Pitani ku nkhani yake

KODI BAIBULO LIMAPHUNZITSA CHIYANI KWENIKWENI? (ZOKUTHANDIZANI POPHUNZIRA)

Yesetsani Kuti Muzilambira Mulungu M’njira Yovomerezeka (Gawo 1)

Zokuthandizani pophunzirazi zachokera m’mutu 16 wa buku lakuti Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni?

Kodi Mulungu amavomereza kugwiritsa ntchito zifaniziro pomulambira? Nanga bwanji kukondwerera masiku obadwa komanso maholide achipembedzo? Onani zimene Baibulo limanena.