Zimene a Mboni za Yehova Amachita

Ntchito Yathu Yofalitsa Mabuku ndi Zinthu Zina

Baibulo la Dziko Latsopano Lokonzedwanso Linatulutsidwa M’Chisipanishi

Kodi omasulira Baibulo anakwanitsa bwanji kumasulira Baibulo limene mawu amodzi amatanthauza zinthu zingapo m’madera ena apadziko lapansi?

Baibulo la Dziko Latsopano Lokonzedwanso Linatulutsidwa M’Chisipanishi

Kodi omasulira Baibulo anakwanitsa bwanji kumasulira Baibulo limene mawu amodzi amatanthauza zinthu zingapo m’madera ena apadziko lapansi?

Zochitika Zapadera

Anthu Anasangalala Kwambiri Pamsonkhano wa M’chilankhulo cha Chitagalogi ku Rome

Ku Europe kuli a Mboni za Yehova ambiri amene amalankhula Chitagalogi ndipo msonkhano wa masiku atatuwu unali woyamba kuchitika m’chilankhulo chawo.

Anthu Anasangalala Kwambiri Pamsonkhano wa M’chilankhulo cha Chitagalogi ku Rome

Ku Europe kuli a Mboni za Yehova ambiri amene amalankhula Chitagalogi ndipo msonkhano wa masiku atatuwu unali woyamba kuchitika m’chilankhulo chawo.