Chichewa
Malo a Nkhani
https://assetsnffrgf-a.akamaihd.net/assets/ct/d71826a198/images/syn_placeholder_sqr.png

Malo a Nkhani

 

2025-12-31

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 8 la 2025

Mulipotili, tiona mmene mavidiyo a Uthenga Wabwino wa Yesu akuthandizira anthu.

2025-11-14

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 7 la 2025

Mu lipotili, muli zinthu zosangalatsa zomwe zili mu Lipoti la Chaka cha Utumiki cha 2025 ndipo likufotokoza mmene Yehova wadalitsira ntchito yathu padziko lonse.

2025-10-01

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 6 la 2025

Mu lipotili tikambirana za lemba la chaka cha 2026 komanso nyimbo yatsopano.

2025-08-22

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 5 la 2025

Mu lipotili, tiona mfundo za m’Baibulo zomwe zingatithandize kusankha mwanzeru pa nkhani ya maphunziro owonjezera.

2025-07-08

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 4 la 2025

Mu lipotili, tikambirana mfundo za m’Baibulo zomwe zingatithandize kuti tizisankha zinthu mwanzeru pa nkhani ya zizindikiro komanso miyambo.

2025-05-21

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti Lachitatu la Bungwe Lolamulira la 2025

Mu lipoti lino tiona zimene tingachite pokonzekera kuchita zambiri potumikira Yehova m’miyezi ikubwerayi.

2025-03-21

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti Lachiwiri la Bungwe Lolamulira la 2025

Mu lipotili, tiona zimene gulu lathu lakhala likuchita pothandiza anthu kuti adziwe kulemba ndi kuwerenga komanso mtendere umene timapeza chifukwa cha nsembe ya dipo ya Yesu. Tionanso za kutulutsidwa kwa nyimbo yatsopano yomwe tidzaimbe pamsonkhano wa 2025.

2025-02-03

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti Loyamba la Bungwe Lolamulira la 2025

Mulipotili, tiona mmene tingagwiritsire ntchito gawo lakuti “Choonadi Chomwe Timakonda Kuphunzitsa Anthu,” lomwe lili mu zakumapeto A m’kabuku kakuti Muzikonda Anthu​—Muziwaphunzitsa. Kuphunzira mfundo za choonadizi kutithandiza kuti tizisangalala tikamakambirana ndi anthu mu utumiki.