Pitani ku nkhani yake

Kugwiritsa Bwino Ntchito Ndalama

Zimene Mungachite Ngati Mukupeza Ndalama Zochepa

Mavuto azachuma akabwera mwadzidzidzi zimadetsa nkhawa, koma mfundo za m’Baibulo zingakuthandizeni kuti muzitha kugwiritsa ntchito ndalama zochepa.

Muzigwiritsa Ntchito Bwino Ndalama

Kodi kukhulupirirana ndiponso kukambirana momasuka n’zothandiza bwanji?

Kodi Baibulo Lingathandize pa Nkhani ya Mavuto Azachuma Ndiponso Ngongole?

Ndalama sizingakuthandizeni kukhala wosangalala koma pali mfundo za m’Baibulo zinayi zimene zingakuthandizeni pa mavuto azachuma.

Kodi Mungatani Kuti Musamawononge Ndalama Zambiri?

Musadikire mpaka ndalama zanu kutha musanayambe kuganizira njira yoyenera yogwiritsira ntchito ndalama. Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zimene mungachite kuti muzigwiritsa ntchito ndalama mosamala.