Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Zimene Zili M’magaziniyi: Baibulo Lingakuthandizeni Kukhala ndi Moyo Wabwino Kwambiri

Zimene Zili M’magaziniyi: Baibulo Lingakuthandizeni Kukhala ndi Moyo Wabwino Kwambiri

Buku Lakale Lokhala ndi Mfundo Zothandiza Masiku Ano

Baibulo ndi buku lofunika kwambiri pa nkhani zachipembedzo. Lilinso ndi malangizo othandiza pa mbali zonse za moyo wathu monga:

  • Kukhala ndi moyo wathanzi

  • Kukhala ndi mtendere wa m’maganizo

  • Kukhala ndi banja labwino komanso mabwenzi abwino

  • Kugwiritsa ntchito bwino ndalama

  • Kukhala pa ubwenzi ndi Mulungu

Buku Lothandiza Kuposa Lililonse

Kwa zaka zambiri, Baibulo lakhala likuthandiza anthu kukhala ndi moyo wabwino. Panopa, Baibulo likupezeka m’zinenero zambiri. Werengani magaziniyi kuti muone mmene Baibulo lingakuthandizireni.