Anthu Okwatirana Komanso Mabanja

Baibulo lomwe ndi buku la anthu onse limapereka malangizo omwe angathandize kuti banja lanu likhale losangalala komanso kuti mulere bwino ana anu. a

a Mu chigawo chino, tasintha maina a anthu ena omwe tawagwira mawu.

ANTHU OKWATIRANA KOMANSO MABANJA

Kodi Mwana Wanga Akhale ndi Foni?

Dzifunseni mafunso awa kuti mudziwe ngati inuyo ndi mwana wanu muli okonzeka.

ANTHU OKWATIRANA KOMANSO MABANJA

Kodi Mwana Wanga Akhale ndi Foni?

Dzifunseni mafunso awa kuti mudziwe ngati inuyo ndi mwana wanu muli okonzeka.

Kulera Ana

Laibulale

Banja Lanu Likhoza Kukhala Losangalala

Mukhoza kukhala ndi banja losangalala mukamatsatira mfundo za m’Baibulo.