JW LIBRARY
Zinthu Zopezeka pa JW Library
Zinthu Zopezeka M’Baibulo
Sankhani Baibulo lomwe mukufuna kugwiritsa ntchito pa Mabaibulo 6 omwe alipo.
Yerekezani zimene Mabaibulo osiyanasiyana amanena podina nambala ya vesilo.
Onani mawu ogwirizana ndi vesilo podina chizindikiro cha mawu a m’musi kapena cha lifalensi.
Mmene Mungawerengere
Ngati mukugwiritsa ntchito tabuleti kapena chipangizo chilichonse cha m’manja, yendetsani ndi chala chanu kumanzere kapena kumanja kuti mupite patsamba lotsatira.
Ikani mabukumaki pa vesi kapena chaputala chimene mukuwerenga kuti musavutike kuchipeza mukafuna kupitiriza kuwerenga.
Gwiritsani ntchito gawo losonyeza zimene mwawerenga m’mbuyo kuti mupeze zimene mwawerenga posachedwapa.
Gwiritsani ntchito gawo lofufuzira kuti mufufuze mawu m’nkhani imene mukuwerenga.