Zochitika pa Moyo wa a Mboni za Yehova

A Mboni za Yehova amayesetsa kulola kuti Baibulo lomwe ndi Mawu a Mulungu lizitsogolera maganizo, zoyankhula ndi zochita zawo. Onani mmene lawathandizira pa moyo wawo komanso pa moyo wa anthu ena.

ZOCHITIKA PA MOYO

Tinasankha Kukhala Moyo Wosalira Zambiri

Nkhani imene inakambidwa kumsonkhano wina inathandiza banja lina la ku Colombia kuti lionenso zinthu zimene linkaika patsogolo.

ZOCHITIKA PA MOYO

Tinasankha Kukhala Moyo Wosalira Zambiri

Nkhani imene inakambidwa kumsonkhano wina inathandiza banja lina la ku Colombia kuti lionenso zinthu zimene linkaika patsogolo.

Baibulo Limasintha Anthu