Malo a Nkhani
Lipoti Lachitatu la Bungwe Lolamulira la 2026
Mulipotili, tiona mmene abale ndi alongo athu ku Russia asonyezera kupirira kungochokera pamene ntchito yathu inaletsedwa m’dzikolo zaka 9 zapitazo. Komanso, tilengeza kutulutsidwa kwa Magawo 4, 5 ndi 6 a vidiyo ya Uthenga Wabwino wa Yesu.
Lipoti Lachiwiri la Bungwe Lolamulira la 2026
Mulipotili, timveketsa mmene tizionera nkhani yokhudza kugwiritsa ntchito magazi ako omwe posankha thandizo lachipatala komanso popangidwa opaleshoni.
Ikusonyeza 1 - 15 ya 981
A Mboni za Yehova Anamangidwa Chifukwa cha Zimene Amakhulupirira—Potengera Dera
Madera amene a Mboni za Yehova anamangidwa, ndipo nthawi zina amazunzidwa kwambiri, chifukwa cha zimene amakhulupirira ngakhale kuti umenewu ndi ufulu wawo.

