Pitani ku nkhani yake

Zokhudza Mboni za Yehova Padziko Lonse

  • Mayiko amene a Mboni za Yehova amalambira Mulungu​—239

  • Mboni za Yehova padziko lonse​—8,699,048

  • Maphunziro a Baibulo aulere​—5,666,996

  • Anthu amene anapezeka pa mwambo wokumbukira imfa ya Yesu Khristu​—19,721,672

  • Mipingo​—117,960

 

Mboni za Yehova Padziko Lonse

Timapezeka padziko lonse ndipo timachokera m’mitundu komanso zikhalidwe zosiyanasiyana. Mwina mukudziwa kuti timagwira ntchito yolalikira koma timagwiranso ntchito zina zothandiza anthu a m’madera athu.

Onaninso

MABUKU

Lipoti la Chaka Chautumiki cha 2022 la Mboni za Yehova Padziko Lonse

Onani mmene ntchito yolalikira yomwe a Mboni za Yehova amagwira yayendera padziko lonse kuchokera mu September 2021 mpaka mu August 2022.

NSANJA YA OLONDA

Kodi a Mboni za Yehova Mumawadziwa Bwinobwino?

Kodi inuyo mumaona a Mboni ngati mmene anthu ena omwe atchulidwa m’nkhaniyi amaganizira?