Zimene a Mboni za Yehova Amachita

Ntchito Yathu Yofalitsa Mabuku ndi Zinthu Zina

“Wokonzeka Mokwanira Kugwira Ntchito Iliyonse Yabwino”

Baibulo la Dziko Latsopano ndi losavuta kuwerenga komanso linamasulira mawu a chinenero choyambirira molondola. M’Baibuloli muli mapu amitundu yosiyanasiyana, matanthauzo a mawu ena a m’Baibulo ndi zakumapeto.

“Wokonzeka Mokwanira Kugwira Ntchito Iliyonse Yabwino”

Baibulo la Dziko Latsopano ndi losavuta kuwerenga komanso linamasulira mawu a chinenero choyambirira molondola. M’Baibuloli muli mapu amitundu yosiyanasiyana, matanthauzo a mawu ena a m’Baibulo ndi zakumapeto.

Zochitika Zapadera

Anthu Anasangalala Kwambiri Pamsonkhano wa M’chilankhulo cha Chitagalogi ku Rome

Ku Europe kuli a Mboni za Yehova ambiri amene amalankhula Chitagalogi ndipo msonkhano wa masiku atatuwu unali woyamba kuchitika m’chilankhulo chawo.

Anthu Anasangalala Kwambiri Pamsonkhano wa M’chilankhulo cha Chitagalogi ku Rome

Ku Europe kuli a Mboni za Yehova ambiri amene amalankhula Chitagalogi ndipo msonkhano wa masiku atatuwu unali woyamba kuchitika m’chilankhulo chawo.