Pitani ku nkhani yake

Mavidiyo Amakatuni Omwe Ana Akuwakonda Kwambiri

Mavidiyo Amakatuni Omwe Ana Akuwakonda Kwambiri

A Mboni za Yehova amapanga mavidiyo amakatuni pofuna kuphunzitsa ana mmene angagwiritsire ntchito mfundo za m’Baibulo. Kodi mavidiyowa amawapanga bwanji? Nanga kodi ana amasangalala akamaonera mavidiyowa? Onerani vidiyoyi kuti mudziwe.

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

NTCHITO YOFALITSA MABUKU

Mavidiyo Amene Amasangalatsa Mitima Yathu

A Mboni za Yehova amatulutsa mavidiyo a makatuni amene amaphunzitsa ana makhalidwe abwino komanso mfundo za m’Baibulo. Kodi mavidiyowa akhudza bwanji anthu?

MAVIDIYO

Phunzirani kwa Anzake a Yehova

Phunzirani zambiri kuchokera kwa anthu otchulidwa m’Baibulo omwe anakhala mabwenzi a Yehova!

ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA

Zoti Ana Achite

Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.