Nkhani Zomwe Zangoikidwa Kumene Patsamba Loyamba la Webusaiti Yathu
Kodi Mungadziwe Bwanji Choyenera ndi Chosayenera?
Kodi mungasankhe bwanji? Nanga malangizo odalirika okuthandizani kusankha moyenera mungawapeze kuti?
Kodi Kusuta Ndi Tchimo?
Popeza kuti m’Baibulo mulibemo nkhani yokhudza kusuta, ndiye zingatheke bwanji kuti liyankhe funso limeneli?
Kufufuza Choonadi
Baibulo limatiuza mayankho olondola a mafunso ofunika kwambiri okhudza moyo.
Baibulo Lomwe Linasowa Lapezekanso
Onerani nkhani yochititsa chidwi yosonyeza mmene Baibulo lina linasowera n’kupezekanso patadutsa zaka 200.
Musamangotengera Zochita za Anzanu
Zinthu 4 zimene zingakuthandizeni kuti muzisankha nokha zochita mwanzeru.
Kodi Mulungu Amaganizira Akazi?
Yankho la funso limeneli lingakuthandizeni kupeza mtendere pamene mukuchitiridwa nkhanza kapena zinthu zina zopanda chilungamo chifukwa choti ndi mkazi.
Kodi M’Baibulo Mungapezemo Mawu Omwe Angakulimbikitseni?
Mawu a m’Baibulo alimbikitsa anthu ambiri omwe akulimbana ndi mavuto ena ake komanso omwe amavutika maganizo chifukwa cha mavuto.
N’chifukwa Chiyani Mulungu Amalola Kuti Anthu Azivutika?
Anthu ambiri amafuna kudziwa kuti n’chifukwa chiyani padzikoli pali mavuto ambiri. Baibulo limapereka yankho logwira mtima pa nkhaniyi.
Kodi Anthu Adzasiya Liti Kumenya Nkhondo?—Zimene Baibulo Limanena
Posachedwapa nkhondo zonse zidzathetsedwa. Baibulo limafotokoza mmene zimenezi zidzachitikire.
Muzithandiza Ena Polimbana Ndi Maganizo Odziona Kuti Muli Nokhanokha
Malangizo ochokera m’Baibulo angakuthandizeni.
Samalani Kuti Musamapusitsike Ndi Nkhani Zabodza
Nkhani zosocheretsa, malipoti abodza ndi mphekesera zafala kwambiri ndipo zingakubweretsereni mavuto.
Kodi Mawu oti “Msamariya Wachifundo” Amatanthauza Chiyani?
Werengani kuti mudziwe kumene mawu odziwikawa anachokera komanso tanthauzo lake.
Kodi Baibulo Limati Chiyani pa Nkhani ya Isitala?
Werengani kuti mudziwe mmene miyambo 5 imene imachitika pa Isitala inayambira.
Zimene Tingachite Kuti Nsembe ya Yesu Izitithandiza
Onani zinthu ziwiri zofunika kwambiri zimene mungachite.
Yesu Adzathetsa Zoipa Zonse
Kodi tingasonyeze bwanji kuti timayamikira zimene Yesu watichitira kale komanso zimene adzatichitire?
N’chiyani Chingakuthandizeni Kumvetsa Baibulo?
Kaya ndife anthu otani, tikhoza kumvetsa uthenga wa Mulungu umene uli m’Malemba Opatulika.
Mungakhale ndi Moyo Wosangalala
Magaziniyi ya Galamukani! Ikufotokoza mmene malangizo anzeru a m’Baibulo angakuthandizireni.
N’chiyani Chingakuthandizeni Kukhala Ndi Tsogolo Labwino?
Kodi ndi maphunziro, ndalama kapena zinthu zina? Werengani magazini ya Nsanja ya Olonda ino kuti mudziwe zambiri.