Mboni za Yehova Padziko Lonse

Kazakhstan

Mfundo Zachidule—Kazakhstan

  • 20,388,000—Chiwerengero cha anthu
  • 17,343—Chiwerengero cha Mboni za Yehova
  • 217—Mipingo
  • Pa anthu 1,185 alionse pali wa Mboni za Yehova m’modzi

GALAMUKANI!

Dziko la Kazakhstan

Kale, anthu a ku Kazakhstan ankakonda kusamukasamuka komanso kukhala m’nyumba zotha kuyenda nazo. Kodi zimene anthuwa amachita masiku ano zikusonyeza bwanji kuti amakondabe chikhalidwe cha makolo awo?