Mfundo Zachidule—Venezuela
- 28,517,000—Chiwerengero cha anthu
- 139,199—Chiwerengero cha Mboni za Yehova
- 1,726—Mipingo
- Pa anthu 206 alionse pali wa Mboni za Yehova m’modzi
KODI ZOPEREKA ZANU ZIMAGWIRITSIDWA NTCHITO BWANJI?
Sitinaiwale Abale ndi Alongo Athu Powathandiza Pangozi Zogwa Mwadzidzidzi mu 2021
M’chaka cha 2021, m’mayiko ena anthu ankafunika kuthandizidwa chifukwa cha mliri wa COVID-19 komanso ngozi zikuluzikulu zam’chilengedwe.
NKHANI
Mmene Zinthu Zilili Panopa ku Venezuela: Ntchito ya a Mboni za Yehova Ikupitabe Patsogolo Ngakhale Kuti Mavuto Sakutha
Ngakhale kuti zinthu zafika poipa, a Mboni za Yehova ku Venezuela akupitiriza kugwira ntchito yolalikira molimba mtima.

