Croatia
A Mboni Anachita Nawo Chionetsero cha Mabuku Pamwambo Wodziwika Kwambiri ku Croatia
A Mboni za Yehova anachita nawo chionetsero chamabuku ku Croatia. Mwambowu unachitika pa 11 mpaka pa 16 November 2014 ndipo unali wa nambala 37. Anthu a m’mayiko osiyanasiyana anapita kukaonetsa mabuku awo.
A Mboni Anathandiza Anthu Okhudzidwa ndi Kusefukira kwa Madzi ku Balkans
Nthawi yomweyo a Mboni za Yehova anayamba kuthandiza ndiponso kulimbikitsa anthu omwe anakhudzidwa ndi ngozi ya madzi osefukira ya pa May 2014 yomwe sinachitikepo ku Bosnia-Herzegovina, Croatia ndi Serbia.