Pitani ku nkhani yake

Phunziro 2: Muzimvera Yehova

Phunziro 2: Muzimvera Yehova

Kodi matoyi amene timaseweretsa angakhale ndi vuto. Dziwani yankho la funsoli limodzi ndi Kalebe amene akufuna kukhala bwenzi la Yehova.

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

MAVIDIYO

Phunzirani kwa Anzake a Yehova

Phunzirani zambiri kuchokera kwa anthu otchulidwa m’Baibulo omwe anakhala mabwenzi a Yehova!

ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA

Zoti Ana Achite

Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.