Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Thailand

 

2017-02-13

THAILAND

Akuluakulu a Boma la Thailand Akugwiritsa Ntchito Mabuku a Mboni za Yehova Pothandiza Anthu a M’dziko Lawo

Kwa zaka zitatu zapitazi, akuluakulu a boma ku Thailand akhala akugwiritsa ntchito mabuku a Mboni pophunzitsa anthu makhalidwe abwino.