Chichewa
Malo a Nkhani
/assets/ct/e5be1b2cc6/images/syn_placeholder_sqr.png

Malo a Nkhani

 

2026-05-22

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti Lachitatu la Bungwe Lolamulira la 2026

Mulipotili, tiona mmene abale ndi alongo athu ku Russia asonyezera kupirira kungochokera pamene ntchito yathu inaletsedwa m’dzikolo zaka 9 zapitazo. Komanso, tilengeza kutulutsidwa kwa Magawo 4, 5 ndi 6 a vidiyo ya Uthenga Wabwino wa Yesu.

2026-03-23

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti Lachiwiri la Bungwe Lolamulira la 2026

Mulipotili, timveketsa mmene tizionera nkhani yokhudza kugwiritsa ntchito magazi ako omwe posankha thandizo lachipatala komanso popangidwa opaleshoni.

A Mboni za Yehova Anamangidwa Chifukwa cha Zimene Amakhulupirira​​—Potengera Dera

Madera amene a Mboni za Yehova anamangidwa, ndipo nthawi zina amazunzidwa kwambiri, chifukwa cha zimene amakhulupirira ngakhale kuti umenewu ndi ufulu wawo.