NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA) October 2015
Magaziniyi ili ndi nkhani zophunzira kuyambira pa November 30 mpaka December 27, 2015.
Tizilemekeza Kwambiri Abale Ngati Amenewa
Kodi ndi abale ati amene amathandiza m’makomiti a Bungwe Lolamulira? Kodi abalewa amachita chiyani?
Kodi Mumaona Dzanja la Mulungu Likukuthandizani?
Kodi Baibulo limatanthauza chiyani likamanena za “dzanja” la Mulungu?
“Tiwonjezereni Chikhulupiriro”
Kodi n’zotheka kukhala ndi chikhulupiriro patokha?
MBIRI YA MOYO WANGA
Sananong’oneze Bondo ndi Zimene Anasankha Ali Mnyamata
Nikolai Dubovinsky anatumikira Yehova mokhulupirika pa nthawi imene ntchito ya Mboni za Yehova inali yoletsedwa ku Soviet Union ndipo ankagwira ntchito yovuta kuposa kukhala kundende.
Tisalole Chilichonse Kutisokoneza Potumikira Yehova
Pafupifupi zaka 60 zapitazo, Nsanja ya Olonda inafotokoza mfundo inayake imene ikukwaniritsidwa masiku ano.
Tiziganizira Kwambiri za Yehova
Kodi mungaganizirebe Mawu a Mulungu ngati mwaletsedwa kukhala ndi Baibulo?
MBIRI YA MOYO WANGA
Kuyandikira kwa Mulungu Ndi Kwabwino
Sarah Maiga anasiya kukula ali ndi zaka 9 koma akutumikira Yehova mwakhama.
‘Munthu Wosadziwa Zinthu Amakhulupirira Mawu Alionse’
Kodi tingadziwe bwanji ngati uthenga umene talandira ndi woona kapena ayi?

