ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA

Baibulo Komanso Sayansi

Chichewa
Baibulo Komanso Sayansi
https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1011552/univ/art/1011552_univ_sqr_xl.jpg

Baibulo Komanso Sayansi

Kodi Baibulo limagwirizana ndi zimene asayansi amaphunzitsa? Kodi Baibulo limanena zolondola pankhani za sayansi? Werengani zimene asayansi amanena komanso zimene chilengedwe chimasonyeza pankhani imeneyi.

GALAMUKANI!

Maso a Kangaude

Kodi kangaude ameneyu amatha bwanji kudziwa kutalika kwa mtunda umene akufuna kudumpha? N’chifukwa chiyani akatswiri akufuna kupanga zinthu potengera kangaudeyu?

GALAMUKANI!

Maso a Kangaude

Kodi kangaude ameneyu amatha bwanji kudziwa kutalika kwa mtunda umene akufuna kudumpha? N’chifukwa chiyani akatswiri akufuna kupanga zinthu potengera kangaudeyu?

Kodi Zinangochitika Zokha?

Laibulale

Kodi Zamoyo Zinachita Kulengedwa?

Zimene mumakhulupirira pa nkhani ya mmene moyo unayambira zimakhudza moyo wanu.

Mmene Moyo Unayambira—Mafunso 5 Ofunika Kwambiri

Onani zimene umboni umanena kenako musankhe nokha kukhulupirira kuti zinthu zinachita kulengedwa kapena zinakhalako zokha.

Zachilengedwe Zimatiphunzitsa za Ulemerero wa Mulungu

Tikamachita chidwi ndi zinthu za m’chilengedwechi, timaphunzira za makhalidwe a Mlengi wathu ndipo zimatithandiza kuti tikhale naye paubwenzi.