GALAMUKANI!

Zamkatimu

Chichewa
Zamkatimu
/assets/ct/fa815d8e9f/images/syn_placeholder_sqr.png
g04 7/8 mas. 1-2
Zamkatimu

Zamkatimu

July 8, 2004

Kuthana ndi Mavuto Amene Amakhalapo Achinyamata Akamakula

Wachinyamata akamakula akuti amakhala ngati akuyenda pa kachingwe koonda popanda chinachake pansipa choti chimuwakhe akagwa. Kodi angatani kuti zinthu zimuyendere bwino?

3 Zosangalatsa ndi Zovuta Zimene Zimakhalapo Achinyamata Akamakula

4 ‘Kodi Chikuchitika N’chiyani M’thupi Mwangamu?’

8 “Ukumbukire Mlengi Wako”

10 Kuyeza Dziko Lapansi ndi Ndodo

11 Kodi Kukhulupirira Mulungu N’kusemphana ndi Sayansi?

13 Zifukwa Zimene Asayansi Ena Amakhulupirira Mulungu

18 Kodi Mayankho Mungawapeze Kuti?

24 Lavenda Mphatso Imene Imasangalatsa Lilime, Maso ndi Mphuno Zathu

26 Lingaliro la Baibulo

Kodi Kukhala Mutu wa Banja Kumatanthauzanji?

32 Mayi Wanzeru

Kodi Ndingatani Kuti Chibwenzi Changa Chisiye Kundizunza? 21

Kodi mungatani ngati muli pachibwenzi ndi munthu amene amakulankhulani mawu opweteka, ngakhale kukumenyani kumene?

Moŵa—Mbiri ya Chakumwa cha Maonekedwe a Golide 28

Anthu akhala akufulula moŵa kwa zaka zambiri. Tamvani mbiri yake yochititsa chidwi.