Loweruka
“Kudzipereka kwanga panyumba yanu kudzakhala ngati moto umene ukuyaka mumtima mwanga”—Yohane 2:17
M’mawa
-
8:20 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo
-
8:30 Nyimbo Na. 93 Komanso Pemphero
-
8:40 “Kodi Mukufunafuna Chiyani?” (Yohane 1:38)
-
8:50 VIDIYO:
Uthenga Wabwino wa Yesu: Gawo 2
“Uyu ndi Mwana Wanga”—Mbali Yachiwiri (Yohane 1:19–2:25)
-
9:20 Nyimbo Na. 54 Komanso Zilengezo
-
9:30 NKHANI YOSIYIRANA: Muzitsanzira Anthu Amene Ankakonda Kulambira Koyera
-
• Yohane M’batizi (Mateyu 11:7-10)
-
• Andireya (Yohane 1:35-42)
-
• Petulo (Luka 5:4-11)
-
• Yohane (Mateyu 20:20, 21)
-
• Yakobo (Maliko 3:17)
-
• Filipo (Yohane 1:43)
-
• Natanayeli (Yohane 1:45-47)
-
-
10:35 NKHANI YA UBATIZO: N’chifukwa Chiyani Mukubatizidwa? (Malaki 3:17; Machitidwe 19:4; 1 Akorinto 10:1, 2)
-
11:05 Nyimbo Na. 52 Komanso Kupuma
Masana
-
12:35 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo
-
12:45 Nyimbo Na. 36
-
12:50 NKHANI YOSIYIRANA: Mmene Tingagwiritsire Ntchito Zomwe Tikuphunzira pa Chozizwitsa Choyambirira cha Yesu
-
• Kusonyeza Chifundo (Agalatiya 6:10; 1 Yohane 3:17)
-
• Kukhala Odzichepetsa (Mateyu 6:2-4; 1 Petulo 5:5)
-
• Kukhala Opatsa (Deuteronomo 15:7, 8; Luka 6:38)
-
-
1:20 Kodi “Mwanawankhosa wa Mulungu” Akuchotsa Bwanji Uchimo? (Yohane 1:29; 3:14-16)
-
1:45 NKHANI YOSIYIRANA: Kukwaniritsidwa kwa Maulosi Onena za Mesiya—Mbali Yachiwiri
-
• Anadzipereka Kwambiri pa Nyumba ya Yehova (Salimo 69:9; Yohane 2:13-17)
-
• Analengeza “Uthenga Wabwino kwa Anthu Ofatsa” (Yesaya 61:1, 2)
-
• Anaonetsa “Kuwala Kwakukulu” ku Galileya (Yesaya 9:1, 2)
-
-
2:20 Nyimbo Na. 117 Komanso Zilengezo
-
2:30 “Chotsani Izi Muno” (Yohane 2:13-16)
-
3:00 “Ine Ndidzamumanga” (Yohane 2:18-22)
-
3:35 Nyimbo Na. 75 Komanso Pemphero Lomaliza

