Zatsopano pa JW.ORG
NYIMBO ZA BROADCASTING
Ndidzayembekezera Yehova
Tiziyembekezera Yehova pomaganizira kwambiri za zinthu zina osati za mavuto omwe tikukumana nawo m’ndende, komanso pomalimbitsa kwambiri chikhulupiriro chathu.
NDANDANDA YA UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU
July–August 2026
KHALANI MASO
Kodi Kuchitira Ena Nkhanza Chifukwa Chodana Nawo Kudzatha?—Zimene Baibulo Limanena
Baibulo limalonjeza kuti zachiwawa zimene anthu amachitira ena chifukwa chodana nawo zidzatha, komanso limapereka malangizo othandiza a mmene tingathetsere chidani masiku ano. Onani zimene Mawu a Mulungu amanena.
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
Munthu Wotchulidwa M’Baibulo: Manayeni Ankaona Kuti Kutumikira Yehova N’kofunika Kwambiri pa Moyo Wake
Onani zimene Manayeni ankachita kuti aziika zinthu zokhudza kulambira pamalo oyamba osati za m’dzikoli.
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
May 2026
M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira July 6–August 9, 2026.
KODI ZINANGOCHITIKA ZOKHA?
Luso la Akalabwi Lokonza Madamu—Kodi Zinangochitika Zokha?
Onani chifukwa chake akalabwi amadziwika kuti ndi akatswiri oteteza zinthu zachilengedwe.
KHALANI MASO
Asayansi Akokera Wotchi Yosonyeza Nthawi ya Kutha kwa Dziko Kuti Iyandikire 12 Koloko Usiku
Wotchi yosonyeza kutha kwa dziko, yayandikila kwambiri 12 koloko usiku kuposa kale lonse. Onani zimene Baibulo limanena zokhudza zomwe zidzachitike m’tsogolo komanso zimene mungachite kuti muziona zinthu moyenera.

