Nkhani Zomwe Zangoikidwa Kumene Patsamba Loyamba la Webusaiti Yathu
Kugwirizana ndi Anthu Ena
Mfundo za m’Baibulozi zingakuthandizeni kukhala mwamtendere ndi anthu ena.
Ndi Ndani Angateteze Anthu Wamba Pankhondo?—Kodi Baibulo Limanena Zotani?
Baibulo linaneneratu kuti Mulungu ‘adzathetsa nkhondo padziko lonse lapansi.’ Kodi adzachita zimenezi motani?
Amachita Zinthu Bwinobwino Ngakhale Kuti Ndi Osaona
Munthu akasiya kuona, ubongo wake umasintha n’kuyamba kugwiritsa ntchito ziwalo zina. Anthu osaona amadalira kwambiri kumva mawu, fungo komanso amadalira manja ndi zala zawo kuti adziwe zinthu
Kodi Mulungu Amaona Bwanji Uchigawenga?
Kodi adzauthetsa?
Kodi Baibulo Limanena Zotani pa Nkhani ya Kuyamikira?
Kukhala ndi mtima woyamikira ndi kothandiza kwambiri. Kodi kungakuthandizeni bwanji ndipo mungatani kuti mukhale ndi mtima woyamikira?
Kodi Dzikoli Lidzakhalanso Bwino?
Onani mmene magazini ya Galamukani! imeneyi ingatithandizire kukhala ndi chiyembekezo.
Kodi N’chiyani Chidzachitike pa Nthawi ya “Mapeto”?
Baibulo limafotokoza momveka bwino zimene zidzachitike pa mapeto komanso zimene sizidzachitike.
Matenda Amaganizo
Malangizo ochokera m’Baibulo angakuthandizeni. Dziwani zambiri powerenga magazini ya Nsanja ya Olonda imeneyi.
Kodi Muli Ndi Mtima Watsankho?
Kodi ndi zinthu ziti zomwe zingasonyeze kuti ndife atsankho?
Mayankho a Mafunso 5 Okhudza Kuvutika
Kuphunzira Baibulo kungakutonthozeni pamene mwakumana ndi mavuto.
Mungatani Kuti Muchepetse Nkhawa
Masiku ano anthu ambiri amavutika ndi nkhawa. Komabe pali zimene mungachite kuti musamakhale ndi nkhawa kwambiri.
Mungakhale ndi Moyo Wosangalala
Magaziniyi ya Galamukani! Ikufotokoza mmene malangizo anzeru a m’Baibulo angakuthandizireni.
Kodi Mukuona Kuti Palibenso Chifukwa Chokhalira ndi Moyo?
Kodi mavuto aakulu amene mwakumana nawo akukuchititsani kuganiza kuti palibenso chifukwa chokhalira ndi moyo?
Kodi Baibulo Lingandithandize Ngati Ndili ndi Maganizo Ofuna Kudzipha?
Kodi Baibulo limapereka malangizo otani kwa munthu amene akufuna kudzipha?