Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

March 27–April 2

YEREMIYA 12-16

March 27–April 2
  • Nyimbo Na. 135 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • Aisiraeli Anaiwala Yehova”: (10 min.)

    • Yer. 13:1-5—Yeremiya anamvera malangizo a Mulungu oti akabise lamba ngakhale kuti zinali zovuta (jr 51 ¶17)

    • Yer. 13:6, 7—Yeremiya atayenda ulendo wautali kuti akatenge lamba uja, anapeza kuti anali atawonongeka (jr 52 ¶18)

    • Yer. 13:8-11—Yehova anasonyeza kuti ubwenzi wolimba umene anali nawo ndi Aisiraeli udzawonongeka, kapena kuti kusokonekera, chifukwa chakuti iwo anali anthu osamva (jr 52 ¶19-20; it-1-E 1121 ¶2)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Yer. 12:1, 2, 14—Kodi Yeremiya anafunsa funso lotani ndipo Yehova anamuyankha bwanji? (jr 118 ¶11)

    • Yer. 15:17—Kodi Yeremiya ankaona bwanji nkhani yosankha anthu ocheza nawo, nanga tingamutsanzire bwanji? (w04 5/1 11 ¶16)

    • Kodi ndaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo ziti zimene ndaphunzira pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno zimene ndingazigwiritse ntchito mu utumiki?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Yer. 13:15-27

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Kapepala koitanira anthu ku Chikumbutso komanso vidiyo—Muuzeni zimene mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) Kapepala koitanira anthu ku Chikumbutso komanso video—Muuzeni zimene mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Nkhani: (6 min.) w16.03 29-31—Mutu: Kodi Anthu a Mulungu Analowa Liti mu Ukapolo wa M’Babulo Wamkulu?

MOYO WATHU WACHIKHRISTU