Mbiri Komanso Baibulo
Baibulo ndi buku lapadera kwambiri tikaganizira zimene zinachitika kuti lisungidwe kwanthawi yaitali, limasuliridwe komanso kufalitsidwa. Zimene akatswiri apeza posachedwapa zikupitirizabe kutsimikizira kuti ndi lolondola. Mosaganizira za chipembedzo chanu, nanunso mungavomereze kuti Baibulo silingafanane ndi buku lina lililonse.
MAVIDIYO
Ankalemekeza Kwambiri Baibulo—Kachigawo ka Vidiyo (William Tyndale)
Umboni wakuti ankakonda kwambiri Baibulo umaonekera mu ntchito imene anagwira imene imatithandizabe masiku ano.
MAVIDIYO
Ankalemekeza Kwambiri Baibulo—Kachigawo ka Vidiyo (William Tyndale)
Umboni wakuti ankakonda kwambiri Baibulo umaonekera mu ntchito imene anagwira imene imatithandizabe masiku ano.
Mbiri ya Baibulo
Kumasulira Mabaibulo Osiyanasiyana
Omasulira Baibulo
Zinthu Zakale Zosonyeza Kuti Baibulo Ndi Lolondola
Laibulale
Kodi Baibulo Lili Ndi Uthenga Wotani?
Kodi mfundo yaikulu yomwe imapezeka m’Baibulo ndi iti?