Zatsopano pa JW.ORG

2025-10-27

NDANDANDA YA UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU

March–April 2026

2025-10-24

PHUNZIRANI KUCHOKERA KWA YESU

Padziko Lonse Padzakhala Mtendere

Onani zimene Yesu adzachite pobweretsa mtendere padziko lonse m’tsogolomu komanso mmene zomwe anaphunzitsa zingakuthandizireni kukhala mwamtendere panopa.

2025-10-24

PHUNZIRANI KUCHOKERA KWA YESU

Kuchita Zachiwawa Sikungathetse Mavuto

Onani zimene Yesu anaphunzitsa posonyeza kuti kuchita zachiwawa sikungakhale njira yothetsera mavuto. Zinthu zolimbikitsa mtendere zimene ankaphunzitsa komanso chitsanzo chake zingatithandize kuti tizichita zinthu zoyenera ena akatichitira zachiwawa.

2025-10-23

KODI ZOPEREKA ZANU ZIMAGWIRITSIDWA NTCHITO BWANJI?

Kusamalira Nyumba za Ufumu

Padziko lonse tili ndi Nyumba za Ufumu zoposa 60,000. Kodi timasamalira bwanji nyumbazi?

2025-10-23

MBIRI YA MOYO WANGA

Oleh Radzyminskyi: Kutsekeredwa M’ndende Sikukanatha Kundilekanitsa ndi Yehova

Chikhulupiriro cha Oleh mwa Yehova chinayesedwa pamene anali kusukulu, m’ndende komanso pa nthawi imene ankafunika thandizo lachipatala mwadzidzidzi. Onani mmene Oleh wasonyezera kudalira Yehova pa moyo wake wonse.

2025-10-20

NYIMBO ZA BROADCASTING

Chikondi Chapamwamba

Ndi madalitso otani omwe akukudikirirani mukawonjezera utumiki wanu kwa Yehova?

2025-10-16

NKHANI ZINA

Baibulo Limanena Zimene Zidzachitikire Zipembedzo

Anthu ambiri amakhumudwa ngakhalenso kunyansidwa kumene ndi zimene zipembedzo zimachita. Kodi Mulungu amamva bwanji ndi zimenezi? Onani zimene ulosi wa m’Baibulo unaneneratu.

2025-10-15

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

Mfundo Zothandiza Pophunzira​​—⁠Muziyerekezera Kuti Mukuona Zomwe Zikuchitika Mukamawerenga Nkhani za M’Baibulo

Muziganizira zimene mungachite kuti muziyerekezera kuti mukuona zomwe zikuchitika mukamawerenga nkhani za M’Baibulo.

2025-10-14

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

January 2026

M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira March 2–​April 5, 2026.