MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Ndandanda ya Upainiya Wokhazikika
Kuti munthu akwanitse kuchita upainiya wokhazikika amafunika kugawa bwino nthawi yake. Ngati mutamalalikira maola 18 pa mlungu, ndiye kuti mukhoza kupeza nthawi ina yochita zinthu zina komanso kupuma. Kuwonjezera pamenepa, simungavutike kukwanitsa maola ngati mutadwala mwadzidzidzi kapena ngati nyengo sili bwino. Ndandanda imene ili m’munsiyi ingakuthandizeni kugawa bwino nthawi yanu ngati mumagwira ntchito yaganyu, ntchito yolembedwa kapena ngati mumadwaladwala. Komanso ngati mutasintha zina ndi zina m’banja lanu, munthu mmodzi kapena angapo akhoza kuyamba upainiya mwezi wa September. Bwanji osakambirana zimenezi pa kulambira kwanu kwa pabanja kwa mlungu wotsatira?
Lolemba |
NTCHITO |
Lachiwiri |
NTCHITO |
Lachitatu |
NTCHITO |
Lachinayi |
Maola 6 |
Lachisanu |
Maola 6 |
Loweruka |
Maola 4 |
Lamlungu |
Maola 2 |
Lolemba |
Maola Awiri |
Lachiwiri |
Maola Awiri |
Lachitatu |
MISONKHANO YA MKATI MWA MLUNGU |
Lachinayi |
Maola Awiri |
Lachisanu |
Maola Awiri |
Loweruka |
Maola 6 |
Lamlungu |
Maola 4 |
Lolemba |
KUPUMA |
Lachiwiri |
Maola 3 |
Lachitatu |
Maola 3 |
Lachinayi |
Maola 3 |
Lachisanu |
Maola 3 |
Loweruka |
Maola 3 |
Lamlungu |
Maola 3 |