Pitani ku nkhani yake

Baibulo Komanso Sayansi

Kodi Baibulo limagwirizana ndi zimene asayansi amaphunzitsa? Kodi Baibulo limanena zolondola pankhani za sayansi? Werengani zimene asayansi amanena komanso zimene chilengedwe chimasonyeza pankhani imeneyi.

NKHANI ZINA

Kodi Moyo Unayamba Bwanji?

Zoona zake n’zakuti pali anthu ambiri ophunzira kuphatikizapo asayansi ena omwe amakayikira zoti zamoyo zinachita kusintha kuchokera ku zinthu zina.

NKHANI ZINA

Kodi Moyo Unayamba Bwanji?

Zoona zake n’zakuti pali anthu ambiri ophunzira kuphatikizapo asayansi ena omwe amakayikira zoti zamoyo zinachita kusintha kuchokera ku zinthu zina.

Kodi Zinangochitika Zokha?

Laibulale

Kodi Zamoyo Zinachita Kulengedwa?

Zimene mumakhulupirira pa nkhani ya mmene moyo unayambira zimakhudza moyo wanu.

Mmene Moyo Unayambira—Mafunso 5 Ofunika Kwambiri

Onani zimene umboni umanena kenako musankhe nokha kukhulupirira kuti zinthu zinachita kulengedwa kapena zinakhalako zokha.

Zachilengedwe Zimatiphunzitsa za Ulemerero wa Mulungu

Tikamachita chidwi ndi zinthu za m’chilengedwechi, timaphunzira za makhalidwe a Mlengi wathu ndipo zimatithandiza kuti tikhale naye paubwenzi.