ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA

Mtendere Komanso Moyo Wosangalala

Chichewa
Mtendere Komanso Moyo Wosangalala
https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1011556/univ/art/1011556_univ_sqr_xl.jpg

Mtendere Komanso Moyo Wosangalala

Tikakumana ndi mavuto aakulu tingayambe kuganiza kuti n’zosatheka kukhala osangalala komanso kukhala ndi mtendere wamumtima. Komatu Baibulo lathandiza anthu ambirimbiri kupirira mavuto omwe amakumana nawo tsiku ndi tsiku. Lawathandizanso kuchepetsako nkhawa komanso kuthana ndi mavuto ena ndipo lawathandiza kuona kuti moyo uli ndi cholinga. Inunso Baibulo lingakuthandizeni kuti muzisangalala.

GALAMUKANI!

Mungatani Kuti Muzikhala Wosangalala​—Kukhala Wathanzi Komanso Wopirira

Kodi kuvutika ndi matenda kungachititse munthu kuti asamasangalale?

GALAMUKANI!

Mungatani Kuti Muzikhala Wosangalala​—Kukhala Wathanzi Komanso Wopirira

Kodi kuvutika ndi matenda kungachititse munthu kuti asamasangalale?

Kupirira Mavuto Aakulu

Moyo Wanthanzi

Kukhala Bwino Ndi Anthu

Baibulo Limasintha Anthu

Anthu azikhalidwe zosiyanasiyana asiya makhalidwe awo oipa ndipo ali pa ubwenzi wabwino ndi Mulungu.

Pamene Munthu Amene Mumakonda Amwalira

Kodi mnzanu kapena m’bale wanu anamwalira ndipo mukufunikira kulimbikitsidwa?

Banja Lanu Likhoza Kukhala Losangalala

Mukhoza kukhala ndi banja losangalala mukamatsatira mfundo za m’Baibulo.

Kuphunzira Baibulo ndi Mboni za Yehova

N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kuphunzira Baibulo—Vidiyo Yathunthu

Baibulo likuthandiza anthu ambirimbiri padziko lonse lapansi kupeza mayankho a mafunso ofunika kwambiri. Kodi inunso mungakonde?

Kodi Phunziro la Baibulo Limachitika Bwanji?

A Mboni za Yehova padziko lonse lapansi amadziwika bwino chifukwa cha ntchito yawo yophunzitsa anthu Baibulo kwaulere. Onani mmene amaphunzitsira.

Pemphani Kuti Tidzakuyendereni

Mutha kukhala ndi mwayi wokambirana nkhani inayake ya m’Baibulo kapena kudziwa zambiri zokhudza Mboni za Yehova.