Nkhani ya Yona Imatiphunzitsa Kukhala Olimba Mtima Komanso Achifundo
Yehova watuma mneneri Yona kuti akapereke uthenga wachiweruzo mumzinda wa Nineve m’dziko la Asuri koma iye akuchita zosemphana ndi zomwe wauzidwa. Mukamaonera vidiyoyi muona kuti Yona waphunzira kukhala wolimba mtima komanso wachifundo chifukwa cha zomwe wakumana nazo.
Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi
TSANZIRANI CHIKHULUPIRIRO CHAWO
Yona—Anaphunzira pa Zolakwa Zake
Kodi mungamvetse chifukwa chake Yona ankaopa kugwira ntchito imene Mulungu anamupatsa? Nkhani ya Yona ikutiphunzitse zambiri zokhudza kuleza mtima ndiponso chifundo cha Yehova.
TSANZIRANI CHIKHULUPIRIRO CHAWO
Yona—Anaphunzira Kufunika Kochitira Ena Chifundo
Kodi nkhani ya Yona ingatithandize bwanji kudzifufuza?