Zatsopano pa JW.ORG
NSANJA YA OLONDA
Kodi N’zotheka Kuti Padziko Lonse Pakhale Mtendere?
N’zotsimikizika kuti padziko lonse padzakhala mtendere. Koma njira imene idzathandize kuti zimenezi zitheke yomwe Baibulo limanena, ingakudabwitseni.
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
Zinthu Zochititsa Chidwi za M’Baibulo—Mtengo Umene Umadzuka M’mawa Kwambiri
Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zinthu zochititsa chidwi zokhudza mtengo wa amondi komanso mmene Baibulo limaugwiritsira ntchito.
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
Mageti a Mzinda M’nthawi ya M’Baibulo
Kodi kale pamageti a mzinda pankachitika zotani?
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
Stéphane Landeroin: Mlengi Wanga Wamkulu Anachita Nane Chidwi
Werengani nkhaniyi kuti muone zomwe Stéphane ndi mkazi wake Claudine anaphunzirapo pa zomwe anakumana nazo pa nthawi yomwe ankachita umishonale, utumiki wa pa Beteli komanso utumiki woyang’anira dera.
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
August 2026
M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira October 5–November 1, 2026.

