Malo a Nkhani
Lipoti Lachiwiri la Bungwe Lolamulira la 2025
Mu lipotili, tiona zimene gulu lathu lakhala likuchita pothandiza anthu kuti adziwe kulemba ndi kuwerenga komanso mtendere umene timapeza chifukwa cha nsembe ya dipo ya Yesu. Tionanso za kutulutsidwa kwa nyimbo yatsopano yomwe tidzaimbe pamsonkhano wa 2025.
Lipoti Loyamba la Bungwe Lolamulira la 2025
Mulipotili, tiona mmene tingagwiritsire ntchito gawo lakuti “Choonadi Chomwe Timakonda Kuphunzitsa Anthu,” lomwe lili mu zakumapeto A m’kabuku kakuti Muzikonda Anthu—Muziwaphunzitsa. Kuphunzira mfundo za choonadizi kutithandiza kuti tizisangalala tikamakambirana ndi anthu mu utumiki.
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 8 la 2024
Mulipotili, tikambirana zimene tingachite kuti tiziona moyenera abale ndi alongo amene amaoneka m’mavidiyo athu.
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 7 la 2024
Mulipotili, timva zokhudza abale ndi alongo athu padziko lonse komanso tionera mbali yocheza ndi abale atsopano a m’Bungwe Lolamulira, omwe ndi M’bale Jody Jedele ndiponso Jacob Rumph.

