Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Zokhudza Mboni za Yehova Padziko Lonse

  • Mayiko amene a Mboni za Yehova amalambira Mulungu​—240

  • Mboni za Yehova padziko lonse​—9,043,460

  • Maphunziro a Baibulo aulere​—7,480,146

  • Anthu amene anapezeka pa mwambo wokumbukira imfa ya Yesu Khristu​—21,119,442

  • Mipingo​—118,767

 

Mboni za Yehova Padziko Lonse

Timapezeka padziko lonse ndipo timachokera m’mitundu komanso zikhalidwe zosiyanasiyana. Mwina mukudziwa kuti timagwira ntchito yolalikira koma timagwiranso ntchito zina zothandiza anthu a m’madera athu.

Onaninso

MABUKU

2024 Lipoti la Chaka cha Utumiki la Mboni za Yehova Padziko Lonse

Onani mmene ntchito yolalikira padziko lonse ya Mboni za Yehova yayendera kuyambira mu September 2023 kukafika mu August 2024.

NSANJA YA OLONDA

Kodi a Mboni za Yehova Mumawadziwa Bwinobwino?

Kodi inuyo mumaona a Mboni ngati mmene anthu ena omwe atchulidwa m’nkhaniyi amaganizira?