Pitani ku nkhani yake

Zoti Muchite Pophunzira Baibulo

Mulungu Anachiritsa Hezekiya

Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zozizwitsa zimene Mulungu anachita poyankha pemphero la Hezekiya. Koperani nkhani ya m’Baibuloyi, iwerengeni, ndipo muiganizire mozama n’kuona mmene ingakuthandizireni.