Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Kukhulupirira Mulungu

Chikhulupiriro n’champhamvu kwambiri ndipo chimathandiza munthu kukhala ndi mtendere wam’maganizo panopa komanso chiyembekezo chodalirika cham’tsogolo. Ngati simunakhulupirirepo Mulungu, munasiya kumukhulupirira kapenanso mukufuna kulimbitsa chikhulupiriro chanu, Baibulo lingakuthandizeni.

TSANZIRANI CHIKHULUPIRIRO CHAWO

Mariya—‘Anaganizira Tanthauzo la Mawu Onsewo Mumtima Mwake’

Zimene Mariya anaona ndiponso kumva ali ku Betelehemu zinamuthandiza kukhulupirira kwambiri malonjezo a Yehova.

TSANZIRANI CHIKHULUPIRIRO CHAWO

Mariya—‘Anaganizira Tanthauzo la Mawu Onsewo Mumtima Mwake’

Zimene Mariya anaona ndiponso kumva ali ku Betelehemu zinamuthandiza kukhulupirira kwambiri malonjezo a Yehova.

Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo—Amuna ndi Akazi Otchulidwa M’Baibulo