKUFA

, Akl 3:5 ziwalo za thupi zakufa

ZAMBIRI

, 1Ak 15:58 muzikhala ndi zochita zambiri

ZAMTENGO WAPATALI

, Miy 3:9 zinthu zamtengo wapatali

ZATSOPANO

, Yes 42:9 ndikulengeza zatsopano

Mac 17:21 kumvetsera nkhani zatsopano

Chv 21:5 zimene ndikupanga ndi zatsopano

ZAZIKULU

, Aef 3:20 kuchita zazikulu kwambiri

ZEDEKIYA

, Yer 52:11 inachititsa khungu Zedekiya

ZEKARIYA 1.

, Lu 11:51 magazi a Zekariya

ZEKARIYA 2.

, Eza 5:1 Zekariya mdzukulu wa Ido

ZEKARIYA 3.

, Lu 1:5 wansembe dzina lake Zekariya

ZEMBA

, Yuda 4 alowa mozemba pakati panu

ZENGEREZA

, Yer 48:10 Munthu wozengereza

ZEU

, Mac 14:12 anayamba kumutchula kuti Zeu

ZIDA

, 2Ak 10:4 Zida zomenyera nkhondoyi

Aef 6:13 nyamulani zida zonse

ZIDA ZANKHONDO

, Aef 6:11 Valani zida zankhondo

ZIDZAKUYENDERA

, 1Mf 2:3 zidzakuyendera bwino

ZIKHALE MOMWEMO

, De 27:15 azidzayankha kuti, Zikhale momwemo!

ZIKONDWERERO

, Le 23:4 Zikondwerero za Yehova

ZIKUMBUTSO

, Sl 119:24 Ndimakonda zikumbutso

ZIKUYENDERENI

, 2Mb 20:20 zinthu zikuyendereni bwino

ZILAKOLAKO

, Aro 1:26 zilakolako zosalamulirika

ZILANKHULO

, Zek 8:23 ochokera mʼzilankhulo zonse

Mac 2:4 ankalankhula zilankhulo zosiyanasiyana

ZILIZONSE

, Afi 4:8 zinthu zilizonse zoona,

ZILOMBO

, Le 26:6 Ndidzachotsa zilombo zoopsa

Eze 34:25 ndidzachotsa zilombo zolusa mʼdzikomo

Da 7:3 zilombo 4 zinatuluka mʼnyanjayo

Ho 2:18 pangano ndi zilombo zakutchire

ZIMENE MUNGATHE

, 2Pe 3:14 yesetsani kuchita zimene mungathe

ZINDIKIRA

, 1Mf 8:47 nʼkuzindikira kulakwa kwawo

Sl 119:99 Ndine wozindikira kuposa aphunzitsi

Miy 19:11 Kuzindikira kumabweza mkwiyo

Da 12:3 Anthu ozindikira adzawala

Mt 24:15 wowerenga adzazindikire

ZINTHU

, Yes 61:6 zinthu zochokera kumitundu

1Ak 2:10 mzimu umafufuza zinthu zozama

Aga 6:2 Pitirizani kunyamulirana zinthu zolemera

Aef 1:18 zinthu zabwino zimene walonjeza

ZINYALALA

, 1Ak 4:13 tikuonedwa ngati zinyalala

Afi 3:8 ndimaziona ngati mulu wa zinyalala

ZIPATSO

, Ge 3:3 zipatso za mtengo wapakati

Mt 7:20 mudzawazindikira ndi zipatso

Mt 21:43 mtundu wobereka zipatso

Lu 8:15 nʼkubereka zipatso mopirira

Yoh 15:2 ibereke zipatso zambiri

Yoh 15:8 kubereka zipatso zambiri

ZIPATSO ZOYAMBIRIRA

, Aro 8:23 zipatso zoyambirira zomwe ndi mzimu

ZIPHASO

, Mt 17:25 amalandira ndalama za ziphaso

ZIPILALA

, Aga 2:9 anali ngati zipilala

ZIPINDA

, Yes 26:20 mukalowe mʼzipinda zamkati

ZIPUMI

, Eze 9:4 ulembe chizindikiro pazipumi

ZITSANZO

, 1Ak 10:6 zimenezi ndi zitsanzo kwa ife

ZITSEKO

, Yoh 20:19 anakhoma zitseko

ZIVOMEREZI

, Lu 21:11 Kudzachitika zivomerezi

ZIWALA

, Yes 40:22 ali ngati ziwala

Yow 1:4 zimene ziwala zowononga zinasiya

ZIWALO

, 1Ak 12:18 Mulungu anaika ziwalo za thupi

ZIWANDA

, 1Ak 10:20 amazipereka kwa ziwanda

1Ak 10:21 kudya patebulo la ziwanda

Aef 6:12 tikulimbana ndi ziwanda

Yak 2:19 ziwanda zimakhulupirira, zimanjenjemera

ZIWETO

, Miy 12:10 Wolungama amasamalira ziweto

ZIYONI

, Sl 2:6 mfumu ikulamulira ku Ziyoni

Sl 48:2 Phiri la Ziyoni

Yes 66:8 Ziyoni anabereka ana aamuna

Chv 14:1 ataimirira paphiri la Ziyoni

ZIZIKUYENDERA

, Yos 1:8 Ukamatero, zizikuyendera

ZIZINDIKIRO

, Lu 21:25 padzakhala zizindikiro

2At 2:9 zizindikiro zabodza, zodabwitsa

ZIZINDIKIRO PAKHUNGU

, Le 19:28 musamadzilembe zizindikiro pakhungu

ZOCHITIKA

, 1Ak 7:31 zochitika zapadzikoli zikusintha

ZODALIRIKA

, Sl 19:7 Zikumbutso za Yehova ndi zodalirika

ZOFIIRA

, Ge 25:30 ndigawireko mphodza zofiira

ZOFUFUMITSA

, Mt 13:33 Ufumu uli ngati zofufumitsa

1Ak 5:6 zofufumitsa zapangʼono zimafufumitsa

ZOFUNIKA

, Mt 23:23 zinthu zofunika za mʼChilamulo

Afi 1:10 zinthu zofunikadi kwambiri

ZOIPA

, De 23:13 muzikwirira zoipazo

1At 5:22 Muzipewa zoipa

ZOKONZEDWERATU

, Yes 65:11 mulungu wa Zokonzedweratu

ZOLAKWA

, Sl 40:12 Zolakwa zanga ndi zochuluka

Sl 130:3 mumayangʼanitsitsa zolakwa

Yes 53:5 chifukwa cha zolakwa zathu

Mt 6:12 Mutikhululukire zolakwa zathu

ZOLEMBEDWA

, 1Ak 4:6 Musapitirire zolembedwa

ZOLINGA

, Miy 16:2 Yehova amafufuza zolinga

ZOLUMIKIZANA

, Aef 4:16 ziwalo zolumikizana bwino

ZONYANSA

, Aro 1:24 kuti achite zonyansa

Aro 1:27 amuna okhaokha kuchitirana zonyansa

ZOONA

, Sl 15:2 kulankhula zoona mumtima mwake

Aef 4:25 aliyense wa inu azilankhula zoona

ZOOPSA

, Miy 3:25 Sudzaopa zoopsa zilizonse

ZOPANDA

, Afi 3:7 ndikuziona kuti nʼzopanda phindu

ZOPANDA PAKE

, Mt 15:9 Chilichonse amachita ndi chopanda pake

Lu 24:11 zinkaoneka ngati zopanda pake

ZOPANDA UMBONI

, 1Ti 1:4 nkhani zopanda umboni

ZOPEREKA

, 2Mb 31:10 anabweretsa zopereka

ZOSANGALATSA

, Lu 8:14 zosangalatsa za moyo

ZOSAONEKA

, 2Ak 4:18 zosaoneka, osati zooneka

ZOSATHEKA

, Mt 19:26 Kwa anthu nʼzosatheka

ZOSAYEMBEKEZEREKA

, Mla 9:11 zinthu zosayembekezereka

ZOSOKONEZA

, 1Ak 7:35 popanda zosokoneza

ZOSOWA

, Aro 12:13 mogwirizana ndi zosowa

ZOTOPETSA

, Mki 1:13 Koma ndiye nʼzotopetsa

ZOUNIKIRA

, Afi 2:15 mukuwala ngati zounikira

ZOVALA

, Ge 3:21 anawapangira zovala zazitali

ZOWAKOMERA

, 2Ti 4:3 zowakomera mʼkhutu

ZOZIKIKA

, 2Ak 10:4 zinthu zozikika molimba

ZUNGULIRA

, Yes 40:22 pamwamba pa dziko lozungulira

ZUNGUZA

, Yoh 6:60 Mawu amenewa ndi ozunguza

ZUNZA

, Sl 119:86 akundizunza popanda chifukwa

Yoh 15:20 Ngati anazunza ine

Mac 22:4 Ndinkazunza otsatira Njira

Aro 12:14 muzidalitsa amene akukuzunzani

1Ak 4:12 akamatizunza, timapirira

ZUNZIDWA

, Mt 5:10 azunzidwa chifukwa cha chilungamo

Mt 13:21 kuzunzidwa chifukwa cha mawuwo

Mko 4:17 kuvutitsidwa kapena kuzunzidwa

Mko 10:30 ana ndi minda, adzazunzidwa

2Ak 4:9 Timazunzidwa, Mulungu samatisiya

1Pe 2:19 akuzunzidwa, Mulungu amasangalala naye

ZUNZIKA

, Lu 21:25 anthu a mitundu ina adzazunzika

0-9

10

, Ge 18:32 chifukwa cha 10 amenewo

Chv 5:11 chinali 10 sauzande

12

, Mko 3:14 12, anawapatsa dzina lakuti atumwi

24

, Chv 4:4 mipando yachifumu 24, akulu 24

70

, Sl 90:10 Masiku a moyo amangokwana zaka 70

Da 9:2 Yerusalemu adzakhala bwinja zaka 70

Da 9:24 Pali milungu 70 imene yaikidwa

Lu 10:1 Ambuye anasankha anthu 70 nʼkuwatumiza

77

, Mt 18:22 osati maulendo 7 okha ayi, koma 77

100

, Mt 13:8 inabereka zipatso 100

Mt 18:12 nkhosa 100 ndipo imodzi nʼkusochera

Mko 10:30 kuwirikiza maulendo 100 mʼnthawi ino

300

, Owe 7:7 Ndidzakupulumutsani ndi amuna 300

500

, 1Ak 15:6 anaonekeranso kwa abale oposa 500

666

, Chv 13:18 Nambala yake ndi 666

1,000

, Sl 91:7 Anthu 1,000 adzagwa

Yes 60:22 adzasanduka anthu 1,000

2Pe 3:8 zaka 1,000 zili ngati tsiku limodzi

Chv 20:2 nʼkumumanga kwa zaka 1,000

Chv 20:4 analamulira ndi Khristu kwa zaka 1,000

4,000

, Mko 8:20 mitanda 7 nʼkudyetsa amuna 4,000

5,000

, Mt 14:21 anadya anali amuna 5,000

144,000

, Chv 7:4 anadindidwa chidindo, 144,000

Chv 14:3 144,000 anagulidwa padziko lapansi

185,000

, 2Mf 19:35 mngelo anapha asilikali 185,000