Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

June 27–July 3

MASALIMO 52-59

June 27–July 3
  • Nyimbo Na. 38 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Gawirani kapepala kamodzi. Mufotokozereni za kachidindo kamene kali patsamba lomaliza.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) Chitani chitsanzo chosonyeza ulendo wobwereza kwa munthu amene analandira kapepala.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) fg phunziro 3 ndime 2-3—Pomaliza mufotokozereni za vidiyo ya pa jw.org yakuti, Kodi Tingadziwe Bwanji Kuti Baibulo Limanena Zoona?

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 56

  • Zofunika pampingo: (7 min.)

  • Mulungu Ndiye Mthandizi Wanga”: (8 min.) Nkhani yokambirana. Onetsetsani kuti mafunso a m’nkhaniyi ayankhidwa ndi anthu ochuluka n’cholinga choti aliyense apindule ndi zimene abale ndi alongo awo anakumana nazo. (Aroma 1:12) Limbikitsani ofalitsa kuti azigwiritsa ntchito Buku Lofufuzira Nkhani pofuna kupeza mfundo za m’Mawu a Mulungu akakumana ndi mavuto.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) ia mutu 1 ndime 1-13

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 121 ndi Pemphero