Thailand
Akuluakulu a Boma la Thailand Akugwiritsa Ntchito Mabuku a Mboni za Yehova Pothandiza Anthu a M’dziko Lawo
Kwa zaka zitatu zapitazi, akuluakulu a boma ku Thailand akhala akugwiritsa ntchito mabuku a Mboni pophunzitsa anthu makhalidwe abwino.