Zatsopano pa JW.ORG

2026-03-03

NYIMBO ZA BROADCASTING

Ndidzayembekezera Yehova

Tiziyembekezera Yehova pomaganizira kwambiri za zinthu zina osati za mavuto omwe tikukumana nawo m’ndende, komanso pomalimbitsa kwambiri chikhulupiriro chathu.

2026-03-02

NDANDANDA YA UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU

July–August 2026

2026-02-27

KHALANI MASO

Kodi Kuchitira Ena Nkhanza Chifukwa Chodana Nawo Kudzatha?—Zimene Baibulo Limanena

Baibulo limalonjeza kuti zachiwawa zimene anthu amachitira ena chifukwa chodana nawo zidzatha, komanso limapereka malangizo othandiza a mmene tingathetsere chidani masiku ano. Onani zimene Mawu a Mulungu amanena.

2026-02-17

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

Munthu Wotchulidwa M’Baibulo: Manayeni Ankaona Kuti Kutumikira Yehova N’kofunika Kwambiri pa Moyo Wake

Onani zimene Manayeni ankachita kuti aziika zinthu zokhudza kulambira pamalo oyamba osati za m’dzikoli.

2026-02-17

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

May 2026

M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira July 6–​August 9, 2026.

2026-02-17

KODI ZINANGOCHITIKA ZOKHA?

Luso la Akalabwi Lokonza Madamu​​—Kodi Zinangochitika Zokha?

Onani chifukwa chake akalabwi amadziwika kuti ndi akatswiri oteteza zinthu zachilengedwe.

2026-02-05

KHALANI MASO

Asayansi Akokera Wotchi Yosonyeza Nthawi ya Kutha kwa Dziko Kuti Iyandikire 12 Koloko Usiku

Wotchi yosonyeza kutha kwa dziko, yayandikila kwambiri 12 koloko usiku kuposa kale lonse. Onani zimene Baibulo limanena zokhudza zomwe zidzachitike m’tsogolo komanso zimene mungachite kuti muziona zinthu moyenera.