Zatsopano pa JW.ORG
NDANDANDA YA UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU
May–June 2026
“Mudzamva phokoso la nkhondo”
Onani zimene Yesu ankatanthauza ponena mawu amenewa.
NKHANI ZINA
Kuthandiza Anthu Amene Ali ndi Vuto Losaona
Onani zimene a Mboni za Yehova akuchita pothandiza anthu amene ali ndi vuto losaona komanso amene amaona movutikira kuti amve uthenga wabwino wa m’Baibulo womwe ndi wopatsa chiyembekezo.
Tracts and Invitations
2026 Memorial Invitation
NKHANI
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 8 la 2025
Mulipotili, tiona mmene mavidiyo a Uthenga Wabwino wa Yesu akuthandizira anthu.
MABUKU
Lipoti la Chaka cha Utumiki la Mboni za Yehova Padziko Lonse la 2025
Onani mmene ntchito yolalikira padziko lonse ya Mboni za Yehova yayendera kuyambira mu September 2024 kukafika mu August 2025.
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
Munthu Wotchulidwa M’Baibulo—Muzikhala Olimba Mtima Komanso Okhulupirika Ngati Benaya
Kodi chitsanzo cha Benaya chikutiphunzitsa chiyani pa nkhani ya kulimba mtima komanso kukhala okhulupirika nthawi zonse?
MBIRI YA MOYO WANGA
David Maza: Banja Losangalala Linakumana ndi Zokhumudwitsa, Kenako Linayambiranso Kusangalalala
Mavuto amene banja lina linakumana nawo anathandiza anthu ena kuti azikhulupirira komanso kudalira Yehova.

