Malo a Nkhani
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 4 la 2026
Mulipotili, timva zinthu zolimbikitsa zokhudza maulendo ochezera nthambi komanso maulendo aubusa amene anachitika posachedwapa. Timvanso mmene milandu yomwe ikukhudza ufulu wathu wolambira yayendera ku Norway ndi ku Sweden.

