Pulogalamu ya Msonkhano wa 2025 Wakuti ”Kulambira Koyera”
Lachisanu
Pulogalamu ya Lachisanu yachokera pa Mateyu 4:10—“Yehova Mulungu wako ndi amene uyenera kumulambira.”
Loweruka
Pulogalamu ya Loweruka yachokera pa Yohane 2:17—“Kudzipereka kwanga panyumba yanu kudzakhala ngati moto umene ukuyaka mumtima mwanga.”
Lamlungu
Pulogalamu ya Lamlungu yachokera pa Yohane 4:23—“Adzalambira Atate motsogoleredwa ndi mzimu ndi choonadi.”
Mawu kwa Osonkhana
Mawu othandiza anthu amene asonkhana.
Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi
ZOKHUDZA IFEYO
Dzabwereni ku Msonkhano wa 2026—“Chimwemwe Chosatha”
Tikukuitanirani ku Msonkhano wa masiku atatu wachaka chino wa Mboni za Yehova.
MISONKHANO IKULUIKULU
Tikukuitanirani Kumsonkhano wa Mboni za Yehova wa 2025 wa Mutu Wakuti: “Kulambira Koyera”
Kodi Yesu anaphunzitsa zotani zokhudza kulambira koona?
MISONKHANO IKULUIKULU
Zimene Zili Muvidiyo Yakuti: Uthenga Wabwino wa Yesu: Gawo 2 ndi 3
Tsopano Yesu wakula ndipo wayamba kusonkhanitsa ophunzira ake. Komabe, anthu ayamba kale kumutsutsa pa utumiki wake.

