Zatsopano pa JW.ORG

2026-01-05

NDANDANDA YA UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU

May–June 2026

2026-01-01

“Mudzamva phokoso la nkhondo”

Onani zimene Yesu ankatanthauza ponena mawu amenewa.

2026-01-01

NKHANI ZINA

Kuthandiza Anthu Amene Ali ndi Vuto Losaona

Onani zimene a Mboni za Yehova akuchita pothandiza anthu amene ali ndi vuto losaona komanso amene amaona movutikira kuti amve uthenga wabwino wa m’Baibulo womwe ndi wopatsa chiyembekezo.

2026-01-01

Tracts and Invitations

2026 Memorial Invitation

2025-12-31

NKHANI

Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 8 la 2025

Mulipotili, tiona mmene mavidiyo a Uthenga Wabwino wa Yesu akuthandizira anthu.

2025-12-29

MABUKU

Lipoti la Chaka cha Utumiki la Mboni za Yehova Padziko Lonse la 2025

Onani mmene ntchito yolalikira padziko lonse ya Mboni za Yehova yayendera kuyambira mu September 2024 kukafika mu August 2025.

2025-12-16

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

Munthu Wotchulidwa M’Baibulo​​—⁠Muzikhala Olimba Mtima Komanso Okhulupirika Ngati Benaya

Kodi chitsanzo cha Benaya chikutiphunzitsa chiyani pa nkhani ya kulimba mtima komanso kukhala okhulupirika nthawi zonse?

2025-12-16

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

March 2026

Nkhaniyi tidzaiphunzira wiki ya May 4–​June 7, 2026.

2025-12-12

MBIRI YA MOYO WANGA

David Maza: Banja Losangalala Linakumana ndi Zokhumudwitsa, Kenako Linayambiranso Kusangalalala

Mavuto amene banja lina linakumana nawo anathandiza anthu ena kuti azikhulupirira komanso kudalira Yehova.