Kukhulupirira Mulungu

Chikhulupiriro n’champhamvu kwambiri ndipo chimathandiza munthu kukhala ndi mtendere wam’maganizo panopa komanso chiyembekezo chodalirika cham’tsogolo. Ngati simunakhulupirirepo Mulungu, munasiya kumukhulupirira kapenanso mukufuna kulimbitsa chikhulupiriro chanu, Baibulo lingakuthandizeni.

TSANZIRANI CHIKHULUPIRIRO CHAWO

Abele​—“Ngakhale Kuti Anafa, Iye Akulankhulabe”

Kodi tingaphunzirepo chiyani pa nkhani ya Abele, ngakhale kuti Baibulo silifotokoza zambiri zokhudza iyeyo komanso chikhulupiriro chake?

TSANZIRANI CHIKHULUPIRIRO CHAWO

Abele​—“Ngakhale Kuti Anafa, Iye Akulankhulabe”

Kodi tingaphunzirepo chiyani pa nkhani ya Abele, ngakhale kuti Baibulo silifotokoza zambiri zokhudza iyeyo komanso chikhulupiriro chake?

Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo—Amuna ndi Akazi Otchulidwa M’Baibulo