Zatsopano pa JW.ORG
KHALANI BWENZI LA YEHOVA—ZOCHITA
Ukhoza Kuchita Upainiya
Thandizani ana anu kukhala ndi cholinga chodzachita upainiya
KHALANI BWENZI LA YEHOVA—ZOCHITA
Yehova Ndi Weniweni
Mungathe kuthandiza ana anu kumudziwa bwino Yehova kudzera mu zinthu zimene analenga.
KHALANI BWENZI LA YEHOVA—ZOCHITA
Khalani Ochereza
Phunzirani zimene banja lanu lingachite kuti likhale lochereza.
NKHANI
“Musaope”
NKHANI ZINA
Mmene Baibulo Lingathandizire Anthu Amene Achitiridwa Zauchigawenga
Kodi mukuvutika maganizo chifukwa cha zimene zinakuchitikirani? Taganizirani mfundo 5 izi zomwe zingakuthandizeni kuti musamavutikenso maganizo.
PHUNZIRANI KWA ANZAKE A YEHOVA—ZOCHITA
Mefiboseti
Mungatani kuti muzisangalalabe, anthu ena akakuchitirani zinthu zopanda chilungamo ngati Mefiboseti?
PHUNZIRANI KWA ANZAKE A YEHOVA—ZOCHITA
Eliya
Kodi tikuphunzira chiyani kwa Eliya yemwe anali mnzake wa Yehova?
PHUNZIRANI KWA ANZAKE A YEHOVA—ZOCHITA
Yoswa ndi Kalebe
Kodi mungaphunzire chiyani kwa Yoswa ndi Kalebe omwe anali anzake a Yehova?
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
October 2026
M’magaziniyi muli nkhani zophunzira wiki ya December 7, 2026–January 3, 2027.
NKHANI
“Yehova Amandikhulupirira”
NYIMBO ZA BROADCASTING
Ukhale Mnzanga Mpaka Kalekale
Tingapirire mavuto aliwonse amene tingakumane nawo ngati tingakhale ogwirizana.
NKHANI ZINA
Kodi N’zotheka Kuti Anthu Azipeza Magetsi, Mafuta Komanso Gasi Wokwanira?—Zimene Baibulo Limanena
Dziwani mmene Ufumu wa Mulungu udzathetsere vuto la magetsi, mafuta komanso gasi, lomwe likukulirakulira komanso onani malangizo abwino amene angakuthandizeni kuti musamagwiritse ntchito magetsi komanso mafuta ambiri panopa.
KHALANI MASO
Anthu Padziko Lonse Akuda Nkhawa, Chifukwa Malo Ochezera a pa Intaneti Akusokoneza Ana
Baibulo lingathandize makolo kuti aziteteza ana awo ku mavuto omwe amabwera chifukwa chogwiritsa ntchito malo ochezera a pa intaneti.
NKHANI
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 4 la 2026
Mulipotili, timva zinthu zolimbikitsa zokhudza maulendo ochezera nthambi komanso maulendo aubusa amene anachitika posachedwapa. Timvanso mmene milandu yomwe ikukhudza ufulu wathu wolambira yayendera ku Norway ndi ku Sweden.
KODI ZOPEREKA ZANU ZIMAGWIRITSIDWA NTCHITO BWANJI?
Ntchito Yopereka Thandizo mu 2023—“Timaona Chikondi cha Yehova”
Kodi ndi zinthu zabwino ziti zomwe zachitika chifukwa cha ntchito yopereka chithandizo pa nthawi ya ngozi zadzidzidzi m’chaka cha 2023? Kodi zimenezi zasonyeza bwanji chikondi cha Yehova?
NDANDANDA YA UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU

