“Aliyense wa inu azikonda mkazi wake ngati mmene amadzikondera yekha komanso mkazi azilemekeza kwambiri mwamuna wake.”—Aefeso 5:33.
Baibulo limanena kuti
-
Anthu okwatirana azikhala okhulupirika m’banja.—Mateyu 19:4-6.
-
Ana amene amalemekeza komanso kumvera makolo awo, zinthu zimawayendera bwino.—Aefeso 6:1-3.
Kuti mudziwe zambiri, pitani pa jw.org.

