BAIBULO LA DZIKO LATSOPANO LA MALEMBA OPATULIKA (LOKONZEDWANSO MU3 2023)

2 Atesalonika—Zimene Zili Mʼbukuli

Chichewa
2 Atesalonika—Zimene Zili Mʼbukuli
https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1001061100/univ/wpub/1001061100_univ_sqr_xl.jpg
nwt 2 Thessalonians

Kalata Yachiwiri Yopita kwa Atesalonika

Machaputala

1 2 3

Mitu

  • 1

    • Moni (1, 2)

    • Chikhulupiriro cha Atesalonika chinkakulirakulira (3-5)

    • Anthu osamvera adzalandira chilango (6-10)

    • Ankapempherera mpingo (11, 12)

  • 2

    • Munthu wosamvera malamulo (1-12)

    • Anawalimbikitsa kuti akhale olimba (13-17)

  • 3

    • Pitirizani kupemphera (1-5)

    • Anawachenjeza kuti apewe makhalidwe osalongosoka (6-15)

    • Moni womaliza (16-18)