Pitani ku nkhani yake

Mbiri Komanso Baibulo

Baibulo ndi buku lapadera kwambiri tikaganizira zimene zinachitika kuti lisungidwe kwanthawi yaitali, limasuliridwe komanso kufalitsidwa. Zimene akatswiri apeza posachedwapa zikupitirizabe kutsimikizira kuti ndi lolondola. Mosaganizira za chipembedzo chanu, nanunso mungavomereze kuti Baibulo silingafanane ndi buku lina lililonse.

NKHANI ZINA

Kodi Zimene Baibulo Limanena Zokhudza Ukapolo wa Ayuda ku Babulo N’zolondola?

Kodi zimene akatswiri ofufuza anapeza zikugwirizana bwanji ndi zimene Mulungu ananena zokhudza moyo wa Ayuda ali ku ukapolo ku Babulo?

NKHANI ZINA

Kodi Zimene Baibulo Limanena Zokhudza Ukapolo wa Ayuda ku Babulo N’zolondola?

Kodi zimene akatswiri ofufuza anapeza zikugwirizana bwanji ndi zimene Mulungu ananena zokhudza moyo wa Ayuda ali ku ukapolo ku Babulo?

Laibulale

Kodi Baibulo Lili Ndi Uthenga Wotani?

Kodi mfundo yaikulu yomwe imapezeka m’Baibulo ndi iti?