Anthu Okwatirana Komanso Mabanja

Baibulo lomwe ndi buku la anthu onse limapereka malangizo omwe angathandize kuti banja lanu likhale losangalala komanso kuti mulere bwino ana anu. a

a Mu chigawo chino, tasintha maina a anthu ena omwe tawagwira mawu.

ANTHU OKWATIRANA KOMANSO MABANJA

Kodi Mungatani Kuti Mukhale Woleza Mtima?

Anthu awiri opanda ungwiro akakwatirana, amakumana ndi mavuto osiyanasiyana. Kuleza mtima n’kofunika kwambiri kuti banja likhale lolimba.

ANTHU OKWATIRANA KOMANSO MABANJA

Kodi Mungatani Kuti Mukhale Woleza Mtima?

Anthu awiri opanda ungwiro akakwatirana, amakumana ndi mavuto osiyanasiyana. Kuleza mtima n’kofunika kwambiri kuti banja likhale lolimba.

Kulera Ana

Laibulale

Banja Lanu Likhoza Kukhala Losangalala

Mukhoza kukhala ndi banja losangalala mukamatsatira mfundo za m’Baibulo.