Yehova Anapereka Cholowa kwa Anthu Omwe Sankamulambira
Ngati Yehova anapereka mphoto kwa anthu omwe sankamulambira chifukwa cha ntchito imene anagwira, ndiye kuli bwanji kwa atumiki ake okhulupirika?
ZIMENE ABABULO ANACHITA
Anagonjetsa mzinda wa Turo
ZIMENE INEYO NDIKUCHITA
Kodi ndikuchita zotani pankhondo yanga yauzimu?
MMENE ABABULO ANADZIPEREKERA
-
Anazinga mzinda wa Turo kwa zaka 13
-
Asilikali a Babulo ankasowa zinthu zina pamoyo wawo
-
Ababulo sanapatsidwe malipiro aliwonse
MMENE NDIKUDZIPEREKERA
Kodi ndimachita zotani potumikira Yehova?
KODI YEHOVA ANAWAPATSA CHIYANI ABABULO?
Yehova anawapatsa dziko la Iguputo kuti alande chuma chake
MADALITSO AMENE YEHOVA WANDIPATSA
Kodi Yehova wandipatsa madalitso otani?