Zatsopano pa JW.ORG
PHUNZIRANI KUCHOKERA KWA YESU
“Ufumu Wanga Si Wamʼdzikoli”
Yesu anaphunzitsa kuti Ufumu wa Mulungu ndi umene udzathetse mavuto a m’dzikoli, osati maboma a anthu. Onani mmene chitsanzo chake chimakhudzira Akhristu masiku ano.
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
Mfundo Yothandiza Pophunzira—Muzikonzekera Ndemanga Zolimbikitsa
Onani mfundo 4 zomwe zingakuthandizeni kuti mukonzekere kukapereka ndemanga zolimbikitsa pamisonkhano.
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
Muziyesetsa Kuti Muyambirenso Kugwirizana Mwamsanga
Tikamachita zonse zomwe tingathe kuti tithetse kusamvana, timathandiza kuti mumpingo mukhale mtendere komanso timateteza mgwirizano wa abale ndi alongo.
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
Ken Kiuchi: Yehova Wakhala Akundithandiza Kuti Ndikhale Munthu Wabwino
Ken Kiuchi akufotokoza mmene Yehova wamuthandizira kukhala ndi makhalidwe abwino pa nthawi yomwe ankachita upainiya, kutumikira pa Beteli komanso pamene anatumizidwa kuti azikatumikira ku filudi.
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
July 2026
M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira September 7–October 4, 2026.
NYIMBO ZA BROADCASTING
Mumatambasula Dzanja Lanu
Kodi kupatsa kwa Yehova kukuthandiza bwanji mlongo wachitsikana kukhala wosangalala akagawira ena zinthu?
TIMAPEPALA NDI ZOITANIRA
2026 Convention Invitation
NYIMBO ZA BROADCASTING
Tikusangalala Chifukwa Maso Athu Amaona (Nyimbo ya Msonkhano wa 2026)
Imvani mmene mawu a Yesu amabweretsera chimwemwe chomwe chimatithandiza kuchepetsa nkhawa ndi kulimbitsa chiyembekezo chathu.
KODI ZOPEREKA ZANU ZIMAGWIRITSIDWA NTCHITO BWANJI?
Kusindikiza Mabuku pa Nthawi Imene Zinthu Zathu Zambiri Zikupezeka pa Intaneti
Chifukwa chiyani tikufunika kupitirizabe kupulinta mabuku ndi zinthu zina?

