Chichewa
Nkhani za Padziko Lonse Zokhudza Mboni za Yehova
/assets/ct/fa815d8e9f/images/syn_placeholder_sqr.png

Nkhani za Padziko Lonse

 

2026-06-30

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 4 la 2026

Mulipotili, timva zinthu zolimbikitsa zokhudza maulendo ochezera nthambi komanso maulendo aubusa amene anachitika posachedwapa. Timvanso mmene milandu yomwe ikukhudza ufulu wathu wolambira yayendera ku Norway ndi ku Sweden.

2026-05-22

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti Lachitatu la Bungwe Lolamulira la 2026

Mulipotili, tiona mmene abale ndi alongo athu ku Russia asonyezera kupirira kungochokera pamene ntchito yathu inaletsedwa m’dzikolo zaka 9 zapitazo. Komanso, tilengeza kutulutsidwa kwa Magawo 4, 5 ndi 6 a vidiyo ya Uthenga Wabwino wa Yesu.

2026-03-23

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti Lachiwiri la Bungwe Lolamulira la 2026

Mulipotili, timveketsa mmene tizionera nkhani yokhudza kugwiritsa ntchito magazi ako omwe posankha thandizo lachipatala komanso popangidwa opaleshoni.