Zochitika pa Moyo wa a Mboni za Yehova

A Mboni za Yehova amayesetsa kulola kuti Baibulo lomwe ndi Mawu a Mulungu lizitsogolera maganizo, zoyankhula ndi zochita zawo. Onani mmene lawathandizira pa moyo wawo komanso pa moyo wa anthu ena.

ZOCHITIKA PA MOYO

Ankabisa Notsi Pansi pa Mashini Ochapira Zovala

Mayi wina anagwiritsa ntchito njira yatsopano pophunzitsa ana ake aakazi mfundo za m’Baibulo.

ZOCHITIKA PA MOYO

Ankabisa Notsi Pansi pa Mashini Ochapira Zovala

Mayi wina anagwiritsa ntchito njira yatsopano pophunzitsa ana ake aakazi mfundo za m’Baibulo.

Baibulo Limasintha Anthu