Mfundo Zachidule—Curacao
- 156,000—Chiwerengero cha anthu
- 1,930—Chiwerengero cha Mboni za Yehova
- 24—Mipingo
- Pa anthu 81 alionse pali wa Mboni za Yehova m’modzi


Ku Punda, mu mzinda wa Willemstad m’dziko la Curaçao. Akuonetsa vidiyo yakuti Kodi Phunziro la Baibulo Limachitika Bwanji?
Ku Punda, mu mzinda wa Willemstad m’dziko la Curaçao. Akuwerenga vesi la m’Baibulo lomwe lili m’kabuku kakuti Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale
Ku Punda, mumzinda wa Willemstad m’dziko la Curaçao. Akulalikira uthenga wa m’Baibulo khomo ndi khomo