Zatsopano pa JW.ORG

2026-07-20

KHALANI BWENZI LA YEHOVA​—ZOCHITA

Ukhoza Kuchita Upainiya

Thandizani ana anu kukhala ndi cholinga chodzachita upainiya

2026-07-20

KHALANI BWENZI LA YEHOVA​—ZOCHITA

Yehova Ndi Weniweni

Mungathe kuthandiza ana anu kumudziwa bwino Yehova kudzera mu zinthu zimene analenga.

2026-07-20

KHALANI BWENZI LA YEHOVA​—ZOCHITA

Khalani Ochereza

Phunzirani zimene banja lanu lingachite kuti likhale lochereza.

2026-07-17

NKHANI

“Musaope”

2026-07-16

NKHANI ZINA

Mmene Baibulo Lingathandizire Anthu Amene Achitiridwa Zauchigawenga

Kodi mukuvutika maganizo chifukwa cha zimene zinakuchitikirani? Taganizirani mfundo 5 izi zomwe zingakuthandizeni kuti musamavutikenso maganizo.

2026-07-16

PHUNZIRANI KWA ANZAKE A YEHOVA—ZOCHITA

Mefiboseti

Mungatani kuti muzisangalalabe, anthu ena akakuchitirani zinthu zopanda chilungamo ngati Mefiboseti?

2026-07-16

PHUNZIRANI KWA ANZAKE A YEHOVA—ZOCHITA

Eliya

Kodi tikuphunzira chiyani kwa Eliya yemwe anali mnzake wa Yehova?

2026-07-16

PHUNZIRANI KWA ANZAKE A YEHOVA—ZOCHITA

Yoswa ndi Kalebe

Kodi mungaphunzire chiyani kwa Yoswa ndi Kalebe omwe anali anzake a Yehova?

2026-07-14

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

October 2026

M’magaziniyi muli nkhani zophunzira wiki ya December 7, 2026–​January 3, 2027.

2026-07-07

NYIMBO ZA BROADCASTING

Ukhale Mnzanga Mpaka Kalekale

Tingapirire mavuto aliwonse amene tingakumane nawo ngati tingakhale ogwirizana.

2026-07-03

NKHANI ZINA

Kodi N’zotheka Kuti Anthu Azipeza Magetsi, Mafuta Komanso Gasi Wokwanira?—Zimene Baibulo Limanena

Dziwani mmene Ufumu wa Mulungu udzathetsere vuto la magetsi, mafuta komanso gasi, lomwe likukulirakulira komanso onani malangizo abwino amene angakuthandizeni kuti musamagwiritse ntchito magetsi komanso mafuta ambiri panopa.

2026-07-03

KHALANI MASO

Anthu Padziko Lonse Akuda Nkhawa, Chifukwa Malo Ochezera a pa Intaneti Akusokoneza Ana

Baibulo lingathandize makolo kuti aziteteza ana awo ku mavuto omwe amabwera chifukwa chogwiritsa ntchito malo ochezera a pa intaneti.

2026-06-30

NKHANI

Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 4 la 2026

Mulipotili, timva zinthu zolimbikitsa zokhudza maulendo ochezera nthambi komanso maulendo aubusa amene anachitika posachedwapa. Timvanso mmene milandu yomwe ikukhudza ufulu wathu wolambira yayendera ku Norway ndi ku Sweden.

2026-06-30

KODI ZOPEREKA ZANU ZIMAGWIRITSIDWA NTCHITO BWANJI?

Ntchito Yopereka Thandizo mu 2023​—“Timaona Chikondi cha Yehova”

Kodi ndi zinthu zabwino ziti zomwe zachitika chifukwa cha ntchito yopereka chithandizo pa nthawi ya ngozi zadzidzidzi m’chaka cha 2023? Kodi zimenezi zasonyeza bwanji chikondi cha Yehova?

2026-06-29

NDANDANDA YA UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU

November–December 2026