Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Malo a Nkhani

 

2024-03-15

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti Lachiwiri la Bungwe Lolamulira la 2024

Mu lipotili, tiona mmene Atate wathu wachikondi Yehova, amasonyezera kuti “akufuna kuti anthu onse alape.” (2 Pet. 3:9) Tionanso zinthu zina zimene zasintha pa nkhani ya mmene tiyenera kuvalira tikamachita zinthu zauzimu.

2024-01-29

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 1 la 2024

Onani mmene kukonda anthu kungatithandizire kuti tizichita khama mu utumiki.