South Korea
Zokhudza Misonkhano ya Mayiko: A Mboni Anatulutsa Baibulo pa Bwalo la Masewera a Mpira wa Padziko Lonse ku Seoul
A Mboni za Yehova anatulutsa Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika pa Msonkhano wa Mayiko wa mutu wakuti, “Pitirizani Kufunafuna Ufumu wa Mulungu Choyamba.”
Oweruza Milandu Akuvutika Maganizo Poweruza Anthu Okana Kulowa Usilikali Chifukwa cha Zimene Amakhulupirira
Oweruza milandu a ku South Korea akuvutika maganizo chifukwa akukakamizika kuweruza mopanda chilungamo anthu amene akukana kulowa usilikali chifukwa cha zimene amakhulupirira, m’malo molemekeza ufulu wawo wachibadwidwe.
Kafukufuku Wasonyeza Kuti Anthu a ku South Korea Akufuna Kuti Anthu Okana Kulowa Usilikali Azipatsidwa Ntchito Zina
Anthu ambiri ku Korea akufuna kuti anthu amene amakana kulowa usilikali chifukwa cha zimene amakhulupirira azipatsidwa ntchito zina.
Dziko la South Korea Lasiya Kuphatikiza Anthu Omangidwa pa Nkhani Zokhudza Chikumbumtima Chawo ndi Akaidi Ena Onse
Dziko la South Korea lachepetsako mavuto a anthu ambirimbiri a Mboni za Yehova amene ali kundende chifukwa chokana kulowa usilikali potsatira zimene amakhulupirira.
Mayiko ndi Mabungwe Akudzudzula Dziko la South Korea Chifukwa cha Zinthu Zopanda Chilungamo Zimene Likuchita
Kabuku katsopano kofalitsidwa ndi Mboni za Yehova kanafotokoza zokhudza anthu ambirimbiri amene amamangidwa chifukwa chokana kulowa usilikali potengera zimene amakhulupira.