Malo a Nkhani
Lipoti Lachiwiri la Bungwe Lolamulira la 2024
Mu lipotili, tiona mmene Atate wathu wachikondi Yehova, amasonyezera kuti “akufuna kuti anthu onse alape.” (2 Pet. 3:9) Tionanso zinthu zina zimene zasintha pa nkhani ya mmene tiyenera kuvalira tikamachita zinthu zauzimu.
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 1 la 2024
Onani mmene kukonda anthu kungatithandizire kuti tizichita khama mu utumiki.