Malo a Nkhani

 

2025-12-31

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 8 la 2025

Mulipotili, tiona mmene mavidiyo a Uthenga Wabwino wa Yesu akuthandizira anthu.

2025-11-14

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 7 la 2025

Mu lipotili, muli zinthu zosangalatsa zomwe zili mu Lipoti la Chaka cha Utumiki cha 2025 ndipo likufotokoza mmene Yehova wadalitsira ntchito yathu padziko lonse.

2025-10-01

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 6 la 2025

Mu lipotili tikambirana za lemba la chaka cha 2026 komanso nyimbo yatsopano.

2025-08-22

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 5 la 2025

Mu lipotili, tiona mfundo za m’Baibulo zomwe zingatithandize kusankha mwanzeru pa nkhani ya maphunziro owonjezera.

2025-07-08

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 4 la 2025

Mu lipotili, tikambirana mfundo za m’Baibulo zomwe zingatithandize kuti tizisankha zinthu mwanzeru pa nkhani ya zizindikiro komanso miyambo.

2025-05-21

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti Lachitatu la Bungwe Lolamulira la 2025

Mu lipoti lino tiona zimene tingachite pokonzekera kuchita zambiri potumikira Yehova m’miyezi ikubwerayi.

A Mboni za Yehova Anamangidwa Chifukwa cha Zimene Amakhulupirira​—Potengera Dera

Madera amene a Mboni za Yehova anamangidwa, ndipo nthawi zina amazunzidwa kwambiri, chifukwa cha zimene amakhulupirira ngakhale kuti umenewu ndi ufulu wawo.