Phunzirani kwa Anzake a Yehova

Phunzirani zambiri kuchokera kwa anthu otchulidwa m’Baibulo omwe anakhala mabwenzi a Yehova!

Eliya

Pa nthawi ina, Eliya ankaona kuti wangotsala yekha amene akuchita zinthu zabwino. Kodi Yehova anamuthandiza bwanji?

Yoswa ndi Kalebe

N’chifukwa chiyani Yoswa ndi Kalebe analimba mtima, pamene ena analephera kulimba mtima?

Abigayeli

Kodi Abigayeli anathandiza bwanji mnzake kuti apewe zoipa n’kuchita zabwino?

Abele

Kodi mungaphunzire chiyani kwa Abele pa nkhani yolimbitsa chikhulupiriro chanu?

Hananiya, Misayeli, ndi Azariya

Kodi ungamvere Yehova mofanana ndi anzake aja​—Hananiya, Misayeli, ndi Azariya?

Pepani, palibe mawu ofanana ndi omwe mwasankha.