Malo a Nkhani
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 8 la 2025
Mulipotili, tiona mmene mavidiyo a Uthenga Wabwino wa Yesu akuthandizira anthu.
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 7 la 2025
Mu lipotili, muli zinthu zosangalatsa zomwe zili mu Lipoti la Chaka cha Utumiki cha 2025 ndipo likufotokoza mmene Yehova wadalitsira ntchito yathu padziko lonse.
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 6 la 2025
Mu lipotili tikambirana za lemba la chaka cha 2026 komanso nyimbo yatsopano.
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 5 la 2025
Mu lipotili, tiona mfundo za m’Baibulo zomwe zingatithandize kusankha mwanzeru pa nkhani ya maphunziro owonjezera.
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 4 la 2025
Mu lipotili, tikambirana mfundo za m’Baibulo zomwe zingatithandize kuti tizisankha zinthu mwanzeru pa nkhani ya zizindikiro komanso miyambo.
Lipoti Lachitatu la Bungwe Lolamulira la 2025
Mu lipoti lino tiona zimene tingachite pokonzekera kuchita zambiri potumikira Yehova m’miyezi ikubwerayi.
A Mboni za Yehova Anamangidwa Chifukwa cha Zimene Amakhulupirira—Potengera Dera
Madera amene a Mboni za Yehova anamangidwa, ndipo nthawi zina amazunzidwa kwambiri, chifukwa cha zimene amakhulupirira ngakhale kuti umenewu ndi ufulu wawo.

