MALO A NKHANI

Mozambique

Chichewa
Mozambique
/assets/ct/fa815d8e9f/images/syn_placeholder_sqr.png

Mozambique

 

2015-05-10

MOZAMBIQUE

A Mboni za Yehova Anathandiza Anthu Okhudzidwa ndi Kusefukira kwa Madzi ku Mozambique

A Mboni za Yehova akupitiriza kupereka zinthu zofunika kwa anthu okhudzidwa ndi kusefukira kwa madzi m’chigawo chakumpoto ndi chapakati m’dziko la Mozambique. Kuwonjezera pamenepa, akuwalimbikitsanso pogwiritsa ntchito mfundo za m’Baibulo.