Mboni za Yehova Padziko Lonse

Switzerland

  • Mzinda wa Zurich, m’dziko la Switzerland​—Akulalikira uthenga wa m’Baibulo pogwiritsa ntchito tizikwangani ta m’manja

  • Mzinda wa Montreux, m’dziko la Switzerland​—Akugawira kabuku kofotokoza Baibulo pafupi ndi nyumba yakale yotchedwa Château de Chillon

  • Lucerne, Switzerland​—Akuonetsa kavidiyo ka pa jw.org

  • Lavaux region, Switzerland—Kulalikira uthenga wa m’Baibulo

Mfundo Zachidule—Switzerland

  • 9,049,000—Chiwerengero cha anthu
  • 20,352—Chiwerengero cha Mboni za Yehova
  • 244—Mipingo
  • Pa anthu 447 alionse pali wa Mboni za Yehova m’modzi

KALE LATHU

Anapereka Zinthu Zawo Zabwino Kwambiri

Kodi a Mboni za Yehova anathandiza bwanji abale awo a ku Germany nkhondo yachiwiri yapadziko lonse itangotha?

KALE LATHU

Anapereka Zinthu Zawo Zabwino Kwambiri

Kodi a Mboni za Yehova anathandiza bwanji abale awo a ku Germany nkhondo yachiwiri yapadziko lonse itatangotha?