Malo a Nkhani
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 8 la 2025
Mulipotili, tiona mmene mavidiyo a Uthenga Wabwino wa Yesu akuthandizira anthu.
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 7 la 2025
Mu lipotili, muli zinthu zosangalatsa zomwe zili mu Lipoti la Chaka cha Utumiki cha 2025 ndipo likufotokoza mmene Yehova wadalitsira ntchito yathu padziko lonse.
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 6 la 2025
Mu lipotili tikambirana za lemba la chaka cha 2026 komanso nyimbo yatsopano.
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 5 la 2025
Mu lipotili, tiona mfundo za m’Baibulo zomwe zingatithandize kusankha mwanzeru pa nkhani ya maphunziro owonjezera.
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 4 la 2025
Mu lipotili, tikambirana mfundo za m’Baibulo zomwe zingatithandize kuti tizisankha zinthu mwanzeru pa nkhani ya zizindikiro komanso miyambo.
Lipoti Lachitatu la Bungwe Lolamulira la 2025
Mu lipoti lino tiona zimene tingachite pokonzekera kuchita zambiri potumikira Yehova m’miyezi ikubwerayi.
Lipoti Lachiwiri la Bungwe Lolamulira la 2025
Mu lipotili, tiona zimene gulu lathu lakhala likuchita pothandiza anthu kuti adziwe kulemba ndi kuwerenga komanso mtendere umene timapeza chifukwa cha nsembe ya dipo ya Yesu. Tionanso za kutulutsidwa kwa nyimbo yatsopano yomwe tidzaimbe pamsonkhano wa 2025.
Lipoti Loyamba la Bungwe Lolamulira la 2025
Mulipotili, tiona mmene tingagwiritsire ntchito gawo lakuti “Choonadi Chomwe Timakonda Kuphunzitsa Anthu,” lomwe lili mu zakumapeto A m’kabuku kakuti Muzikonda Anthu—Muziwaphunzitsa. Kuphunzira mfundo za choonadizi kutithandiza kuti tizisangalala tikamakambirana ndi anthu mu utumiki.

