Baibulo Komanso Sayansi
Kodi Baibulo limagwirizana ndi zimene asayansi amaphunzitsa? Kodi Baibulo limanena zolondola pankhani za sayansi? Werengani zimene asayansi amanena komanso zimene chilengedwe chimasonyeza pankhani imeneyi.
GALAMUKANI!
“Sindimakayikiranso Zoti Mulungu Analenga Zamoyo”
Werengani nkhaniyi kuti mudziwe chifukwa chake wasayansi wina anasintha maganizo pa nkhani yoti asintha maganizo ake pa nkhani yoti zamoyo zinachita kusanduka, zinthu zonse zinachita kulengedwa komanso pa nkhani ya Baibulo.
GALAMUKANI!
“Sindimakayikiranso Zoti Mulungu Analenga Zamoyo”
Werengani nkhaniyi kuti mudziwe chifukwa chake wasayansi wina anasintha maganizo pa nkhani yoti asintha maganizo ake pa nkhani yoti zamoyo zinachita kusanduka, zinthu zonse zinachita kulengedwa komanso pa nkhani ya Baibulo.
Zokhudza Mmene Moyo Unayambira
Kodi Zinangochitika Zokha?
Kodi Zamoyo Zinachita Kusintha Kapena Zinalengedwa?
Umboni Wasayansi Wosonyeza Kuti Baibulo Ndi Lolondola
Laibulale
Kodi Zamoyo Zinachita Kulengedwa?
Zimene mumakhulupirira pa nkhani ya mmene moyo unayambira zimakhudza moyo wanu.
Mmene Moyo Unayambira—Mafunso 5 Ofunika Kwambiri
Onani zimene umboni umanena kenako musankhe nokha kukhulupirira kuti zinthu zinachita kulengedwa kapena zinakhalako zokha.
Zachilengedwe Zimatiphunzitsa za Ulemerero wa Mulungu
Tikamachita chidwi ndi zinthu za m’chilengedwechi, timaphunzira za makhalidwe a Mlengi wathu ndipo zimatithandiza kuti tikhale naye paubwenzi.

