GALAMUKANI!

Zamkatimu

Chichewa
Zamkatimu
/assets/ct/fa815d8e9f/images/syn_placeholder_sqr.png
g00 7/8 mas. 1-2
Zamkatimu

Zamkatimu

July 8, 2000

Kodi Moyo N’ngwotsika Mtengo Chonchi?

M’zaka zaposachedwapa kukukhala ngati kwayambika “chikhalidwe cha imfa” pakati pa achinyamata. Kodi chikuchititsa khalidweli n’chiyani? Kodi pali njira yolithetsera?

3 Kodi Moyo Ukutsikiratsikira Mtengo?

5 Kodi “Chikhalidwe cha Imfa” Chimalimbikitsidwa Motani?

8 Kuthandiza Achinyamata Kuthawa “Chikhalidwe cha Imfa”

11 Nkhani Zokopa Zingaphetse Anthu

12 Kupotoza Nkhani

17 Musanyengedwe ndi Nkhani Zokopa!

20 Kodi Ndizimwa Asipilini Tsiku N’tsiku?

22 Lingaliro la Baibulo

Kodi Mtumiki Ndani?

26 Achinyamata Akufunsa Kuti . . .

Kodi Ndisamukire Kudziko lina?

32 “Ndimakonda Mmene Imalongosolera Nkhani”

Zoopsa za Kukwera Matola 24

Kwa anthu amene amakwera matola, kodi ndi machenjezo ati amene ali ofunika kuti asagwe m’mavuto?

Mwetulirani—N’zothandiza kwa Inu! 29

Kodi kumwetulira kungakuthandizeni m’njira iliyonse m’moyo wanu wa tsiku n’tsiku?

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

AP Photo/Laura Rauch