Peru
Ofesi ya Kazembe wa ku Thailand “Inayamikira Komanso Kupereka Ulemu” kwa a Mboni za Yehova ku Peru Chifukwa Chothandiza Akaidi a ku Thailand
Oimira Ofesi ya Kazembe wa dziko la Thailand anakayendera a Mboni za Yehova ku Peru kuti akawayamikire chifukwa cha ntchito yawo komanso zimene anachitira akaidi a ku Thailand.