Zatsopano pa JW.ORG
NDANDANDA YA UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU
March–April 2026
PHUNZIRANI KUCHOKERA KWA YESU
Padziko Lonse Padzakhala Mtendere
Onani zimene Yesu adzachite pobweretsa mtendere padziko lonse m’tsogolomu komanso mmene zomwe anaphunzitsa zingakuthandizireni kukhala mwamtendere panopa.
PHUNZIRANI KUCHOKERA KWA YESU
Kuchita Zachiwawa Sikungathetse Mavuto
Onani zimene Yesu anaphunzitsa posonyeza kuti kuchita zachiwawa sikungakhale njira yothetsera mavuto. Zinthu zolimbikitsa mtendere zimene ankaphunzitsa komanso chitsanzo chake zingatithandize kuti tizichita zinthu zoyenera ena akatichitira zachiwawa.
KODI ZOPEREKA ZANU ZIMAGWIRITSIDWA NTCHITO BWANJI?
Kusamalira Nyumba za Ufumu
Padziko lonse tili ndi Nyumba za Ufumu zoposa 60,000. Kodi timasamalira bwanji nyumbazi?
MBIRI YA MOYO WANGA
Oleh Radzyminskyi: Kutsekeredwa M’ndende Sikukanatha Kundilekanitsa ndi Yehova
Chikhulupiriro cha Oleh mwa Yehova chinayesedwa pamene anali kusukulu, m’ndende komanso pa nthawi imene ankafunika thandizo lachipatala mwadzidzidzi. Onani mmene Oleh wasonyezera kudalira Yehova pa moyo wake wonse.
NYIMBO ZA BROADCASTING
Chikondi Chapamwamba
Ndi madalitso otani omwe akukudikirirani mukawonjezera utumiki wanu kwa Yehova?
NKHANI ZINA
Baibulo Limanena Zimene Zidzachitikire Zipembedzo
Anthu ambiri amakhumudwa ngakhalenso kunyansidwa kumene ndi zimene zipembedzo zimachita. Kodi Mulungu amamva bwanji ndi zimenezi? Onani zimene ulosi wa m’Baibulo unaneneratu.
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
Mfundo Zothandiza Pophunzira—Muziyerekezera Kuti Mukuona Zomwe Zikuchitika Mukamawerenga Nkhani za M’Baibulo
Muziganizira zimene mungachite kuti muziyerekezera kuti mukuona zomwe zikuchitika mukamawerenga nkhani za M’Baibulo.
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
January 2026
M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira March 2–April 5, 2026.

