Baibulo Komanso Sayansi
Kodi Baibulo limagwirizana ndi zimene asayansi amaphunzitsa? Kodi Baibulo limanena zolondola pankhani za sayansi? Werengani zimene asayansi amanena komanso zimene chilengedwe chimasonyeza pankhani imeneyi.
NKHANI ZINA
Kodi Moyo Unayamba Bwanji?
Zoona zake n’zakuti pali anthu ambiri ophunzira kuphatikizapo asayansi ena omwe amakayikira zoti zamoyo zinachita kusintha kuchokera ku zinthu zina.
NKHANI ZINA
Kodi Moyo Unayamba Bwanji?
Zoona zake n’zakuti pali anthu ambiri ophunzira kuphatikizapo asayansi ena omwe amakayikira zoti zamoyo zinachita kusintha kuchokera ku zinthu zina.
Zokhudza Mmene Moyo Unayambira
Kodi Zinangochitika Zokha?
Kodi Zamoyo Zinachita Kusintha Kapena Zinalengedwa?
Umboni Wasayansi Wosonyeza Kuti Baibulo Ndi Lolondola
Laibulale
Kodi Zamoyo Zinachita Kulengedwa?
Zimene mumakhulupirira pa nkhani ya mmene moyo unayambira zimakhudza moyo wanu.
Mmene Moyo Unayambira—Mafunso 5 Ofunika Kwambiri
Onani zimene umboni umanena kenako musankhe nokha kukhulupirira kuti zinthu zinachita kulengedwa kapena zinakhalako zokha.
Zachilengedwe Zimatiphunzitsa za Ulemerero wa Mulungu
Tikamachita chidwi ndi zinthu za m’chilengedwechi, timaphunzira za makhalidwe a Mlengi wathu ndipo zimatithandiza kuti tikhale naye paubwenzi.