Mayiko Amene a Mboni za Yehova Akumangidwa Chifukwa Chotsatira Zimene Amakhulupirira
Mayiko amene a Mboni za Yehova akuikidwa m’ndende, mmene nthawi zina amakumana ndi mavuto aakulu, chifukwa chotsatira zimene amakhulupirira komanso ufulu wawo wachibadwidwe.

