Become Jehovah’s Friend—Posters
Posita: Yehova Akuthandiza Kuti Ukhale Wolimba Mtima
Panga dawunilodi n’kupulinta posita ya vidiyoyi imene ingakukumbutse kuti Yehova akuthandiza kuti ukhale wolimba mtima.
Posita: Uzisangalatsa Yehova
pangani dawunilodi ndi kusindikiza positayi kenako muiike pa zinthu zomwe munapanga dawunilodi.
Posita: Yehova Amakhululuka
Pangani dawunilodi ndi kusindikiza posita imene ikutiuza mmene Yehova amakhululukira anthu okhulupirika akalakwitsa zinazake.
Posita: Kodi Yehova Amayankha Mapemphero?
Pangani Dawunilodi n’kusindikiza posita ya vidiyoyi kenako muisunge pabwino.
Posita: Ndi Ndani Angakhale Mnzanga?
Sindikizani positayi ndi kuiika pamalo omwe muzitha kuiona pafupipafupi.

