Zatsopano pa JW.ORG

2026-09-15

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

Mawu a M’Baibulo—“Ngati N’kotheka, . . . Muzikhala Mwamtendere ndi Anthu Onse”

Akhristu enieni amayesetsa kuti azikhala mwamtendere ndi anthu onse, koma nthawi zina zimenezi zimakhala zovuta. N’chifukwa chiyani?

2026-09-15

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

Mfundo Zitatu Zothandiza Kuti Muzipemphera kwa Nthawi Yaitali

How can you pray long enough to express your thoughts and feelings fully to God?

2026-09-15

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

Muzipeza Nthawi Yokhala Panokha

Onani zimene Yesu ankachita kuti azipeza nthawi yokhala payekha komanso chifukwa chake ifenso tiyenera kuchita chimodzimodzi.

2026-09-15

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

Kodi Mukukumbukira?​—December 2026

Kodi mwawerenga mosamala magazini a Nsanja ya Olonda a chaka chino? Taonani ngati mukukumbukira.

2026-09-15

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

December 2026

M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira wiki ya February 1-28, 2027.

2026-09-08

NYIMBO ZA BROADCASTING

Mwa Chikhulupiriro

Banja lina likuona mmene Yehova akuwathandizila kukhalabe ndi chiyembekezo komanso chikhulupiriro champhamvu ngakhale kuti akukhala ku dela komwe ndikosowa mtendere ndi zachuma.

2026-08-31

NYIMBO ZA BROADCASTING

“Kuposa Mpheta Zambiri”

Yehova amaona kuti ndinu ofunika kwambiri ngakhale kuti pena simungadzione choncho. Vidiyo ya nyimboyi ikutikumbutsa kuti ndife ofunika kwambiri kwa Yehova komanso kwa anthu omwe amamukonda.

2026-08-24

PHUNZIRANI KUCHOKERA KWA YESU

Kodi Yesu Ananena Chiyani Zokhudza “Zivomerezi Zamphamvu”?

’Zaka pafupifupi 2, 000 zapitazo, Yesu ananeneratu kuti kudzachitika zivomerezi zamphamvu. Nchifukwa chiyani mawu a Yesu amenewa ali ofunika kwambiri masiku ano?

2026-08-18

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

Mfundo Zothandiza Pophunzira​—Zimene Mungachite Kuti Muzipindula Kwambiri Mukamaonera Mavidiyo

Onani mfundo zimene zingakuthandizeni kuti muzipindula mukamaonera mavidiyo pa jw.org.

2026-08-18

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

Tiziyamikira Kukhala ndi Abale ndi Alongo Osiyanasiyana Mumpingo

Kodi tingatani kuti tiziona zinthu moyenera n’kumayamikira mwayi wokhala ndi abale ndi alongo a makhalidwe osiyanasiyana?

2026-08-18

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

Kodi Asilikali Oteteza Mfumu ankavala zovala zotani?

Onani mmene asilikali apadera ankavalira komanso zimene zinkathandiza kuti anthu awazindikire.

2026-08-18

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

Kodi Tingatani Kuti Tizikhala Okhutira pa Nthawi ya Mavuto Azachuma?

Onani mfundo 4 za m’Baibulo zimene zingakuthandizeni kuti muzikhala okhutira posatengera mmene zinthu zilili pamoyo wanu.

2026-08-18

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

November 2026

M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira wiki ya January 4-31, 2027.