Ghana
A Mboni za Yehova Anathandiza ku Ghana Kutasefukira Madzi
Ofesi ya nthambi ya Mboni za Yehova ya ku Ghana inakhazikitsa komiti yomwe cholinga chake chinali kukathandiza anthu ndipo inapereka madzi komanso thandizo la mankhwala kwa anthu amene anakhudzidwa ndi ngozi ya kusefukira kwa madzi.