Yesetsani Kuti Mukhale Oyang’anira
Zimakhala bwino kwambiri abale akayamba kuchita zambiri mumpingo adakali aang’ono. Zimenezi zimawapatsa mpata woti asonyeze kuti ndi woyenerera kudzakhala atumiki othandiza akadzakula. (1 Tim. 3:10) Kodi m’bale angatani kuti akhale ndi udindo mumpingo? Ayenera kuyesetsa kumachita zinthu zotsatirazi:
-
Kudzipereka.—km 7/13 2-3 ¶2
-
Kukonda zinthu zauzimu.—km 7/13 3 ¶3
-
Kukhala wodalirika komanso wokhulupirika.—km 7/13 3 ¶4