Zatsopano pa JW.ORG
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
Mfundo Zothandiza Pophunzira—Muzimvetsa Mawu a M’Baibulo Oyerekezera Zinthu
Mfundo zitatu zomwe zingakuthandizeni kumvetsa bwino mawu a m’Baibulo oyerekezera zinthu.
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
David Splane: Yehova Wakhala Akundiphunzitsa Kuyambira Ndili Mwana
Poganizira zimene zachitika zaka 80 zapitazo, M’bale David Splane akufotokoza mmene Yehova wakhala akumuphunzitsira mwachikondi pogwiritsa ntchito gulu lake komanso abale ndi alongo odziwa zambiri.
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
April 2026
M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira wiki ya June 8–July 5, 2026.
NDANDANDA YA UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU
May–June 2026
“Mudzamva phokoso la nkhondo”
Onani zimene Yesu ankatanthauza ponena mawu amenewa.
NKHANI ZINA
Kuthandiza Anthu Amene Ali ndi Vuto Losaona
Onani zimene a Mboni za Yehova akuchita pothandiza anthu amene ali ndi vuto losaona komanso amene amaona movutikira kuti amve uthenga wabwino wa m’Baibulo womwe ndi wopatsa chiyembekezo.
Tracts and Invitations
2026 Memorial Invitation
NKHANI
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 8 la 2025
Mulipotili, tiona mmene mavidiyo a Uthenga Wabwino wa Yesu akuthandizira anthu.
MABUKU
Lipoti la Chaka cha Utumiki la Mboni za Yehova Padziko Lonse la 2025
Onani mmene ntchito yolalikira padziko lonse ya Mboni za Yehova yayendera kuyambira mu September 2024 kukafika mu August 2025.
NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)
Munthu Wotchulidwa M’Baibulo—Muzikhala Olimba Mtima Komanso Okhulupirika Ngati Benaya
Kodi chitsanzo cha Benaya chikutiphunzitsa chiyani pa nkhani ya kulimba mtima komanso kukhala okhulupirika nthawi zonse?

