Mozambique
A Mboni za Yehova Anathandiza Anthu Okhudzidwa ndi Kusefukira kwa Madzi ku Mozambique
A Mboni za Yehova akupitiriza kupereka zinthu zofunika kwa anthu okhudzidwa ndi kusefukira kwa madzi m’chigawo chakumpoto ndi chapakati m’dziko la Mozambique. Kuwonjezera pamenepa, akuwalimbikitsanso pogwiritsa ntchito mfundo za m’Baibulo.