Malo a Nkhani
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 4 la 2024
Mu lipotili, tiona zimene abale ndi alongo athu amene ali m’ndende chifukwa cha zimene amakhulupirira akuchita kuti ‘apitirize kugonjetsa choipa pochita chabwino.’—Aroma 12:21.
Lipoti Lachiwiri la Bungwe Lolamulira la 2024
Mu lipotili, tiona mmene Atate wathu wachikondi Yehova, amasonyezera kuti “akufuna kuti anthu onse alape.” (2 Pet. 3:9) Tionanso zinthu zina zimene zasintha pa nkhani ya mmene tiyenera kuvalira tikamachita zinthu zauzimu.

