Zatsopano pa JW.ORG
KHALANI MASO
Kodi Anthu Adzasiya Liti Kumenya Nkhondo?—Zimene Baibulo Limanena
Posachedwapa nkhondo zonse zidzathetsedwa. Baibulo limafotokoza mmene zimenezi zidzachitikire.
NKHANI ZINA
Kodi Choonadi Ndi Chofunikabe Masiku Ano?
Baibulo lingakuthandizeni kudziwa choonadi m’dziko lomwe anthu ambiri akumafalitsa mabodza.
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
Muziphunzira Mwakhama Kuti Mukhale Maso
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
Mafunso Ochokera kwa Owerenga—July 2024
Kodi “mkazi” wotchulidwa pa Yesaya 60:1 ndi ndani, nanga ‘anaimirira’ bwanji komanso anaonetsa bwanji “kuwala”?
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
Kodi Mungatani Kuti Muzolowere Mukasamukira Mumpingo Wina?
Akhristu ambiri zimawayendera bwino akasamukira mumpingo watsopano. Kodi n’chiyani chingakuthandizeni ngati mwasamukira mumpingo wina? Onani mfundo 4 zimene zingakuthandizeni kuti muzolowere msanga mpingo watsopanowo.
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
July 2024
M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira September 9–October 6, 2024.
NYIMBO ZA BROADCASTING
“Uthenga Wabwino” (Nyimbo ya Msonkhano wa 2024)
Kuyambira kale mpaka pano, anthu akhala akulalikira za uthenga wabwino mosangalala. Ntchitoyi ndi yaikulu kwambiri. Yesu ndi amene amaitsogolera ndipo angelo amathandiza nawo pa ntchitoyi.
NKHANI ZINA
Muzithandiza Ena Kuti Musamasungulumwe—Kodi Baibulo Limati Chiyani?
Onani njira ziwiri zimene mungachite kuti mupindule pothandiza anthu ena.
NDANDANDA YA UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU